12.07.2015 Views

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

SHOW MORE
SHOW LESS
  • No tags were found...

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

ndi kwa <strong>Yesu</strong> powauza kwa iwo za <strong>Yesu</strong> ali ndi moyo ndi thupi lake ndimpingo sichimene upitako, ndi chimene uli ndi Banja osati bungwemungathe kutero pamene wina afunsa muli mu mpingo uti – pokhapomuli ndi chizindikiro chifukwa ngati sakhulupirira inu adzaganiza mulimonga m’modzi amene amapita ku nyumba zomangidwa ngati musiyanamu chikhulupiriro ndi zimene amachita iwo, koma ngati mulibe dzinamonga mipingo ya m’baibulo imene inalibe dzina lirilonse ndiye akafunsadzina la mpingo munganene za banja lodabwitsa la thupi la <strong>Yesu</strong> ndi moyowamoyo ukhala mwa anthu ake.“Mundondomeko chikhulupiriro” -Chotchinga chinaChifukwa china chimene kuli zipembedzo ndi kuzikonda kwa anthu chinandi kusiyana kwa maonekedwe. Kusiyana kwa zotsatira mu chikhulupiriropamene mbusa ndi munthu uja ndilankhula kale anayamba kulankhulanasamadziwa zimene mnzakeyo amakhulupirira ngati munthuwo ndiabale ena adakadziwa bwino munthu winayo anakatha kulankhula zinazosiyana mukuchokera mu mgwilizano wawo. Anakatha kulankhulakubadwa kwa <strong>Yesu</strong> komanso muimfa yake ndi kuuka kwa <strong>Yesu</strong>; komansozoti ali kubweranso kw aanthu ake. Adzayamba kuyankhula kuti Mkristundi ndani? Kuti ngati sungataye moyo wako kwa <strong>Yesu</strong> sungathe kumpezaiye, komanso ngati sungatenge mtanda wako sungathe kukhala ophunzirawake. Mu mgwilizano angayamba kugwira ntchito kuti mndondomeko yachikhulupiriro ndi otani.Muli ndi ana ndi amai? Ndondomeko ya chikhulupiriro chanu ndi yotanimu banja lanu? Pali zambiri zimene zili zofunika mu banja lanu koma mulibemdnodomeko wa chikhulupiriro m’banja lanu. Inde zimatero koma osatimotero sumaika pa chipupa koma zimakhala mu mtima wanu ndi m’mitimaya ana anu chifukwa munawaphunzitsa iwo ngati ndabwera pa nyumbayanu kudzakhala ndipo simundiuza iwe za “ndondomeko ya chikhulupiriro”ndidzaona pa nkhope yanu. Ndidzaona m’mene mumatchalira ndi akanzindi ana anu ndidzaonanso m’mene mumalimbikira ntchito ndipa chakudyapagome ndipo ndikakupezani kuti mwapinda mabondo anu ndi kupempherapa mbali poterosimunaike muzipupa koma ndondomekowo ulipo ndithu.Pamene mpingo ukhala banja ndi zofanana motere sitiika zinthu muzipupa, koma pamene mwatidziwa ife mumaona mu mitima. Ngatiwina adzakhala mbanja lathu, mpingo wathu (umene uli ndi anthu zanala anthu). Ndipo sakhulupirira zakubadwa kwa <strong>Yesu</strong> ndikuti iye ndimwana wa Mulungu ndikuti mwazi wa <strong>Kristo</strong> ndi umene unatiombola ifekuchokera kumachimo, sitingawapatse ndondomeko ya chikhulupirirochifukwa ndife banja silimodzi lokha monganso banja silikhala limodzilokha koma chifukwa tili nawo mi mitima yathu, monga mmene banjalichitira. Sipapita nthawi tisanakambilane zinthu zofunika.Bvuto lokhala ndi ndondomeko wa chikhulupiriro ndikuika pa chipupa ndizofanana kukhala ndi dzina la mpingo. Zimamanga zipupa ndi zotchingapakati pa anthu, ngati munthu angabwere kwa ine, nati “ndina mbabatisiti?Ine nditi, inde ndine mbabatisiti adzaganiza kuti amandidziwa, komasandidziwa koma zimene adziwa ndi zimene mubabatisiti amachita ndiyekumaganiza kuti amandidziwa. Mwa ichi ngati ndili mkristu opandachizindikiro ndiye sadzaopa ine chifukwa adzaganiza kuti wandidziwa kaletsopano adzalankhula kwa ine kuti ndine ndani chifukwa sindinabisaremu chizindikiro cha Babatisiti adzalankhula kwina zazinthu zina –monga mwazi wa <strong>Yesu</strong> ndipo ndingamuuze m’mene ndimakhulupirirangati ndikulakwitsa angathe kundithandiza kusintha koma ngati ndili waBabatisiti amanenatu kuti “chabwino” pamene tilibe zotchinga pamenepotidzakhala ndi mulumikizo umene tingathandize wina ndi mnzake.Kukonda anthu, koma mudane ndi zosakanizapamene mpingo mu Baibulo suli ndi kugawikana pa dzina posiyanitsakudziwika ndi a<strong>Kristo</strong> a mu mzinda wina pali chinthu ichi monga mwampingo pa wokha ndikunena ichi chifukwa ndi chofunika kukhala muubale ogwilizana ndi wina ndi mnzake. Mu dziko la Amerika pali kapenamitundu itatu pazochitika mu dziko la chikristu. Loyamba ndi mbaliya chipembedzo chokhala ndi chizindikiro. Alipo anthu abwino muchipembedzo zimenezi ndi ena oipanso. Pali anthu amene anachoka muchipembedzo koma sanathe kupeleka moyo wawo kwa okhulupirikaena ndipo pali kutayana. Amakonda <strong>Yesu</strong> ndipo amakhulupira choonadikoma amafuna anthu nthawi iliyonse. Malembo amati dandaulilananiwina ndi mnzake tsiku ndi tsiku pamene patchedwa lero. Ndipo8 9


ngati sitidandaulilana wina ndi mnzake potchedwa lero. Ndipo ngatisitidandaulilana wina ndi mnzake potchedwa tsiku ndipo tidzaumitsidwamtima ndi kuunitsidwa (Ahebri 3:12-13).Pali ena amalowana mukulumikizidwa pamodzi tsiku ndi tsiku mu moyo.Sali mbali ya chipembedzo, koma amakonda anthu a chipembedzo.Amakonda tsiku ndi tsiku ndipo ali mpingo. Sangoyenda chisawawa aliamene Baibulo amati “olungamitsidwa pamodzi ndi mitchempha” pamenembali ina yafooka, onse amafooka. Pamene mbali ina pali mdalitso, onseamakondwera amaima ndi kukhala pansi ndi kulankhula onse pamodzi.Uwu ndiwo mpingo opanda dzina ndi zinyumba zomangidwa kapenakuwonelera ndipo mamembala ake ali mu moyo kukondana wina ndimnzake tsiku lililonse.Ndiye magulu atatu amenewa. Ambiri amapita mumachitidwe oterenthawi zambiri. Ambiri tinaonetsedwa kwa <strong>Yesu</strong> mwa chipembedzo,ndipo zabwino zabwera kuchokera mukutero. Chifukwa ambiri ndi ofewakuganiza kwawo amaona kuti sangathe kupitiliza mu chipembedzo. <strong>Yesu</strong>anati ndidzalavula otentha chabe mkamwa mwake. Muchipembedzomuli anthu otentha ndi ozizira. Pamene musakaniza kutentha ndi kuzizirandipo amene amaganiza monga <strong>Yesu</strong> adzakhala ndi zobvuta pameneakhala ndi machitidwe otere. Tingakhala umasuka ndi kusatsaniza ngatindife osalumikidwa ndi <strong>Yesu</strong> chifukwa iye sakonda kusakaniza. Ndipotimakhala ndi zobvuta. Timakonda anthu, timafuna kutumikira ndikuthandiza ndiponso timawafunanso. Koma pamene pali kusakanizasitidziwa tidzachitanji. Anthu ena amachoka muzimenezo. Kapenansoamachotsedwa, amachoka mokhumudwa ndipo ali paokha. Timafunsa kutiakhale ndi anzawo mofulumira mu moyo wa tsiku ndi tsiku ndikusakhalapaokha nthawi yayitali. Tiyenera kupemphera zipembedzo ndi anthuapadera-dera amaene ali kumeneko, koma zipupa ziyenera kugwetsedwandi kutentha chabe kuyenera kutha. Malemba anati kuchotsa chotupitsamkate. Ichi ndi cholinga chathu – kuthandiza kuchotsa chotupitsa.Zimathandauza Chiani KukhalaWa NsembeKuchita Zinthu mu njira ya <strong>Yesu</strong>Mzuzu, Malawi, Africa, 1996Popanda maudindo – ndife tonse Asembe.Mu bukhu la Chibvumbulutso limati <strong>Yesu</strong> anatigula ife kukhala ufumuwa nsembe kutumikira Mulungu wathu (Chibvumbulutso 5) ngati tonsetingakhale ansembe tiyenera kudziwa kuti kukhala wansembe ndi chianingati tikufuna kukhala ndi mphamvu m’moyo mwathu tiyenera kukhala ndimaganizo a Mulungu pamoyo yathu. <strong>Yesu</strong> anati “pitani ndipo ndidzakhalananu” Anatiphunzitsa, chitani chifuniro changa ndipo ndidzakupatsaniinu moyo ndi mphamvu.Chikristo chonama kwa nthawi yaitali chapondeleza anthu pansi.Zatengera anthu ochepa ena ndi kuwakweza ndikuwapanga Atsogoleriolemera ndi otchuka ndi a mphamvu, potero ndikupondereza ena pansi,ku America, India, Poland, Romania, Brazil ndi malo ozongulira kuliakhristu apa mwamba ndi apansi. Izi ndi zoipa. <strong>Yesu</strong> ananena kwa Atumwikhumi mu Mateyu 23 musamutche wina Mphunzitsi, musamutche Atate,musamutche wina mtsogoleri win aAmbuye, kapena (Rabbi) mphunzitsikapena Mbusa kapena a Reverendi.Pakuti muli nonse abale ndi Atate m’modzi palibe otchuka mu Chikristochoona koma <strong>Yesu</strong> yekha. Pasakhale mabwana olemekezeka ameneakuchita zonse pa okha, ndalama, ndi anthu omwe pokhapo <strong>Yesu</strong> mwaanthu ake mwa Mzimu wake.Nsembe ya MoyoPamene Mulungu afuna kuti ife tikhale ansembe anali ndi malingaliromu maganizo ake. Wansembe amapeleka nsembe zauzimu kwa Mulungu.Mungathe kutero ndithu. Mulungu afuna kuti mutero. Sizaiwo utchuka10 11


okha ai ndi zawina ali yense wa ife. Nsembe ya uzimu monga Pauloananena ndi kupeleka matupi athu monga nsembe ya moyo. <strong>Yesu</strong> amafunalilime, maso anu ndi makutu. Amafuna maganizo anu, manja ndi mapanzi.Mungathe kupeleka ziwalo zathupi lanu monga zida za chilungamo chokha.Kapena mungapeleke ku uchimo, kuzikonda, kunyada, chilakolako ndimantha. Koma <strong>Yesu</strong> amafuna ife kupeleka ziwalo za thupi lathu mongansembe tsiku lililonse ndipo tidzakhala ansembe.Ambiri amadziwa mbali iyi yoyamba ya unsembe kupeleka thupi mongansembe. Anthu ambiri saatha izi ai, koma ambiri amadziwa zimenezi kodimudzachita?Kutumukira anthu ndi kuthandiza wina ndi mnzakekukhala <strong>Yesu</strong>!Ntchito ina pambali ya unsembe mu chipangano chakale zimene anthuambiri sadziwa ndi kutumikira anthu – osati kupeleka nsembe zopsyelezakokha koma kutumikira anthu. Ansembe mu chipangano chakaleamabweletsa Mulungu kw anthu. Tsopano, mu chipangano chatsopano ifetonse ndife ansembe ngati muli otsatira wake wa <strong>Yesu</strong> ndinu wansembe.Sitingokhala ndikuona wansembe alikuchita ntchito ya Mulungu. Ndifea nsembe mukhulupilira mumtima mwanu kuti ndinu wansembe?Bweletsani Mulungu kwa anthu. Pali njira ziwiri zomwe mungabweletsereMulungu kwa anthu ina ndikuwauza anthu za <strong>Yesu</strong> kwa okhala nawopafupi. Ndife tonse ansembe, choncho timabweletsa <strong>Yesu</strong> kwa okhalanawo pafupi ndi anzathu ndi mabanja awo Amen?Wansembe amabweletsanso <strong>Yesu</strong> ku banja la Mulungu timawauza anthuena za <strong>Yesu</strong> ndi njira zake, koma pali njira imene timabweletsa <strong>Yesu</strong>kwa anthu. Lolani ndilankhula mu zodziwika ngati muli wansembemudzathandiza ena kukhala ngati <strong>Yesu</strong>. Ngati mungaone chithunzicha <strong>Yesu</strong> mu mtima wanu ndi kuona kuti ali otani, ndiye yang’ananimlongo mbale amene ali ndi inu ndikaona kusiyana kwawo ndi <strong>Yesu</strong>ngati ansembe timafafanitsa kukhala otero ndi iye. Kodi <strong>Yesu</strong> ndiozikonda? Mbale wina kapena mlongo ozikonda? Inu ndinu wansembe,athandizeni, mudzathandiza ena. Kodi <strong>Yesu</strong> amaopa? Mbale wina kapenamlongo akamaopa, athandizeni kodi <strong>Yesu</strong> amasamalila ana? Kodi anati“Bweletsani ana adze kwa ine? Ngati muona mbale, mlongo amenesakonda ana ang’ono ndi kuwasamala, ndiye thandizani kusintha ndizimene wansembe amachita. Timathandiza aliyense kukhala monga <strong>Yesu</strong>ali ngati <strong>Yesu</strong> anakakwatira anakakhala okwiya ndi ukali kwa mkazi wake?Ngati <strong>Yesu</strong> anakakhala mkazi anakakhala okwiya kapena kuzikonda kwamwamuna wake? Mudziwa mayankho ake ku mafunso amenewa <strong>Yesu</strong>odabwitsa mu zinthu zonse.Inu ndinu ansembe thandizani abale ndi alongo kukhala monga <strong>Yesu</strong>analiri. Izi ndi zopweteka, izi ndi zobvuta. Chifukwa wina adzaganizakuti muli woziyeneleza kapena oweluza chabe koma ai, inu ndinuwansembe monga wansembe monga Mulungu wakuitanilani. Sitifunakukhala wozikonda kapena woweluza chabe. Tikufuna kukhala ozama,kuzama mu chikondi mu mtima yathu kwa aliyense. Koma tiyenenlakwafunsa kusintha kuti akhale monga <strong>Yesu</strong> – chifukwa ife ndife ansembea chifumu.Aliyense waife ndi wansembe wa Mulungu. Koma ndili ndi mabvuto athuameneyonso, zilipo zinthu zimene aliyense waife sakwanitsa monga <strong>Yesu</strong>ngati ndikhulupilira kuti muli wansembe, ndiye ndiyenera kumvera kwainu kuwona zinthu pa moyo umene sulingana ndi <strong>Yesu</strong>.Ndikuitaneni inu monga wansembe kuona mu moyo ndi kuthandizaena. Tili ndi kulimbika ndi kuzichepetsa pofuna anzathu kutithandizandikulankhula ndi moyo wathu. Mpingo sikumalo amene umapita aimpingo ndi anthu pokhala ansembe pamodzi, umakhala mpingo pamenealiyense akuthandiza wina ndi mnzake tsiku ndi tsiku kukhala monga<strong>Yesu</strong>. Simuli mpingo chifukwa muli pena ndipo mukumvera. Ndinumpingo umatchedwa thupi la <strong>Kristo</strong>.Ngati sitithandiza ena kukhala monga <strong>Kristo</strong> ndiye kuti sitili kumbali yathupi lake. Tiyenera kuthandizana wina ndi mzake.Atate, woyera Ambuye Mulungu wa mphamvu, ndi pempherotonse pamodzi kuti mutsegule maso athu ndi ana onse kulikonse.Mulungu woyera, tionetseni kwa ife mmene tingakhalire ansembe.Tipempha inu pakulimbika, kuthandiza ndi nzeru zimenezingakhudze moyo wa ena. Tikupemphani mu kuzichepetsandi kulimbika polora anthu ena kulankhula ndi miyoyo yathu.12 13


Tikufunani kwambiri, tifuna kukhala mpingo wanu. Tifunansokugwetsa makomo a ndende ndi kukondana wina ndi mzake mwapamwamba. Mzimu woyera, thandizani ife. Phunzitsani ife njirazanu, thandizani ife kusintha mofulumira. Tikukondani koposa.Tipatseni ife nzeru yanu. Tidziwa kuti nyumba yanu imangidwandi nzeru, ndipo tifuna koposa. AMEN.Kuthetsa MabvutoNdipo ngati mbale wako akuchimwira iwe, pita mulangize pa nokha iwendi iye, ngati akumvera iwe, wambweza mbale wako. Koma ngati samvera,onjeza kutenga ndi iwe m’modzi kapena awiri kuti atsimikizidwe mau onsepakamwa pa mboni ziwiri kapena zitatu. Ndipo ngati iyee samvera iwo,uuze mpingo, ndipo ngati mpingo ngati iye samveranso mpingowo, akhalekwa iwe monga wakunja ndi wamsonkho. Indetu ndinena kwa inu zilizonsemukazimanga padziko lapansi zidzakhala zomangidwa kumwambandipo zili zonse mukazimasula pa dziko lapansi, zidzakhala zomasulidwakumwamba. Ndiponso ndinena kw ainu kuti ngati awiri a inu abvimerezanapansi pano chinthu chilichonse akachipempha, Atate wanga wakumwambaadzawachitira. Pakuti kumene kuli awiri kapena atatu asonkhanira m’dzinalanga ndili komweko pakati pawo. (Mateyu 18- 15-20)Anthu ambiri amene amamva vesi 20 amaganiza ndi pamene mpingowonse ukumana ndi pamene tili okondwa kuti <strong>Yesu</strong> ali pompo. Timaimbamatamando kwa <strong>Yesu</strong>, timamva bwino ndi kumva kupezeka kwakwe.Pamene zimenezi zili zoona sizimene Vesi 20 limanena ndime imeneyi.Sinena za anthu kukhala pafupi ndi kuti <strong>Yesu</strong> ali pakati pawo, komasalankhulanso za kulambira pano. Akulankhula kuthetsa mabvuto. Akutipamene tili ansembe ndikuthandiza ena monga <strong>Yesu</strong> ali pali nthawi imenetimayenera kubwela mu moyo wa aliyense. Mukaona ine kuzikondamuyenera kubwela ndi kundiuza. Pamene mlongo wina aona mlongowina akunena za wina. Mulankhuleni za zimenezi. Mjedo ndi chimo,mjedo umaswa mtima wa <strong>Yesu</strong>. Njedo ndi mwano ndi umapweteka <strong>Yesu</strong>ndiye pamene taona kuti ndi uchimo ndipo labvulaza <strong>Yesu</strong> mu thupi lake,monga wansembe ndi thupi la Kristu. Tiyenera kuthandizana.<strong>Yesu</strong> anati ngati pali utchimo muyenera kupita kwa iyeyo basi (ndime 15)sitifuna kuchititsa manyazi ena. Mu chikondi timafuna akhale monga <strong>Yesu</strong>,ngati ali wozikonda kapena a njedo sangathe kumva Mulungu. Pokhalandifuna kuti amve Mulungu, Tiyenera kuthandiza ngati ali wonyadakapena kuzikweza ndi a mwano, mdiye sangakonde Mulungu kapenaAnthu mwabwino. Choncho monga Ansembe tiyenera kupita kwa iwokuti akhale monga <strong>Yesu</strong>. Koma, tiyenera kuzichepetsa. Sitikuloza chalandi kuloza tagwira miyendo yawo ndi kuwapempha kuti apelike moyowawo kwa <strong>Yesu</strong>. Tikufuna iwo kuti akhale pa ubwenzi ndi Mulungu ndiyesangathe kutero ndi Mulungu ngati pali tchimo mu mitima yawo, ndiyeAmbuye ndi Mphunzitsi <strong>Yesu</strong> amati tipite kwa iye yekha. Musachititsemanyazi kapena kuwauza iwo akondeni. Koma pitani kwa iwo ndimuwathandize ndinu wansembe, mupite.Ngati awiri kapena atatu ndi enanso<strong>Yesu</strong> amabwelanso, pomwepo!<strong>Yesu</strong> amapeleka mayankho ku mabvuto pamene zinthu zabvuta. Pamenetapita kwa mbale kapena mlongo mu kuzichepetsa kuyesela kuzichepetsandi kunena kuti, chokani, sindifuna kumva kapena osandiweluza ine.Chotsani chitsotso mu diso lanu. <strong>Yesu</strong> amapeleka yankho pabvuto ili.Pali mbali yoti mungalakwe koma muyenerabe kupita ngati mukuganizakuti sindinu olakwa. Yesaniso ngati mukuopa kuyesa, ndiye sindinuwansembe. Simungakondweletse <strong>Yesu</strong> ngati mpaka mutayensa. Mwinamwalakwitsadi choncho ndi bwino kutero, chifukwa adzaphunzilanso paichi <strong>Yesu</strong> anati ngati mukupita kwa mbale kapena mlongo ndiye samvera,tengani awiri kapena atatu kuyesela kuthandiza. Ichi sichiphunzitsocha “makhalidwe a mu mpingo” Ichi ndi chiphunzitso cha mmenetingathandizire wina ndi mzake.Pakuti kumene kuli awiri kapena atatu asonkhana mdzina langa,ndilikomweko paka ati pawo. (Mateyu 18:20)Pamene pali awiri kapena atatu asonkhana pogwira ntchito yake, <strong>Yesu</strong>amabwera. Malembo awa sinthawi ya kulambira. Uku ndi kugwirantchito pamodzi kuthandiza ena kukhala monga <strong>Yesu</strong>. Ngati tipita kwambale kapena mlongo, ndipo sakumvera chifukwa sakumvetsa kapenakufuna izi, pamene tibweletse abale awiri kapena atatu ena tonse. Ili ndilamulo la <strong>Yesu</strong>. Sanati ngati samvera inu muiwala kapena kupemphera.14 15


Anati ngati samvera inu, tengani awiri kapena atatu alongo kapena abale,ndipo <strong>Yesu</strong> adzabweranso.Ngati tibwera mu dzina lake pochita ntchito yake. Iye adzabwera ndikuthandiza. Ananenanso kuti ngati iye samvelanso awiri kapena mbonizitatu. Ndipo uzani mpingo wonse. Kenanso, ichi “simakhalidwe a mumpingo” ichi ndi kubweletsa ansembe pamodzi kuyensa kuthetsa bvuto.Zimenezi ndi zabwino.<strong>Yesu</strong> wathu ndi wanzeru zosawelengeka. Iye ndi wauphungu wodabwitsasichoncho kodi? <strong>Yesu</strong> anati kuti ngati pali mabvuto bweletsani ansembekuyesa kuthandiza wina ndi mzake, tingabweletsenso anthu enakudzathandiza, ngati ndibwera ndikuona kuti pali tchimo mu moyo ndiposimubvomeleza, poti kapena ine ndalakwitsa – kapena sindiona zinthubwino. Pamene tibweletsa awiri kapena mbino zitatu mwina adzanenakuti ndalakwitsa. Choncho <strong>Yesu</strong> amapambana, ndi onse amakula. Izindi zopambana kuzidziwa ngati muli Ansembe. Zinthu siziyenda bwinonthawi zonse, koma tiyenela kukhala ndi kulimbika ndi chikondi. Tiyenerakumvera <strong>Yesu</strong> mu zimene anena nafe pamene zinthu sizili bwino. Ngatizinthu sizingayende bwino titenge anthu ena ndi kumvera pamodzi <strong>Yesu</strong>.Nthawi zina munthu m’modzi amakhoza mwinanso winayo ndi okhonza.Ndi nthawi zina onse ndi okhonza ndipo zimakhala kusamvetsana bwino.Mwinanso onse ndi olakwa, koma akamvela malamulo a <strong>Yesu</strong> pobweletsaawiri kapena atatu – ngati timvela kwa <strong>Yesu</strong> ndipo tisamalitsa – pamenepo<strong>Yesu</strong> adzabwera kudzathetsa mabvutowo ndi kutithandiza.Chida chodabwitsaWamkulu wa nsembe adzathandiza ansembe onse, koma tiyenerakuchita mu njira yake osati, ulesi posalankhulitsana kwa wina ndi mzake.Tisachite mantha kubweletsa ena ndi kulankhula za izi ndipo ngati winawabwera kudzalankhula nafe. Chifukwa ndimakonda <strong>Yesu</strong> ndi choonadi,ndipo ndaona kuti ndachimwa. Kuitana ena kuthandiza ndi kuonetsarakudabwitsa mu nzeru ya Mulungu. Ndidziwa kuti ngati awiri kapena atatuena abwera. <strong>Yesu</strong> amabweranso.Monga Ansembe, tiyenera kuganiza za izi ndi kuziika mu ntchito.Simasewero chabe sitikuyensa kukwanitsana wina ndi mzake pamenetikubwelera polankhulana nthawi zonse. Sikuti taikidwa ngati a polisi.Koma ndi kukondana wina ndi mzake mokwana ndi kuyensa kuthandiza.Pamene pali uchimo makutu amakhala otseka pakusamva Mulungu.Pamene pali uchimo maso amakhala osaona Mulungu ndiye mongaansembe tiyenera kuthandizana kumva Mulungu ndi kuona Mulungupothandiza kuchotsa chimo.<strong>Yesu</strong> anatipanga zida izi mu zoikira zida ngati sitingathese mabvutoamodzi ndi amodzi. Pamenepo anatipatsa ife zida zobweletsa enakuthandiza kuthetsa zobvuta. Uwu ndiye ukwati weniweni ngati akazianga ali ndi bvuto ndi ine ndipo sindikumvera, ndikudikira kuti amvera<strong>Yesu</strong> ndikubweletsa awiri kapena atatu ena. <strong>Yesu</strong>, sananene kuti zonsendi zotero koma mu ukwati ai. Iye anati zonse ndi zoona kwa anthu onseokhulupilira. Zonse ndi zoona kwa ansembe onse. Ngati akazi anga aonauchimo paine ndipo sindikumvera ayenera kutenga awiri kapena atatuena. Ndifuna iye atero, chifukwa ndikonda <strong>Yesu</strong> ndi zimene wina wa inuafuna? Izi ndi zolimbikitsa.Landilani mpeni ….. muchilitsidwe.Nthawi zonse, mpeni umapweteka, koma <strong>Yesu</strong> ndi sing’ang’a wamkuluamachotsa khasa kuti tikhale wabwino ndi mphamvu. Zimene talankhulazindi zopweteka pang’ono nthawi zina, koma mukamvera njira ya <strong>Yesu</strong> ndikuzichepesa ndi kukonda ndiye adzakupangani inu a mphamvu ndi nzerundi wopambana. Adzachilitsa nthenda zathu zonse za mu mtima ndi thupi.Adzaika chikondi chozama mu mtima ndi kukupatsani moyo mudzakhalamitsinje ya moyo yotuphuka kuchokera mwa inu ndi Mtendere zimenezidutsa kudziwa konse. Mudzakhala ndi chimwemwe chosaneneka chodzadzacha mu ulemerero. Mudzakhala ndi mphamvu ya moyo wa ngwiro, ngatimudzachita mu njira ya <strong>Yesu</strong> ndikukhala ansembe simudzakhala anthu chabe.Mudzakhala ndi kudzadza kwa mzimu woyera ndi nzeru koma muyenerakulandira mpeni podula uchimo wonse. Muyenera kukhala okonzekerampeni kudula chimo. Mukhale okondwa pothandizidwa, ngakhale pamenezipweteka uwu ndi maganizo a ophunzira wa <strong>Yesu</strong>.Aliyense angathe kukhala mu chinyumba ndi kumvetsera mau onse. Koma<strong>Yesu</strong> watiitana ife kukhala ansembe ndi mafumu. Paulo anakalipira abale16 17


akwa Akorintho pamene anati “mulikuchita ngati anthu wamba mongaadziko la anthu” koma Mulungu watiitana ife kuweluza angelo, watiitanaife kukhala odzadza ndi moyo ndi ulemerero ndi mphamvu monga mwanawake, <strong>Yesu</strong>. Koma tiyenera kulandira mpeni podula uchimo. Tiyenerakuthandizana pochita zimenezi kwa ife ndi mpingo, zimenezi ndi zeni-zenizoona Mulungu anti “Yesani, ine yesani ine muona” kumvera njira ya <strong>Yesu</strong>ndi kukhala ansembe tsiku ndi tsiku. Khalani ansembe pa okuzungulilanipelekani matupi anu monga nsembe ya moyo ndi kuthandiza ena kukhalangati <strong>Yesu</strong> ndipo Mulungu adzathira madalitso mu mtima mwanu.Bwelani MudzapelekePali mbali ina imene pokhala wansembe uyenera kuidziwa. Iyi ndiyochepa polingana ndi zina zimene talankhula kale. Muyenera kupelekanokha monga nsembe ya moyo ndi kubweletsa <strong>Yesu</strong> kwa anthu,kuwathandiza iwo kukhala monga <strong>Yesu</strong> analiri. Koma plai mbali inapokhala wansembe imene imakhudza pa msonkhano kapena pokumana.Ngati simunapeleke matupi anu monga nsembe yamoyo pokonda anthumu malo amene mukhala, ndi kuthandiza ena kukhala ofanana naye<strong>Yesu</strong> mu moyo wa tsiku ndi tsiku ndiye kuti msonkhano ulibe kanthukoma ngati mukuchita zimenezi pokhala wansembe ukunso ndi mbaliyokhala wa nsembe.Ngati <strong>Yesu</strong> adakakhala muthupi mu chipinda chino nthawi yino. Akonzakukhala phee nthawi zina koma nthawi zina <strong>Yesu</strong> amakhala ndi zofunikakulankhula. <strong>Yesu</strong> ali pompano ngati mukhulupirira kuti muli ansembechifukwa Mulungu adatero mu mwazi wa <strong>Yesu</strong> (osati mukumva motero,nzeru kapena mphamvu) ndiye muyenera kukhala wa nsembe panthawi imene woyera ali pamodzinso. Ngati <strong>Yesu</strong> akhala mwa inu ndipomunabatizidwa mwa iye mu moyo ndi mzimu wake, pameneponsomungamvenso Mulungu. Monga wansembe, mudzabwera kupeleka.Bukhu la Ahebri limalankhula za izi“Ndipo tiganizire wina ndi mzake kuti tifulumizane ku chikondano ndi ntchitozabwino osaleka kusonkhana kwanthu pamodzi monga amachita ena komatutidandaulirane, ndiko koposa monga momwe muona tsiku lilikuyanduka.”Ahebri 10:24–25.Taganizirani kufunika kwa kukondana ndi ntchito yabwino chonchomong wa nsembe ndi mabwera pakati pa abale ndi kuona menetingaperekere, ndingaperekere motaninso. Muyenera kunkhala olimbikamtima Kunene zimene <strong>Yesu</strong> afuna. Osaopa kulakwitsa ngati mwalakwitsamudzakula ndiye motero kofunika kuklhala nonse pamodzi mujsakhaleanthu osafunana khalani nonse nthawi yonse pamene muyembekezerakudza patsiku la Ambuye, Monga <strong>Yesu</strong> adza posachedwa.Osazimbaitsa, Mwamva<strong>Yesu</strong> anakwiya, anakwiya pa zinthu zochepa. <strong>Yesu</strong> anakwiya kwa onyenga.Anakwiya kw anthu amene amayelekeza kukhala njira ina pamene mumtima muli kusiyana njira. <strong>Yesu</strong> anakwiya pa zimenezo ndipo ali chonchompaka lero. Tisanyenge kuti tili otere pamene sichoncho. Pamene zoonamu moyo tili mu njira yosiyana. Tiyenera kulankhula za izi ndi abale athundi kufuna kuthetsa mabvuto poyera ndi moona. Mulungu anati “muulureuchimo kwa wina ndi mzake” kuulura ndi kupemphera kuti tichilitsidwe.Anthu ambiri ali odwala mkati muuzimu kapena mthupi chifukwasatsegula mitima yawo ndi kunena machimo awo kwa anzawo, amaopakuchita chomwechi. Koma mu nyumba ya Mulungu tisamaope ali chifukwatimakondana wina ndi mzake ndipo tifuna kuthandiza. Sitichita misechesitidzakanana. Tidzathandizana wina ndi mzake, choncho tingawuluremachimo athu mwaufulu. Tidzamva chisoni koma osaopa konse. <strong>Yesu</strong>adzathandiza ife ndikutitchuka ife koma ngati tinama kuti tilibe uchimo,ndiye tili achinyengo ndipo <strong>Yesu</strong> amakwiya. <strong>Yesu</strong> anakwiya, amakwiyangati tili achinyengo sitifuna <strong>Yesu</strong> akwiye chifukw acha ife. Timachita ife?Choncho titsegule mitima yathu.Musakwirire Luntha lanu<strong>Yesu</strong> anakwiyanso ndi munthu wina, anakwiya kwa munthu ameneanakwirira luntha lake. Ndipo <strong>Yesu</strong> anamutcha munthuyo wantchito oipa.Anamutulutsa kunja ku mdima. Chimene ndili kulankhula nanu ndi ichi,monga wansembe simuyenera kubisa luntha lanu. Mulungu anapelekakwa wina aliyense wa inu china chake chapatali pa moyo wake. Ngati muliwa nsembe, gwilitsani ntchito chimene Mulungu anakupatsani. Munthuuyu mu fanizo limene anakwirira ndalama ali wamantha.18 19


