29.12.2012 Views

Untitled - Yesu Kristo

Untitled - Yesu Kristo

Untitled - Yesu Kristo

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

Mulungu pamene Kristu adzaonelera ndiye moyo wathu pamenepo<br />

inunso mudzawonekera pamodzi ndi iye mu ulemerero chifukwa<br />

chake fetsani ziwalo zili dziko, dama chidetso chifuniro cha manyazi.<br />

Chilakolako, choipa ndi chisiliro chimene chili kupembedza mafano<br />

chifukwa cha izi zomwe ukudza mkwiyo wa Mulungu pa ana<br />

akusamvera zimene munayendamo inunso kale pamene tayani<br />

inunso zonsezi mkwiyo, kupsya mtima, dumbo, mwano, zonyasa<br />

zotuluka mkamwa mwanu. Musamanamizana wina ndi mzake<br />

popeza mudabvula munthu wakale pamodzi ndi ntchito zake<br />

ndipo munabvala watsopano amene alikukonzeka watsopano kuti<br />

akhale nacho chizindikilitso monga mwa chifaniziro cha iye amene<br />

anamulenga iye.<br />

Pano pali chinthuci cha mayambidwe a moyo wa ophunzira.<br />

Anafa ndi kuuka pamodzi ndi Kristu ndipo analandira watsopano<br />

amene al okonzedwanso mu chidziwitso mu chidzalo cha mwini<br />

mulengi. Ndipo tsopano pali tsopano kuchoka mu ifa ndikuchoka<br />

mu ukapolo wa chimo.<br />

Payenera kuti ophunzira aliyense pagulu wayenda mu maziko<br />

amenewa. Kuukitsidwanso kwa mtima ndi kulora chitsimikizo<br />

cha ophunzira amenewa palibe aliyense amene angachite monga<br />

thupi Sali thupi ungalero kuti ali osakanizilana mgwilizano ndi<br />

chiyanjano cha mtima ndi kuunika pamene pali chotupitsa ndipo<br />

ndi mtanda wonse.<br />

Funso lonse la <strong>Yesu</strong> limatengera gulu lonse kuzilakolako monga<br />

thupi la anthu osamva ndi obvuta. Ambirir a iwo ali monga<br />

atsogoleri ndipo salinso mmanja ndi chitsogozo chake cha Mulungu<br />

okhawo amene anaika moyo wawo pansi la gome lansembe kw a<strong>Yesu</strong>.<br />

Kutaya machitidwe adziko lapansi ndiyo amene angasese chifuniro<br />

chake cha Mulungu mwamva? (Aroma 12) ndipo machitidwe<br />

otero monga gulu ndi ngozi yaikulu ngati utsogoleri uli otekeseka<br />

anakumana muzitseko zomata ndi kusankha nkhani. Ndikuzipeleka<br />

kwa anthu polonjeza zinthu ndi zakuwaopsyeza. Kuwanyengelera<br />

ndi kuchita zones mozikondi chisokonezo. Ngati utsogoleri uli<br />

wangwiro wotero ndikukhala ndi zokwanilitsidwa za mumtima ndiye<br />

kuti adzawamanga anthu ndi malamulo. Zoonetsetsa anzanga ambiri<br />

a ife takhalapo mu magulu otere ndi kukhalanso mu utsogoleri<br />

otere. Ndipo ndi ife mboni kuti uzimu wokhala osokonekera mu<br />

machitidwe otere. Sichifukwa chake kodi kuti zones za uzimu<br />

zakhala zosayenda bwino pa ulamuliro ndi kugonjera?<br />

Koma sitiyenera kutero ai, ku moyo wathu wakale ndikulandira<br />

watsopano ndikupilira kuphunzira kuyenda moyo obisika wa<br />

<strong>Yesu</strong> mwa Mulungu. Simungathe kuchita chinyengo padzanja la<br />

mphamvu ndi kupsinja anthu ena?<br />

Ndiye pali malembo ena mu Akolose 3 pamene palibe Mheleni<br />

ndi Ayuda, mdulidwe ndi kusadulidwa watchedwa wakunja, mskuti<br />

kapolo, mfulu, komati Kristu ndiye zonse ndi zonse.<br />

Pano pakati pa anthu opachikidwa ndi kuuka ndi potheka<br />

kuti Kristu achite zones kuti athane ndi zosiyana kuti zither<br />

ndi kuchitidwa. Nkhani ya umodzi, kapenanso kulumikizidwa<br />

pamodzi pokhala miyala yamoyo ndipo yoikidwa kukhala kachisi<br />

woyera mw aAmbuye ndi izinso ndi zofunika kwabasi ngati muli<br />

anthu chabe amene magwilidwe ake ndi osalumikizidwa bwino<br />

ndiye kuti ndi zobvuta izi ndi zoona pakuonetsedwa ndi kumvera<br />

kwa Kristu. Izi ndiye zoyembekezedwa koma nthawi zina sitili<br />

otero mungwilizano wathu kwa amene Sali pa umodzi ndi ife.<br />

Tili ndi ufulu otero ndi udindo popeleka malangizo kwa ana<br />

athu, koma sitingaterenso popeleka ufulu otero kwa iwo amene<br />

tangokumana nawo kukogula katundu.<br />

Zanditengela ine nthawi ndidziwe zinthu ngati izi chifukwatu<br />

sindinali otero kwa nthawi yaitali zaka zitatu kapena zinai<br />

zapitanso ndinali kuwatchula molakwa kuti anali mpingo.<br />

Timafuna kuti tikhale amodzi ndipo ndinali okhala odandaula<br />

ngati sizingatero Mike Petyers anandiuza ine nthawi ina siya kuti<br />

ubweletse anthu pamodzi ndi kuwatcha mkati mwa mpingo<br />

ndikuwauza kuti adzikhala moyo wina kweza <strong>Yesu</strong> ndipo<br />

muloleni kuti abweletse anthu kw aiye yekha. Ndipo musalore<br />

kuti adandaule ndi kuzungulidwa. Linali langizo labwino koma<br />

lobvuta kuti ndilikwanilitse.<br />

40 41

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!