Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
Mulungu pamene Kristu adzaonelera ndiye moyo wathu pamenepo<br />
inunso mudzawonekera pamodzi ndi iye mu ulemerero chifukwa<br />
chake fetsani ziwalo zili dziko, dama chidetso chifuniro cha manyazi.<br />
Chilakolako, choipa ndi chisiliro chimene chili kupembedza mafano<br />
chifukwa cha izi zomwe ukudza mkwiyo wa Mulungu pa ana<br />
akusamvera zimene munayendamo inunso kale pamene tayani<br />
inunso zonsezi mkwiyo, kupsya mtima, dumbo, mwano, zonyasa<br />
zotuluka mkamwa mwanu. Musamanamizana wina ndi mzake<br />
popeza mudabvula munthu wakale pamodzi ndi ntchito zake<br />
ndipo munabvala watsopano amene alikukonzeka watsopano kuti<br />
akhale nacho chizindikilitso monga mwa chifaniziro cha iye amene<br />
anamulenga iye.<br />
Pano pali chinthuci cha mayambidwe a moyo wa ophunzira.<br />
Anafa ndi kuuka pamodzi ndi Kristu ndipo analandira watsopano<br />
amene al okonzedwanso mu chidziwitso mu chidzalo cha mwini<br />
mulengi. Ndipo tsopano pali tsopano kuchoka mu ifa ndikuchoka<br />
mu ukapolo wa chimo.<br />
Payenera kuti ophunzira aliyense pagulu wayenda mu maziko<br />
amenewa. Kuukitsidwanso kwa mtima ndi kulora chitsimikizo<br />
cha ophunzira amenewa palibe aliyense amene angachite monga<br />
thupi Sali thupi ungalero kuti ali osakanizilana mgwilizano ndi<br />
chiyanjano cha mtima ndi kuunika pamene pali chotupitsa ndipo<br />
ndi mtanda wonse.<br />
Funso lonse la <strong>Yesu</strong> limatengera gulu lonse kuzilakolako monga<br />
thupi la anthu osamva ndi obvuta. Ambirir a iwo ali monga<br />
atsogoleri ndipo salinso mmanja ndi chitsogozo chake cha Mulungu<br />
okhawo amene anaika moyo wawo pansi la gome lansembe kw a<strong>Yesu</strong>.<br />
Kutaya machitidwe adziko lapansi ndiyo amene angasese chifuniro<br />
chake cha Mulungu mwamva? (Aroma 12) ndipo machitidwe<br />
otero monga gulu ndi ngozi yaikulu ngati utsogoleri uli otekeseka<br />
anakumana muzitseko zomata ndi kusankha nkhani. Ndikuzipeleka<br />
kwa anthu polonjeza zinthu ndi zakuwaopsyeza. Kuwanyengelera<br />
ndi kuchita zones mozikondi chisokonezo. Ngati utsogoleri uli<br />
wangwiro wotero ndikukhala ndi zokwanilitsidwa za mumtima ndiye<br />
kuti adzawamanga anthu ndi malamulo. Zoonetsetsa anzanga ambiri<br />
a ife takhalapo mu magulu otere ndi kukhalanso mu utsogoleri<br />
otere. Ndipo ndi ife mboni kuti uzimu wokhala osokonekera mu<br />
machitidwe otere. Sichifukwa chake kodi kuti zones za uzimu<br />
zakhala zosayenda bwino pa ulamuliro ndi kugonjera?<br />
Koma sitiyenera kutero ai, ku moyo wathu wakale ndikulandira<br />
watsopano ndikupilira kuphunzira kuyenda moyo obisika wa<br />
<strong>Yesu</strong> mwa Mulungu. Simungathe kuchita chinyengo padzanja la<br />
mphamvu ndi kupsinja anthu ena?<br />
Ndiye pali malembo ena mu Akolose 3 pamene palibe Mheleni<br />
ndi Ayuda, mdulidwe ndi kusadulidwa watchedwa wakunja, mskuti<br />
kapolo, mfulu, komati Kristu ndiye zonse ndi zonse.<br />
Pano pakati pa anthu opachikidwa ndi kuuka ndi potheka<br />
kuti Kristu achite zones kuti athane ndi zosiyana kuti zither<br />
ndi kuchitidwa. Nkhani ya umodzi, kapenanso kulumikizidwa<br />
pamodzi pokhala miyala yamoyo ndipo yoikidwa kukhala kachisi<br />
woyera mw aAmbuye ndi izinso ndi zofunika kwabasi ngati muli<br />
anthu chabe amene magwilidwe ake ndi osalumikizidwa bwino<br />
ndiye kuti ndi zobvuta izi ndi zoona pakuonetsedwa ndi kumvera<br />
kwa Kristu. Izi ndiye zoyembekezedwa koma nthawi zina sitili<br />
otero mungwilizano wathu kwa amene Sali pa umodzi ndi ife.<br />
Tili ndi ufulu otero ndi udindo popeleka malangizo kwa ana<br />
athu, koma sitingaterenso popeleka ufulu otero kwa iwo amene<br />
tangokumana nawo kukogula katundu.<br />
Zanditengela ine nthawi ndidziwe zinthu ngati izi chifukwatu<br />
sindinali otero kwa nthawi yaitali zaka zitatu kapena zinai<br />
zapitanso ndinali kuwatchula molakwa kuti anali mpingo.<br />
Timafuna kuti tikhale amodzi ndipo ndinali okhala odandaula<br />
ngati sizingatero Mike Petyers anandiuza ine nthawi ina siya kuti<br />
ubweletse anthu pamodzi ndi kuwatcha mkati mwa mpingo<br />
ndikuwauza kuti adzikhala moyo wina kweza <strong>Yesu</strong> ndipo<br />
muloleni kuti abweletse anthu kw aiye yekha. Ndipo musalore<br />
kuti adandaule ndi kuzungulidwa. Linali langizo labwino koma<br />
lobvuta kuti ndilikwanilitse.<br />
40 41