<strong>Yesu</strong> sanakondwere naye ai pokwririra luntha lake. Pamene oyera mtimaali pamodzi <strong>Yesu</strong> safuna kuti mungokhala, kumvetsera ai. Safuna kutiinu mukwirire chimene anaika mwa inu inu ndinu ansembe. Limbikani,mphamvu ndi chikhulupiriro mwa Mulungu kuti mungakwanitsekulankhula mu mphatso imene anakupatsani inu, aliyense wa inu ndipomusaope monga munthu uyu mu fanizo.Lingalirani monga mmene mungachitire ndi ena ngati muli wansembepamodzi ndi anthu ozungulira nanu ndi okhulupirira ndi thupi lanu chonchomungathe kukhala wansembe pamene abale ali pamodzi. Muyenerakufuna kubweletsa nyimbo imene ili pamtima wanu. Aphunzitseni anzanunyimbo imene mwaphunzira pamene mumapephera ndi <strong>Yesu</strong> m’mawa,kapena muzawelenga limodzi la Masalimo ndipo mudzafunsa <strong>Yesu</strong> kutiakupatseni mang’ombe abwino pa nyimboyo. Ndiye monga wa nsembebwelani ndi kubweletsa woyera mtima pamodzi, ndi kuphunzitsa nyimboimene <strong>Yesu</strong> wapeleka kwa inu. Ndiye wa nsembe muyenera kutero ngatiwansembe musakwirire luntha lanu.Mwina mbale adzabwera nalankhula za uchimo mu moyo wanu.Mumveleni iye ndipo zibweletsa misonzi mu maso mwanu. Monganthawi imene Natani adalankhula kwa Devedi ndipo Devedi anaswekamtima, Mulungu anatuma Natani – mbale kwa inu ndipo adzanenazauchimo ndipo uzaswa mtima wanu. Mudzalankhula ndi <strong>Yesu</strong> paizindipo ndi kulingalira malembo ena pa izi. Kenaka mudzabweletsa abalepamodzi pa malo amodzi ndi kuwauza m’mene <strong>Yesu</strong> waphunzitsira inu.Auzeni malemba amene mwawaphunzira amene asintha moyo wanu.Auzeni m’mene munagwera ndi m’mene iwo sangagwelenso. Awonetsenizinthu zimene Mulungu waonetsa kwa inu. Ameneyo ndiye wansembe.Inu ndinu ansembe mungatenge zinthu zimene Mulungu wachita mwainu ndi kutsegula kwa abale ndi alongo. Mulungu akufuna kuti tidziterotonse amene. Muli wolora kutero?Choncho tabwera pamodzi mudzina la <strong>Yesu</strong> ndikumvetsera. Koma<strong>Yesu</strong> sakhala chete kwa nthawi ngati zinthu zili chete kwa nthawi yaitalichifukwa ndi choti wina siwansembe wabwino, kapena ndikumvetsera.Koma <strong>Yesu</strong> sakhala chete kwa nthawi ngati zinthu zili chete kwa nthawiyaitali chifukwa ndi choti wina siwansembe wabwino, kapena <strong>Yesu</strong> afunakuti inu mugawe nyimbo ndipo mukuopa. Kapenanso <strong>Yesu</strong> akufunakuwelenga malembo amene anali apamtima wanga m’mawa uno, komandimaganiza Ai, sindili wabwino konse sindingathe kutero. Kenakazii, chifukwa <strong>Yesu</strong> amafuna kugwiritsa ntchito ine koma sindinamulorendifuna kuti ndikwilire luntha langa ngati <strong>Yesu</strong> anakakhala pano mu thupi,sanakakhala chete kwa nthawi yaitali chifukwa pali zambiri zimene <strong>Yesu</strong>amafuna kuti zichitike m’moyo mwathu. Ngati ife tili ansembeabwino,tidzamvera <strong>Yesu</strong>. <strong>Yesu</strong> adzagwiritsa ntchito aliyense wa ife. Adzakhalamwa ife kubyalera mw ansembe ake, ngati tili ofuna, muli ofuna kutero?Landilani <strong>Yesu</strong> agwiritse inu ntchito.Akufuna kuchita zodabwitsaKumbukirani kuti <strong>Yesu</strong> pamene anapita ku malo ena anafuna kuchitamirakulu kumeneko, koma sanachite chifukwa anthu anali osakhulupira.Muyenera inu kukhulupira mu mtima mwanu kuti Mulungu afunakukugwiritsirani ntchito. Muyenera kulankhula ndi <strong>Yesu</strong> pa zinthu izi.Muuzeni iye:Ndimakhulupilira ndithandizeni “kusakhulupirira” funsaniiye kuti mukhale ofewa ndi ozichepesa. Funsani <strong>Yesu</strong> kuti akuthandizenikuti mulimbike kuona mphatso yanu, funsani <strong>Yesu</strong> kuchotsa kunyada,chifukwa nthawi zina mudzakhala olakwa. Koma ndizabwino kulakwandipo tonse tingathandizane. Ndibwino kulakwa kusiyana ndi kukwiritaluso lanu. Ngati mwalakwatsa tikhonza kukhala tonse pamodzi, komangati mungakwirire luso lanu. <strong>Yesu</strong> ali okwiya, ndiye funsani <strong>Yesu</strong> kutiakuthandizeni inu kuti mukhale wansembe wabwino.Izi sizofunika kuganiza mozama kapena kulankhura bwino. Izi ndikufunsa <strong>Yesu</strong> kuti athandize inu. Iye ndi wamoyo, akufuna kugwirantchito yodabwitsa mu mitima kuphyola mu mitima ya ena. Koma kwaiye kuti achite mirakuli, tiyenera kukhulupilira, ndiye lankhulani ndi <strong>Yesu</strong>za zimenezi. Mwangoganiza chabe mu mutu wanu ndi kubvomeleza izochabe. Malomwake, lankhulani ndi <strong>Yesu</strong> wa moyo pa zinthu izi ndipoadzatithandiza ife tonse, ku ulemerero wake.Afunseni kuti akhale AnsembePamene muli ansembe kwa abale anu mungathenso kuwathandizakuphunzira kudziwa <strong>Yesu</strong> ngati ali kumbali ya chipembedzo kwina kake,20 21


apempheni kuti akhale ansembe kumene akhalako, Apempheni kugwilitsamphatso kwa anthu amene azungulira. Asangopita ku misonkhano kwawokukamvera chabe. Funsani iwo kuti ayang’ane kuti ayang’anire miyoyoya zongulira iwo ndikuwathandiza kuti akhale monga <strong>Yesu</strong>. Ngati winakulikonse achita izi. dziko lizasintha. Zimenezi ndi zamphamvu – chifukwandalora kuti <strong>Yesu</strong> akhale <strong>Yesu</strong>. Ngati sindingathe ansembe <strong>Yesu</strong> amakhalamu botolo kapena mu Bukhu, ngati tili ansembe ndi kufunsa wina aliyenseamene abvala <strong>Yesu</strong> kukhala wa nsembe. <strong>Yesu</strong> adzaloledwa kuti akhale <strong>Yesu</strong>PALIPONSE! Midzi yathu idzasintha mizinda yathu idzasintha. Maikondi maiko akulu onse adzasinthika ndipo <strong>Yesu</strong> adzakhala <strong>Yesu</strong> ngatindidzakhala ansembe! Amen?Pamene tinadziwa <strong>Yesu</strong> zaka khumi zapitazo, taphunzira mopitilira mmenempingo uli ndi wansembe alili, ndi mmene tingakhalire wansembe.Pamene taphunzira zinthu izi zinatitengera ife kumachitidwe odziwakuchita ndi chipembedzo. Anthu a chipembedzo si adani athu. Ambiriali kumeneko chifukwa ndi zimene iwo adazidziwa. Ngati atidziwa <strong>Yesu</strong>kwambiri adzakondwa kumutsata. Ndiye ndi chofunika kuti tikonde anthungakhale a muchipembedzo. Ife tili osamalitsa kuti tisanyade. PameneMulungu akupatsa ife opempha monga ife chakudya cha nyenyekwa.Tiyenera kugawa chakudya ndipo osaweluza ena pokhala alibe chakudya.Iyi ndi njira ya <strong>Yesu</strong> kugawa chakudya chimene wapeleka kw aife – osatitigawikane chifukwa cha chakudya, koma kupeleka chakudya.Zinthu izi ndi zofunika kwambiri kukhala mu mitima ndi mmaganizo.Sitidzalora kutentha chabe kapena kunyengalera. Koma timakhulupirirra<strong>Yesu</strong> adzamanga mpingo wake, ndiye pamene tipeza anthu amene akonda<strong>Yesu</strong> mu zipemphedzo, kapena tisati chaokani, chokani mmalo mwake“mvelani <strong>Yesu</strong> ndi anthu amene muwadziwa “Timawaphunzitsa njira ya<strong>Yesu</strong> monga mmene anatiphunzitsira ife. Timawafunsa kuti aphunzitsealiyense amene amudziwa njira ya <strong>Yesu</strong>. Ngati achita motere mu mipingoadzathamangitsidwa mu chipembedzo anthu ambiri samvera Mulunguena amamvera, komanso ena ai.Mu mpingo woona umene <strong>Yesu</strong> akumanga, ALIYENSE amafunakumvera Mulungu ndipo ALIYENSE amakonda <strong>Yesu</strong>. Chifukwa tonsetili ansembe ndipo timathandizana wina ndi mzake ngati wina sakonda<strong>Yesu</strong> amathawa.Mu uneneri mu Yeremiya 31 wa mpingo wa chipangano chatsopanondi oti, “onse adzandidziwa ine kuyambira aong’ono mpakana akulu” mumpingo woona onse amadziwa <strong>Yesu</strong>. Mu chipembedzo chimene sichoonandi mmene muli kutentha chabe.Anthu amakonda dziko ndipo amakhala mu uchimo ndipo sasintha. Ndizoipa izi ndi zobvuta kwambiri. Koma plainso anthu abwino mu chipembetso. ntchito yathu sikuti anthu achokeko. Ntchito yathu ndi kuthandiza iwokukhala ansembe kumalo amene iwo ali. Ngati adzakhala ansembe pamaloamene ali anthu ambiri adzasintha kapena atachotsedwa.Pamene <strong>Yesu</strong> ali ---------- chimo silingakhaleNgati mbale kapena mlongo afana ndi <strong>Yesu</strong> ku chipembedzo, kapenachipembedzocho chidzasintha, kapena chidzawapha kapena kuwataya(monga momwe adachitira ndi <strong>Yesu</strong>) sitikuopa zipembedzo. Ali ngatikhoka lalikulu limene lisunga nsomba zosiyana siyana. Pali nsombazina za bwino mu khoka ndipo zina nsomba zoipa. Ntchito yathu ngatiansembe ndi kuitana nsomba zonse zabwino kuti zikhale ansembekumene iwo akhalako.Kodi Neneveh anasintha? Yona analabvulidwa ku kamwa kw ansombanalowa mu mzinda oipa uja. Uchimo umalipo kumeneko koma mzindaonse anasintha kwa Mulungu ngakhale mfumu. Tiyenera kukhulupiriraMulungu kuti angapange mu chipembedzo. Tikhulupilire kuti angachiteizi ku Mzuzu, ndiye ngati tili ndi abwezi kapena anthu amene timadziwamu chipembedzo, sitimauza kuti achoke, timawauza kuti akhale ngati <strong>Yesu</strong>ndi mtima wawo yonse kulankhula mau a Mulungu kwa aliyense ameneamuone kumeneko, kutaya moyo wawo, kukonda anthu osanyengelerakapena kuopa kunyengeledwa. Anthu a ku Neneve nasintha ndimoyo wathu ku chipembedzo kumene tikhale ansembe ndi kuyesakusintha. Tidzayensa kuthandiza anthu abwino amene timawadziwa kuchipembedzo ndi kuwafunsa kuti akhale ansembe kume ali kuthandizaanthu owazungulira kusintha.22 23


Timupempha Mulungu ndi misonzi yambiri kuti chipembedzo chisinthe<strong>Yesu</strong> analira. Anathets amisonzi ndi Yerusalemu. Anati ndinakakusunga iwemonga mmene nkhuku imasungira anapiye ake. Koma Yerusalemu sanafunendipo anamkana iye – Anamupha. Ngati tili ansembe okhulupilika,adzatipha kapena mzinda wonse udzasintha. Koma tiyenera kukhalaansembe okhulupilika. Tiyenera kufunsa ansembe amene timawadziwakuti akhale okhulupirika ku malo amene akhala. Ngati adzayese kuthandizaanthu amene amawadziwa, adzakhala olimba kapena kuchotsedwa komandiye kuti akhonza kukhala ndi okhulupirira ena amene ali ndi moyoumodzi, titayensa ndi anthu otizungulira ife. Ndizimene wansembeamachita. Tiyenera kukonda amene ali mu chipembedzo. Ndi zimene <strong>Yesu</strong>anachita. Koma tisalore kunyengedwa. Tiyenera kukhala mu choonadindi kufuna mu choonadicho. Ngati aliyense adzatero, pamenepo <strong>Yesu</strong>adzamanga mpingo wake.Uwu ndi uthenga wabwino wa <strong>Yesu</strong>. Tiyenera kukhala njira yotere kwaanthu okhala nawo. Osanyengelera osakhala ozizira---- koma tiyenerakuwakonda ndi kuthandiza iwo. Pasakhale kusiyana kukhale chifukwawina safuna kumvera <strong>Yesu</strong>. Sitidziwa izi mpaka titayesa. Umu ndi mmenetingakhalire ndi chipembedzo. Tiyenera kutaya moyo wathu kwa iwo ndikuchita chilichonse chimene tingapeleke mkate wa moyo ndi kufunsaiwo kuchita ndi anthu amene amawadziwa ndiye tiona ndi kuyang’anirachimene <strong>Yesu</strong>achite ndi chimenecho. <strong>Yesu</strong> anati ngati tidzachita mbaliyathu. Iye adzamanga mpingo wake ndi makomo a ndende ya mtimasidzaima. Tikhononga mzinda wa Satana kuphwasula ndi kuwonongamakomo onse. Timakonda anthu ndi kuwabweletsa kuchokera ku Mtimandi ku kuwala. Sitikusiyana pa maina koma tikonda anthu – mphakaku imfa. Timachita ntchito yawa nsembe ndipo Ambuye adzamangampingo wake.<strong>Yesu</strong> Yekha Ndiye BwanaMlowe, Africa 1996Chimene chipanga Mtsogoleri?Pali mitundu iwiri ya atsogoleri, wina ndi mtsogoleri ochokera mu mtima,kuchokera mu mulumikizo ndi Mulungu wina ndi mtsogoleri wa undindondi mpando ndi olemekezeka “wamkulu” Bwana olemekezeka, <strong>Yesu</strong> anatimtsogoleri utero asakhalepo. Atsogoleri a mpingo ndi amene akuyendandi pafupi ndi Mulungu LERO ngati mbale kapena mlongo sakuyendapafupi ndi Mulungu lero, sayenera kuganiziridwa kukhala mtsogoleri.Ngati munthu sabata yatha samayenda ndi Mulungu koma walapa pamachimo a mu moyo ndipo akumva Mulungu, ndipo ali mtsogoleri lerokoposa sabata yatha. Kukhala mtsogoleri zimachokera ubale ndi Mulungundi anthu a Mulungu sizichokera pa ofesi kapena undindo. 1Tili ndi atsogoleri kumene ine ndimakhala, koma kulibe “maofesara”mtsogoleri lero koma sabata in ai. <strong>Yesu</strong> anati ulamuliro yonsem’mwamba ndi pansi pano uli PAINE. Zimenezi ndi zoona, choncho,m’mene tingamvere <strong>Yesu</strong>, amene ali ndi, amene ali ndi ulamuliro. Ndim’menenso ali ndi ulamuliro nawo – pamene akwanitsa kumva <strong>Yesu</strong>, ndichoncho. Ulamuliro wonse “kumwamba ndi pansi pano” uli pa <strong>Yesu</strong>. Iyeanati munthu amene sadziwa <strong>Yesu</strong> angakhale ngati choyelekeza chabe.Munthu ameneyu amafuna adziopedwa pamene afuna zitero, ngati alindi mpando koma ali mtsogoleri ngati amadziwa, kukonda, ndi kumveramutu <strong>Yesu</strong>.Kubadwa kuchokera mu UlesiPali mayambidwe ochokera mu ulesi mwa ife zimene zimapangitsa ifekubisala pansi pa nthaka ndi kulora wina atimenyere nkhondo ndi zimeneakulu ndi opanda undindo zinayambira. Poyambilira pomwe mu mbiri yampingo kumbuyo ndithu zaka zikwi ziwiri zapitazo zaka 1800 zapitazoanthu anayamba kufuna mfumu kuti adzawalamulira. Anafuna kuti“munthu oyera” akhala mtsogoleri wa mpingo.24 25


Mwina munthuyo analidi pafupi ndi Mulungu koma mmalo mufunakuti aliyense akhale wansembe. Anthu a Mulungu anafuna kukhala ndimunthu mmodzi woyera kuti adzimenyera nkhondo. Anafuna kutengamunthu mmodzi ndi kumuika kukhala “mfumu wa mpingo”Munthuyo mwina anali wabwino. Bvuto siloti munthuyu anali pa ubwenzindi Mulungu. Mwina munthuyu anali ndi mphamvu ndi mphatso, komapamene ayikidwa padela monga ya padera ndikutchedwa “bwana wampingo” Pamanepo pali bvuto malo amenewo ndi a <strong>Yesu</strong> yekha <strong>Yesu</strong> ndibwana wa mpingo woona. “Abusa sayenera kukhala bwana wa mpingopalibe mabwana koma <strong>Yesu</strong>.Pali chitsanzo m’Baibulo cha mautsogoleri awiri amenewa. Samuelindi Sauli onse adali atsogoleri a anthu a Mulungu, Israeli. Samueliadali munthu wa Mulungu amene adali ndi chikoka mu fuko chifukwaamadziwa Mulungu. Samueli adali ndi zothekera zambiri zaufumu kuIsraeli—koma Samueli sadali mfumu! Komabe, Sauli adatchedwa mfumu.Israeli imafuna kukhala ndi mfumu—amafuna kukhala ndi munthumodzi kukhala bwana. Amafuna wina kuti alowe mmalo mwa Samuelindipo amafuna “mfumu” monga mafuko onse owazungulira. Munjiraina utsogoleriwu ukhonza kuwoneka mofanafana, koma Samueli alibe“mpando” wa ulamuliro. Samueli amagwira ntchito kuchokera paubalewake ndi Mulungu, ndipo Sauli amagwira ntchito kuchokera pampandowake. Samueli adalibe ofesi, mlembi kapena malipiro (salare). Iye sadalimuudindo wa mpando ngati mfumu. Samueli adali chabe munthu waMulungu amene amalemekezedwa ngati mfumu koma adalibe mpandokapena ofesi. Iye sadali mfumu iye sadali “mbusa”. Iye amangokondaMulungu ndi mtima wake onse.Ndipo chifukwa choti amamvera Mulungu, adali ndi chikoka. Adalibempando adali ndi chikoka. Ngati munthu moonadi adziwa Mulungu,adzathandiza anthu a Mulungu. Ngati wayitanidwa ndi Mulungu,adzakhala akuthandizila anthu. Ndibwerezanso: Munthu wa Mulunguoona alibe mpando… ali ndi chikoka. Yobtu 29, ikulongosola za munthuolemekezedwa ndi Mulungu ndi anthu, ndi woopedwa ndi odedwa ndisatana. Munthu otere safuna ofesi kapena dzina kapena malipiro. Ngatimuli ngati <strong>Yesu</strong>, simudzafuna “mphamvu.”Monga mwachitsanzo, ngati ndili m’misili, ndi mapanga zinthu ndi matabwa.Ndimapanga mpando, tebulo kapena chitseko kuchokera ku matabwa.Ngati ndili omanga, ndiye kuti ndimanga zinthu ndi njerwa. Chinachakechomwe ndipanga kuchokera ku njerwa ndi umboni oti ndine omanga.China chake dzomwe ndipanga kuchokera kuthabwa ndi umboni oti ndinem’misili. Tsopano, mu Baibulo mau awa “mbusa” (kutathauza kolakwika)koma atanthauzira kuti mphatso ya ubusa wa nkhosa, ogwira ntchito tsikundi tsiku pakati pa anthu a Mulungu moyendezana (mwapambali) pamphatso zina—osati bwana kapena “olankhula wamkulu” pamsonkhano.Kodi umboni uli pati kuti ndine Mbusa weniweni? Umboni ndi wakuti inendimakonda anthu a Mulungu! Ndimawathandiza iwo usana ndi utsiku.Sindifuna dzina, sindifuna kukhala bwana. Ndimangokonda anthu ndimphatso yomwe ndili nayoyi, ndikuwathandiza. Umboni waumusili ndimpando omwe ndapanga umboni woti ndine Mbusa weniweni ndi wotindimadyetsa anthu a Mulungu tsiku ndi tsiku, ndipo ali chifupi ndi <strong>Yesu</strong>chifukwa cha ine. Ngati ndiwona kuti m’modzi mwa anthu a Mulungu alindi njala, chimandiswa mtima. Ngati ndiwona kuti m’modzi mwa anthua Mulungu ali muvuto kapena muzoopsa, mtima waubusa mkati mwangauthamangira iwo kukawateteza. Uwu ndiye umboni oti ndine odzodzedwawa Mulungu kukhala m’busa. Sindifuna mayina opatsidwa. Sindifunachitupa chopachika pakhomo ndi chochokera ku Sukulu ya Baibulo.Ndifunitsa mtima okonda ndi kuchita ntchito ya Mulungu, ndipo kenakondizabala zipatso zauzimu mumbali iliyonse yomwe iye azandipatsa ine.Tsono, ndinu m’misili? Ndiye pangani mpando. Muli ndi mphatso yaubusa. Ndiye kondani anthu—adyetseni, atetezeni ndipo athandizeni.Ichi ndi choona pa mphatso iliyonse! Umboni wa mphatso iliyonse ulimudzipatso zimene umabereka.Zotsutsana za zonsezi ndi zoonanso ndithu. Ndifundo yodabwitsa kutiamafano mu sayansi ndi mankhwala ndi malonda amalamula kuti ameneali ndi maganizo ndi mtsutso ndi odzitcha okha “akatswiri” ali ndi chinachoti awonetse, zipatso mumiyoyo yawo, awonekera kuti ali dni ufuluwolamulira, kuphunzitsa kapena kutsutsa ena. Mudziko lachipembedzo,modabwitsa, ali ndi ungiro ochepa kuposa ngakhale zimene amafanoamaonetsera. Muchipembedzo, ngakhale, anthu ali akhungu ndiwozunguzidwa kwambiri.26 27


Mtsutso, ukatswiri, zigamulo, ndi ngakhale ubale ndi zonyoza zimayendamophweka kuchokera kwa iwo azipatso zoyipa miyoyo yawo, m’mabanjandi m’mabwalo awo. Zodabwitsa, koma zoona ngati inu muonachipembedzo chamunthu mosamalitsa ndi moona. Munthu ameneamapanga zinthu zotere ngati bodza kapena m’nyozo kapena kukhalangati katswiri pa njiniaring’I, zamakhwala kapena malonda akhonzakusonkhanitsa pamodzi gulu lomvera mpphweka anthu akuopa, m’meneakhonza kunderedwa pansi, kapena kuyamikiridwa mpusitsa ku—kuzipereka ku makina osabereka zipatso ndi “akatswiri” zonga zamisalakoma ndi zoona. Zimachitika kunthawi zonse, chifukwa umu ndi m’menemaufumu a vuto amasungira nambala yao. Mantha ndi kuyimikirakopusitsa, mjedo, m’nyozo kapena kuyenderedwa pansi. Nchifukwachake ziri zosadabwitsa kuti <strong>Yesu</strong> sanapange bwino mu chipembedzochovomerezedwa kudziko lapansi cha munthawi yake. Koma, likhonzakuphunzira kwa iye ndi kusunga malembo, ndi kuyang’ana zipatso, osatikumvera—kunena kwa mfundo ndi mabanjeti, ndiponso kunena kufunakwa yenkha kwa munthu kuti ateteze.Pamenepo mwatengapo mfundo.:)“Mwandikana ine”!Izi ndi zoona kwa mphatso iliyonse koma anthu aononga kwambiri chi<strong>Kristo</strong> pofuna kukhala ndi mfumu Samuel sanali mfumu, anali munthuwa Mulungu. Sauli anali mfumu ndipo anaononga anthu a Mulungu.Mulungu anati “sanakukane iwe, Samuel, Akana Mulungu. Samueli analiwa chikoka chifukwa amadziwa Mulungu, sichifukwa choti anali paudindo wa Ufumu.Ndipo iwo anatengera, sanatengere? Wina wochokera dziko lina amanenaakafika ku Israel, muli ndi mfumu! ‘Samueli ndi mfumu yanu”! A Israelamati “inde” tikudziwa akuoneka ngati mfumu, chifukwa ali otamandikandi opatsidwa ulemu koma Sali mfumu. Tilibe mfumu ife, tilibe mfumukoma Mulungu. Samueli amadziwa Mulungu bwino, ndiye tikupatsaulemu ndi kumukonda. Maiko ena maganiza kuti a Israel anali ndi mfumu,mfumu Samueli koma sanali mfumu anali munthu wa Mulungu. Analibempando. Mapita pano ndi uko kenako osaonekanso, ndi kubwelanso.Mafumu sapangaz zimenezo. Amuna a Mulungu amatero. A Israeli anafunakuika wina mmalo mwa Samuel pamene anakalamba anafuna kukhala ndiMfumu monga maiko ena onse (kapena monga zipembedo zina).Pamene tifuna munthu wina kukhala bwana wa ife kuti atimenyerenkhondo, ndiye takana Mulungu 1 Samueli 18:7 “sanakane iwe, Samueli,andikana ine” tisayese kukhala ndi anthu okhala bwana. Tiyenerakuwakonda ma Samuel pakati pathu amene adziwa Mulungu, talemekezendi kuwamvera, pamene sakukhala ndi udindo kapena bwana kupatula<strong>Yesu</strong> yekha basi, timvere <strong>Yesu</strong>, kulankhula mwa Samueli, Lolani Samueliwoyamba akhale pansi. Izi ndi zabwino.Zotsatira zakeNdikufuna kuti mumve zimene inu ngati mukhala ndi mfumu. Pamenemufuna kukhala ndi “Bwana wanu” Bwana wa mpingo. Izi ndi chipatsozochokera mwa izo“Nati, Awa ndi makhalidwe a mfumu imene idzaweluza idzatenga ana anu amuna,akhale akusunga magaleta ndi akavalo ake ndipo adzathamanga ndi kutsogoleramagaleta ake adzawaika akhale atsogoleri zikwi ndi atsogoleri makumi asanundipo adzaika ena ndi kulima minda ndi kutema zinthu zake ndi kumpangirazipangizo za nkhondo, ndi zipangizo za magareta ndipo adzatenga ana anuakanzi apange zonunkhira naphikire naumbe mikate ndipo adzalanda mindayanu ndi minda ya mphesa yanu ndi minda ya azitona inde minda yoposayo,nadzaipatsa anyamata ake ndipo adzatenga limodzi la mayawo khumi la mbeuzanu ndi minda yanu ya mphesa nazaipatsa akapitawo ake ndi anyamata ake.Ndipo adzatenga akaporo, ndi azakazi anu ndi anyamata anu okongola koposandi abale anu nidzagwiritsa ntchito zake. Idzatenga limodzi la magawo khumila zoweta zanu ndipo inu mudzakhala akaporo ake, ndipo tsiku lija mudzafuulachifukwa cha mfumu yanu munadzisankhira nokha, koma Yehova sadzayankhainu tsiku lijalo. Koma anthu anakana kumvera mau a Samueli nati Iai, komatikufuna kukhala nayo mfumu yathu kuti ifenso tikafanane nao anthu a mitunduyonse kuti mfumu yathuyo ikatiweluzire ndi kutuluka kutitsogolera ndi kuponyanafe nkhondo zathu. (1 Samueli 8:11 –20)Pamene tifuna mfumu atilamulire, pamene tifuna olemekezeka bwanamu mpingo, iye adzaba masomphenya adzaba ana athu ndi ndalama28 29


zathu ndipo tidzakhala ife otigwilitsa ntchito chabe. Zinthu izi sizabwinokoma zikuchitika mu dziko lonse la chipembedzo. Kumaiko ena onseamene tapitako pamene pali bwana ndi munthu wamba, pamene palianthu osiyana akristo. Bwana ndi munthu wamba – mitima ya anthundi mphatso sizimagwira ntchito. Mphatso ya chifundo ndi mphatso yakuthandiza imachotsedwa pamene munthu mmodzi ali mtsogoleri otereosati <strong>Yesu</strong> kukhala bwana, mitima ya anthu imabedwa.Anthu a Mulungu anali opeza bwino mu ulamuliro wa Samuel iye sanalindi udindo, anali ndi mphatso zinali ngati zophweka kusintha kuchoka kwaSamueli kupita kwa Sauli chifukwa amaoneka ngati onse ndi mfumu. Komaina inali mphatso ndi ina udindo, pamene pali mphatso, Anthu a Mulunguamalemera. Pamene pali udindo olamulira anthu, anthu a Mulunguamabvutika, molingana ndi mau a Mulungu. Mulungu angagwiritsidwentchito pa zabwino zokha. Devedi anali mfumu yabwino. Zinthu zinazabwino zingaoneke ngakhale kuti njira ndi yoipa. Koma Mulungu anati“Ndili nayo njira yabwino” njirawo ndi Samueli, osati Sauli, iye anati,Ndingachite zinthu zina zabwino ngati mukhala ndi mfumu, koma pamenemabvuto abwera mudzalira kwa ine ndipo ine sindidzayankha” Izi ndizimene zikuchitika mu chipembedzo, chifukwa amamanga pa mphatsoya munthu kukhala mfumu. Sauli ndipo analoledwa kumuika kukhalamfumu.Zinthu zina zabwino zikhonza kuchitika koma mu tsiku la zowawaadzalira kwa Mulungu ndipo sadzamvera iwo, ndipo zinthu zidzataikilana.Padzakhala ndale ndi mphamvu kuchitidwa ndipo padzakhala misechendi zamwano ndipo matemberero onse adzakhala amene Mulunguanawanena. Pamene Mulungu angathe kuchita zinthu zambiri mu zochitazilizonse. Timafuna zabwino zokha. Sizabwino zimenezi? Mulunguangadalitse chilichonse mu chifundo chabe kukoma mtima ndi kupilira.Koma tiyeni timange kuti tilandire madalitso ambiri! Tikhale ndi maSamueli pakati pathu mmalo mwa Sauli m’modzi. AMEN?Chinanso chimene chachitika ndi choti munthu kupita ku seminarekukatenga chizindikiro cha chipemphetso, angakhale kuti mtimaungakhale wabwino amakakamizidwa ndi udindo kukhala zimene iyesaali. Angakhale ndi mabvuto nyumba mwake, ndi ukwati ndi ana ake ndiogona nawo limodzi ndi makolo mwachoncho, chifukwa ali ndi udindowa chipembedzo anthu amayankhana kwa iye, mmalo mokhala mbalepakati pa abale. Amachita zinthu zina munjira ina kusiyana ndi mmeneamachitira kunyumba, monga kuyenera kukhala mbale pakati pa abale.Pali zina zimene zili mkato mwa ife zimene zimapangitsa ife kusafunsamoyo wa Bwana. Pamenepo atsogoleri mu mpingo asafune maudindozimene zingaimitse zinthu zothandiza ena mu moyo wawo.1. Mau oti ofesi amathandauza ngati ndi olemekezeka” okhalapo chilichosechokhalapo pa anthu a Mulungu kaya mu nyumba kapena munthu odziwika.30 31


Devedi Living’isitoni Ndi MkateOchokera KumwambaChilembe, Africa 1996Mkate wa MoyoMbale analankhula za Devedi Livingstoni kubweletsa mkate ku Afrika.Devedi anabweletsa ku afrika chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> mwana wa Mulungu.Anabweletsa uthenga mmene <strong>Yesu</strong> amakondera anthu, amafunirakukhulukira machimo athu onse ndi kubweletsa moyo wa tsopano.Tikudziwa kuti uwu ndi uthenga wabwino kwa ife. Devedi anabweletsamkate m’mbale ndi chobvundikira, ndipo ndamva mmene mkatewounali kukoma.Timabwera tonse la Mulungu ndi kulankhula za mmene mkate unaliri ndichiphunzitso choona. Mkate ndi wabwino ndithu mbali ya uthenga umeneMulungu watiitanilako ife sikungophunzitsa mmene mkate, koma zimeneBaibulo amati “mafungulo a mu ufumu” ziphunzitso za <strong>Yesu</strong> mmenetingatsegulire khomo ndi ziphunzitso mmene tingachotsere chovindikirandi kutilora ife kudya mkate umenewu.<strong>Yesu</strong> sanangatikhululukira machimo monga zodabwitsa monga zilirikapena kuti tiganize za chiphunzitso chake. <strong>Yesu</strong> anabwera kuti ife tikhalendi moyo umene iye anakhalira ndi Atate – osati kudzakhala chabe, kufandi kupita kumwamba. Monga Baibulo linena. Anabwera kuno kuti tikhalemu “mphamvu ya moyo wagwiro” kukhala mu chiyanjano ndi moyo ndichikondi pamodzi ndi atate ndi abale amene <strong>Yesu</strong> anachita.<strong>Yesu</strong> amafuna ife kukhala kuthyola ziphunzitso za mkate mu mphaka,akufuna ife tidye mkate umene iye anadya ndi Atate ake.Mkate UmodziZambiri zimene chipembedzo ndi chikristo chachita kwa zaka zambirindikutiphunzitsa mozama za mkate. Ndi nthawi yoti tidye mkate ndi33


nthawi tsopano tichoke kuchokera kuphunzira ziphunzitso za mpingondi kukhala mpingo (Aefeso 3:10, Mateyu 16:18) <strong>Yesu</strong> sanabwere kutitikhala ongooneka bwino. Anabwela kudzatipatsa ife moyo ochuluka –tikhale mu moyo wake tsiku lililonse wina ndi mnzake, osati kulankhulamau wake obweleka ndi kuyimba ndi kupemphera mau a chipembedzo.Anabwera kudzatipasa MOYO! “Ana ang’ono, kondani ndi mzake” uwuunali chiphunzitso cha Mulungu mutu ndi <strong>Yesu</strong> NDI Yohane ndi Paulondi Petro.Timaphunzitsa za banja la Mulungu, osati chipembedzo chokaonera.Kodi ife timaonera zochitika m’banja lathu? Kapena tikhala mchikondindi mabanja tsiku lonse? Simungaonelere banja mukhonza kukhala banja.Baibulo limalankhula bwino za izi. simungaonelere chipembedzo choona,mukhonza kukhala mpingo woona. Banja limene mungaonere ndi losungaana amasiye osati banja lowona. Kusunga ana amasiye kumakhala bwanawake ndipo amasonkhana onse kudzadya chakudya. Mwina amapita ndikusewera pamodzi ndi kulandira chiphunzitso kuchokera kwa mabwanaawo. Choncho limachita zambiri zimene banja limachita, koma ndi anaamasiye osati banja. Mulungu waitana ife kukhala banja tsopano ngatisimuli banja, padzakhala kusintha kumene kudzakhala popeza <strong>Yesu</strong>.Pofuna kudziwa <strong>Yesu</strong> ndi kudya mkate, tiyenera kukhala mkate ndipongati tingakhale banja la <strong>Yesu</strong>, tiyenera kuthandizana zedi. Sitiyenerakukhala wozikonda. Tiyenera kusiya kunyada ndi kufuna kutsegula kwaanzathu za <strong>Yesu</strong> kusintha moyo wathu.Tiyenera kukhala okhulupirika wina ndi mzake zamene tikumvera.Sitiyenera kubisa kumbuyo ka nkhope kapna chophimba koma tiyenerakutsegula miyoyo yathu ndi kulankhura pa zimene tikumva, pa izi ndipamene <strong>Yesu</strong> adzathandiza <strong>Yesu</strong> anakwiya ndi chinyengo. Chifukwa chakesikuti anada anthu. <strong>Yesu</strong> amadziwa kuti ngati pali kunamizira kukhalanjira ina pamene mu miyoyo ndi munjira ina sangathe kuchilitsa ife mkatimonga m’mene ankafunira.<strong>Yesu</strong> anamutcha satana ndi tate wa mabodza. <strong>Yesu</strong> ali okwiya ndi chinyengondipo Sali okondwa ndi ife. Izi ndi mbali ya banja – pokhala okhulupirikandi wina ndi mzake. Pazimene tikumva ndi mmene tikuchitira. Komamuyenera kuzipereka, kwa wina ndi mzake kuchokera mkati, sindingakhaleodandaula kapena yopambana. Ndikufuna kukhulupirira Mulungu kutiangathandize ine. Koma ndi sangozinyenga kuti angandithandize ine.Koma ndi sangozinyenga kuti zonse zili bwino pamene sizili motere.Ndiyenera kuzichepesa kupeza abale abwino ndi azilongo kulankhulapa zinthu izi chifukwa pamene awiri kapena atatu ali pamodzi <strong>Yesu</strong>amabwera kudzakhala nafe, choncho ngati ndili ofuna kutsegula pang’onomtima wanga, udidzalora Mzimu Woyera kubwera ndikuchiritsa ndipo<strong>Yesu</strong> adzakondwa. Ngati ndimanga makoma pozungulira ine ndekhandi kufuna kukhala wamphamvu ine ndekha, pamenepo mphamvu yamachiritso ya <strong>Yesu</strong> sidzafika.<strong>Yesu</strong> akufuna kukhala banja limene tingatsegule miyoyo wina ndi mzake.Anatipeza ife pa malo amene tinali odzichepetsa. <strong>Yesu</strong> safuna kuti ifetikhale odandaula ndi kwidzi koma, modzichepetsa pakupempha enakupemphera, kuthandiza ndi nzeru.Iyi ndi njira imene banja liyenera kukhalira, koma izi sizingatheke laMulungu m’mawa wokha. Mpingo wowona ndi banja pamodzi, mongabanja lilolonse ndi banja tsiku liri lonse. Funani ndi kuyembekeza zimenezimwa inu nokha “kwa <strong>Yesu</strong> amene akonda ine, ndidzatsegula mtima wangakwa enanso. Ichi ndi chisankho chimene muyenera kuchita. Mungasankhekukhala kumbuyo kwa chotchinga posatsegula moyo wanu ndi kulankhurandi abale ndi azilongo pa zimene mukumvera. Mungasankhe kubisalakumbuyo kwa misonzi ndi zowawa kuchokera kw aanzanu. Koma mgatimungatero simudzapeza mphamvu ya machilitso ya <strong>Yesu</strong>. Adzatsenuliramoyo wake kwa ife ngati tili banja <strong>Yesu</strong> adzakhala kutali mmalo mwakusintha miyoyo yathu ndi kukhala mnjira imene afuna. Akufuna ifekugwira ntchito imeneyi pamodzi monga banja. Ndipo pamene titsegulamiyoyo yathu <strong>Yesu</strong> mu mphamvu yake yonse ndi chikondi ndi ulemererokupeza ifeyo. Koma ngati tili ndi kunyada kwambiri ndi mantha ndi zimeneena angaganize kapena kunena za ife, ndiye <strong>Yesu</strong> sadzatipeza ndikutipatsamoyo ndi mphamvu imene afuna atipatse.Kudya mkate wokondana wina ndi mzakeChoncho tabwera mu dzina la <strong>Yesu</strong> ndi umboni wa moyo ndi mphamvuya Mulungu, tikufunsani kudya mkate umenewu usangowelenga, ndikukufunsani kuti mukhale mpingo ndi banja lowona, osati kuonera. <strong>Yesu</strong>34 35


afuna malo amene angakhalemo sakhala nyumba zomangidwa ndi manjaa anthu. Amakhala mu banja, ndipo mubanja basi. Akufuna malo ameneangakhale amene inu muli osati anthu wowerenga za mkate ndi kuwonera“mpingo” koma malo amene banja liri ndinu mpingo tsiku lirilonse.Mzimu Woyera kudzera mwa Paulo anati masiku wonse ayenera kukhalaofanana. Zipembedzo zina ali ndi masiku apadera masiku “woyera” koma<strong>Yesu</strong> njira yake imodzi ndi kuti tsiku lirilonse ndi lofanana. <strong>Yesu</strong> ndiyesabata la mpumuro. Pamene tikhala mwa Ysu tsiku lirilonse, pameneposotili pa mpumulo. Mulungu aitana inu kukhala banja . Tidzasankha kukhalabanja? Ngati pali chokoma pakati pa inu mlongo muli mudzagwetsakusamva nako? Mudzagwira bondo lawo ndi kupempha iwo kuti afewetsemiyoyo yawo? Mudzapita ku phiri ndi kupemphera ndi misozi kwaiwo kuti afewetse mitima yawo? Mudzatsegula miyoyo yawo kwa iwo?Mudzapeleka moyo wanu kwa iwo tsiku lirilonse, kuzipeleka molimba,kupelekedwa onse atunthu ndi aphumphu mwa <strong>Kristo</strong>, ndi kulira mokwezakwa Mulungu pa mirakulu ya chikondi! Mudzapanga zimenezi kwamuombori <strong>Yesu</strong>? Safuna inu kuti mungodziwa za moyo wake. Akufunakuti inu mukhale moyo wake.Umenewu ndiwo uthenga wabwino wa ufumu. Muli mkuitanidwamu moyo wake ngati mudzathawe kuchokera mu kunyada, kuzikwezandi ku ulesi. Mulikuitanidwa kukhala <strong>Yesu</strong>, osati kungodziwa iye.Tsiku lirilonse kondanani wina ndi mzake kuchokera mu mtima ndikukhuzidwa ndi miyoyo ya ena, kuthandizana ndi ana ang’ono kukhalamonga <strong>Yesu</strong> tsiku lirilonse.Uku ndi kuitana kwa Mulungu, uku ndi kukuitanani mkate wa chikondipamodzi tsiku ndi tsiku ndipo <strong>Yesu</strong> adzadza miyoyo ndi kupanga inutunthu monga m’mene sizinakhaleko pachiyambi. Adzachapa ndi kutchukamantha anu ndi kuumitsidwa kwa mtima. Mtsinje wa <strong>Yesu</strong> udzathiriramadzi, mu moyo ndi kukhala bwalo ya chonde. Chikondano ndi chikondindi Atate chidzakula kulirabe. Mudzaona nkhope yeniyeni ya Mulungumonga m’mene mukondana wina ndi mzake uwu ndi uthenga wabwino.Lero ngati mumvera mau ake, musaumitse miyoyo. Fewetsani pamaso paMulungu. Funani kuti tsiku lirilonse limene mutsegule miyoyo yanu kwaiwo wokuzungulirani ndipo simudzasiyana kuchokera kwa wina, chifukwamuchita izi kw A<strong>Yesu</strong> muombori.Mpingo monga banjaMu mabanja ambiri muli mabanja eni eni amene anabadwa ndi maindi bambo amene timawatcha “Ana obvuta” Ana ena ali obvuta kuposaanzawo, koma ngati ali banja, ali banja, ndipo tidzathandiza kuthetsamabvutowo. Sititenga ana eni – eni a mbanja ndi kupita nawo kuphiri ndikuwasiya kumeneko. Timafunsa Mulungu mu nzeru kapena kukubweletsakunyumba mu banja.Pokuthandizani kuti mukhale ndi chithunzi cha mmene zingakhalirepamene mpingo uli pamodzi, taganizani mu kulingalira banja nyumbayanu, ndi ana amuna asanu akazi atatu ndi mai ndi Bambo. Kodi bambondi amene amalankhura munyumbamo? Ngati mmodzi mwa anayamatawa zaka khumi ndi zitatu ali ndi kanthu kolankhura, sangathe kunenakodi? Kodi amai sapeleka maganizo awo mu banja? Nanga kodi anaochepa sangaongolere banja? Kodi pali ufulu nthawi zonse mbanja kwamm’odzi yekha olankhura? Kodi pali mbali kwa ana ochepera kulira ndikulankhura zofunika? Ziyeneranso kutero pamene mpingo wonse ulipamodzi, angakhale ang’ono angatsegule moyo ndi kulira pa chosowa,mwina mai angathandize kuthesa bvutolo ndikunena za mai wa uzimu,pamene mpingo uli pamodzi. Mwinanso bambo wa uzimu angathensokuthetsa bvuto la mwanayo. Koma umu ndi mmene mpingo ungakhalirepamene ukumana pamodzi. Aliyense wa banjalo angathe kutsegula miyoyondi enawo a m’banjalo angathandize zosowazo. Izi simu msonkhanowokha. Pamene alongo ali kuchapa pamodzi pamene ali kuyimba nyimbomu msonkhano onse, Bwanji sangathenso kuyimba nyimbo pamene alikuchapa pamodzi?Ngati mungalankhure ndi Atate pamodzi mu msonkhanowo, Anansoonse sangathe kulankhura ndi <strong>Yesu</strong> pamodzi pamene ali mkuyenda onsepamseu pamodzi siza Mulungu mmawa ndi lachitatu madzulo. Palibezimene zingachitike mu msonkhano zimene sizingachitike pamene tilimkuyenda pa msewu pamodzi.Sitidikira msonkhano kuwauza abale ndi alongo pazimene <strong>Yesu</strong>wationetsera lero. Sitidikira msonkhano kutsegula miyoyo ndi kufunsakuthandizidwa ndi china chake. Tili chimodzi – modzi ali ndi bvutoangakhale ndi mwana wa ng’ono ali ndi bvuto angakhale ndi masiku36 37


apadera limene aloledwa kulankhura za bvutolo, kapena adzalankhulanthawi iliyonse chifukwa pali chikondi mbanja? Uwu ndiwo mpingowoona, pamene tsiku liri lonse tingathandizane. Palibe kusiyana pakatipa msonkhano ndi popanda misonkhano. Chifukwa timabweletsachiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> kwa aliyense tsiku ndi tsiku. Timalambirakuchokera pansi pa mtima ndi wina ndi mzake tsiku ndi tsiku, m’mawandi usiku pamene tipita kopeza chakudya, timapemphera tonse ndikulambira pamodzi. Uwu ndiye banja la <strong>Yesu</strong>.Penanso, pamene tikhala banja limodzi lalikulu, ngati muli kupitakumudzi ndi kumenya mkazi wanu, kapena kukhala ndi nkhanza ndiiye, Ayenera kukwanitsa kunena kwa inu. “Umu simmene njira ya <strong>Yesu</strong>pamodzi <strong>Yesu</strong> anati mwamuna ameneyu samvera kwa iye mkaziwoayenara kupita ndikupeza awiri kapena atatu ena a mu bajja la Mulungu,ndi onse ayenera pamodzi kulankhura ndi munthu amene ali ndinkhanza. Ndizimene anatiphunzitsa ife mu Mateyu 18, manyumbaathu simalo obisalira kuchokera mu chowonadi. Sitingathe kukhalaoweluza nyumba yathu ndi kukhala osasamala chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong>.Tsopano tili tonse banja la Mulungu ndi nyumba zathu zili za ife tonse,choncho tsopano mlongo angathe kubweletsa ena kudzalankhura ndimwamuna wake. Sitipeputsa chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> mu zinyumbazathu. Chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> sichili cha “nyumba ya mpingo” Tsopanoali pamodzi pamene tipita ku msika kapena tipita ku zinyumba kapenapamene tipita kophunzira. Tsopano chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> chilli munyengo ndi muzochitika zosiyana siyana. Tili banja limodzi tsiku lirilonsemasiku onse, usiku onse.Kumanga njira ya <strong>Yesu</strong><strong>Yesu</strong> anati kuti ngati mudzafika mau anga mu wochita, pamene chimphepochibwera (ndipo adzaima) pamenepo nyumbayo idzaima. Idzaimachifukwa inamangidwa pa mwala olimba poika mau ake mu moyoosati poganiza chabe, kapena kuimba za mau ake ngati tidzaimba za izi,Pemphelani ndi kulankhula za izi ndipo tidzasinthe njira imene timakhalapomvera mau ake wina ndi mzake, pamene mphepo idzabwera, angakhalekuti nyumbayo ndi yokongola mmaonekedwe idzagwa yonse pansi. Izindi zimene <strong>Yesu</strong> analonjeza mu Mateyu 7, ndiye mangani mu mu njirayake, ndikuchita kanthu ndi choonadi chake. Mvekani zimenezi, ndipomphepo sidzaonongamo.Mu njira imene mbalame yaing’ono kapena mpira zimakhalira mu miyalapamene mphepo ya mkuntho imabwera, mungakhale mu khumbi lamapiko a <strong>Yesu</strong> ngati mudzamanga munjira imeneyi ndikuloza nkhopeyanu kwa iye pamene abwera, mudzakhala mu khumbi la mapiko ake.Mphepo ya mkutho idzapita ndipo Dzuwa lowala lidzaonekera, mbalamezidzayamba kuyimbanso ndipo moyo udzakhala wa bwino ndi watsopano.Choonde mangani mu njira ya <strong>Yesu</strong>. Awa ndiwo mau a Ambuye lero.Mmene mungadyere Mkate woonawu.Palinso gawo lina mu Yohane 6 ananena mau amene ali olimba. Anatiidyani thupi langa ndi mwazi wanga. Anayesetsa kuwauza kuti zimvekebwino. Baibulo limati anthu ambiri amene amamulonda iye anamuleka iye.Anamusiya <strong>Yesu</strong> ndi kupita kwina chifukwa sanamvetsetse ndi maganizoawo. <strong>Yesu</strong> sanawatsatire ndi kuwauza kuti anali kwa iwo kumvetsa.Anacheukira kwa ophunzira ake ndi kufunsa, “mukufuna nanaunsokukhoka ndipo Petro anatti, Ambuye <strong>Yesu</strong>, muli ndi mana moyo a moyo,sitifuna kupita kwina kuli konse. Tifuna kukhala ndithu.<strong>Yesu</strong> anafuna anthu amutsate iye amene angathe kumva ndi mitima ndimizimu. <strong>Yesu</strong> angaike zinthu zobvuta ndi cholinga patsogolo paife zinthuzimene sitingathe kuzidziwa – mmalo mwa kupatutsa nkhosa kuchokeraku mbuzi. Anthu amene angadziwe ndi maganizo awo koma osafunakumva ndi mizimu yawo sangathe kumutsata iye <strong>Yesu</strong> weniweni. <strong>Yesu</strong>weniweni amapanga zinthu,zachilendo poyesa mitima yathu. Ananenandi ife za zinthu zooneka zobvuta monga “Idyani thupi langa ndiImwani magazi anga” zimamveka molakwika ndithu, zimene angakhaleBaibulo silingabvomereze kuti ndi zabwino. Chonsecho, <strong>Yesu</strong> amayesaamene amabvetsera ndi mtima ndi amene amava ndi makutu awo. <strong>Yesu</strong>amayesa amene amakonda Mzimu wa <strong>Yesu</strong> ndi amene amakonda zakunjakokha. Pali zambiri monga izi mu zambiri mu Baibulo pamene Mulunguamasiyanitsa anthu amene amamva ndi makutu awo kuchokera kwaamene amavetsera mu mizimu yawo. Iyi ndi njira ya Mulungu, ndi imeneinakhalapo muzochitika mu Yohane 6, mmene ambiri anathawa <strong>Yesu</strong>,38 39


zapitirira mu mbadwo wina uli wonse kale angakhalenso tsopano pano.Ife sindife Mulungu. Iye ndiye Mulungu. Timazipeleka ku zinthu zimenezili za Mulungu kaya sitikuzimvetsa ndi maganizo athu kapena ai. Izinsondi zimene zili mbuku la Yobu.Tsiku lililonse <strong>Yesu</strong> ali kulankhula mu mkuluwiko umene uli obvutakuumvetsa, poonetsa amene amamukonda iye mu mizimu yawo,kusiyana ndi amene amagwiritsa maganizo awo kumva bwino chabe.Ngakhalenso lero iye ali kulankhula mu mkuluwiko otero umeneuli obvuta kumvetsetsa, kuti aone amene angachoke ndi ena ameneanganene, “Tidzapita kuti ? mwa inu muli kuwala ndi moyo” zilinsochoncho lero monga zinalili kalelo.<strong>Yesu</strong> Mkate Mwa ife“Ngati mukonda ine, sungani malamulo anga. Ndipo ndidzapempha Atate,ndipo adzakupatsani inu nkhoswe yina kuti akhale ndi inu kunthawi yonse.Ndiye Mzimu wa choonadi amaene dziko lapansi silingathe kumulandira,pakuti silimuona iye, kapena kumuzindikira iye. Inu sindidzakusiya inumukhale ana amasiye, ndidzakwa inu katsala kanthawi, ndipo dziko lapansisindiona ine, koma inu mudzandidzindikira kuti ndili ine mwa Atate wangandi inu mwa inu” Yohane 14:15 – 20.Ndidzabwino, ndi choonadi chodabwitsa zimene <strong>Yesu</strong> sanapitilirekupita kwani apamene iye adali kuno ndi kuyimba nyimbo kw aiye ndikuyesa kumvera ziphunzitso zimene anapeleka kwa ife ndiye tsiku linakutsogoloku ndikubwera kwa ife. Zodabwitsa za chiphunzitso chakendi choti adzakhala ndi ife mpaka nthawi yamalekezero a dziko ndiposadzatisiya ife ngati a masiye. Anauza ophunzira ake kuti pameneiyeadzabwera anthu sadzamuona iye koma inu. Ndipo timamuona iye osatindi maso athuwa koma ndi maonekedwe a mzimu anati, mvelani ine ndikukonda ine. Kondanani wina ndi mzake ndi kukhala amodzi monga inendi atate tili amodzi. Dziko silidzandiona ine koma inu mudzandiona inechifukwa ine ndidzabwera ndi kukhala nyumba mwa inu. Ndakhala ndiinu, koma ndidzakhala ndi inu.Sichiphunzitso chonyenga ichi, ichi ndi zoonadi, ali woona monga mumpingo woona monga analili nthawi ya thupi. Zoona ndi izi <strong>Yesu</strong> anatizidzakhala bwino kuti kupita, kusiyana ndi kungoima pamene abwelanso.Awa simau wamba kapena ndi oshashalika chabe kapena chiphunzitsochopeka. Ichi ndi chenicheni. <strong>Yesu</strong> yemweyo amene anayenda panyanjandi kuikitsa akufa ku moyonso adzabwelanso ndikukhala mkati mwaife mu mphamvu ndi chikondi ndi ulemerero. Sadzabwera pamene disola dziko limuona iye koma tingakonde iye ndikupeleka miyoyo yathupachilichonse chimene tifuna pa moyo wathu, ndikukondana wina ndimzake kuchokera pansi pa mtima, kenako <strong>Yesu</strong> yemwewu amene anayendapanyanja ndi kutidzera pa khomo lotcheka ndi kupeleka maso kwa osaonaadzakhala pakati pathu mwa ife ndi kulola ife kuti tikhale pa ubwenzi ndiiye ndi atate ndi wina ndi mzake.Anthu ena sanaone imfa asanaone <strong>Yesu</strong> asanabweranso mu mphamvuchifukwa tsiku la pentekositi linali litangodutsa masiku makumi asanupasaka. Anabweranso kwa ife mu masiku makumi asanu. Sanabwerekudzakhala ndi ife koma kudzakhala mkati mwa ife. Ichi ndi chinsinsichimene chinabisika kwa zaka ndi mibadwo yonse mu Akolose 1,chopambana cha nyengo chonse ndi ichi osati <strong>Kristo</strong> ndi inu, osati Kristukungobwera chabe kwa inu (ngakhale zili choncho) koma <strong>Kristo</strong> mwainu, chiyembekezo cha ulemerero izi ndi za iwo amene adzakonda iyendi kupeleka miyoyo yawo pa cholinga cha iye. Halleluya! Sadzatisiya ifeamasiye ndipo ambiri sanalawe imfa mpaka adzabweranso mu ulemererokukhala mkati mwathu. Izi ndi zimene <strong>Yesu</strong> ananena mu Yohane 14.40 41


Mulungu Wa Dongosolo NdiAefenso 4Malemia, Malawi, Africa 1996Mfumu Yogonjetsa Ndi Mphatso Kwa AnthuMulungu wathu odabwitsa sanalephere kutipatsa zapamtima wake kuMpingo wake ngati mungaone bwino ndi tcheru ku malemba, mungaonekupambana ndi zopambana za <strong>Yesu</strong> <strong>Kristo</strong> ndi ufumu wake.<strong>Yesu</strong> anali ogonjetsa wamphamvu. Mu Efeso 4:8 imati: “Anatsogoleraogwidwa ukaporo anapeleka mphatso kwa anthu” (NIT) kuonetsera m’menemfumu wogonjetsa imabwelera kuchokera ku dziko lachilendo atapezaGolidi, Siliva ndi zinthu zina zodula kuchokera kwa ogwidwawo. <strong>Yesu</strong>wagonjedwa adaniwo ndi kubwelerako pachionetsera cha chigonjetsoatapeleka mphatso kwa anthu ake. Mphatso zimene zaikidwa mu Afeso4:11 - Atumwi, Aneneri, Alaliki, Abusa ndi Aphunzitsi - ali mbali yamtunduwa <strong>Yesu</strong> pamene <strong>Yesu</strong> anakwera kumwamba mu mitambo ndikutumiza mzimu wake woyera. Sanangoika mzimu wake kukhala mkatimwa ife amene takhulupilira. Koma anatenganso mbali ya iye mwinindikupeleka kwa anthu osiyanasiyana amene akhulupilira iye. <strong>Yesu</strong> analiwansembe wa mkulu ndi okhulupirika mnyumba ya Mulungu yosne.Anali mtumwi, mneneli. Mbusa wabwino ndi mphunzitsi wa mkulu. Analiuthenga wabwino kuonekera mu thupi.Thupi limafuna mphatso zonseBaibulo limati pamene <strong>Yesu</strong> anapita kumwamba ndi kutumiza mzimuwake, anatenga mbali ya iye ndikutumiza zonse pathupi la Khristo, mpingozidziwika kwa ife ndizoti ziwalo zosiyanasiyana za mbali ya matupi athuamapanga zinthu zosiyasiyana. Mungathe kuona ndi maso anu ndipomungathe kumva ndi makutu anu. Koma simungathe kumva ndi mphuno,ndi kuona ndi pakamwa) ziwalo zonsezi sizili zofanana, mwachoncho,ziyenera kudalirana china ndi mnzake kwambiri.43


Tisanapitilire ndi Aefeso 4:11, muyenera kudziwa m’mene mukufunirathupi lonse la <strong>Kristo</strong>. Timafuna tonse thupi la <strong>Kristo</strong>. 1 Akorinto 12 amatisitinganene kwa anzathu kodi “sindili kukufuna” m’malo mwake tiyenera“Ndili kukufuna iwe” “Ndili kukufuna iwe” uwu ndi mtima otere umeneumakondweretsa <strong>Yesu</strong> kwambiri. <strong>Yesu</strong> anali ndi mphatso mwa iye yekhandipo zina zazimenezi zili mu Aefeso 4. Mu mpingo wa Mulungu, thupila <strong>Kristo</strong> liyenera kufuna mphatso zonsezi mwachoncho, mpingo wina uliwonse pawokha sungathe kukhala ndi mphatso zonse. payenera kukhalamlumikizo weniweni pakati pa amidzi ndi amu mzindawo mulumikizowondi wabwino ndi ofunika.Galimoto lili ndi ziwalo zambiri, zitsulo, galasi ndi rabala. Ilinso ndiinjini, chiongolero, nyali, hutala ndi matayala. Ngati tingaike zidazonsezi za galimoto mu chipinda ndiye kuti sitidzakwanitsa kuyendetsagalimotowo, Angakhale kuti zidazo ndizabwino, sumulowa mu galimotondi kuyendetsa mphaka zida zonse pamodzi zitakhala m’malo mwake.Munjira ina idzakhala kuunjika zitsulo, osakhala ndi zochita zabwino. Izizimaonetsera kufunika kwa mphatso ya mtumwi.Mbali iyi ya <strong>Yesu</strong> - mphatso ya mtumwi, ndi mphatso imene imaonauika zinthu zonse pamodzi ndi kupangitsa “galimoto” kuyenda. PalibeAtumwi ambiri mu dziko lapansi komanso m’mene zinalili ndi zakazambiri za chikristo.Baibulo linasindikiza atumwi osapitilira makumi awiri ndi asanu ndim’modzi 26 mu nyengo zonse za zaka 100. Poyambirira 12 kenako 14atumwi ena , angakhale enawo anali ndi mtima woona ndi kukonda ntchitoya Mulungu sanali ndi mphatso yoika zinthu pamodzi mu Galimoto. Enansopopanda mphatso za atumwi, sangathe kuwona m’mene angatengere zidazina mu mpingo ndikuziika pamodzi ndikukhala mpingo wamphamvu -okhala ndi mtima umodzi, maganizo amodzi, ndi cholinga chimodzi.Mphatso Ya MneneriMphatso ya chiwiri kuikidwa mu Aefeso 4 ndi mphatso ya uneneri.Mneneri ali othekera kuona ndi kumva fungo loipa kapena labwino.Iye sadalira pazimene maso ake ndi makutu ake a dziko lapansi. Iyeamakwanitsa kumva fungo limene lili la <strong>Yesu</strong> kapena ai. Munjira imeneyi,mneneri amathandiza kupeleka milimo yabwino yoyenera kumamangidwakuti Mtumwi amange. Mphatso zonse zinayi kapena zisanu zimenezatchulidwazi zili ndi malo ake ake mu thupi la <strong>Kristo</strong>, ndipo ngati mulibemphatso zimenezi pa msonkhano pano, muyenera kugwira ntchitomolimbika kumanga ubale ndi mphatso zinazo ndi anthu a mizinda ina.Mukawerenga mubukhu la Machitidwe, mudzaona kuti zimachitikapafupi - pafupi. Mphatso zimene zalembedwa mu Aefeso 4 zimayendakuchokera mu mzinda wina kupita kwina ndikuthandiza polimbikitsa ndikumanga, woyera mtima onse pamodzi.Pofuna kukwaniritsa izi, mphatso ya Atumwi ndi Mneneri ndi yofunikamu mbali zisanu ndi zitatu kapena zisanu ndi zinayi mu zonse pamodzi.Popanda mphatsozi anthu a Mulungu adzakhala ndi umphawi weniweni.Ayenera kukhala amtima ofunitsitsa kukonda Mulungu kwambiri,ndikukhumudwa ndi zobvuta zina. Koma ndi kuthandizidwa ndi mphatsozobvuta zidzachotsedwa.Kusoka Thupi La <strong>Kristo</strong>Mphatso yamu Aefeso 4:12 ndi zofunika kukonzeketsera anthu a Mulunguku ntchito yotumikira. Mau oti kukonzeketsera limathandauza kuti“Kulumikiza kapena kuphatikiza pamodzi” muchigiriki ndi mau ameneanasankha kuthandauza kwa mphatso zisanu zimene zinali kugwirirantchito - kuthandiza kuika fupa pa malo ake, ngati dzanja ndi losweka.Sing’anga amaika fupalo pamalo ake nthawi zina zimawawa kuika fupapa malo ake. Koma ndizofunika kapena thupi kukhala lopunduka ndilopanda pake. Mphatso zimene tanenazi mu Aefeso 4:12 zimalumikizathupi la <strong>Kristo</strong> pamodzi ndikuika mbali ili yonse pamalo ake.Kulumikizitsidwa Ndi Kudziwa ChuphunzitsoCha <strong>Yesu</strong>Mu Aefenso 4:13 taona kuti mphatso zimachita pamalo ali yonse -zidzatithandiza umodzi wachikhulupiriro! tawuzidwa kale mu bukhula aefenso kugwiritsitsa umodzi wa mzimu. Mulungu akuyembekezeraife kukhala ndi umodzi wa Mzimu ndipo Mulungu watilamulira kutitikondane wina ndi mnzake.44 45


Mwachoncho, pali kusiyana pakati pa umodzi wa mzimu ndi umodziwa chikhulupiriro. Popanda mphatsozi, (zonenedwa mu Aefenso 4:14)kukhala mu mgwirizano ndi malo amene timakhala, tidzakhumudwa pazokhulupirira zathu. Ndipa mphatso imeneyi imene tili okonekeletsedwamu umodzi wa chikhulupiriro. Popanda mphatsozi (zonenedwa muAefeso 4:14) kukhala mu mgwirizano ndi malo amene timakhala,tidzakhumudwa pa zokhulupirira zathu. Ndipamphatso imeneyi imenetili okonzekeletsedwa mu umodzi wa chikhulupiriro.Umodzi wa uzimu umalumikizidwa ndi ali yense amene anagulidwandi mwazi wa <strong>Yesu</strong>. Timalandira ali yense ndi kukonda amene mwaziwa <strong>Yesu</strong> unamubisa iwo. Timakonda kulandira iwo munjira imenetimalandilira <strong>Yesu</strong>. Umodzi wa chikhulupiriro ndi kudziwana pamodzi zachiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> - zaubatizo, kuika dzanja, kulambira, kusonkhanapamodzi ndi mphatso ya mzimu. Mphatso imeneyi idzathandiza m’menetingakondere wina ndi mnzake ndi m’mene utsogoleri uli, ndi m’menem’<strong>Kristo</strong> ali, zoona zake ndithu, ngati misonkhano ilibe kulumikizitsidwandi mphatso zisanu. Sitingakhale ndi umodzi wa chikhulupiriro, ndipotidzasokonezedwa kuya kwa mgwirizano.Kudzama Kwa ChikondiAefenso 4:13 amanenanso kuti mphatso imatithandiza ife kukhala ndichidziwitso cha mwana wa Mulungu, chikhumbo cha Atate ndiye kutitidziwe zili zonse za <strong>Yesu</strong>. mawu oti, “Nzeru zonse” mu malemba awa ndi“EPIGNOSIS” ndi mau amene amati ndikhale pamodzi ndi <strong>Yesu</strong>. Mulunguanasankha mawu awa ponena kuti tiyenera kukhala ndi mgwirizanoweniweni wa ukwati ndi mwana wake. Awa simau enieni a ukwati ndimwana wake. Awa simau ochokera m’mutu ai koma ndichidziwitso chamumtima. Ndi mau omwewa amene Maria ndi Yosefesanadziwane winandi mnzake mphaka <strong>Yesu</strong> atabadwa ndi mau omwewa anagwiritsidwantchito. pamene adam anadziwa “Eva” ndipo anakhala ndi mwana.Choncho mphatso izi zisanu ndi kwenikweni zofunikira pa mpingo.Zimathandiza anthu a Mulungu kukhala ndi kulumikizidwa ndi <strong>Yesu</strong> ndikuyang’ana nkhope zawo kwa iye ndi kupeza mpumulo ndi mphamvumwa iye pamene zinthu zili zolimba. Adzaphunzira kutchula dzina laAmbuye ndipo sadzachita manyazi kapena kukhukudwa.Mau a nyimbo ina amati, “<strong>Yesu</strong> ndiye bwenzi leni leni, machimo athu ndizopsyinja zidzatha. Tili ndi mphotho yotitengera kwa iye mu pemphero“Mphatso zisanu izi ndi zofunikira kuthandiza anthu a Mulungu kukhalamchiyanjano ndi <strong>Kristo</strong> - mlumikizitso weniweni ndi iye kuti pamenemphepo uamkuntho ibwera osaiwala kubisala mwa <strong>Yesu</strong>. Amatembenuzankhope zawo kwa iye ndikuona kukondwa kwa pa nkhope yake ndipoanaklwanitsa kupyola mu mphepo imeneyi. Mphatso zisanu zimene zilizoyenelera kukhala ndi nzeru zonse mulumikizo weniweni wa <strong>Yesu</strong>.Kuimba Mu MphepoAefeso 4:13 imatilonjeza kuti mphatso ndi zofunika ku munthu wangwirokumuyeso wa msinkhu wa chidzalo cha <strong>Kristo</strong>. Izi ndizothandauza kutiumunthu wathu uyenera kukhala ofanana naye <strong>Yesu</strong> ndikuti tisatengedwendi mphepo yoomba ya chiphunzitso choipa chi machitidwe. Tidzakhalaotheka kuima mwamphamvu, chikondi cha Mulungu. Pamene mphepoiomba modutsa ndi kugwedeza zonse zimene zingagwedezeke, noyo wa<strong>Yesu</strong> mkati mwa ife udzakwanitsa kukula ndikukhala wamphamvu. Mulungunthawi zina amalola kuti tigwedezeke ndikutilengera ife ku zobvuta.Atate anachita izi ndi mwana wake <strong>Yesu</strong>, ndi Paulo ndi Mtumwi wina,“anabvutika mu moyo” malemba amati, “uwu ndi mwai kuti atate apelekaife kukhala monga iye ali. Pamene mphepo ifika ndi mafunde kuomba ndimphepo, tisatengedwe tengedwe uku ndi uko, ai. Tidzakhala amphamvundi mphamvu pamene tikhala pafupi ndi <strong>Yesu</strong> ndi wina ndi mnzake.Kulankhura Mu ChikondiAefeso 4:15 amati kuti tidzaphunzira kulankhula choonadi ndi chikondi.Mphatso zimenezi zimathandiza ife kuti tilankhule wina ndi mnzake muchikondi ndimnjira yowonadi. Izi ndi chinthu chofunika mu mgwirizanowa chikondi. Kulankhula choonadi muchikondi ndi kupeza njirayokondweretsa Atate ina ndi kulankhulana bwino. Tiyenera kulankhulachoonadi, koma chiyenera kubvekedwa ndi chikondi, kudekha ndi kukomamtima, ziyenera kuonekera motere mu kudekha konse. Chikondi chathundi kuonetsera mu mtendere ziphatso zimathandiza ife kuti tingathekulankhulana mu chikondi munjira imene sitingathe popanda izo.46 47


Kuphunzira Kukhulupilira Mbuye OkondewaMalemba amanenanso mu Aefeso 4:15 kuti mphatso zonsezizimathandiza ife kukula kufikira kumutu amene ali <strong>Kristo</strong>, <strong>Yesu</strong> ndiyemutu wa chili chonse. Ali bwana ndi Ambuye pa panyanja ndi pamtunda.Iye ali mbuye wa mitambo imene imapeleka mvula ndi mphepo imeneimaomba. Ali Mbuye wa zonse zokwawa zazing’ono ndi nyama zazikuluzomwe. Alinso wambalame za mulenga lenga, ali wa miyala yonse yokhalapamsewu. Ambuye <strong>Yesu</strong> ali mbuye wa nyenyezi zokhala mu m’mwambandi mwezi ndi dzuwa. Afunanso kuti akhale bwana, koma akutiitanaife kulowa mu sukulu ya <strong>Yesu</strong> kumene timaphunzira kudziwa kuti aliAmbuye. Timaphunzira kukhulupilira iye. Timaphunzira kuti ali ndinzeru zopambana zodziwa zili zonse, ndi kuti ali ndi mphamvu zotetezaife. Ngati sitilola iye kukhala Ambuye ndi chifukwa choti sitikhulupiliraiye mokwanira kapena kuti njira zake ndi zabwino ndi chikondi chake ndichopambana, kuti sichilephera.Mphatso zimene zimatipangitsa ife kukula msinkhu mu ufumu wa <strong>Yesu</strong>,kuona m’mene iye ali odabwita - ali wokhulupirikira, wamphamvu,wanzeru ndi okonda. Munjir aimeneyi ndingakhulupilire iye popangazimene iye afuna kuti tichite.David, okondeka wa Mulungu, analemba nyimbo zambiri za chikondikwa Atate. Atatenso analemba nyimbo ya chikondi kwa iyenso, yoti alimunthu wapamtima wa Mulungu. Cholinga chimene Mulungu ananenakuti anali wapa mtima pake chifukwa anali kudziwa Mulungu ali wabwino,wodabwitsa ndipo sanamukhumudwitse ndikumupititsa munjirayolakwika. Mulungu sanamukhumudwitse ai kapena kumuononga iyeMulungu sanamupatse mwala pamene anafuna mkate, Mulungu alikumupatsa zonse kwa iye.“Ndili Kufuna Iwe”Aefenso 4:16 limati thupi lonse ndi lo “lumikizika pamodzi ndi misempha”monga momwe manja ndi miendo ili yolumikizika muthupi, mphatsozimenezi zimathandiza thupi la <strong>Kristo</strong> kubwera pamudzi kukwaniritsakugwira ntchito ya Mulungu. Taganizani kuti thupi lamunthu silingagwirentchito ngati manja ndi miendo zili zotayana mu malo osiyanasiyanazingakhale ziwalo zodabwitsa ndi mphamvu pazokha, koma ngati sizilizolumikizika. Kwa zina mu chikondi kulumikizika ndi mutu kuti mutuolamulire, ndiye thupi lingakhale lopanda ntchito lake.Ndifuna kulimbikitsana inu, oyera mtima, nonse kuti muphunzire ntchitoya mphatso zimenezi ndi kuona zodabwitsa zonse zimene zikubwerandi izo. Lolani ndi kulandira Abale ndi Alongo ochokera madera enakukuthandizani kukhala muzodabwits zambiri zimene zimachitikapochokera mu mgwilizano wa mphatsozi. Ndiye tidzakhala odalilika kwa<strong>Yesu</strong>. Tingakhale okonda ndi nzeru monga <strong>Yesu</strong> ali. Tingakhale othekerapofikira anthu amene timakhala nawo, kopambananso kuthekera pokhalandi mabanja, wokondana. Koposanso kuthekera pokweza chikondi, anaomvera, ndi koposera pogwiritsa ntchito mphatso mu chikondi, chifukwatalora mphatso zisanu zimenezi mu malo amene tikhale. Palibe pamaloamodzi amene (sindinaone), mwachoncho Mulungu amafuna kutitifanane wina ndi mnzake kuchokeramudzi wina ndi wina, mzinda ndimzinda. Akufuna kuti tikule MUKUDZADZA KWA MWANA WAKE.Mulungu amapeleka zinthu zambiri kwa iye ngati amayang’anira pa iyekunjira zake zonse. David amachita chili chonse chimene Atate amafunsaiye osati kuti anali omvera mouzidwa, koma anali okhulupirira chikondicha Atate ndi anzeru kwambiri. Izi ndi zimene tonse timaphunzira ndimphatso zimenezi. Atate ali odalilika ndi okhulupirika, ndiposno<strong>Yesu</strong> amapeleka mphatso zabwino, osati zoipa, kwa ana ake. Ndiyetingamukhulupilire iye kukhala mutu wathu, chifukwa iye ali wabwinokwa ife.48 49


Maziko A <strong>Yesu</strong>Chisitu, Africa 1996Anthu --- osati zomangaBaibulo limatiphunzitsa kuti Mulungu sagona nyumba zomangidwa ndimanja anthu. Efeso 2 ndi malemba ena otere amati ndife malo okhalamoMulungu mu Mzimu Oyera – mpingo.Timadziwa mmene mpingo wumaonekera ndiye ngati nyumba yaMulungu ndi anthu osati nyumba, Nanga imaoneka bwanji?Pamene muyenda muyenda mu msewu ndiye mumaona zomangidwandi zipembedzo ndiye poti mpingo ndi opangidwa ndi anthu osatinyumba zomangidwa. Ndiye zimaoneka motani. Tingasiyanitse motanindi mpingowo ona ndi osaona? Awa ndi maonokedwe a mpingo umeneumamangidwa ndi anthu osati miyala.Pamene <strong>Yesu</strong> ayenda uko ndi uko kufuna mpingo woona adzaudzidwabwanji? Mpingo woona omangidwa ndi miala ya moyo umene <strong>Yesu</strong>anaukonda uyenera kukhala ndi zida zabwino. Ngati nyumba imangidwandi zida zoola ndiye kuti idzagwa. Ngati matabwa yogwilizana kumwambandi woola idzagwa pansi. Njerwa zofewa zosaumbidwa bwino kapenakuchokera ku zolakwika sizingathe kuthandiza, ndipo idzagwa. Mpingowoona umene umangidwa ndi Mulungu, osati manja anthu, ndi umeneupangidwa ndi miala ya moyo - Akristo woona osati akufa. Njerwa kapenazidina ngati ndi nyumba ya Mulungu kuchokera kwa amai ndi abambokuti ikhale yothekera. Siyenera kukhala miyala woipa (1 Akorinto 3-5)Kuchokera Ang’ono mpaka Akulu Onse SadziwaMulunguUneneri wa chipangano chatsopano umati mpingo wa Mulungu umeneali kumanga ( Jer 31, Aher8, Ahebri 10) ndiwo mpingo woona umenekuyambira ang’ono mpaka akulu onse adzadziwa Mulungu wamoyo.51


Mu mpingo wakale umakhala membara chifukwa kuti makolo ako ndiAyuda ndiye ngati ukhulupilira chinthu chabwino ndi kuti makoloali kumeneko ndinso iweyo umapita kawiri kawiri ndi kumapelekachakhumi ndiye kuti membara wa mpingo umenewo. Mu chipanganochatsopanomu mpingo wa <strong>Yesu</strong> izi sizoona ai. Uyenera kupeleka mtimawako kwa Mulungu ………… Uneneri wa chipangano chatsopanochinali mpingo umene Mulungu akumanga Jer 3, Ahebri 10) ndiyempingo woona ndiye kuti wang’ono mpaka wamkulu ONSE adzadziwaMulungu wa moyo. Ngati munthu sadziwa Mulungu sangathe kukhalamembala wa <strong>Yesu</strong>. Udzakhala monga zomangidwa zimene zilizofewa kapena kuwola – Nyumba imene <strong>Yesu</strong> akumanga ndi nyumbayopambana ndipo <strong>Yesu</strong> adzagwilitsa ntchito zida zabwino zokhapomanga nyumba imeneyi.OsanyengeleraMachitidwe 3 imati <strong>Yesu</strong> anali Mneneri ndipo anamanga nyumba yake(Mpingo) ndipo ali yense amene samvera iye adzachotsedwa pakati paanthu. Izi ni zimene <strong>Yesu</strong> analankhula mu Mateyu 18 kuti ngati munthuapitirira kuda mnzake. Kuuma mtima kuzikonda ndikupitilira kumwamoyo, kukalipira mkazi kapena ana ndikuchita zakuba mu malonda awo,kunama kapena ulesi ndiye tipita kwa iwo ndikuwatandiza, mwachonchongati sasamala pakumvera chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> ndiye tiyenerakubweretsa awiri kapena atatu ena ndi kulankhura ndi munthuyo. Ngatisakumevlanso pazimene <strong>Yesu</strong> anena ndikuti sakusintha, ndiye tilankhurendi mpingo wonse ndi kumufunsa kuti achoke.1 Akorinto 5 limati tiyenera kuchotsa isiti kuchokera pa chakudya.<strong>Yesu</strong> anatilamulira osadya kapena kukhala pamodzi ndi munthu amenesadzasintha moyo wawo ku chiphunzisto cha <strong>Yesu</strong>. Pasakhale chigwilizanondi iwo, ndikuti achotsedwe pakati pathu. Baibulo limatero “<strong>Yesu</strong> ndiomanga wamkulu. Iye sadzamanga ndi zofewa ndi zowola akufunakumanga nyumba yapamwamba kuti akhalemo - imene ili yoyeneraMfumu monga iye.Kusankha Zida ZomangiraChoncho zida zomangira mu nyumba ya Mulungu ziyenera zapamwamba, izisizoti munthu ali yense ndi wabwino ai. Sizoti munthu ali yense ndi wabwinoai. Koma, zithandauza munthu, akonde ndi kumvera <strong>Yesu</strong> ndipo sanyoserakuthandiza kwa ena, amene afuna kuthandiza iwo kukonda ndi kumvera <strong>Yesu</strong>,afuna kuthandizika zomangila zabwino za nyumba ya Mulungu ndi pamenemunthu amene safuna chithandizo iye amati, “osandiweluza ine” “samalazako amaziteteza,” “chotsa choipa m’maso mwako” zimenezo ndi zomangilazoipa, zimene Mulungu salora mnyumba yake. <strong>Yesu</strong> sadzamanga nyumbayake motelo. Iyi ndi mitengo wowola ndipo udzadulidwa pakati pa anthu.(Machitidwe 3:23, Mat 18, 1 Akorinto 5) Mu mpingo woona amene atelosaloledwa. Ngakhale atakhala ndi ndalama zochuluka, kapena amadziwaBaibulo motani angakhalenso mtsogoleri” koma ngati sabvomeleza mpingowa <strong>Yesu</strong> mofewa ku chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong>, ndiye sangakhale ku mbali yampingo woona umene uchitika mu mzimu. Ngati akana, chikondi ndikupepsa nzeru, kuthandiza ndi kudekha mtima, ndi kuwalola kukhala pakatipa abale ndiye tikutsutsa <strong>Yesu</strong> ngakhale malamulo ake.<strong>Yesu</strong> adzamanga ndi zida zomangira zabwino, ngati tili ndi mitimawofewa, kukonda chiphunzitso chake, kwenikweni tifuna kusintha zinthumu moyo wathu umene ufunika kusintha, ndikubwera ndi nkhope zathukwa iye munthawi ya zobvuta kapena kuyesedwa. Kumufuna iye ndi abaleathu kuthandiza ifeyo. Ndiye kuti mwala yamoyo yokongola kumangirayomangidwa ndi nzeru.Nyumba Yomangidwa Ndi NzeruNyumba, tikutenga zomangira zonse zimene zili zoyenelera kumangiranyumba. Miyala yonse ndi matabwa onse ndi zida zonse zimene <strong>Yesu</strong>wazisankha pa nyumba yake. Tsopano zonse tiziike malo amodzi -ndiye kuti tilibe nyumba. Nyumba ya Mulungu imafunika kuposamitengo wabwino yokha. Simungathe kugona mnyumba imene zidazake zangoikidwa pamalo amodzi sizidzakupulumutsani ku mphepo yamkuntho, angakhale ndi zomangira zapamwamba.Palinso njira imene tingamangire nyumba ndi zida zabwino - njiraimene<strong>Yesu</strong> afuna pogwilitsa miyala ya moyo. Monga mmene52 53


achipembedzo chomwecho mpingo woona umakhalir sumangidwandi miyala, koma anthu, miyala ya moyo. Ndipo iyenera kuoneka ndimaonekedwe ena kuti ikhale nyumba ya bwino yoyenera kukhala <strong>Yesu</strong>.Palinso njira ina yomangira nyumba kuti yosabvuta kukhala komansomphepo osaigwetsa. <strong>Yesu</strong> ndi omanga wa nzeru ndipo amanganyumba motere; Ndikuuzani maonekedwe anyumbayo chifukwa ngatisitingamange motere nyumba idzagwa pamene mphepo idzabwera ndimmene tingamangire nyumbayo ndi zomangira zapamwamba ndithuzida zoipa ndi zosaloledwa mu nyumba imeneyi pokhapo pali kusinthikandi kukhala zida zabwino monga <strong>Yesu</strong> afunira.Mnyamata olemera anauzidwa kuti anali wabwino. Koma sanaliololedwa pa nthawiyo chifukwa anali ndi umbombo mu mtima mwake.Anali kudalira ndalama zake koposa Mulungu, anali wa chisoni kupelekandalama ndiye <strong>Yesu</strong> anati, “Sungakhale ku mbali ya Mpingo munjirayotere mpaka mutasintha moyo wanu. Simuli ololedwa kukhala miyalaya moyo mu nyumba yake, umu ndi mmene <strong>Yesu</strong> ali kumangira nyumbayake. Amationa ife ndi kutikonda ife monga adachitira ndi munthuuja komanso akatiuza kuti tisinthe. Ngati sitingasinthe, potipabe ifechikondi ndi malonjezo onse anatipatsa sadzakwanitsa kutigwiritsira ifentchito monga mwala wa moyo. Adzatiika pambali mpaka nditafewetsamtima yathu.Kusendeza Pamodzi Monga AmodziNdipamene miala ikhala pamodzi ndi kulumikiza ndi moyo wa tsikumu chikondi ndi kupezana ndi kumanga ndi makonzedwe a Mulungu.Mulungu akhalidzamoNdipamene miala yonse ikhala pamodzi ndi mamangidwe ndimakonzedwe amene tonse tingakhale ngati kwathu. Zimenezi ndi zoonakwa <strong>Yesu</strong>. Nyumba ya <strong>Yesu</strong> imangidwa ndi mamangidwe ake ndithuosati athu. mamangidwe ake ndi oti abambo zana, Amayi, Abale ndialongo. Makonzedwe ake ndi kuti tichitsilike. Makonzedwe ake ndi otititengeleni zobvuta ndi kukwanilista lamulo la <strong>Kristo</strong>. makonzedwe akendi oti tikhale pamodzi monga iye ndi Atate ali - Amodzi monga tikaonaTimu, mwaonanso David mukaona mwana mwaonanso atate. <strong>Yesu</strong> anatitidzakhala amodzi monganso iwo ali tiyenelanso kukhalanso otere osatimyala yosiyanasiyana ndi kubwera pamodzi la Mulungu, koma banjalomangidwa pamodzi tsiku ndi tsiku.Uku ndi kumanga kwa <strong>Yesu</strong> Mphepo idzabwera ndipo nyumbayiyidzaimabe. <strong>Yesu</strong> adzabwera ndi kukhala pa nyumbayi ndipoidzabweretsa iye kukondwera ichi ndi chifuniro cha Mulungukwa anthu ake mu dziko lili lonse, ndipo tikuitanani ku zinthu izimwa changu.Atate Chikwi, Amayi, Abale, AlongoAtate chikwi, Amayi, Abale, Alongo <strong>Yesu</strong> anati ngati mundimvera inemudzakhaladi atate chikwi Amayi, Abale, Alongo osati chikwi cha okhalapafupi koma chikwi cha abale apa banja. Ichi ndi chifuniro cha Mulungu.Ichi ndi chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> kuti amange ndi zida zabwino. Zidazoipa sizololedwa ngati sizisintha. Nyumba ya <strong>Yesu</strong> ndi yomangidwa ndimamangidwe ake osati athu ndipo mamangidwe ake ndi Atate chikwiAmayi, Abale, ndi Alongo mamangidwe ake ndi oti tiyenera kuwuluramachimo kwa wina ndi mzake kuti tichiridziwe manangidwe ake ndi yotititengelane zothobwitsa ndi kukwaniritsa lamulo la ambuye. Manangidweake ndi oti tiyenera kukhala amodzi woti ukaona Timu wawonansoDevedi. Ukaona mwana wawonanso Atate. <strong>Yesu</strong> anati tiyenera kukhalaamodzi monga iwo ali ifenso tikhalenso munjira yotereyo osati miyalayosiyana imene imabwela la Mulungu koma banja lomangidwa pamodzitsiku ndi tsiku.Kubweretsa Chokoma Kwa <strong>Yesu</strong>Ngati pali zosintha zina zimene zili zofunika kuchitika. <strong>Yesu</strong> anati “Ngatiundikonda ine” mudzasunga malamulo anga” ndiye chonde sinthanipazimene <strong>Yesu</strong> akuitamilani. Musaope ai, Ambiri safuna kukondachikondi ndi choonadi ndipo adzakhala okwiya ndi zinthu izi chifukwaali ndi zinthu zobisika mu moyo wawo, njira yoona ya Mulungu imakhalayokanidwa ndi Satana, Mdani.Ndiye limbikani, pililani ndi kudekha mu zinthu zonse izi, wonetsanichikodni kwa <strong>Yesu</strong> pakuchita chili chonse chimene pa chiphunzitso cha54 55


<strong>Yesu</strong>. Pepani abale ndi alongo amene kungathe kukhala nawo, pemphelanindi iwo lankhulani ndi iwo. Onongani zopinga pakati pa abale ndialongo, zopinga za mantha ndi kunyada, zopinga za ulesi kapendazochititsa manyazi, zopinga za ulesi kapena zochititsa manyazi, zopingaza manyazi, zopinga za chiweruzo, tengani zonsezi ndi kuchapa zonsepachifuniro cha <strong>Yesu</strong>. Phunzilani kukondana wina ndi mnzake tsiku nditsiku. Izi sizidzangobweretsa <strong>Yesu</strong> chimwene chokha, chifukwa choti ndimamangidwa a mpingo wake, koma sizidzasintha moyo wanu kopambanamuyeseni Ambuye lero, zinthu izi ndi zoona.Kwa inu a <strong>Kristo</strong> woonadi, amene muli ndi mzimu woyera wamoyo inu,tsiku lina, sitidzakhala ndi chilankhulidwe chosiyanasiyana. Matembeleroa Babelo adzaonongedwa, miyala yonse ya moyo idzakhala ndi kuthekerapokhala ndi kulankhula ndi mgwirizano odzaza wina ndi mnzake.Nyumba Ya MulunguKomba, Malawi, Africa 1996Banja La “Thanzi”- Mkwatibwi WokonzekaPosachedwa, <strong>Yesu</strong> abwera chifukwa cha mkwatibwi wake. Bayibulo likuti<strong>Yesu</strong> adzabwelera mkwatibwi yemwe wadzikhonzekeletsa yekha. Koditingayikidzike bwanji miyoyo yathu kukhala yokonzekera? Chabwino,lingalirani chithunzithunzi ichi ndi ine.Pamene zipembedzo zathu kapena uzimu ukachitika pamalo patsikulimodzi musabata, ndiye dzili ngati kudya chakudya chimodzi sabatailiyonse. Umu simomwe atate anati tikhale. Tayenera kudyetsa matupiathu tsiku lililonse kuti tikhale. Anapangisanso mizimu yathu kudyanthawi zambiri musabata – kudya mkate wochokera kumwamba ndikukondana wina ndi nzake tsiku, ndi tsiku , ndi tsiku. Anatipanga kukhalamu ufumu wa ansembe pamodzi ndiku bweletsa mkate wamoyo kwaaliyense pamene tikudzukira m’mwamba, pamene tikukhala pansi ndipamene tikuyenda munjira.Kupembedza kwa <strong>Yesu</strong> kuli ngati kudula nkhuni ndiponso ngati tichapaMalaya pamodzi. Timaphunzisana mau a Mulungu mumalo a miyoyoyathu. Pamene tiyenda mu misika pamodzi. Ngati tiona munthu amene aliwovutitsa mkazi wake, timamubweretsela mawu a Mulungu ndikuyambakumuthandiza kuona <strong>Yesu</strong>. Pamene tiona mwamuna kapena mkazi ameneali wozikonda ndi zimene alinazo. Timawakonda ndi mau a Mulungu tsikulililonse. Sitidikila wina ku “lalikira uthenga” okhunzana ndi izo la Mulungu,koma timawapatsa mau a Mulungu chifukwa tonse ndife a nsembe.Mwana wang’ono amene amadya chakudya chimodzi sabata iliyonseakhodza kudwala ndi kufowoka. Izi ndi zowona za mkwatibwi wa <strong>Yesu</strong>.Tayenera kudzidyetsa tsiku ndi tsiku ndi utsiku, tsiku ndi usiku – kutitikule a mphamvu. Timadyetsana mau a Mulungu. Timapembeza limodzitsiku lililonse. Timamufunsa Mulungu kuti atithandize tsiku lililonse.Anthu ambiri atha kuganiza kuti banja la thupi lingadwale kwambiri ngatilingamasonkhane la Mulungu ndi la chitatu lokha lokha. Mu bayibulo,56 57


tikuwerenga dza banja la Mulungu ku Machitidwe 2. Akunena bwinobwino kuti adali pamodzi tsiku lililonse ndipo amadzipereka tsikulililonse kudziphunzitsa za atumwi, kutumikirana m’modzi ndi nzake.Ndikupemphera limodzi. Tsiku lililonse, usiku uliwonse. Samadzitengelazomwe alinazo ngati zawo. Adanyema mkate ndi kudya limodzimumanyumba awo tsiku lililonse.Tidanzidwa zaka zambiri kuti chikhristu ndi mpingo ndi chinthu chimenetingochionerela ndikubwereranso ku moyo wa kale linja. Tili ndi mayikoawiri kapena atatu osiyana. Tili ndi dziko la kunyumba kwathu ndi banja,dziko la ku ntchito ndi kukhala, ndi dziko la “mpingo” wathu. <strong>Yesu</strong> wathuadatiphunzitsa kuti mayiko onsewa ali pamodzi ndiponso ali chimodzi.Aliyense amene wapereka miyoyo yawo kwa <strong>Yesu</strong> ali ndi dzana (100)la atate, azimayi, abale, alongo, malo ndi zinthu – osati dzana la anthu.Oyandikana nawo ndi okuwadziwapo ena, koma dzana la amayi ndiabambo. Izi ndi zomwe <strong>Yesu</strong> adatimphunzitsa. Ichi ndi chomwe mpingoukuthandauza. Tsimalo opitako, koma chomwe tili tsiku lililonse. Mpingouli ngati kukhala pamodzi ndi pafupi ndi wina ndi mzache ngati mayi ndimwana wongobadwa kumene. Awa ndi mau eni eni a <strong>Yesu</strong>.ZotsingaSono chimatipangasa kuti tidzitsiye zinthunzi ndi chiyani?Chotsinga choyamba ndi chiphunzitso chotsamalizika chomwetidaphunzitsika dzaka zapita zambiri. Koma chomwe tikazindikiraziphunzitso za <strong>Yesu</strong> zokhudza zinthuzi. Pali zotsekereza kapena zotsingazotipangitsa kutsiya njira yomwe <strong>Yesu</strong> afuna kuti tikhale ngati mpingo.Ngati tikhala odzikonda kapena aulesi. Sitikufuna kukhala mpingo womwe<strong>Yesu</strong> afuna kuti tikakhale. Tikufuna kukhala moyo wathu m’mene tafunirakukhalira. Ngati wina abwera kwa inu kapena kwa ine ndi kubweretselauthenga wa <strong>Yesu</strong> za momwe tikukhalira ndi akazi athu kapena amunaathu. Munthu wozikonda amati, “dziwa zako. Pitani kutali ndi ine.Koma iyi sinjira ya <strong>Yesu</strong> akuti, “Aliyense amene andidziwa ndi kundikondaine akonda dziphunzitso zomwe ndi phunzitsa.” Wokond <strong>Yesu</strong> adzanena“Dzikomo kwambiri chifukwa chondithandiza.” Ndikufuna kumudziwa<strong>Yesu</strong> kwambiri. Ndinali wosaona koma mwandithandiza kuonansopang’ono, ndikuthokoza pa ichi.” Umu ndi momwe banja la Mulungulayenera kukhalira pamodzi tsiku lililonse. Timathandizana kudziwabwino <strong>Yesu</strong> pothandizzana kusiya tchimo, kondanani wina ndi nzake, ndikusamalira monga tidzisamala ife eni. Izi ndi ziphunzitso za <strong>Yesu</strong>. Umundi momwe adakhala moyo wake ndi ife, ndi momwe watiyitanila kukhalamoyo uwu ndi wina ndi mzache. Umu ndi momwe mkwatibwi wayenelakukhonzekera kubweranso kwa mkwati <strong>Yesu</strong>.Ichi ndi chifunilo cha Atate kuti “tisakhuze mkwatibwi” koma kukhalamkwatibwi. Titha kupanga ichi ngati tikondana ndi kusinthana miyoyondi wina ndi mzache tsiku ndi tsiku. Izi zipotsa kuti “Hi!” ndi kuti“ndimakukonda!” ndi kamayenda. M’malo mwake. Nditsekula mtimawanga kwa iwe ndikukufunsa kuti undithandize. Ngati muona tchimom’moyo mwanga, simupita njira yina ndi kuyisala. Inu ndinu a kazembeake a <strong>Yesu</strong> monga momwe Mulungu amandiuzila kudzera mwa inu.Uwu ndi mpingo – kukhala moyo uwu tsiku lililonse, osati kupita kunyumba ya Mulungu, koma kukhala malo omwe Mulungu amakhala.Ndiye manyumba athu, m’malo ogwilira ntchito athu ndi mipingoyathu yonse ili limodzi, ndi yayikulu. Palibenso zotsekereza kumtimawanga ndi wanu komanso dzotsekereza kunyumba kwanga ndi kwanu.Ndikutchosa kudzikonda kwanga ndi kudzikuza, ndikuchotsa ulesiwanga ndi kusakhulupirila ndipo ndikukonda ena ngati momwe <strong>Yesu</strong>adandikondera. Ngati wina aliyense achita izi, kuchokera ang’ono mpakaaakulu, <strong>Yesu</strong> adzathira mafuta amachiritso ndipo ife ndife mpingo ndimkwatibwi wokongola. Ngati sitidzafuna kukhala nawo m’mawa wa tsikula sabata, ife tidzasemphana ndi mtima womwe uitana za Mulungu, ndipotisakhale zipembezo zomwe zili zopanda phindu.Utsogoleri M’nyumba Ya MulunguKumachitidwe 20, Paulo amalankhula kwa atsogoleri ena ndikuti,“ndali Mzimu Woyela womwe adakupangitsani kukhala wamkuluwoyang’anira.” Izi ndi zotsiyana ndi njira ya munthu. M’mayiko ambiriomwe takhala tikupitako, njira yomwe munthu amakhalira mtsogolerim’nyumba ya Mulungu ndi pokha pokha apita ku sukulu ya dzabayibulo kapena ku seminare, kapena awerenge kupotsa momw anthu58 59


ena amgathe, koma zonsezi ndi zifukwa zosayenera. Izi si njira zomweMulungu amapangira atsogoleri.Padali nthawi zomwe takhala tikuyenda mumipingo yosiyana siyanamuma tauni ndipo tidafunsidwa kulankhula ndi atsogoleri. Panthawiyo,padali njira ziwiri zomwe tidaganiza omwe ali tsogoleri. Njira yapafupindiyoganiza kuti, “Kodi amene ali mu utsogoleri ndi ndani, kapena kodindi ati amene adatsankhidwa ndi anthu kukhala atsogoleri?” chabwinoatsogoleri ndi okhawo amene amakhala ndi a maudindo awo, mwachisanzo “Abusa kapena abusa aakulu”.Koma umu ndi momwe Mulungu amasankhira atsogoleri ake. Sadasankheanthu chifukwa cha sukulu ya baibulo kapena seminare. Adasankha anthumomwe adaona mumitima yawo ndi kuona kuti adali okonzeka kusiyamachimo awo ndi dzikhumbo khumbo pa moyo wa munthu ndi kumtsatapokhapokha iye kuwapulumutsa iwo dzingavute maka. Sono, ngatitafunsidwa kulankhula ndi atsogoleri muma tauni kapena mumayikoosiyana siyana. M’malo moyitana aliyense amene ali ndi udindo kapenam’maina kuti abwere, talankhula kuti, aliyense amene apita kukagonanapempherela anthu oyela mtima, amene masana amasamala oyera mtimaena ndi ena osakhulupirira, amene ali ndi mtima womusata cholinga chaMulungu mu dziko, amuna kapena akazi, ang’ono kapena akulu, ngatimusamalira mizimu ya anthu ena osati pa inu nokha, ndiye kuti ndinumtsogoleri. Bwerani tiyeni tilankhule umu ndi momwe mzimu woyeraumapangira oyang’anira aakulu. Izi dzikusiyana kusankha mtsogolerikamba ka udindo kapena maphunziro.Machitidwe 6, padali ntchito yaikulu yochita ku Yerusalemu. Sadanenekuti sankhani anthu awiri amene ali ndi seminare yamaphunziro ndikutsogolera bwino kapena kulankhula bwino kusiyana ndi ena.” Iwo anati,“sankhani anthu asanu ndi awiri mwa inu amene ali odzazidwa ndi mzimuwoyera ndi nzeru.” Mukuona anthu achikondi ndi anthu othandiza moyowawo wa tsiku ndi tsiku. Awa ndi amuna ndi akazi amene Mzimu Oyeraukuwadzutsa. Sidzitengera pepala lamaphunziro lomwe aliyika pakhomandi chizindikiro cha golide. Dzimatengela mtima wosweka ndi chizindikicha Mzimu woyera. Sono izi ndi ziphunzitso zina za utsogoleri, chifukwaMulungu akufuna kusankha adzitsogoleri pa anthu onse.Zomwe munthu amaganiza kuti ndi zofunikira, Mulungu saganizachoncho. Pamene Samueli amafuna kusankha munthu wokhala mfumu,ambiri adzibale a Davide adaoneka kuti adzakhala atsogoleri abwino. Komawang’ono, kanyamata kabusa nkhosa kadali komwe Mulungu adasankha,tsalabada za mkati mwa mbale kapena mlongo. Amaona za bwino ndiukulu wa mtima wa munthu ameneyo. Davide amafunitsitsa kutetezamoyo wake ndi wa nkhosa zake ku mkango ndi dzi mbalangondo. Davideali wang’ono adapha mkango ndi chimbalangondo kuti apulumutsekankhosa kamodzi ka Mulungu. Davide adamuuza Sauli “ndaphamkango” ndapha chimbalangondo ndithanso kupha Goliyati.” ChifukwaDavide adali wodzipereka kupulumutsa nkhosa, Mulungu adaona kutiDavide athanso kupereka moyo wake pa ana ake. Ichi ndi chizindikiro chamwamuna ndi mkazi chomwe Mulungu adzutse kukhala mtsogoleri, osatimwamuna kapena mkazi omwe adachita bwino mumaphunziro, komamunthu yemwe adzazipereka moyo wake pa nkhosa za Mulungu.Bukhu la Machitidwe likulankhulanso za Davide kuti adali wakufuna kwaMulungu chifukwa amachita zonse zomwe Mulungu amafuna. Davideadalakwa m’moyo wake, tikudziwa zimenezi. Koma mtima wake udali wotiakachite zonse zomwe Mulungu anena. Pa chifukwa chimenechi Mulunguamapungulira mafuta an’dalitso pa iye ndi kumuvomereza Davide kukhalamtsogoleri pa anthu ake – chifukwa amdzipereka moyo wake pa nkhosa zaMulungu ndi kuchita zonse zomwe mbuye wafuna kuti akachite. Ichi ndichikondi cha Mulungu: Amuna, Akazi ndi ana amene adzapereka miyoyoyawo pa nkhosa za Mulungu, ndi omwe adzachite zonse zomwe Mulunguadzanena, omwe adzachite zonse zomwe Mulungu adzafunse – iwo aliamuna, akazi ndi ana omwe ali akumtima wake wa Mulungu. Ameni?60 61


Mtima, Moyo, Maganizo NdiMphamvuOctober 1999, AFRICAPOSACHEDWA, ndinalankhula ndi atate zatathauzo lakukondaiye. Kukambirana kwithu kunali kukhuza ine. Kulingana ndi mutuwakukonda iye kuchoka pa mtima wabwera kulingana ndi nyimbo imenembale anayamba kale. Ndikumva ngati ndinene zimene iye anayambakuphunzitsa ine posachedwapa. Ngati ziri choncho, ndifuna ndigawanenanu zimene Mulungu wawonesela ine zokhuza kumukonda iye.Ndidziwa tonsefe lamulo lalikulu zikupanga nzeru kwa ine kuti ngatisitimvera lamulo lirilonse tisayambe ndikusamvera lamulo lalikulu.Inde popeza sitifuna kusamvera malamulowa ingakhale limodzi la iwo;koma limene anena <strong>Yesu</strong> ndi lalikulu pa onsewa ndilofunika kulionandi chidwi chachikulu. Nditafunsa atate tanthauzo lake lakukonda iye,anandikumbutsa za lamulo lalikulu, anandifunsa kuti ndigwirizane nayezatanthauzo la lamulo lake.Mulungu anati timukonde ndi mtima wathu wonse, timukonde ndimoyo wathu wonse, timukonde ndi maganizo athu onse, timukondensondi mphamvu zathu zonse. Tikaganiza tonse pamodzi za tanthauzola zimenezi, ndinaganiza ndikulemba za izo; ndinapanga izi mwa inendekha, ndi chiyanjano changa ndi iye; ngati mufuna tikhoza kugawanazomwe tidakamba.Mtima Wathu WonsePamene iye anati timukonde ndi mtima wathu onse. Panali zinthuzapadera zimene iye anali kutanthauza. Kutanthauza kuti tizipeleke kwaiye mwatunthu. Safuna mpikisano pakudzipeleka kwa mtima wathu; ngatindi mvera lamulo lakukonda iye ndi mtima wanga wonse; ndisamalizendi mtima wanga wonse. Ndipange chisankho cha mtima wanga. Tonsefetimasamira pakuzipereka za zinthu zosiyanasiyana.63


Anthu ena amazipeleka pakudya zinthu. Mumayoko ena, kuzipeleka pachakudya chiri chinthu chofunika kwambiri. M’dziko la itale, mwa chisanzoamanunkha chakudya ndi kuti ziri bwino amachipatsa ulemu chakudyachondikuchikonda zedi; ndi kukonda kununkhila kwa chakudya.Mulungu anati sindizakonda kuti ukhale osusukira chakudya mu mtimamwako (mtundu wa chakudya chotere) ndi kuti kodi ichi sichodabwitsachakudyachi ndi chingwiro, chikumukhila bwino, ndi chodyeka bwino.Chakudyachi chiri chokongola m’maonekedwe. Mulungu wati iyayiusazipeleke pa zinthu zopirira, anthu akutayika za zimenezi Mbuye anati,ndifuna uzipeleke kwa ine, osati pachakudya, chakudya m’chabwino komausazipeleke mwatunthu ku icho.M’maiko ena, mdzikhalidwe, zathu mpingo saunvetsa, ndipo kuti mpingosi banja leni-leni. Anthu anapeleka mtima wawo ku mabanja a thupi.Taonani, ili ndi banja langa, mmalo mopeleka mtima wanga kuzimene<strong>Yesu</strong> ananena kukhuza athu a Mulungu ngati banja lake, amakhala ndichidwi chapadera dera anakhalanso ndi Nsanje ya banja anthu awa atindidzina langa lotsiliza la ine.Anthu awa awoneka ngati ine – Abambo anga, Amayi anga ndi Anaanga. Amalora chakudya, mwazi, chinyengo, chikhale chosusa mzimu wachoonadi wa khristu ndikutiuza tanthauzo leni leni la banja pamene ifetabadwa mwatsopano. <strong>Yesu</strong> amati chiani za ichi? Azimayi zana abale ndialongo, amayi anga ndani? Abale kapena alongo? Amene achita cholingacha Mulungu basi.Anthu ena a chipembedzo a ali ndi mtima wokonda banja lawo la thupibasi munjira yopusisa athu kuti asaziwe m’mene tiyenera kukhalira moyowosangalasa Yehova.Ngati ziri m’mene tionere ife zokhuza banja tisamale banja lathu la thupi;ndife oipisisa kuposa anthu osapemphera. Mawu amati, ndithu tikondeakazi athu, amuna athu ndi ana athu. Koma mtima wanga akaziperekapa ichi ndikupatsa khungu anthu ena ndiye zingokhala kuti ine, ine, ine!Uku ndikulakwitsa kwakukuru. Mtumwi Paulo anati kwa ife ndi Mzimuamane anali ndi akazi akhale ngati alibe, umu ndi m’mene mawu anenera.Mawu sakuti, musawakonde akazi anu ndikuwasamala chimodzi amunaanu ndi ana anu. Mulungu anati, ndiri ndi nsanje ndi kudzipereka kwamtima wako. Mulungu akuti uzipeleke mwatunthu kwa ife. Kenakondisazigawa kwa anthu ena tisakhale eni ma banja ndilatengedwa ndi iwomonga a khungu.Mitima yathu ili ya kwa Mulungu, mitima yathu yonse.Ndaonapo anthu akuzipeleka kuzinthu zopusa; amangoyenda mtundawopanda chirichonse.Akhoza kuyima pa nyanja ndikuyang’ana mafunde chifukwa amakondakuona madzi. Muganiza za ine ndi chilengedwe changa. Musatayechikondi chanu ndi kuzipeleka kwanu pa zinthu zonse ndinalenga.Anthu ena amazipeleka ku zinthu za dziko. Amakhala ndi nsanje pa dzikolawo. Mukaonera mpira, kapena kanema, pamakhala mpira wa dzikolonse, dziko ndi dziko kusewera mpira. M’malo amenewa anthu amaimachifukwa timu yawo yalephera. Ambiri amakhala ndi chimwemwe pamenetimu yawo yapambana.Mulungu anati, iyayi mtima wanu ukhale kwa ine basi. Usapelekemtima wako ku zinthu popanda pake. Ukhoza kuonera moira, ukhozakukondwera pamene timu yako ipambana, koma kulira ndi kukondwausiyire ine atero Mulungu.Mulungu wati afuna, mtima wathu wonse, ndikaona zimenezi kubweramtima wanga, kaya ndi pachakudya kapena pa banja, kapena pamaseweraa mpira, ndiope Mulungu basi, ndisazipereka pang’ono ku zinthu za iye.Iye anati, ndifuna mtima wako wonse, ndifuna kuzipereka kwakokonse kwa ine. Ili ndi lamulo, choncho ndichite chimenechi ndikaonamtima wanga ukufuna zina ndi bweze kuti ulowele kwa ambuye basi.Ndilamulo choncho, chisankho chimene ndingapange chikhale chotere.Ndiziperekeletu kwa iye basi osati ku zinthu zina ayi.Moyo Wathu WonseChinthu chinanso ndi chakuti “Moyo wanga wonse” ichi chitanthauzazinthu zambiri. Zikuchitachita ndi mawu woti (kuzikuza) zichitechitendi zinthu zimene muli chizindikiro changa. Ine ndine ndani? Kapenandiganiza kuti ndine ndani? Uwu ndi moyo wanga. Ndakangalika pozilora64 65


ndekha kunyadira pa zinthu zimene ndakwanilitsa. Ndachita zazikulu mumalonda ndipo ndikumva bwino pa zimenezi. Ndikuchimva kuti ndineodala ndikumva bwino ndikuzimverera ndekha kuti zanga ziri bwino.Ndine waukhondo ndipo zanga ziri bwino. Ndine wochenjera ndipozanga ziri bwino. Ndikhonza kupangisa anthu kuseka.Ndikhonza kunena nthano kapena nkhani ndikumva bwino pazimenezi.Ana anga ndimawasamalira, kuposa anthu ena ndimamva bwinopazimenezi. Ndiri ndikusunga kwa zinthu kuposa mmene eana achitira,choncho ndimamvanso bwino. Sindigonja, ena amataya mtima, koma inendine wamphamvu, ndipo ine sindigonja.Uwu ndi “moyo wanga” ndipo uku ndikulakwa kwakulu pamasopa Mulungu kukhuza zinthu zotelezi makhoza kulingalira zambiri.Kumbukirani m’mene satana anachotsedwa kumwamba. Satana anali ndimzimu woti ine, ine, ine nthawi zambiri. Sanaphe mngelo kumwamba.Iyeyu sanaze katundu wa mngelo aliyense. Koma anali ndi maganizooyipa. Anaganiza za yekha osati Mulungu.Iye anati, ndine wokongola, ndizakwera nakhala ngati wamkulu kulu. Ndilinayo mphatso yakuyimba, ndipo ndinawala kuposa miyala yamtengowake, ndiri nawo ufulu woonedwa kuti ndilipo komanso wofunika.Ndiri nawo ufulu woti anthu aziziwa kuti ndilipo, komanso kutchelezakwa ine chifukwa ndine wofunika, ndiwapadera ndili ndi uzimu kuposaangelo onsewa.Mulungu anati, ndakuchosa pakupezeka kwanga Mulungu akuti,undikonde ine ndi mtima wako wonse, uchengetere mtima wako ndi moyowako, kuti undipembeze ine ndikundikonda ndi moyo wako wonse.Mtumwi Paulo anati, ndiri nazo zoti ndikhoza kunyadira, koma ndiyenerakuti ndinyadire mwa <strong>Yesu</strong> ndi iye wopachikidwayo. Ndapachikidwa kudziko ndipo dziko – lapachikidwa kwa ine.Iye anati, ine ndine wamkulu wawo chimwa ndine woipitsisa ndiwochepetsetsa mwa iwo wokhulupira Mulungu. Ndinyadire muzopekazanga, uyu anali Paulo Mtumwi amene anli munthu wabwino. Komaanapanga chisankho chokonda ambuye, ndi mtima wache wonseanakondanso Mulungu wache ndi moyo wache wonse. Sananyadechifukwa chazimene iye anachita kapena m’mene iye anakhaliramuzochita zache.Munthu ameneyu (Paulo) anapita mmwamba nthawi yina kumeneMulungu anakhala. Koma sanafune kunena za zonsezi, iye anati, ndiziwamunthu amane zaka zambiri zapitazo sananyade, ine ndine Paulomtumwi, ine ndinapitako kumwamba. Anali wozichepesa kuti alankhulezimenezi sanafune kuzisangalasa yekha. Sanafune kukhala wozindikirayekha, sanafune kuti azikwezedwa monga Yohane mbatizi, anazichepesakuti <strong>Yesu</strong> mwa iye akwezeke.Nthawi zonse timakonda kuzilabadira tokha pakuganiza za ife tokha,tikuzipatula tonse kwa Mulungu. Nthawi zonse timapanga zisankhozokondweresa tokha; kuposa monga momwe tiriri, tikuzipatula tokhakwa Mulungu wathu. Nthawi zonse tikamaweluza anzathu timayesa kutindife apamwamba kuposa ena; tikuzipatula tokha ndi Mulungu wathu.Mulungu anati undikonde ndi mtima wako wonse. Iwe yense ukondeMulungu ndi zinthu zonse zimene ziri zofunika kwa iwe zikonde inendikutumikila ine upezeke mwa <strong>Yesu</strong> ndi chizindikiro chako chonse.Undikonde ndi moyo wako wonse, upeze chizindikiro chako mwa<strong>Yesu</strong> ndi mwazi wake; zida zonse uli nazo zikuthandize kutumikira ine.Palibe mwini wa zinthu zonsezi ndi Mulungu basi. Tisanyade chifukwacha zomwe Mulungu wachita ndi zake, ndipo ndizaiye yekha. Pamenetimanga nyumba ndi manja athu tikabwera kunyumba imeneyi tisayendendikuti, ee! Ntchito yabwino ndayichita; kapena kuti ndamanga nyumbayabwino; ndamanga ndi manja anga, ndagwira ntchito yabwino pokuzaana anga tisazipatse mphamvu tokha.Moyo wathu uli wa <strong>Yesu</strong> ndi atate Mulungu akuti undikonde ndi mtimawako wonse ndi moyo wako wonse.Malingaliro Athu OnseNdinafunsa atate tanthauzo la zimenezi, ndifuna iwe undikonde ndimaganizo ako onse. Nthawi zina zinthu izi zimasokoneza. Koma chinthuchimodzi anandionetsa chokhuza kukonda iye ndimaganizo wonsemaganizo amane amabwera aziyimilira chisankho chimene ndimapanga.Ngati ndimkonda iye ndi malingaliro anga onse, ndiye pafunika ndizipanga66 67


chisankho pa lingaliro lililonse lobwera kwa ine. Mawu amati, mwa Paulomtumwi tirimange lingaliro lililonse. Tizilisusa lingaliro lililonse loyipalomwe lichite chilungamo.Mulungu amati chiri chonse chabwino chokoma, chiri chonse choyera,choyenera matamando, ganizani za zinthu zimenezi. Paulo amati,timasinthika pamene takonza malingaliro athu.Aroma 8 amati malingaliro amene amatsogozedwa ndi mzimu waMulungu ali moyo Mtendere.Kodi ena mwa inu mumakhalapo ndi mkwiyo wam’maganizo? Kapenalingaliro la Nsanje? Kapena la ukali? Kapena la chilakolako? Kapena lakunyada? Awa ndi malingaliro amene amzionetsela okha mwa iwe. Zilingati munthu wa chichepela walowa m’malingaliro anu ndikuti, ndifunandikuonetseni kulingalira.Mphamvu Zathu ZonseTonsefe tiri ndi zisankho zathu, tsiku lililonse, tizasankha kapena kutimaonekedwe athu apita kapena ayi pamene timkonda Mulungu ndi mtimawathu wonse. Tizasankha zimene moyo wathu watilora kuchita kapenaayi. Moyo wanga wandilora kupeza chizindikiro changa mu zinthu zina,kupatula mwa <strong>Yesu</strong>. Paulo anati, ndapachikidwa ndi <strong>Yesu</strong> akhala wa moyomwa ine. Paulo anaconda Mulungu ndi moyo wake wonse. Chizindikirochake chinali, mwazi wa <strong>Yesu</strong> basi.Anathandauza <strong>Yesu</strong> basi osati chinanso. Ngati timakonda <strong>Yesu</strong> ndimoyo wathu wonse, tizalora mawu a Mulungu ndi malingaliro akem’maganizo athu.Sitizalora, kuphingika, kapena chilakolako kapena mantha ayitizawachotsa m’malingaliro athu. Sitizalora malangizo a mkwiyo, kapenakusakhululuka, kapena Nsanje, kutilamulira ife tizachotsa m’malingaliroathu - sitizakhala ngati anthu a chikunja m’malingaliro koma anthuosinthika ndi otsimikika.Tizakonda Mulungu ndi malingaliro athu onse. Tizaganiza za iyeyekha basi.Atate amandionetsa kuti mphamvu zathu zimatengera zinthu zambiri.Tikamkonda ndi mphamvu zathu zonse ndiye aziwe kuti nthawi yathuili ya kwa iye. Nkhani yathu ili gawo la mphamvu yathu timulore <strong>Yesu</strong>,chikondi cha moyo wathu atiphunzitse m’mene tingapelekele nthawiyathu kwa iye. Sitizalowa zinthu zoononga mphamvu yathu kutionongaife, tizalora chikondi cha Mulungu pasi kuyenda mmoyo wathu, chakudyachathu chikhale gawo la mphamvu yathu.Mfumu Davide mtundu wa <strong>Yesu</strong>, Ambuye akutionetsa chinthu chinachofunika pankhani yakukonda Mulungu ndi mphamvu zathu zonse.Anthu ake akhondo anayenera kuziyiwala pamene iwo anali kumenyankhondo (1 Samueli 21:5)Kuti tichite zazikulu za Mulungu zitengela mmene timagwiritsilantchito mphamvu zathu. Tikagwiritsa ntchito mphamvu zathu pa chinachilichonse, ndikunena kuti ndatopa sundingatumikire Mulungu,pamenepo ndiye kuti sitikonda Mulungu. Tizipanga chisankho chimenechingatipatse mphamvu zotumikira Mulungu mu nyengo zonse.Ndalama zathu ziri gawo la mphamvu zathu. Ndalama zimachokeraku ntchito ya manja athu. Gawo la chisankho chimene timapangapogwiritsa ntchito ndalama timatengera mphamvu zathu. Mtumwi Pauloanati, pamene iye anayenda mzinda ndi mzinda dziko ndi dziko. Anati,chifukwa ndasintha moyo wanu ndakupatsani choonadi chauzimu; ndirindi ufulu kukuuzani kuti mundipatse ndalama pa zonzezi.Munkhozanso kudnipatsa mkate, koma iye anati, iyayi, ndikupatsanichisanzo cha momwe ndimagwirira ntchito ndi manja anga; usana ndiusiku kuti ndikhale wakuthekera kukupatsani ngakhale moyo wanundifuna chifukwa cha zinthu za uzimu. Ndakuphunzitsani, sindifunakukuuzani, kapena zovala zanu, ingakhalenso ndalama. Ndinena njiraya momwe ndingachitire. Ambuye wati, kupatsa kumadaritsa kuposakupeleka; kotero ndizeza ntchito ya momwe ndingachitire nanu.Paulo anati azera njira imene angathandizike nayo kuti atumikireMulungu.Mawu akuti tizipeleke matupi athu ngati nsembe ya moyo, ndi gawo lathupi lathu ngati zida za chilungamo. Paulo ndi atumwi ena a Mulunguanapachika matupi awo chifukwa cha kusagona tulo ndi kutopa.68 69


Amapachika thupi lake pena akakhala ndi njala, kapena kulumidwa ndizigawenga.Pamene amaenyedwa nakhala tayile wakufa mu mzinda, chifukwa chakutianaconda Mulungu ndi mphamvu zake zonse. Analalikilabe mawu osatopaingakhale anaganiza kuti iye wafa. Petro ndi Yohane anali ndi mabala azowawa zomwe anamva chifukwa chotumikira <strong>Yesu</strong>. Analalikirabe zankhani ya bwino ya <strong>Yesu</strong> Khristu.Stefano, Yakobo, Yohane mbatizi – anazipeleka kwa anthu potumikira<strong>Yesu</strong> ndi mphamvu zawo zonse. Ifenso tisakonde moyo wathu okha komaMulungu, ngakhale mpaka imfa itipeze tikutumikira <strong>Yesu</strong>, tiyeni tidalire<strong>Yesu</strong> nthawi zonse.mtima wathu wonse, moyo wathu wonse, komanso mphamvu zathu –zonse. Akaona wina pafupi ndi iwe akhoza kukhala mbale kapena mlongo,sakonda Mulungu ndi mtima wawo, moyo wawo, kapena mphamvu zawo,Mulungu akuti tiwathandize kuti azitero.Akuzitora okha komanso panthawi yomweyo abela Mulungu, tikatero,mpingo uzakhala chinthu chakuKoma zimenezi zimayenda ndi ife ngati munthu m’modzi. Mawu akutimkondeni iye ndi mtima, moyo komanso ndi mphamvu zanu zonse.Ichi chinali chakwa ine pakatipa ine ndi Mulungu, koma ngati ndizothandizakwa inu, pamenepo ndingati ndinali nawo mwayi woti tikambirane.Kulowetsa Kwa KuyaNditamfunsa Mulungu za ichi kuti chitanthauzanji? Ndinadabwa yankholomwe iye anandipatsa akundifuna kuti ndimukonde iye ndi mtimawanga wonse. Chifukwa iye ndi Mulungu wa Nsanje afuna ndimukondendi moyo wanga wonse, chifukwa iye ndiwa sanje. Afuna ndimukondendi malingaliro anga onse. Ndikalimbana nazo zimeneyi ndikuona kutimoyo wanga ukuyandikira ku zimenezi, ndiona kuti iye akunditengelakw a<strong>Yesu</strong> mozama. Akundipanga ine wanzeru, ndiwokonda komansowomasuka. Akhonza kupangitsa mitsinje ya madzi kuchoka mwa inemonga <strong>Yesu</strong> analonjeza, akhonza kuzika zinthu zodabwitsa mwa ine ndimphamvu yake, akhoza kuyika zida za chilungamo kudzanja langa lamazere ndi lamanja.Eliya munthu ngati ife analamula mitambo isavumbitse mvula,amalamulanso kuti mvula igwe ndipo inagwa. Mawu akuti, Eliya analingati ife, palibe chovuta ndi ife ngati tiri ndi <strong>Yesu</strong>, ndikukonda Mulungundi moyo wathu mtima wathu ndi mphamvu zathu zonse. Anthu ambirisakonda Mulungu ndi chiri chonse chawo. Mukondeni Mulungu ndimtima, moyo ndi mphamvu zanu zonse.Ndikuthandizana Wina Ndi MzakeGawo liomdzi lakukonda iye limachita chita pamene ife tikonda anzathuamene tikhala nawo limodzi. Kuwakonda ndi zonse zomwe tiri nazo70 71


Mapelekedwe A Ndalama MuUfumu Wa MulunguOctober 6, 1999 Lilongwe, Malawi AfricaKu mpingo umene ine ndimakhala kulibe aliyense amene amalipidwandalama palibe aliyense amene amatenga ndalama kwa iwo wokha palibensoamene amaphunzitsa kuti apeze ndalama. Koma aliyense ali otanganidwakupereka monga takhaliramo sitiyendetsa nsengwa koma koma winaaliyense amathandizidwa ku nchito ya Mulungu mu chuma. Pali anthuambiri amene amapatsidwa udindo mu nyumba mwawo mwa nseri umeneabale ndi alongo amapereka pochita zimenezi timafuna kuti dzanja lamanjalisadziwe zimene la manzere likuchita. Sapita kutsogolo kukapereka ndikuona anthu onse koma amapereka kuchokera pa mtima pawo.Pali zinthu zambiri zimene anthu ayenera kupereka. Abale ena amaikamu enevolope ndi kujlemba kuseri kuti zigwire nchito yoti. Akhozakuti kwa “osauka” kuti amene ali osowa pakati pathu kapena mu maloamene timakhalamo angalembenso “zosindikizira mabuku” Mongamwa mabuku amene mwalandorawa ambiri oyera mtima anaperekazopeza zawo chifukwa linali pemphero lawo ndi mtima kugawa choonadichimene chinali chopambana kwa iwo. Ena angathe kupereka kwa mbaleamene akutumikira Ambuye kwambiri, mwina ali ndi ulendo wopitakwina. Sali pa ntchito yomwe amagwira koma chifukwa akufuna kutiakakhale ndi okhulupilira ena kwina amapereka mbali ya zopereka zawopa chifukwa chimenechi.Kulemba kuseri kwa enivolopu kumathandiza kulumikiza miyoyo yawo pazimene zikuchitika. Osangopereka ndalama mosawonetsetsa mu nsengwaai. Koma ndalamazo zikuimira nchito ya Mulungu. Pamenepo ayenerakulumikiza ntchito imene ili yofunika ku maganizo awo. Sangadziwe kutisabata ino akapereka kwa ndani ndiye angaike kuti atsogoleri pali zambirizochitika ndithu.Mu zaka zoyambilira Chikhristu nthawi zina anthu amaguritsa nyumbandi kuika ndalama pa mapazi a tumwi ndi kutumizidwa monga kufunikira73


ndiye nthawi zina zimatero. Kwa nthawi amapereka kwa zinthu zodziwikabwino chifukwa palibe amene ali kuona zingakhalenso ndi ulesi chifukwadzanja la manzere silikuona la manja. Mungakhale aulesi mukuperekakwanu. Aliyense ayenera kukhala osamala kuti asalore izi kutero. Anthuambiri ku Amerika amalandira pa ssabata iliyonse uku ndi chabwinokukumbutsa kuti atenga ndalama ku ntchito ya Mulungu. Kodi zayankhafunso lanu? Palinso lina? Kodi ndasiya zina zimene zikanathandiza.Nanga Za Chakhumi?Chiphunzitso cha chakhumi sichili mu Chipangano chatsopano ngatimukufuna kupereka chakhumi ndiye kuti muyanera kupereka nsembeya nyama. Ndi chiphunzitso cha Chipangano Chakale. ChipanganoChakalelinali kumvera pa zimene Mulungu ananena kwa anthu ake muChipangano Chakale. Chakhumi sichilinso mbali ya nsembe za nyamakapena munthu woyera kapwna wa nsembe kapena kupembedza kwakuasinsi zinali mbali ya phangano la mwazi wa <strong>Yesu</strong>, Sali chakhumimulibenso. Palibe kupereka chakhumi mu mgwilizano watsopano.Anthu amapeza ndalama kwa nkhosa za Mulungu pazogula (zomanga zachipembedzo) ndikulipira malipiro kwa anthu. Potenga malamulo akalendi malembo kuti anthu a Mulungu apereke, motero anthuomwewasanenanso za loweruka monga (sabata) kupembedza ku Yerusalemumkansinsi) kapenanso nsembe za nyama zimene zili mu gawo limeneli.Ndi kusakhulupilika kuchotsa zinthu zina ndi kusakhulupilika kuchotsazinthu zina ndi kulowetsa zina ndi kuti zinthu zidzikhala motero.Paulo aanaphunzitsa ndithu kuti tinafa ndi machismo athu ndi mwaziwa <strong>Yesu</strong> ndi osakwanira kwa ife ngati tikhale mu pangano la kuumbalandi kusunga sabata ndi kupereka Chakhumi. Palibe gawo lina kupita kwambusa mu Baibolo. Iyi sinjira ya Mulungu.Mu pagano ili Mulungu amafuna ndipo alikufuna kuchokera mu mtima ndikuti zichokera mu Mzimu. <strong>Yesu</strong> anati ngati mungapambane chilungamocha Afarisi simungathe kulowa mu ufumu. Mu pagano limeneli liyenerakukhala mu UBWENZI mu moyo, chikondi chalero ndi Messiah.Kupereka kwathu mu pangano la tsopanoli liyenera kukhala kudziperekamonga mwa kulamula kwake ndi kumvera kwa Mzimu wa Mulungu tsikundi tsiku.Pamene <strong>Yesu</strong> anaima pa kasinsi mkati anaona mzimayi amane anaperekakwambirimu choperekera ndalama sizidali zochuluka ai monga mwamyezo. <strong>Yesu</strong> sanati anapereka gawo khumi. Sanaperekanso chakhumikoma anapereka anapereka ndalama zake zogulira chakudya. Mulunguanali opambana kwa iye koposa chakudya. Anakonda Mulungu wake ndimtima wake wonse moyo, Maganizo ndi mphamvu zake zonse. Sanalifkufuna njira yoperekera mbali ya gawo. Amafuna kupereka Mphatsoimene inalipo ndipo <strong>Yesu</strong> anati Taonani mzimayi uyu Angelo ali kuimbanthungululu ndi kuomba mmanja kwa iye chifukwa sanaganize zachakhumi anapereka mtima wake wonse, maganizo, moyo ndi mphamvuzake zonse. Uwu ndi uthenga wa Chipangano Chatsopano ndipoChipangano chakale ndi chofooka monga mmene chilili.Popanda CholowaPamene Paulo amalemba kwa mipingo anati, “sitifuna phindu ku mawu aMulungu.” Paulo samaona ku Mphatso yake ngati chinthu choti amangireanthu osati kuti apeze ndalama kuchokera kwa anthu. Iye anayesetsakupereka monga tanena kale ena anazipereka kuti mabukhu amenetabwera nawo asindikizidwe. Sitikugulitsa mabukhuwa tikuperekamabukhuwa kwa inu ndi kwa ena onse. Ziphunzitso za mabukhuwa ndia <strong>Yesu</strong> osati Iye <strong>Yesu</strong> anagawa zinthu zimenezi kwa ife mwaulere ndiyendithu tifunanso kugawa kwa inu ulereNdikujyembekeza kuti sipakhala wina ogulitsa limodzi la mabakhu kwaaliyense. Ndi Mphatso imene <strong>Yesu</strong> wapereka kwa inu, ngati ndi chiphunnzitsongati ndi nzeru ngati ndi chidziwitso ngati ndi kuimba kapena kusewera ndichoimbira ngati ndi kuthekera kwa kulankhula bwino ndi zinthu zimenezaikidwa ndi Ambuye kuti muzisalire ndipomphatso imeneyi ndi ya <strong>Yesu</strong>koma waizeza kwa inu kuti zipindulire anthu ena tsiku lina <strong>Yesu</strong> analankhulandi Afarisi ngati mungapemphere kuti ena akuyamikireni ndiye kutimwalandiratu phindu lake izinso ndi zoona mu nkhani ya ndalama. Ngatimungaphunzitse kapena kuelmba nyimbo kuti ena akulipireni ndiye kutindalama imeneyo ndiye malipiro anu. Koma ngati mukufuna kuperekamwaufulu pa zimene <strong>Yesu</strong> wapereka kwa inu ndipo malipiro ndi akulu.Madalitso ake ndi ochuluka mu miyoyo yokuzungulirani ndipo uzdakhalakulemekeza Mulungu.74 75


Mu zochitika zinanso, aliyense anachita chiganizo kwa Mulungu musabata inailiyonse monga angakhalire opereka mmene angaperekerezinthu zawo pakati pa iwo ndi Mulungu amapanga cholinga chifukwachoti amamukonda ndi mtima wawo wonse. Amachita chisankho ndiyeamaganiza kuti angapereke ndalama zimenezo. Pali okhala nawo pafupiamane abale oyera mtima amakhala nawo pamodzi. Timaika box kumodzikwa nyumba zotere ndiye abale amene amakhala mu zinyumbazi zakumeneko amapita mwakachetechete ndiye amapempha Mulungu kutialandire Mphatso yawo. Analemba kalata ndi Mphatso ndi nchito yakeimene yaperekedwera ndiye amaika mu choikira ndi kuchoka.Ndiye tili ndi abale awiri kapena atatu amene amapita ku zinyumbazimenezo (midzi yaing’onondiye amatenga ndalama kuika malo amodzindiye abale osankhidwawa, okhulupilika amagwira ntchito pamodziamatenga ndalama zimene zalembedwa kwa osauka ndi kutumiza kwaosauka mokhala mwathu. Ndalama zimene zaikidwa kusindikiza mabukuodzafika ndalama zonse pamalo amodzi ndi kupereka kwa iwo ameneamasindikiza, ngati pali mbale kapena mlongo amene moyo wawo easinthamabanja awo asintha pa Mphatso ya anthuwo angathenso kulemba dzinaangathenso kulemba dzina la munthuyo ndiye abale okhulupilidwaamagwira ntchito pamodzi amapereka kwa iwo amene maina awoanalembedwa pa envolopu kuti alandire moyenera. Monga Paulo abaleenawo ndi alongo oyenera kupanga ma tenti kapena nchito ina chifukwaPaulo anakhuzidwa ndi miyoyo ya anthu ku Filipi ndi Atosolonika,amatumizira Mphatso pa ntchito kumeneko ndiponso amawasamiraena osowa ndi Mphatso. Amathandizanso abale ena monga Timoteyondi Taitasi ndiye kuti sanali kumanga tenti nthawi ndi nthawi mu kalatayak u Afilipi. Paulo anati timalandira nthawi zina ai. Nthawi zina analukamatenti nthawi zina ai. Ngati Mulungu amawathandiza pa zosowa zawomu njira ina ndiye kuti zinali zabwino ngati ai. Anali kumanga matenti ndikuthandizanso anthu ena. Popanda vuto choncho abale amene amatolorendalama anagawa kwa amene dzina lake lalembedwa pa envolopu ndiyesatenga kanthu paiwo wokha kodi zikumveka zimenezi.Pamene wina akupereka ndalama kwa mzake amene wasintha moyo palibeamene amati alandire ndalama chifukwa kuti moyo wake wasinthika.Palibe amene amati ndilandire ndalama. Aliyense amafuna kutumikira<strong>Yesu</strong> pa Mphatso ili yonse ali nayo. Aliyense osati abusa ndi anthu enaonse. Aliyense mphatsozina ndi zothandiza. Pamene Mphatso zimenezizikuthandiza inu timafuna kuthandiza mwaulere kuti Mphatso ithandizeenachoncho nthawi zina zimachitika koma osati chifukwa wina akuchitamalonda mau a Mulungu ku phindu. Cholinga chawo ndi kuthandizandi kutumikira sakufuna kupeza ndalama susunthuka kwa iwo kumangakwa nthawi zaka zisanu kapenanso amasulidwa kwa nthawi amatumikiraAmbuye ndi moyo wawo nthawi zonse. Izi ndi zosiyana mmene dziko lachipembedzo limachitira. Anthu amaona mau a Mulungu monga ntchiyo.Sintchito monga umisiri wa matabwa zimenezi mulibe mu Baibolo.Ndi Bwino KuperekaTiwonjezenso <strong>Yesu</strong> amati tikudalitsika kupereka koposa kulandira ndikwabwino kulandira koma kwabwino kupereka koma sikwabwino kufunakupatsidwa osati ana anga akandiuze abambo, abambo tipatseni kanthuine ndi kumapitiriza ndikulira. Chimene ndingapereke ndi monyinyirikakoma ndikuona ana anga ali kugawa ndi ena ndi kukonda anthu ena .Ndidzakhuzidwa ndi kumudodometsa ndi Mphatso. Izi ndi zoona mubanja la <strong>Yesu</strong> pasaoneke wina amene ali kuumiliza kuti alandire ndalamapalibe amene anene mau anati, tili ndi zonse mofanana muyenerakundipatsa ndalama wina asadziyerekeze kunena kuti malemba amati,“ngati uli ndi Malaya awiri pereka limodzi kwa mbale, muli ndi Malayaawiri linalo ndi langa kumeneku ndi kuchimwira kumeneko ndiyekudzikonda choncho ngati wina ali kuumiliza ndalama kapena kena kalikonse mpingo usamupatse kwambino kuti awawitsidwe mtima ngatizoonadi kuti ofunikadi kuthandizidwa ndipo abale aonadi kufunika ndimu chikondi ndi kufnika kugwira nchito ya <strong>Yesu</strong> amapereka ndi zabwinondipo ndi zobvamerezeka.Aliyense Amagwirira Nchito Mulungu Kwa NthawiYonsePamene Paulo anayenda kuchokera mu mkzinda ndi mdziko kuphunzitsaena, Paulo sananene inde ndine mtumwi wa Mulungu wapamvandu!Sindingadzitsitse ndekha kupanga matenti. Ndine mtumwi wa Mulungu76 77


wamoyo. Paulo anali kupanga matenti pamene amafuna ndalama ngatiMulungu amampatsa mu njira ina zinali bwino koma sanali odandaula kutiali kumanga matenti. Ngati amamanga matenti ndiye kuti amakuna ndianthu amenenso amachita chomwecho amene amafuna nsaru zopangiramatenti anthu amene amadzagula ,matenti amene amawamanga ndizimene iye amachita. Iye samasamala kuti anthu apeza ku msika kapenansomusunagogi, moyo wake wonse unali kukonda Mulungu ndi anthu ndikwa anthu onse mu nthawi ina iliyonse ngati anali ku ndende amayenerakumusandutsa wa ndende ngati anali pa maso a mfumu kudikira mulanduamayesa kusandutsa mfumu ngati akupanga tenti amayesa kusandulitsaomugulawo mmene amapezera moyo wake sizinasinthe kanthu kali konse.Ngati Mulungu apereka zosowa kuchokera kwa abale ndi alongo ameneakonda Iye ndipo ali oyamika ndipo anali omasulidwa kumanga tentikwa kanthawi ndiye anali ndi mpata woyenda nkdi sailasi ndi abale enakupita ku mizinda ina ngati analibe ndalama monga mmene ananeneramu kalata ya Afilipi monga amachitira. Amapanga matenti kwa kanthawipopanda bvuto.Miyambo ya anthu zatiphunzitsa ife zoipa pa kunena kuti ndife azitumikia Mulungu. Paulo anali wamtumiki wa mphamvu koposa anthu ang’onootenga ndalama kapena osatenga ndalama. Paulo amagwira nchitomolimbika ndi manja ake usiku nsi usana ndi kulipira chakudya changapamene ndinali ndi inu. Mukandipezera chakudya koma ndinalipirandekha ndimagwira nchito molimbika ndimanja potero kuti tikwaniritsezosowa zanga ndi ena.Ngati ndizoona mu Mphatso yaikulu monga Paulo bwanji Mphatsozazing’ono zinaganiza kuti ndizosafunika kuti asamagwire nchito ndimanja awo? Ngati Mulungu angatithandize mu njira zina ndabwinokoma tisayembekezere kapena kuwumiliza. Ngati anthu a Mulungu alindi mtima opereka ndi kutimasula kuti tisamange matenti ndi zabwino.Ngati titumikire tiyenera kupanga matenti ndiye tidzapanga matenti ndikutumiza kwa zosowa za anthu ena.Choncho zimenezi ndi zimene takhala tikuchita kwa zaka khumi ndizisanu(15) kwa iwo ambiri anali a Zimbusa kapenaso atsogoleri anasiyamalipilo awo ndi zolandira zawo ndipo Mulungu wakhala okhulupilikandipo palibe mwayiwo ali ndi njala ndipo ali kutumikira Mulungu nthawizonse. Oyera mtima onse ndi ana alikutumikira Mulungu nthawi zonse,satumikira Mulungu polandira ndalama amatumikira chifukwa chachikondi ndipo Mulungu amawapatsa njira zosiyanasiyana. Ichi ndiyechoonadi changwiro koma ndichochititsa mantha nthawi zina kutitisiye miyambo ya anthu. Pamene ndalama sizikhalanso mumatumbaathu palibe amene anatumikira Ambuye munjira imeneyi, Mulungundikulephera. Ambuye ndiokhulupilika ndipo amasamala akhwangwalaake, amasamalanso mbalame zamulengalenga, amasamalanso iwo ameneakonda iye. Palibe opambana anzawo muchikristu.Palibe muchikhristu pamene anthu amagulitsa mphatso zawo, pamene enaalibiletu mphatso. Palibe amene agulitsa mphatso yake mumpingo ndipoMulungu amaona aliyese monga kufunika kwake, ndipo Mulungu ndiyeamafuna kuti kuchitike ndi zofunika zathu. Ndiye atumiki ake Amulungunthawi zonse amatumikira kaya ndi kusika, kapena ku ndende,kunyumbakwathu zonsezi ndi choonadi chofunikira. Tiyenera kugwedeza mtengowa miyambo ya anthu ndikuyigwetsa pansi. Mulungu ndiokhulupilikandipo azatiteteza ife ngati tichita chomwecho.Mwachitsanzo ambale ena ndi alongo anafunitsitsa kuti ife tibwere kunosikuti tidangoganiza choncho kapena kuti ndife odziwika, kotero kutitingapite kwina kulikonse. Sitili monga choncho, ndife akapolo chabemonganso inunso muli. Kunali kufuna kwao osati kwathu aziperekansokulipila zithu zina, pamene ife tili kuno.Sitinawafuse kuti atero . Anthu amulungu amamva Mulungu ndikuganizapamodzi kuti tibwere, ndimmene zinakhalira.Mayeso amene <strong>Yesu</strong> anawapeza pakati mkachisi ndi amene ali ofanafanandiamene ifenso nthawi zina timakhala nawo, sichoncho?Kodi tikhulupilira zimenezi?Funso (La Msiska) Pamene tafuna kupereka uthenga wa mfumu ndi umfumuwake ndi abale amene ali kuchipembedzo pokhudzana ndi ndalama zimeneiwo amalandira tingawauze chiyani pokhudzana ndi ndalama zimeneamalandira? pamene iwo adalira ndalamazo pa moyo wawo.78 79


Ngati munthu afuna kukhala kuchipembedzo chifukwa cha ndalamaMulungu adzamuweruza kwambiri. Ngati munthu akana choonadi chaMulungu chifukwa cha ndalama, ndiye kuti ndiwopembedza wa Satana.Tikulankhulazi siza ndalama! Izi ndi za Mulungu, amene ali wamkulukoposa ndalama! Tiyenera kunkhulupilira Mulungu ndikumumvera iyemuzowawa zonse. Ngati ndizowawa za m´banja kaya ndi nyumba, kaya ndintchito, kaya ndalama zathu zonse-zimenezi ndizithu za <strong>Yesu</strong> zomuyeneramuzilizonse zokumana nazo.Petulo ndi Yohane adati, “siliva ndi golide NDILIBE. Koma ndilindi <strong>Yesu</strong> ameneyo ndikupatsa iwe”.Ngati chipembedzo chimwazandalama kwa wanthu ndiye kudalira kwawo, ndipo anthu amenewoakayamba kumvera <strong>Yesu</strong> polandira zowawa zilizonse, chithu chimodzikapena ziwiri zidzachitika choyamba kuchitika, ndiye choonadi chaMulungu chidzabwera chipembedzocho ndikusintha chipembedzochonsecho. Anthu adzayamba kupeleka ndalama chifukwa miyoyo yawoyasinthika. Chinanso chidzachitika kuti chipembedzocho chidzasiyakupeleka ndalama. Ndipo ngati asiya kupeleka ndalama……. Ndiyekuti “ZIDZAKHALA CHONCHO!” Ambuye adzapereka kwa omverandiokhulupilika.Kodi timankhulupilira kuti Mulungu ali ndi ng’ombe m’mapiri? Koditimakhulupilira kuti tikafunsa iye m’dzina la <strong>Yesu</strong> adzatipatsa? Koditimankhulupilira kuti amatikonda kwambiri koposa khungumbwi ndimaluwa ammunda? Kodi chingakhale kuti ndi chipembedzo chabechofuna kupeza zithu mwa ife tokha? Ngati mutsata njira ya Mulungupotsata ndalama, kapena ngati munyengelera ndikusiya choonadi chaMulungu chifukwa cha ndalama ndiye ndikuuzani chithu chimodzimonga Paulo adati kwa Simoni wa nyanga. “Iwe ndi ndalama yako utaikanayo ku Jehena” Tisakhudzidwe ndi ndalama. Tinkhulupilire Mulungundikumvera Mulungu muzowawa zili zonse iye ndiye atate odabwitsaamene akonda kupeleka mphatso zabwino kwa ana ake.Ganizirani zimenezi……..Pamene Ethiopia lidali dziko la chikristu ndipo anthu ndikumaopaMulungu,Ethiopia adatchedwa mkate mundengu la Afrika.Chabwino ndi Mulungu amene amamvubwitsa mvula, kuti mela ukule ndiziweto kusangalala ndiponso dziko kutukuka. Pamene Ethiopia anakhaladziko la chisilamu ndipo chihristu chinapeputsidwa, Mulungu anaweruzadzikolo ndipo mvula inasiya kugwa. Ethiopia lero ndichipululu osatimkate odzadza.Siyani ndi kuganizira zimenezi chifukwa chimene ndikulankhulachi ndichimene chimabwezeletsa choona mmbuyo. Ngati tidzamanga nyumbaya Mulungu osati mmamangidwe athu ndipo ngati tidzapeleka tokhapoteteza chuma chathu ndiye kuti Mulungu adzakulitsa mbeu yathu.Adzagwetsa mvula, ndipo ma bizinezi athu adzatukuka, ndipo adzapezanjira yotisamala pa zofuna zathuNgati Njira ina tiziteteza tokha ndi kunyengelera pakusamvera choonadichichifukwa cha mantha pa zimene zingatigwere, ndiye Mulungu adzatilanga.Kotero kuti matumba athu adzakhala obowoka . Ndalama zomwetimaganizira zizizakhalanso motero. Mbeu zomwe tizabzala mmundazizakula moyenera koma ngati tikulupilira Mulungu adzatisamala ifetonse choncho ngati sitimvera adzatiweluza ife monga anena( HaggaiChaputala Choyamba)Ndiliti Mulungu adzakhala ndi athu amene amukhulupilira iye kotheratundi kumvera iye mu zowawa zirizonse? Kodi mudzakhala muli inuyo?Ngati sichoncho mudzaola . Mudzakhala opambana mu ULEMELEROWA MULUNGUAmbuye Mulungu wamphamvu , choonde mvetselani pempherolathu tsopano, Tikupemphani inu tsopano kuti mutsegule kumwamba. Choonde pitilizani kuthila bvumbulutso kwa abale ndialongo okhulupilikawa, pitilizani kuthila mafuta a chikonwelerokwa iwo amene amvera. Pitilizani kumanga mpingo wanu ndinzeru za kuya Chikondi ndi kudzipeleka kwaiwo onvera inumudipo lilonse tikupemphaninso Atate Mulungu monga mwamalonjezo anu mubuku la Detolonome kuti mudzabweretsamatembelero ndi ma weluzo kwa iwo osamvera inu tikufunsaninsokuti mukhale Atate athu ngati tikonda ndi kumvera inu tikufunsanikuti mukhale oweruza ngati sitimvera inu tikudziwa kuti simufuna80 81


kubweletsa zoipa koma tidziwa kuti tiyenera kumva zowawapokonzaso mizimu yathu tikupemphaninso kuti mukonze mitimayoumitsa ngati tili nayo tikupemphaninso kuti mutikumbatirendi kuthandiza kufowoka kwathu. Chonde chotsani kuukilakwathu ndipo mutithandize pa kufowoka kwathu . Tikukuitananitambasulani nkono wanu kuti muchite zonse munjira yaUmulungu. Tidziwa kuti inu mulipo wamoyo ndi waulemelero.Awa simasewera chabe sikuti tikungokusankhani inu kukhalaMulungu wathu.INU NDINU MULUNGU, Ndipo tiyenera kugwadira inu. Ndifeopusa ndi ofowoka nthawi zonse, koma tikuitanani kuti tikhaleabambo ndi amayi a Mulungu, onongani kuwukira kwathu.Tipeleka ullemero kwainu Oyamba ndi Mlengi okonda miyoyoyathu ndi mmisiri wa mpingo wanu,lilemekezeke dzina lanuAMENKufunduka Kwa Gulugufe.October 1999, Africa.Funso: Pamene tikugawana ndi anthu choonadi cha <strong>Yesu</strong> ndipo anthu akufunakulapa ndi kufuna kutuluka mu zipembedzo zawo, Tingawauze chiani?Ngakhale kuti anthu akufuna kuchoka muzipembedzo, ndizabwinokusakana ngati kungatheke chifukwa chache ndi ichi; ngati atadziwa,kapena apeza choonadi chi cha Mulungu monga kulapa machimo kwa winandimn’zake, kutengelana zo thobwetsa, kuchengetana wina ndi mnzaketsiku ndi tsiku, ndi kuchotsa chotupitsa pakati pa abale. (Choonadi ichichakhala chili mu Baibulo kwa nthawi zonse, koma chaiwalidwa kapenakuiwalidwa kapenanso kutchutsidwa) ndiye ayenera kugawa zinthu izikwaanzawo apafupi. Tiyenera kukankha anthu kuti atenge choonadi ichichimene aona kuchokera kwa Mulungu ndi kugawiranso kwa anthu enaamuchipembedzo.Ali ndi abwenzi ndi apabanja amene ali m’bali ya chipembedzo.baibulo limati amene wapatsidwa kukhulupilidwa ayenera kusonyezakukhulupirlika pa chinthucho. Ngati munthu amene takumana nayeyoali ndi mphatso yochokera kwa Mulungu kudzera mu mau a Mulungu,atenera kukhala okhulupilika ndi omvera ndi mgwilizano umene ulipokale pamene anthu ali omvera ndi okhulupirika ndi mgwirizano umeneulipo, ndiye kuti zinthu chimodzai kapena ziwiri zidzachitika. Miyoyoya ambiri kapena monga Yeremiay, munthu amene akuyesa mukukhalamu choonadi cha Mulungu adzachotsedwanso nawo pamodzi, ndikuthamangitsidwa kuchokera mu chipembedzo.Koma amene walapa potulukira kunja kwa chisteko sakukhalaokhulupirika ndi choonadi chimene Mulungu wapatsa iwo. Ngati mulimu Hotela ndikuthawa fugo la usti ndikuona kuti muli moto ngatimungothawira kutulukira kumbuyo kwa chitseko mudzakhala ndi dzanjapa anthu amene afawo. Ngati wina wadziwa kuti chipembedzo chili kupsyausangowasiya kuti atulukire ku mbuyo ya chitseko. Timawaphunzitsaanthu kufuura pamwamba pa nyumba, “Dziwani njira za Mulungu!82 83


mvelani Mulungu! Ndili ndi uthenga wabwino - zilipo zambiri zimeneangakhale tsopano sitinadziwe pa choonadichi! Tingamasulidwe kuchokakudziwe pa choonadichi! Tingamasulidwe kuchoka kuchimo! Tingakhaleanthu amodzi m’malo mwake kapena otayanatayana aliyense! Tingakhalempingo woona umene makomo andende akufa sangathe kupambana.Choncho timawapempha anthu kuti akhalebe mu chipembedzo ndikukhala okhulupirika ndi mabanja awo ndi abwenzi awo ndiye mirakuluidzaoneka kapena adzathamangitsidwa koma sitimalora kutuluka kumbuyo kwa chitseko pamene fungo la moto lawoneka.Ngati aliyense ndi omvera munjira imeneyi ndi kuitana wina ali yensekukhala okhulupirika mu njirayi, ndiye kuti siife amene akumangampingo wake. Sitikupeza anthu anthu amene amaganiza monga ifetimaganizira. Tikufuna kuti wina ali yense amvere njira ya Mulungu. Kutikonse kumene ali ndipo pamene <strong>Yesu</strong> agwedeza mtengo zipatso zabwinozimagwa. Akhonza kukhala anthu khumi abwino mu chipembedzocho.Angakhalanse anthu zana limodzi mu chipembedzocho. Koma ngatiwina athawira kukhomo la kunja ndi kusiya chipembedzo kachete chete,ndiye kuti pali anthu khumi kapena zana amene anakatha kusinthikamiyoyo yawo ndipo sadzadziwa.Ngati muli ndi khungwa lagulugube ndipo mutenga reza ndikutsegulamkati mwa Gulugufe, sadzauluka. Ndi ndondomeko yomenyera Gulugufeimene Gulugufe amakhala ndi mphamvu wowulukira!Afunseni anthu amene ayamba kale kuwoona choonadi ichi cha Mulungukukhala ndi kukhulupirika ndi anansi awo ndi mabanja awo asanyengelereayi komanso kukhotera mu kusamvera. Afunseni kuti aime ndi kulimbikamuchoonadi chimene apeza kuchokera kwa Mulungu. Ngati adzakhalaokhulupirika, omvera, olimbika, ndi kulola kupeleka dipo posawelengerakukanidwa, ndipo adzakhala monga MBOZI imene ikusandulikaGulugufe ndi kuchoka mu chikhombe chake.Anthu ambiri adzaphunzira njira ya Mulungu pakukanidwa kumenekwachitidwa ndi moyo wawo. Ndiye sitiba kukula kuchokera mudulapoyera chikhungwa ndi kutenga Gulugufeyo. Timayetsetsa kuti njirayotulukira ipezeke - choncho kuti AKHONZA KUWULUKA.Zochitika Mu Dziko LaChipembedzoOctober 2, 1999, Salima, Malawi, AfricaNdifuna kulankhula nanu kwa kanthawi yochepayi za anthu a Mulunguamene anakhala zaka zikwi zitatu zapitazo. Amenewa anali Aisrael, adalindi kachisi ku Yerusalem pa phiri lotchedwa Wazion. Linali nyumbayomangidwa. Idali yokutidwa ndi Golidi ndi kukutidwa ndi matabwaokongola. Nthawi zambiri pa chaka anthu amabwera kunyumbayi. Analindi masiku opatulika. Anali ndi nthawi yopuma imene ali kukumanako.Anali kupeleka nsembe kwa Mulungu. Anali kufuna kubwera pafupi ndiMulungu. Ansembe anali kuthandiza anthu ku Kachisi. Ansembe analikuthandiza anthu kufika pafupi ndi Mulungu, Ansembe amapeleka nsembeza nyama. Ansembe anali kupha nyama ndi kuwaza mwazi pa guwa kutimachimo a anthu akhululukidwe ndi kufika kwa Mulungu pafupi.Izi inali zaka zikwi zitatu zapitazo, tiyeni tilankhule za anthu alero.TIlankhure za Israel woona. Abale ndi alongo ngati munapereka moyowanu kwa <strong>Yesu</strong> ndinu Israel woona wa Mulungu, Amen ngati munapelekamoyo wanu kwa <strong>Yesu</strong>. Ali mfumu yanu ndinu Israel wa Mulungu.Ndinali kukhala pano ndipo ndinaona munthu alimkututsa, pamene alikudutsa panali chithunzi kumbuyo kwake. Pamene munthuyo amayenda,chithizichonso chimayenda pamene anakweza dzanja lake. Chithunzichosochimakwezanso dzanja, chithunzicho chinali ndi miendo. Chithunzichochinali ndi mutu. Kodi chithunzicho chinali munthu? Ai, chithunzichosichinali cichinali cheni-cheni. Chimaoneka ngati munthu. Chimayendamonga munthu koma mafanizidwe a munthu. Abale ndi alongo ana aMulungu mu zaka zikwi zapitazo anali mthunzi wa ana a Mulungu. Lerotilankhule za chithunzi chimenechi.Kale, kunali kasichi, lero tilibe kachisi omangidwa ndi manda. Leroinu ndinu kachisi wa Mulungu. Mulungu sakhalanso mu nyumbazomangidwa ndi manja. Lero, inu ndinu Kachisis wa Mulungu. Mulungu84 85


sakhala munyumba. <strong>Yesu</strong> amakhala mu mitima ya amene anamusankhaiye monga Mfumu. Simufunikanso kupita ku malo opatulika. Ngati muliwoyera ndiye kuti ano ndi malo wopatulika. Simufunikanso kupita kwinakuti mupeze pafupi Mulungu mungadziwe MUlungu mu mtima yanu.Ndinu Kachisi.Abale ndi Alongo simufunikanso masiku apadera dera. Lero ndi tsiku lachipulumutso, LInena, “Lero musaumitse mitima yanu. Samalanani winandi mnzake tsiku ndi tsiku. Sitidikira tsiku la Mulungu, sitidikira nthawiyolambira. Masiku asanu pasabata ndi maora makumi awiri ndi anai patsiku tingakhale pafupi ndi Mulungu ndiye sitifunikanso kukhala ndimalo apadera kapena nthawi yapadera.Nanga za ansembe? Ntchito yawo inali yoyandikitsa anthu kwa Mulungu.Tsopano tilibe chithunzi, tili ndi choonadi. Lero ansembe a Mulungu ndiINU. Ntchito yanu ndi kuziyandikitsa nokha kwa Mulungu mu mitimayanu ndi anthu ena pafupi ndi Mulungu. Potero simufunikanso munthukubvala zobvala zapadera kapena kuzitcha ndi maina ena chifukwa muthakukhala wansembe wa Mulungu.Lero Ufumu wa Mulungu suli mu malo. Suli mu nthawi, suli munyimbo zapadera. Uli mwa anthu amene akhala mwa iye. Anthu ameneangatumukire <strong>Yesu</strong> kasanu ndi kawiri pa Sabata, makumi awiri ndi anaipa tsiku. Anthu amene amakonda iye ndi mtima wawo wonse. Maganizo,umunthu ndi mphamvu zonse pamene <strong>Yesu</strong> anali kuyenda pa dzikolapansi pano, adalankhula ndi mzimayi. Adamfunsa funso; Tingalambirekuti Mulungu? Kodi ndi mphiri ili? Kapena linali? <strong>Yesu</strong> anayankha, “Osatimalo ano” Ufumu wa Mulungu suli pano kapena uko “Ufumu wa Mulunguuli mwa inu.”Opembedza otere amene Atate afuna kuti ampembedze iye mu mzimu ndimchoonadi. Amen Anthu a Mulungu ndi amene amapembedza Mulungukasanu ndi kawiri pa Sabata. Makumi awiri ndi anai patsiku pakukondandi miyoyo yawo palinso zambiri za kachisi. Munthu m’modzi sangakhalekachisi, Inde, Mulungu angakhale mu mtima wa munthu m’modzi. Komaali yense ndi mwala omangidwa pamodzi ndi miyala ina kukhala kachisi.Tiyenera kufunana wina ndi mnzake. Ndingapembedza Mulungu motanitsiku lili lonse? Kolingana ndi mau a Mulungu pokhapo nditalimbikitsidwakuchokera kwa abale ndi alongo tsiku ndi tsiku. Mtima wanga udzaumakwa Mulungu moyo wanga udzadzaza ndi chimo. Ndidzaumilitsidwa ndichimo. Ndiyenera kupeza abale ndi alongo kundilimbikitsa ndi kutonthozaine, ziyenera kuchitika tsiku ndi tsiku. Mnjira imeneyi tidzakhala kachisiwa Mulungu munjira imeneyi opembedza oona a Mulungu adzapelekedwamu mitima yathu.Tilankhure za kulambira mwa kamphindi chabe, lero sitifunansokukhala ndi nsembe yanyama. Kodi ndi nsembe yotani yopelekedwakwa Mulungu? Monga mwa baibulo, nsembe yopelekedwa ndi mtimayathu. Ife sindife nsembe ya kufa ndi nsembe ya mvyo. Maganizo athu salingati maganizo adziko lapansi, tiyenera kuganiza ndi maganizo a Kristu.Tiyenera kudzipereka tokha kwa Mulungu. Tidzakhala nsembe za moyo.Kumeneko ndiye kupembedza Mulungu, ngakhale sitikuimba kapenakupemphera. Tingapembedze Mulungu pamene tili kugwira ncthito.Tingapembedze Mulungu pamene tikuphika kapena kuchapa zobvalakapena kukhala pansi ndi anzathu.Ngati tili ndi maganizo amene amalamulidwa ndi <strong>Yesu</strong> ndipo tizipelekatokha monga nsembe tikupembedza Mulungu. Abale ndi alongoamenewa ndiye Ufumu wa Mulunguosati malo, osati nthawi, koma anthu.Anthu amene ali monga ansembe a Mulungu nthawi zonse tsiku lonsekulimbikitsana ndi kuthandizana wina ndi mnzake kuti akonde Mulungundi mtima wawo wonse maganizo, umunthu ndi mphamvu, choncho kutiapeleke miyoyo kwa Iye tsiku lili lonse. Ichi ndi cholowa chathu mongaanthu ake. Tingakhale munjira imeneyi sitifunikanso kukhala mongachithunzi chija. Tingakhale munthu weni weni. Izi ndi zinthu zimeneMulungu afuna kwa ife lero. ndizimene mufunanso? Chabwino, tiyenitiphunzire kukhala monga choncho pamodzi.Kumanga Molingana Ndi MakonzedweNdikudziwa kuti zambiri zimene mwamva lero, zingakhale pang’onozobvuta. Koma taona dziko lonse lapansi kuti ndi uthenga wabwino.Tabwera Unifu kwa tili osangalala kukuuzani njira imene Mulungu akhalaakufuna kumanga nyumba yake. Takumana ndi anthu ambiri amene aliabwino. Ena ndi Achi pentekosti, ena ndi bapatisti, ndi ena ndi azipembedzo86 87


zina. Akhala akusiyanasiyana miyoyo yawo yogawidwa kuchokera kwawina. Akhala ndi miyoyo yawo yosweka ndi chimo. Choncho anthuambiri ataya miyoyo yawo nd zokhumidwitsa ndi mgwirizano mubanja. Zokhumudwitsa zambiri zawoneka osati ngati <strong>Yesu</strong>. Ngakhalensozokhumudwisa mwa ife tokha, zinthu zimene tikudziwa tiyenera kuchitira<strong>Yesu</strong> ngati sitichita. Chimo limene likufunika kuchotsa ndiye timapezekatokha ofooka kuti lichoke.Baibulo limati mu Yohane 3:8 kuti mwana wa munthu anabwera kudziko kuononga chimo. Sanangobwera kudzakhululukira chimo lokha. Sichoncho? Amen. Komanso akufuna tigonjetse chimo. Akufuna kutengasatana ndi kumugonjetsa pansi pa mapanzi ake. Ichi ndi cholowa cha ana aMulungu, kuononga satana osati kungopulumuka, koma kuononga ntchitoya Mdyerekezi. Mwazina zimene sitinawone Mulungu akuonekera kuchilitsamitima yosweka ndi kuwononga chimo, si chifukwa palibe anthu odabwitsa- alipo, sikuti palibe mphatso zabwino mu thupi la Khristo - zilipo mphatsozambiri. Zambiri zotere zachitika chifukwa zikhumbo za mitima zalepherakukondweretsa Mulungu chifukwa chosamanga mu njira ya Mulungu.Chithunzi chimene takamba za nyumba za Mulungu. Kachisi ya Mulungu muchipangano chakale chinayenera kumangidwa ndi maonekedwe. Mulunguanawauza m’mene angamangire kachisiyo, ndi kumanga munjira ya Mulunguimene adanena. Zinakhala zotani ngati anakatenga miyala yonse ndi Golidewa kachisi ndi kuchita m’mene amafunira? Mulungu sanakakondwa ndiponyumba bwezni itagwa pansi.Tikufuna kulankhula m’mene anthu angafikire kothekera kotere tsopano.Tingalore mphatso mu thupi la <strong>Kristo</strong> kumangidwa pamodzi kukhalamokhalirapo Mulungu, kudzazidwa ndi ulemerero wa Mulungu. Iliponjira imene Mulungu akufuna kuti timange kuti mphamvu ya machimosiphwasulidwe mu moyo osati waukaporo ku zofooka zathu. Lingaliro laMulungu ndi kumanga ife mu kulumikizana osati kukhala ndi mabvutonthawi zonse. Mulungu ali ndi njira yodabwitsa pomanga nyumba yakendi anthu ake odabwitsa chipembedzo mu dziko, mphaka tsopano,zakhala zomangidwa mu zolakwika, ndi anthu ena monga mabwanandi anthu woyera ndi kuchita misonkhano ndi kumasulira kwawokuti “Mpingo”.Mu dziko lowonekali, taphunzira kwa zaka ndithu m’mene tingamangirendi zolimba. pali muyezo wa mchenga ndi kupita mu (Konterete) ndimadzinso pang’ono. Ngati mukathira simenti kapena mchenga wambirikoncrete silimba. taphunzira kuzungulira dziko lapansi kuti tipangekoncrete wamphamvu muyenera kuika zitsulo zolimba mu izo kutipasakhale ming’alu pamene pakhala kutentha ndi kuzizira. Tikudziwa kutingati tipanga njerwa kapena zidina, pali njira zina zimene timamangiranyumba ndi m’mene tingaikire njerwa mu ng’anjo. Pali zinthu zambiritaphunzira pazomanga mu dziko lino. Sitinadziwe m’mene tingamangirekoma tsopano tiyenera kudziwa kumanga. Mulungu anati tiyenerakusamala m’mene tikumangiraChoncho, mwachiyembekezo mu chisomo cha Mulungu tidzalankhulazambiri pa kanthawi inai. M’mene anzathu amisiri Engineers anaphunziliram’mene angagwiritsire ntchito konkerete mmene angakhalire wabwinokuti akhale wa mphamvu, momwemonso anthu a Mulungu ayenerakudziwa m’mene kumanga kwabwino kuti ikhale yolimba. Anthu abwinowokhala ndi mphatso zabwino amamanga bwino amamanga nyumbayotamandika ndi zimene timafuna kulankhulapo. m’mene tingamangirenyumba ya Mulungu bwino ndi anthu abwino omwewo. sikuti tikunyozazakale, sitikudanana ndi machitidwe akaleyo, ndi mtima odzichepetsatikungofuna kunena ndi nthawi yoi tipirire mstogolo tsopano. kale ndikale tiyeni tikule msinkhu tsopano mu chikondi ndi kudekha mtima ndikukoma mtima. Tiyeni tiyende pastogolo tsopano taonong zaka zambirikukhala ana a chaka chimodzi. Ndi nthawi yoti tiyende tsopano, ndi manjaathu otseguka.Mzimu woyera watipatsa ise zoti tiganize ndingofuna kuwonjezera ndimau achilimbikitso kanthawi kena tinayimba ndi nyimbo zina zinali zamuchingelezi ndipo ndimadziwa m’modzi mwa nyimboyi inali “Ambuyendinu olemekezeka, ndikudziwa kuti ndinu olemekezeka” ndi nyimboyoona. <strong>Yesu</strong> ndi olemekezeka. Ndikuganiza malembo mu 1 Petro 2:9 komandinu mbadwa zasankhidwa, Ansembe a chifumu, mtundu woyera, anthumwini wake Mulungu kuti mukalalikire zolemekezedwa za iye ameneakuitanani inu kuchoka mu mtima ndi kulowa mu kuwala kodabwitsa”Ambuye athu <strong>Yesu</strong> watiitana ife kuchokera mu mdima ndi kulowa mukuwala, ndipo ndife othokoza. Muli othokoza inunso? Amen. Mukufuna88 89


kuti mulengeze kuti ali olemekezeka? Alipo anthu ambiri otizunguliraamene akufuna kumva kuti Ambuye <strong>Yesu</strong> ndi olemekezedwa. M’mawauno tinadutsana ndi achisilamu, kodi mukufuna kuti adziwe kuti <strong>Yesu</strong> ndiolemekezeka? Ndikufuna kuti adziwe zazimenezi.Kuzungulira dziko lapansi pano tapeza anthu amene amapembedzaanthu akufa kapena mafano ndi enanso amene sapembedza chili chonse.Akufunika kuti adziwe kuti <strong>Yesu</strong> ndi olemekezeka, ndi ntchito yathukukawawonetsa. Koma nkhani iyi yoonetsa <strong>Yesu</strong> kuti ndi olemekezekandi zotengera m’mene ife tili osati kulankhula chabe, m’mene Peturo anatipano. Anati ife ndi “Ansembe a talankhula zimenezi kum’mawaku kutisikuti pali wansembe m’modzi yekha koma ansembe ambiri ndi kunenansokuti ndife mtundu wapadera, anthu ake a Mulungu. Kunenanso kuti pakatipa Akristo Ambuye <strong>Yesu</strong> ndi mfumu ndipo timamumvera iye mu ieytidzalengeza matamando.Ine ndimakhala ku Amerika, pa ulendo wathu ndabweretsa chitupa chaAmerika. Koma sindine, mukuona kwenikweni ndine mbadwa ya America.Ine ndine mbadwa ya ufumu wa Mulungu. Inu ndinu mbadwa za Malawi,koma a ufumu wa Mulungu, mwa choncho mbwadwa za ufumu wa Mulunguali mbadwa zabwino mu dziko lawo chifukwa amamvera malamulo osatikuchokera mu mantha koma kufuna kumvera basi. Koma ngati dziko lawolinena kuti asamvere Mulungu amati “Ai sitidza tidzamvera Mulungu osatimunthu” Ndizimene zimathandauza kukhala mbadwa zosankhidwa. Munjiraimeneyi sitidzalora chikhalidwe chathu kutiuza ife zochita. Tidzalora Mulungukutiuza zochita. Ndikuchokera ku dziko lomwe chikhalidwe chake ndi chauchimo chikhalidwe cha Amerika chaiwala kuchita manyazi ndi chimo.Sindidzamvera chikhalidwe changa. Ndidzamvera Mulungu Amen.Ine sindidziwa chikhalidwe chachi Malawi komanso inunso muyeneraMulungu, osati chikhalidwe chanu. M’menemo ndiye mbali yokhala mu ufumuwa Mulungu. Chomwechonso ndi zoona ndi chipembedzo. Lero m’mawatadutsa nyumba yolembedwa “Mpingo wa Nazarene” Ndikudutsanso maloena otchedwa Luzarene” Tinadutsanso pena analemba “Mpingo wa Khristu”onsewa akukumana lero. Onsenso ali kustatira miyambo yawo. Mbali ina yaUfumu wa Mulungu ndi kumvera Mulungu koposa miyambo chabe Amen?Miambo sali mfumu yathu, <strong>Yesu</strong> Khristu ndiye mfumu yathu. Tili mtundowapaderadera, tidzaimba ndi kulengeza olemekezeka <strong>Yesu</strong> <strong>Kristo</strong>. Ndifemtundu woyera. Zolengeza zahu ndi zomverka bwino, sizosokoneza, ndipoamuna onse adzafunsidwa ngati adzapinde mabondo awo ndi kumvera iye.M’mawa uno sitinabweretse chipembedzo china chatsopano. Tabweretsaufumu wa Mulungu, tiyeni tikhale munjira imeneyi tonse, AMEN.90 91


Madziko Anayi A ChoonadiSalima, Malawi, Africa, October 3, 1999(Izi zidayankhulidwa ndi abale atatu pamene adayima pamudzi winaku Malawi ku africa, pakuonetsera zokhudza mpingo ya chipentekositi.MUTSIKU LIMODZI “Mpingo” wonse udatembenukira kwa <strong>Yesu</strong> ndiposiwunayang’anepo m’mbuyo. Polipilira mtengo waukulu, munthu ali yensepayekha, zosintha zambiri zidapangidwa kwamuyaya, kusintha anthuambiri, ndikhalenso gawo lawo laza chuma m’mudzi wawo kumaguluena achipembedzokuti china chake chodabwitsa chikuchitika pakatipawo. Ndikufunitsitsa kukadakhala kotheka tikadajambula zinthu zomwezidanenedwa ndi abale ochokera m’mudzi umenewu ku Africa muolulotsatira patatha nthawi imene maganizo awa adayikidwa ndi oyera mtimakumeneko. Ichi chidali ndipo ndichodabwitsa ndi …………, ndithudi,kuwona kulimbika mtima kwao ndi “changu chao pa nyumba ya Atate”zowonetseredwa ndi “chikondi cha choonadi” ndi machitachita munthawikuchokera pa tsiku limenelo.)Chuma chamtengo wapatali ndi kudzutsa ndi kuchangamutsa anthua Mulungu padziko lapansi munthawi yino. Chilimo chilungamochapadera chomwe chakhala chili m’Baibulo lanu nthawi yonseyichimene chidzasintha moyo wanu ndikusinthanso njira imenempingo umaonetseredwa, kuti koposaposa tikakweze Mfumu <strong>Yesu</strong>ndikuwona loto lake likukwaniritsidwa. Ndichiyembekezo chathu, mwamzimu oyera, kuti maso athu onse akatseguke ndikuwona choonadichokongola ichi. Mulungu akufuna kumanga nyumba yake kuti tonsetikhale amphamvu pamodzi. Iye akufuna kumanga nyumba yake kutimakomo a ndende asadzailakenso konse. Iye akufuna kumanga nyumbayake kuti ubale ukhonze kuchilitsidwa. Iy akufuna kumanga nyumbayake kuti iye akhale omasuka kuchiza matupi athu, malingaliro athundinso moyo yathu. Iye akufuna kumanga nyumba yake kuti ife tikhaleamphamu ndi nzeru, ndi kuti uthenga wabwino wa <strong>Yesu</strong> upite patsogolo,mwamphamvu kuposa kale.93


Kodi muli nako kulimbika mtima pakumva zinthu izi? Kodi mumveramau a Mulungu pamene mukumva zinthu izi? Kodi mwasintha miyoyoyanu posawerengera mtengo wake? Ngati muli nako kulimbika mtimakuti mumvera ndi kudzipereka, ndiye chonde werenganibe.Pali choonadi chinayi chimene ife tiyenera kumangapo. Popandachimenechi, nyumba ya Mulungu sidzakhala yamphamvu, ndipomakomo a ndende adzapitiliza kudzetsa chisokonezo pa nyumbayi.Komabe, ngati ife timvetsetsa zinthu zinayi izi ndikuzimvera izo, ndipongati ife tifunitsitsa kudzipereka, ngakhale chowawa chidze, pa choonadicha Mulungu chinayi chimenechi, kenako Mulungu adzalemekezedwaichi ndipo iye adzatumidza mphamvu yake mumiyoyo yake. Osaukaadzachita bwino ndipo ofooka adzapeza mphamvu. Uwu wakhala ulimtima wa Mulungu ndi cholinga chake. Komabe, chuma ichi chokhalachitabedwa kuchokera kwa ife kuchokera mzaka zoyamba mpaka tsono.Ife talandidwa ndi miyambo ya anthu yachabechabe.Choonadi Choyamba: Kodi Mkhristu Ndi Ndani?Choonadi chamadziko choyamba ndi kufotokoza moyenera chimenemkhristu ali. Ife takhala tili otayirira padziko lonse lapansi ndimumiyambo yonse pazokhudza ichi. Chifukwa takhala osadziwamwachindunji zokhudzana ndi chimene Mkhristu ali, tamangakwambiri kwa nyumba ya Mulungu pa mchenga. Ifeyo tafotokozerandi kutanthauzira zimene zimampangitsa munthu kukhala Mkhristukudzera mu zinthu zomwe sizenizeni, kapena mamvedwe a matupiathu kapena mmene timalerera banja. tatanthauzira chimene Mkhristukudzera mkati ngati wina amayimba bwino, kapena amakhala nawom’misonkhano kwambiri, kapena amapereka chakhumi bwino. Umosim’mene <strong>Yesu</strong> adatanthauzira Mkhristu.<strong>Yesu</strong> adati, “Pokhapokha inu mutataya zonse, simungakhale ophunziraanga.” <strong>Yesu</strong> adati “pokhapokha inu mutasenza mtanda wanu tsiku nditsiku, simunganditsate ine.” Mubukhu la Machitidwe, Baibuo limati,“Ophunzira adatchedwa ‘akhristu’ koyamba ku Antiyokea. Tsonopamene muona liu loti ‘ophunzira’ muziphunzitso za <strong>Yesu</strong>, ganiziranimumalingaliro anu zaliu loti, “Mkhristu” pamene <strong>Yesu</strong> ananena kuti,“pokhapokha mutataya zonse, simungakhale ophunzira anga” Iyeamatanthauza kuti simungakhale a Khristu ngati inu simutaya kapenakupereka moyo wau. Iye sadanene kuti, “pokhapokha mutakhala nawomumisonkhano, simungakhale a Khristu” Iye adanena kuti , “pokhapokhamutafa kwa inu nokha, simungakhale a Khristu.<strong>Yesu</strong> akuyitana kwa anthu amene adafa kwa iwo okha. Iwo adzataya chilichonse nkumutsatira iye. Iwo adzataya kunyada kwawo ndi chuma chawokuti amutsatire iye. Iwo adzatembenuka kumachimo awo ndi kudzikonda.Iwe adzakonda ena koposa m’mene amadzikondera eni. Ubale umenewuwapakati pa iwo ndi <strong>Yesu</strong> udzasintha m’mene amachitira zinthu zawotsiku liri lonse.Pokhapokha ife titanthauzira liu loti “Mkhristu” munjira yomwe <strong>Yesu</strong>atanthauzira, nyumbayi idzatitimira mumchenga ndikukokoledwa. Lelindi chimene <strong>Yesu</strong> Mfumu adalonjedza kuti chidzachitika tikamanga pamchenga wa kumva, kuyimba ndi kuyankhula, koma osamvera. Nyumbaimene timanga idzakhala, mwina chinthu chimene chili chongosangalatsaife,koma sochidzatanthauza kanthu kwa <strong>Yesu</strong>. Nyumba imene timangaikonza kutisangalatsa ife chifukwa tikuyimba ndi kukhala pamodzi, komasiyitanthauza kali konse ngati Mulungu siali okondwa nayo. Sichitanthauzakali konse ngati satana akadagonjetsabe pa nkhondoyi m’miyoyo yathu.Ngati ife sitimanga moyo ndi Mpingo zomwe zibweretsa kusangalala kwa<strong>Yesu</strong>, ndiye kuti ife tikungotaya nthawi yathu ndi nthawi ya Mulungu.Mkwingwirima yakeMwala wa madziko oyamba pakumanga nyumba ya Mulungu ndikufotokoza chimene Mkhristu ali munjira yomwe Baibulo limafotokozerachimene Mkhristu ali. Ife tiyenera kupanga chisankho mwakulingana ndiamene Mulungu amamutcha Khristu. Kodi munthu nkutheka kukhalamembala wa Mpingo wa Mulungu koma osakhala Mkhristu? Nzosatheka!Koma pa dziko lapansi anthu akuphunzitsidwa kuti ndi zabwino bwinokuti Mkhristu ndi amene siali Mkhristu kukhala gawo la Mpingo. Baibulolimati ichi sichoona! Mu Akorinto oyamba 5, Baibulo limati “chotsanidzotupitsa mumkate” chotsani tchimo mu Mpingo. Ichi ndi chofunikirakumvetsetsa, chifukwa Mulungu adati, “chotupitsa pang’ono chimatupitsamkate onse”94 95


Kodi inu mukukumbuka pamene malinga a Yeriko anagwa pansi? Anthua Mulungu adali a mphamvu munjira yodabwitsa. Komabe, patangothakugwa kwa malinga a Yeriko, Israel idagonjetsedwa pankhondo. Iwoadamenyedwa! Nchifukwa chiyani, Israel idagonjetsedwa pa nkhondoyo?Chifukwa choti munthu mwa Israel adachimwa mu hema yake. Mulunguadakwiya chifukwamunthu m’modzi mu Mpingo wonse adachimwamumoyo wake umene udabisika. Munthu ameneyu, Akani, adali ndifanizo (mulungu osema) litakwiliridwa pansi pa hema yake. Mulunguadapangitsa a Israel onse kuvutika ndi chigonjetsocho chifukwa chatchimolo. Mulungu ali yemweyo dzulo, lero ndi kunthawi zonse.Sichoncho? Mulungu akadali osakondwa pamene anthu mu Mpingowake abisa tchimo miyoyo yawo. Ichi chimaswa mtima wake. Baibulolinena kuti Mulungu amabweretsa chiweruzo pa ichi.Kodi ndi chabwinobwino kwaife kunena kuti wina wake amenesadapereke moyo wake kwatunthu kwenikweni kwa <strong>Yesu</strong> akhonzakubwera ndikukhala mbali ya Mpingo? Ayi! Ichi ndi chibwana kwambiri.Mulungu amabweretsa chiweruzo pa nyumba yonse chifukwa cha munthum’modzi amene akunamizira kukhala Mkhristu, koma sanapereke moyokwatunthu kwenikweni kwa <strong>Yesu</strong>. Tsono, ngati ife tikufuna kuona Nyumbaya Ulemerero imene imagwira ntchito ya Mulungu, chinthu choyambachimene tingachite ndikutanthauzira liu loti “Mkhristu” munjira yomweyoyomwe <strong>Yesu</strong> anenera. malemba anena “pokhapokha mutataya zonse,simungakhale ophunzira anga” “Ngati mukonda abambo, amai ndi ana anukoposa ine, simungakhale ophunzira anga, ngati mukonda dziko lapansindi zinthu zamdzikoli, mwasanduka mdani wanga, Mulungu amadanandi odzitamandira ndipo amapereka chisomo kwa odzichepetsa”.Ife tiyenera molondola, kutanthauzira chimene Mkhristu membala waMpingo - ali chenicheni! Inuyo simunganamizire kusambitsidwa mumwazi wa <strong>Yesu</strong>, ndi kukhala chiwalo cha thupi la <strong>Yesu</strong> ndi kuyesedzerakuti Mkhristu ngati mtima wanu siuli kwa <strong>Yesu</strong> pamene muli kunyumba,kapena kuntchito, kapena m’minda. Ngati ubale wanu siuli ubale oyera,muyenera kulapa ndi kupereka moyo wanu kwa <strong>Yesu</strong>.Choonadi Chachiwiri: Kodi Utsogoleri Nchiyani?Chinthu chachiwiri chimene tiyenera kutanthauzira, mwala wachiwiriwa madziko pakumanga Nyumba ya Mulungu, zikhudzana ndi chimeneutsogoleri mu Nyumba ya Mulungu. Ichi ndicho choonadi chodabwitsakwambiri! ichi chidzabweretsa chimwemwe pa inu ndi kusintha moyowanu. Mu maiko padziko lonse lapansi, tapanga chibwana chachikulukwambiri pankhani yokhudza utsogoleri mu Mpingo. Mumalo ambirimunthu amene adaphunzira Baibulo ku seminale kapena kusukuluya Baibulo, kapena odziwa zamalonda kapena odziwa kuyankhulaamapatsidwa “ubusa”. Ife taona ku India ndi maiko ena kuti nthawi zambiri,munthu amene ndi njinga amenenso angathe kuwerenga amasankhidwakukhala mtsogoleri. Ichi sinjira ya Mulungu! utsogoleri wa Mulungusiugona pa iwo amene angathe kuyankhula bwino, kapena amene ali ndiluso pa malonda, kapena amene ali ndi chuma kapena maphunziro kapenamankhwala kapena maonekedwe abwino kapena njinga.Kukhala monga <strong>Yesu</strong>Ine ndikupatsani chitsanzo kuchokera mumalemba. Machitidwe 6, padaliazimayi amasiye achi Greek amene amakhala anjala kwambiri kwa nthawizambiri chifukwa choti amayiwalidwa. Pamene chakudya chimagawidwaiwo amasiyidwa ndi kusasalidwa bwino. Mpingo mu Yerusalemuadayenera kupanga ganizo la m’mene akadathetsera vuto ili. iwo adaganizakuti asankhe anthu ena kuti athetse vutoli. Ngati mungawerenge Baibulolanu, mupeza kuti padali njira ina yosankhila anthu amenewo. KodiBaibulo likunena kuti, “sankhani kuchokera pakati pa anthu asanu ndiawiriwa amene amadziwa ma Baibulo awo? Ayi. “Sankhani kuchokerapakati pa anthu asanu ndi awiri amene angayimbe bwino?” Ayi, sankhanikuchokera pakati pa anthuwa amene ali ndi luso pa malonda, kapena pamalonda a zakudya? Ayi, “Sankhani kuchokera pakati pa anthuwa ameneakhonza kuyankhula bwino?” Ayi. Njira yothetsera vutoli idali, “zisakhalirekuchokera pakati panu anthu asanu ndi awiri amene ali ozadzidwa ndiMzimu oyera ndi ozadzidwa ndi nzeru.Awa adali anthu amene amayesedwa tsiku liri lonse. Awa sadali anthu ameneadapita kusukulu kuti akhale auzimu, kapena amene amangoyankhulabwino chabe. Awa adali anthu amene adali abwenzi a Mulungu ndiposno96 97


abwenzi akuya abale ndi alongo apakti pawo tsiku liri lonse. Stefanondi Filipi ndi anthu asanu ndi awiri awa amapezeka mnyumba za anthutsiku liri lonse, kuyetsetsa kuthandiza anthuwo. iwo amakhonza kugwiramanja a ana a anzawo ndikuyankhula nawo ndi kuwaphunzitsa. iwoamakhonza kutungira madzi okhulupirira ena ndi kuwathandiza iwo.Iwo amakhonza kupita kunyumba za anthu pamene iwo akutaya mtima.Iwo amakhonza kupita m’malo ogwira ntchito a anthu mkati mwa tsikundikukawalimbikitsa iwo. Ndi iwo sadali ngakhale kutchedwa atsogoleri!iwo adali abale chabe amene amakhala umoyo wa <strong>Yesu</strong> tsiku liri lonse.“Zisankhileni nokha kuchokera pakati panu anthu asanu ndi awiri ameneawoneka ngati <strong>Yesu</strong>, asanu ndi awiri amene angathe kuona Mulungundi kumva Mulungu.” Sankhani anthu asanu ndi awiri amene akutsukamapazi a oyera mtima tsiku liri lonse”. “Abale asanu ndi awiri amene aliabale chabe tsiku lirilons amene amakodna Mulungu mozama kuchokerapansi pa mtima ndi kuonetsera kulumikizika kodabwitsa kwa Messiah.”Chifukwa anthu amenewa awoneka ngati <strong>Yesu</strong>, tsiku liri lonse munyumbaza anthu, ndiye kuti ife timadziwa kuti iwo ali odzadzidwa ndi mzimu oyera.Iwo siali odzadzidwa ndi mzimu oyera chifukwa choti iwo amayankhulamokweza kapena kuyimba bwino kapena amayankhula zinthu zambiri.Iwo ali ozdadzidwa ndi mzimu oyera chifukwa choti iwo amayankhulamokweza kapena kuyimba bwino kapena amayankhula zinthu zambiri.Iwo ali ozadzidwa ndi mzimu oyera wa <strong>Yesu</strong> chifukwa choti iwo amaonekangati <strong>Yesu</strong> ndi moyo wawo wa tsiku ndi tsiku. Uwu ndi mtundu okhawowa utsogoleri m’Baibulo. Mu chipangano cha tsopano, <strong>Yesu</strong> adauzaatumwi khumi ndi awiri aja kuti asatchule munthu kuti mphunzitsi, tate,mtsogoleri, mbuye, rabbi, m’busa, pakuti onse ndi abale! Tsopano ife tilindi maganizo odabwitsa, osiyana a utsogoleri.Zosiyana ndi zadziko lapansiKuphunzira ichi chidali chovuta kwambiri kwa ine pandekha. Muzakazambiri zapitazo ndidali “m’busa” kufikira nditazindikira zimeneBaibulo lidanena, zoti ndimayenera kungokhala m’bale pakati pa abale.Ndimayenera kugwiritsa ntchito mphatso ili yonse ndingakhale nayo“pakati pa abale, monga m’modzi amene atumikira” - osati monga bwanakapena wina wake oti adzionereredwa panthawi zonse. Ngati chimenechichidali choona kwa Petro, Yohane, Yakobo ndi atumwi ena, chiyenerakukhalanso choona kwa wina ali yense wa ife, opanda kuchotserapo!“Muli nonse abale chabe.”Ndidatuluka kuchokera ku ndalama zambiri zomwe ndimapangamudziko lamalonda pakukhala “m’busa”. Ndipo tsopano ndidayenerakusiyana nazo ndalama ndi mipando yakukhala osati monga mwa Baibuloimene anthu amaitcha “M’busa” wa mpingo. Ndidayenera kupangachisankho kuti ndiyenera kukhala m’bale pakati pa abale. Chili chonsechimene <strong>Yesu</strong> wapanga m’moyo wanga chikaonekera munyumba ndim’miyoyo ina pamene ndigwirana manja ndi ana. Ine sindimayeneransokukhala chipolopolo chachikulu ayi. Sindimayenerera kukhala munthuwamkulu ayi. Ndikadangopanga zimene Paulo adanena kuti adapanga ndiAtesalonika, ndi Afilipi, ndi okhulupirira mu mzinda wa Korinto ndipochimenechi ndiko kukonda anthu monga tate ndi m’bwenzi, ndiponsomonga m’bale kuchokera nyumba ina kufikira nyumba ina.Paulo adati, “Ndidapita kuchokera nyumba kufikira ina ndi misonzi” Iyeadakonda anthu monga tate, kapena monga m’bale. Iye analera m’moyoyawo monga mai angalerere mwana okhulupirira ena adamichitiransoiye chimodzimodzi, uwi ndiye utsogoleri woona mu Mpingo Owona waChipangano Chatsopano.<strong>Yesu</strong> adati kwa atumwi, “Amitundu ali ndi njira ina yokhalira ndi utsogoleri,koma izi siziri choncho ndi inu.” Mu mpingo woonadi, Mpingo umenemakomo a ndende sangaulake, utsogoleri wake ndi wosiyana kwambiri ndinjira ya dziko lapansi. Utsogoleri umabwera kuchokera mkati kati, osati“kuwupatsa mphamvu” kuchokera pamwamba.Mphatso ndi ulamuliro wa <strong>Yesu</strong>Ndiloleni ndikupangireni chithunzi inu. Baibulo limanena ku Aefeso4 kuti pamene <strong>Yesu</strong> adakwera kumwamba, iye adapereka mphatso kwaanthu. <strong>Yesu</strong> adatenga mphatso zonse zimene anali nazo (ndipo <strong>Yesu</strong> analindi mphatso zauzimu zambiri, sochoncho kodi?) ndipo iye adaperekamphatsozi kwa anthu ake onse. Iye sadatenga mphatso zonse zimene adalinazo ndikuziyika pa “m’busa” kapena pa “munthu m’modzi wa Mulungu”Malembo akunena kuti iye adatenga zonse mwa mphatso zake ndipo98 99


adazipereka izo kwa thupi lake lonse. Baibulo linena kuti mzimu uyikidwandi kuperekedwa ngati mphatso, monga mwa amene Mzimu ufunira,pa Mpingo wake onse. Ngati inu muli Mkhristu oona, ngati mwatayadimoyo wanu chifukwa cha <strong>Yesu</strong>, ndiye kuti Mzimu oyera ukupatsani inumphatso yapadera uoposa. Mphatso yanu ndi gawo kapena kuti chiwalocha <strong>Yesu</strong>.<strong>Yesu</strong> asadapite kubwerera kumwamba, adati, “ulamuliro onse ku Mwambandi padziko zapatsidwa kwa ine” Kodi mukukumbuka kuti <strong>Yesu</strong> adanenazimenezi? Ulamuliro onse uli kwa <strong>Yesu</strong> ndipo osati wina ali yense! Tsonongati <strong>Yesu</strong> anapereka gawo la iye yekha kwa inu, gawo lina kwa munthuuyu ndi gawo lina kwa munthu uyo, ndiye kuti mphatso yauzimu ina iliyonse adapereka kwa wina ali yense wa inu, pali ulamuliro mu mphatsoimeneyo. <strong>Yesu</strong> adapereka mphatso ndipo iye ali ndi ulamuliro onse.Pali mphatso zamitundu yambiri zomwe zidalembedwa m’Baibulo.Mzimu Oyera, mwachitsanzo, umapereka chifundo ngati mphatso.Mphatso ya chifundo ndi gawo la <strong>Yesu</strong> limene iye adapereka kwa anthuena. Ndi mphatso yodabwitsa. Tonse a ife tiyenera kukhala ndi chifundo,sichoncho? Koma pali chifundo chodabwitsa chimene chili mphatso yaMzimu Oyera. Tsono, ngati iye adapereka kwa inu mphatso yapadera yachifundoyi, inu mwapatsidwa ulamuliro kumbali ya chifundo. Ngati inumuli ndi mphatso yodabwitsa ya chifundoyi ndipo ine ndilibe, ndipo ngatiulamuliro onse uli kwa <strong>Yesu</strong> ndi inu muli ndi mbali ya <strong>Yesu</strong>, ndiye kutiine ndilemekeze mphatso imeneyi mwa inu. Muli ndi ulamuliro kumbaliimeneyo. Kodi mukumvetsetsa? Ichi ndi chimene utsogoleri uli!Ulamuliro onse uli kwa <strong>Yesu</strong> ndipo ife tonse tili nayo mphatso zathuzapadera. Mwachitsanzo, pali mphatso ya uphunzitsi. Ahebri 5 imati,“tonse tayenera kukhala aphunzitsi tsopano” Komanso ku Aefeso 4ndi Aroma 12 limati pali mphatso zauzimu za uphunzitsi zimene <strong>Yesu</strong>amapereka. Ichi chitanthauza kuti pali ulamuliro mu mphatso imeneyichifukwa <strong>Yesu</strong> amapereka mphatsoyi ndipo Iye ali ndi ulamuliro onse. Ifetidzipereke kwa wina ndi mnzake mu ichi. Koma kuphunzitsa ndi gawolimodzi lokha ndi mphatso imodzi yokha ya <strong>Yesu</strong>. Palinso mphatso zinazambiri. Pakuti ulamuliro onse uli kwa ali yense wa ife ndi gawo la <strong>Yesu</strong>,ndiye tikuyenera kudzipereka ku mphatso zomwe zili mwa wina ali yensewa ife chifukwa <strong>Yesu</strong> ndi amene waikamo mwa ife mphatsozi.Palibe ulamuliro wina wake umene uli mwa “munthu wa Mulungu”m’modzi ndipo wina ali yense angokhala chabe ndikuonerera. Chifukwachanjira zimene anthu amangira Mpingo zaka zodutsa 1800 zapitazo,ife takhala ndi machitidwe onga ngati pali mphatso imodzi yokha basi -mphatso ya “ubusa”. (Kapena mwina wina ali yense ali ololedwa kukhalandi mphatso yopereka ndalama yokha!”) Koma m’busa / ubusa ndiyemphatso yokha basi! Ngati ife timanga molakwika, tonse tiluza. Ngati,munthu m’modzi akankhilidwa kutsogolo kukhala “m’busa” ndipo winaali yense kungokhala pansi ndi kumvetsera nthawi zonse, ndiye kutiwina ali yense sakugawana nawo mphatso yanuyo. Iwo amangotengamphatso “ya ubusayo”. Ichi ndi chochepa kwambiri ndi chachinyengo!Ngati tikufuna kuti tione ukulu wa Mulungu, ndipo ngati tikufuna kuonamiyoyo yathu yonse ikusintha ndipo miyoyo ya ana athu ikusintha, apa ifepafunika zigawo za <strong>Yesu</strong>, Amen? Ife sitiyenera kukhazikika pa gawo chabela <strong>Yesu</strong>. Amen?Kulimbika mtima kukusintha ndi kulimbikamtima kukuthamangaKodi mukuona chifukwa chimene tikunenera kuti tiyenera kulimbikiramtima? Zinthu ziyenera kusintha! Simungapitirire kuchita zomwe mwakhalamukuchita. Mupanga chisankho kugwiritsa ntchito mphatso yanu kwambirindiponso kulandira enanso kuti nawonso atero. Mupanga chisankhokukhala omvera ndipo kukhala ndi kulimbika mtima. Ngati mupitirirakukhala pa mpando wanu kapena pansi nthawi zonse ndiponso osagwiritsantchito yanu kwambiri ngati mmene zimayenera kukhalira, mphatso yanuidzapitirira kulowa pansi. “Iye amene wapatsidwa mphatso akuyenerakuonetsa kukhulupirika.” Kodi mukukumbuka zimene zidachitika kwamunthu amene adakwirira talente yake? <strong>Yesu</strong> adati, “Iwe oipa, wantchitowaulesi.” Icho ndi chimene <strong>Yesu</strong> amanena kwa ife pamene ife sitipangazomwe tiyenera kuchita. Ngati ine sindigwiritsa ntchito mphatso yangakapena inu kugwiritsa ntchito mphatso yanu, ife tili “oipa ndi aulesi”.Kodi mukuona m’mene miyambo ya anthu ikubela ndi kulanda mau aMulungu? Bwanji inu mutakhala othamanga wa Olympic mwagona pabedi ndi wina wake watenga chingwe ndipo wamanga kuzungulira inupamodzi ndi bedi? Ngakhale mutakhala opambana pamasewero olimbitsa100 101


thupi, ngati inu mwamangidwa pamenepo pamodzi ndi bedi minofu yanuikulungala ndipo kenako inu mufa. Mphamvu ndi kuthekera kwanu konsekupita pachabe chifukwa mwamangidwa kubedi kwa miyezi kapena zaka.Kodi inu mukuona m’mene miyambo ya anthu imabela ndi kulanda Maua Mulungu? Njira imene tamangira mzaka zoposa 1800 mu Nyumba yaMulungu zamanga anthu a Mulungu ambiri kumodzi ndi bedi. Iwo akhalaopanda kuthekera koima ndi kothamanga ndi kokwaniritsa masomphenyaawo chifukwa anthu amanga molakwika, mosatsatira mau a Mulungu.Ngati ife tamanga kapena kukonza Mpingo munjira imene makwezamunthu m’modzi kapena “waudindo” ndi kuzima mphatso zaena, ife tilizigawenga mu Bwalo la milandu la kumwamba chifukwa cha zowongeka ndizowawa zimene ena awawidwa nazo chifukwa cha “chotupitsa mu mkate”ndiponso mphatso zosagwiritsidwa! Sikuti ndi chifukwa choti anthu ndi“oipa” chimene ife tamangira molakwika. Kwenikweni ndi chifukwa chotiife sitikudziwa kumanga Nyumba ya Mulungu ndi Mapangidwe ake.Tsono kumbukirani kuti mwala omangira oyamba wa madziko oonadi ndiakuti okhawo ali Akhristu oonadi okhonza kuzitcha okha mamembala aMpingo. Mwala wa madziko wachiwiri umene ungamange Nyumba yaMulungu ndi kuti tiyenera kumvetsetsa utsogoleri bwinobwino. Ife tayikamunthu m’modzi kukhala olamulira kwa zaka 1800. Ife tatenga mphatsoimodzi, mphatso ya “mbusa” (kapena ubusa, kutanthauzira kwabwino)ndipo tayipanga kukhala mphatso yoyambirira. Ichi ndi kutali ndichoonadi mu Mpingo mu Baibulo!Ndipo sichiyenera kukhala chilungamo ngakhale pano. Ichi chamangiriraambiri mwa anthu a Mulungu ku bedi kuti iwo asakhalenso m’meneMulungu adawaitanira iwo kuti akhale. Utsogoleri uli mwa anthu onse aMulungu. Baibulo limatcha ife Ufumu wa ansembe. Baibulo silinanenekuti Ufumu okhala ndi ansembe, koma Ufumu wa ansembe. Palibegulu lapadera monga ngati ansembe achilevi aku Chipangano chakale.Muchipangano chatsopano onse a anthu a Mulungu ali oyenera kukhalaansembe jwawina ndi mnzake. MULUNGU adati, “pemene bvumbulutsolidza kwachiwiri, siyani oyambayo akhale pansi!!!!!!Ngati inu muli odzadzidwa ndi mzimu oyera ndi odzadzidwa ndinzeru, ndiye kuti ndinu mtsogoleri.Sikuti ndingoti unapita kusukulu, kapena ngati umayankhula bwino.Sikuti ndingati uli wam’muna kapena wamkazi, kapena wamng’onokapena wamkulu. Utsogoleri ndi munthu amene ali ndi mphatso ya <strong>Yesu</strong>ndi ubale ndi <strong>Yesu</strong>, adzadzidwa ndi Mzimu Oyera ndi nzeru. Utsogolerindi kugwirana manja ndi ana tsiku liri lonse. Utsogoleri ndi kuchizamabala a anthu a Mulungu kuchokera nyumba ina kufukira nyumba inatsiku liri losne. Utsogoleri ndi kuthandiza kuthetsa mavuto a tchimomu miyoyo ya abale ndi kusambitsa mapazi awo tsiku liri lonse. Ichi ndichimene utsogoleri uli ndipo ndi mtundu okha wa utsogoleri umenebaibulo limankhula, kugwiritsa ntchito gawo la <strong>Yesu</strong> limene Mzimu Oyeraudayikamo mwa wina ndi mnzake wa ife. Ichi ndi mbali ya utsogoleri ndiulamuliro. Ichi chitanthauza kuti ife tiyenera kusintha m’mene timachitiratsopano. Ife tiyenera kusintha m’mene timaonera utsogoleri ndi m’meneife timachitira pa ndondomeko ya utsogoleri.Ichi ndi chosintha kwambiri. Ichi chisintha m’mene timachitira mumisonkhano yathu, m’mene ife timachitira mu moyo wathu wa tsikuliri lonse. pali mtengo omwe tiyenera kulipira pa ichi. Koma Mulunguamapereka mphoto kwa ife kokwana zana limodzi pa chili chonsetimapereka, monga mwa lonjezano la <strong>Yesu</strong>.Pamene ine ndidali “m’busa” ndidaganiza kuti ndikhale mosiyana ndipoyamba. Ine ndidaganiza kuti ndikhulupirire ndi kumvera malembopazokhudza utsogoleri. Ndidasankha kukhala m’bale pakati pa abalekoposa kukhala kutsogolo kwa abale. Kunena moona, ndidaopa.Ndidaopa za m’mene ndidzasamlira banja langa. Ndidaopanso kutimwina ndidzataya ubale wanga ndi Mulungu mwinamwake ndi kuti anthusadzandilemekeza inenso ayi. Ndidali ndi mantha pa zinthu zambiri.Koma ndidadziwa kuti Mulungu adanena mu Baibulo. Iye amafuna inekuti ndikhale m’bale pakati pa abale. Mu moyo wanga wa tsiku ndi tsiku,sindidzakhalanso bwana ayi. Ndidzangokhala chabe m’modzi mwa abale,ndipo ndidzapitilira kugwiritsa ntchito mphatso yanga kuchokera kwa<strong>Yesu</strong> monga “m’bale pakati pa abale” amene mofanana agwiritsa ntchitomphatso zao. Izi zidasintha chili chonse pa ine, koma Mulungu adaliokhulupirika kwambiri. Iye adalonjeza kuti palibe amene adasuya chilichonse amene adzalephera kulandira koposa zana limodzi kapena kuposazomwe adataya. Mulungu amasunga lonjezano lake! Amen?102 103


Kuchokera pa zintchito, ndikufuna ndiyikepo maganizo anga pa inu akutingati tifunitsadi kuti tilemekze mphatso zimene ziri mwa wina ali yensemwa ife, ndikutulutsa poyera mphatso zimene zili mwa anthu onse aMulungu, ndiye tifunika kusintha zinthu zambiri. Monga mopusa m’menechikumvekeramu, chimodzi mwa zinthu zimenezo chikhonza kukhalammene timakhalira pamene tisonkhana pamodzi. Pamene <strong>Yesu</strong> analipano, Iye adali ndi anthu omuzungulira Iye - awa ndiwo amayi anga, abaleanga, ndi alongo anga” (Mariko 3) Kukhala mwabwalo omuzunguliraIye! Ichi sichinthu chachizolowezi kupanga, pamen ife tasonkha pamodzikuti timumve IYE, ndipo osati munthu chabe wa mphatso zowerengeka.Ichi chikhonza kumveka ngati chopepuka kwambiri kwa inu, ndichikhonza kusamveka ngati cha phindu ndi chofunikira, koma ndikufunandikutsimikizireni inu kuti ichi ndi chofunikira. Ndamva kuti mau ayimira“Gome” ndi “mnofu” amanenedwa munjira imodzimodzi. chi Faransa.Ngati wina wake kumalo ogwirira ntchito kapena kumsika anena chinthuchina kwa inu, kodi chili ndi kanthu mmene achinenera? Zoona chili ndikanthu! Ngati iwe akutsamira, kapena kukhala motsamira kumwala ndikunena china chake motsitsa kwanaku akuyatsamula, chimenechi chikhalachosiyana koposa ngati iwo akadanena chinthu chomwecho ndi nkhopeyao yoima moyang’anizana ndi yanu ndipo akuyang’ana m’maso anu ndimoto. M’MENE chili chonse chinenedwa chili ndi kanthu kwakukulu.Pamene tikhala ndi wina ali yense akuyang’ana kutsogolo, chimabweransokumvetsera konse kwa munthu m’modzi. Ife sitilinso ofananana pakati paofanananso ayi. Ine ndili odzipereka kwa ali yense amene watenga mpandoolamulira kustogolo kwa ine monga mbuye wanga, kapena kondakitarakapena wapolisi wamagalimoto kapena kadaulo wa china chake. Komadziwani ichi bwino lomwe! Wantchito oona wa Mulungu sakhumbirakufuna kumveredwa pa iye yekha. Yohane mbatizi, amene adali munthuwa mphamvu obadwa mwa mzimayi adati, “<strong>Yesu</strong> ayenera akulire, inendiyenera ndichepere. Ine sindifuna anthu adziyang’ana pa ine nthawizonse monga munthu amene ali ndi mayankho onse. Ine ndikungofunakukonda ndi kutumikira <strong>Yesu</strong>, ndi kuthandiza ali yense kupanga ichinso.<strong>Yesu</strong> ayenera kukwezeka, ine ndiyenera kuchepera.Munthu wa Mulungu awona ali yense amafuna kudzibwenza kuti <strong>Yesu</strong>adzitengere ulamuliro koposa iye mwini. Ndiponso, ena adzanena kuti ichindi chopanda tanthauzo, koma mukukhala mkuyenda kwanga m’mayikoambiri ndi m’mizinda ndikutsimikizani inu, sikuti ndichosafunika. Ichindi chofunika kwambiri, m’mene tinganenere chinthu china chake.Pamene ife tiyika mipando m’mizere malo mwa mabwalo, ichi chikukhalangati kuyatsa nyali pamunthu m’modzi. Ali yense amangokhala ngatiodzangoonerera ndipo munthu m’modzi ndiye ali wachikoka. Icho ndichinthu cholakwika chifukwa pali mphatso zambiri pakati pathu, ndipo palizigawo zonse za <strong>Yesu</strong>. Ngati ife tiyika aliyense mwakuyang’ana kustogolondiye kuti likukwezga mphatso imodzi yokha basi. Kodi ndikunyadakwanji komwe munthu angakhale nako pakuzivomereza yekha nthawizonse kukhala “mpando wa ufumu” kapena nyali younikira.Tsono, bwanji ngati m’malo mwake mphatso zonse zitakhala ndi maloofanana? Mwina pali wina wake ndi mphatso ya ubusa atakhala mwa bwalo.Mwina wina wake ndi mphatso ya uphunzitsi atakhala pamenepa ndipowa mphatso ya chifundo atakhala pamenepa. Mphatso ya kuthandizaitakhala pamenepa ndipo mphatso ya uneneri itakhala pamenepa. Zonsemwa mphatso zili ndi malo ofanana chifukwa zonse ndi za <strong>Yesu</strong>! Kodi ichichikupereka nzeru? (Ngati muli ndi makina a Kompuyuta, onani pa iwo.Aii at his feet.com / Jesus as Head kuti muone “chithunzi” cha ichi.Tsopano, ngati mzimayi ali mubwalomu ali m’misonzi pa zakaleredwe ka anaake, mphatso ya uphunzitsi ikhonza kuyankhula naye ndi kumuphunzitsazokhudzana ndi zimene Paulo adanena mubuku la Tilo zokhudza azimayi.Mphatso ya chifundo ikhonza kupereka lingaliro la chifundo, mwina iyeali ndi ana a ang’ono kupereka panthawi imodzi ndipo akhonza kugawazakuwawa za ichi. Mphatso imene ili ndi chidziwitso chauneneri ikhonzakuona mu mtima za chifukwa chimene mlongo uyu ali ndi mavuto ndi anaake, ndi choncho. Tsopano, pomaliza, likhonza kumveradi moona lamulolochokera kwa Mulungu, “pamene bvumbulutso libwera kwawachiwiri,siyani oyamba akhale pansi”. Allelluya!!!!!!! (Mikuwo, ibwerenza)Ali yense, ndiofunikira mofananaMu Akorinto oyamba 14, Mulungu adanenanso “pamene mubwerapamodzi, abale, ndipo Mpingo uli pamodzi, lekani chili chonse chichitikemwakumanga kwa thupi la Khristu. Ali yense wa inu ali ndi inu la chilangizosalimo, bvumbulutso” Palibe bwana koma <strong>Yesu</strong> yekha! “Musaitane104 105


munthu mtsogoleri, mbuye, mphunzitsi kapena m’busa. Nonse ndinuabale”. Inu nonse muli ndi <strong>Yesu</strong> ndipo Iye ali chimodzi chimodzi mwawina ali yense wa inu.Mwachidziwikire pali kusiyana m’makhwimidwe, ndipo mphatso zinazili za “pachigulu” pamene mphatso zina zili zachete kapena zosaonekeraonekera pa gulu. Koma, zonse zilipo ndipo zili ndi mwayi. Nthawi zinatimafuna chifundo cha <strong>Yesu</strong> ndi nthawi zina timafuna chiphunzitso cha<strong>Yesu</strong>. Nthawi zina timafuna nyimbo za <strong>Yesu</strong> ndipo nthawi zina timafunathandizo la <strong>Yesu</strong> kuti tithetse vuto. Koma zonse ndi za <strong>Yesu</strong> mofanana.Chonde werengani Akorinto oyamba 14:26-40.Kodi mukhonza kuona kuti zimafunika kulimba mtima? Kodi mukhonzakuona kuti zimatengera chikhulupiriro ndi kumvera? Kodi mukhonzakuona kuti ichi chisintha moyo wanu ngati muyamba kukhala mu ichi?Kodi inu simungadzamangidwanso kumodzi ndi bedi! Mphatso yanundiyosiyana ndi yanga, koma yanu ndi chimodzimodzi ndi yanga. Inendikufuna mphatso yanu kwambiri monga inusno mufunitsa yanga.Zinthu zina zofunika zimene zachitika mmoyo wanga zachitika chifukwacha mwana wa zaka khumi ndi ziwiri ndi mphatso yake kukhudzamoyo wanga. Azimayi kukhudza moyo wanga ndi ana kukhudza moyowanga. Anthu okalamba kukhudza moyo wanga ndipo osati pa m’mawa,Lamulungu lokha ayi, koma tsiku liri lonse.Ife tiri Ufumu wa ansembe tsiku liri lonse. Misonkhano ndizongoonjezerapo ndithu. Mbali yokwana makumi asanu ndi anayiakukula kwathu imachokera mukukhala pamodzi, ndipo mwina mbaliyokwana khumi limodzi chabe ndi m’mene imachokera mmisonkha. Ichichitanthauza kuti muyenera kutuluka mnyumba zanu ndipo mulowemnyumba za anthu ena. Inu munyamule madzi, kapena chakudya, kapenazovala popita kunyumba zawo. Pamene inu muona kuti ali ndi njalapamodzi ndi mwana, muyenera kuwatengera pambali ndikuyankhulanawo ndi kuyenda nawo. Pamene inu muona kuti ali ndi njala pamodzindi mwana, muyenera kuwatengera pambali ndikuyankhula nawo ndikuyenda nawo. Pamene muona kudzitukumura mmoyo wawo, muyikedzanja lanu kuzungulira iwo ndi kuwafunsa iwo kuti sayenera kukhalaoditukumura. Pamene inu muona kudzikonda mwa m’bale, inu muyenerakuyika dzanja lanu mozungulira iye ndipo nati, “Chonde usakhalensoodzikonda ayi”. Ife sitimangotseka maso athu kufikira msonkhano wina.Ife timakhala pakati pa moyo wa wina ndi mnzake tsiku liri lonse mongaansembe akuchita ntchito ya Mulungu, ndipo monga “zana la amai, abalendi alongo” Ichinso ndi lamulo kuchokera kwa Mulungu mu Ahebri 3ndiponso m’malemba ambiri.Mwala wa madziko oyamba ndi “Kodi mkhristu ndi ndani? Kodi umembalawa Mpingo uti? Ngati inu muli ndi anthu amene siali otembenukiramoona kwa <strong>Yesu</strong> mu Mpingo, ndiye kuti inu mudzakhala mapafupipafupi ndi nkhondo ndi ndewu imene simuyenera kukhala nayo. baibulolinena, “kuchokera kwa ang’ono kufikira kwa akulu, onse adzamudziwaiye.” Pamene wina ali yense amene amadzitcha yekha membala moonadiali m’chikondi ndi <strong>Yesu</strong>, pamakhala mtendere kwambiri - popanda ndeu,popanda mijedo. Ndipo pamakhala chikondi chakuya pa wina ndimnzake tsiku liri lonse. Inu simungakhale membala woona wa Mpingowa <strong>Yesu</strong> pokhapokha inu mutataya moyo wanu. Ndi Mkhristu yekhaangakhale membala wa Mpingo. Ali yense ndi alendo chabe, koma iwosakhala mamembala a Mpingo wa <strong>Yesu</strong>.Ichi ndicho chenicheni cha zimene Baibulo linena. Ndipo “chotupitsa”chiyenera kuchotsedwa mu mktae, kapena ife sitimukonda <strong>Yesu</strong> mongam’mene tinenera. “Ngati mundikonda Ine, mudzamvera malamulo anga.”Mpingo uli kulumikiza ndi kulimbikitsa ndi kuphunzitsa ndiponsokuteteza kwa amene adasambitsidwa mu Mwazi wa <strong>Yesu</strong>, atasankha kufakwa iwo okha kuti akwatiwe ndi Mbuye, <strong>Yesu</strong> kwamuyaya. Ali yenseamene sanapange chisankho, wakuyikiridwa umboni ndi moyo wawondi chosankha chawo, ndipo ndikuti ngati kapena ayi, “akonda kuwala”(Yoh 3, 1 Yoh 1), sayenera kudziyesa yekha Mkhristu kapena membala waThupi la Mkhristu. ichi ndi chimene Mulungu adanena.Tanthauzo liri losne la “mpingo” ndi lopangidwa ndi munthu, ndipo“makomo a ndende” adzalaka chifanifani chotere. tayang’anani, inumudzaona ichi mu mseu uli wonse mu mzinda ndi mzinda, fuko ndi fuko. Ichisimalingaliro a Mulungu, koma china chake chomwe chimangokwaniritsamamvedwe a anthu, pamene akugwiritsa ntchito dzina la <strong>Yesu</strong> kutiachotsere nthumadzi zawo. Koma palibe kuchiritsidwa apo! Messiah yekhandi amene amazungulira pamene Iye angasiyepo nyali!106 107


Mwala wa madziko wachiwiri uli ndi chochita ndi mtsogoleri. Mzimu ndiMoyo wapano wa Khristu Owukistidwa, ndiye mtsogoleri yekha wathu.Dziko silidzandiona ine, koma inu mudzandiona! Mulingo wa Mzimuumene munthu ali nao, mphatso imene wina ali nayo, kukula ndi kuyakwenikweni kumene ubale wa moyo ndi <strong>Yesu</strong> wa Moyo umene ali nawo -icho ndiye matanthauziro a Baibulo a “Utsogoleri.”Choonadi chachitatu: moyo wa tsiku ndi tsikuMwala wa madziko wa chitatu uli ndi chochita ndi moy wathu wa tsikundi tsiku pamodzi ndipo ife tayankhulapo mochepa pa zaichi. Moyowa tsiku ndi tsiku ulibe chochita ndi misonkhano imene timakhalanayo, koma koposa m’mene timakhalirana, ife timakhala tsiku liri lonsemonga ansembe mumabanja ndipo ndi ana athu amene atizunguliraife, ndipo ndi magwiridwe ntchito ndi makhalidwe ofanana ndi anthuamene atizungulira ife? Kodi ife tikukhala tsiku liri losne pa muyesowa pa mtima ndi abale ndi alongo? Kodi ife “timasenzerana winandi mnzake chipsyinjo ndi kukwaniritsa Lamulo la Khristu? Kodi ife“timavomereza ndi kuululirana machimo athu wina ndi mnzake ndikuti tichiritsidwe? Kodi ife “timakhala monga munthu m’modzi pachikhulupiriro,” “molumikizana ndi kulukana pamodzi ndi munyewayothandizira”, ndipo osavomereza chili chonse kupatula “Mpingowoona ndi “Thupi la Khristu”? Pamene pokha ndipamene mudzapezachimene <strong>Yesu</strong> amatanthauza pakuti, Ndidzamanga Mpingo Wangakuti makomo a ndende sadzaugonjetsa kapena kuyima!” Chinthuchili chonse ndi “nyumba yomangidwa pa mchenga” wa kunyalanyaza,kufunda, kusamvera, kusalumikizana. Ndipo udzabereka chipatsochoyenerera, mwatsoka. Mulungu adati chili ndi kanthu kapenatanthauzo m’mene timangira!Ine ndikuonetsani Malembo, amodzi ndipo asintha moyo wanu onsengati mungamvere. Ngati inu mungachite malembo awa amodzi, inumudzadabwitsidwa zam’mene zinthu zina izi zikuperekera tanthauzo.Ichi ndi lamulo kuchokera kwa <strong>Yesu</strong>. Kodi mupanga ichi? Kodimutero? Kodi inu mumukonda Iye? ichi chidzasintha moyo wanu onsekuti MUPANGE chimene Iye anena koposa kungogwirizana nachokapena kungochiphunzira chabe kapena kungoyimba za icho kapenakungokumnana pa zaichi. Tiyeni tiyang’ane pa ichi limodzi. malembowondi Ahebri 3:12-14Penyani abale, kuti kapena ukakhale mwa wina wa inu, mtima woipawosakhulupirika wakulekana ndi Mulungu wamoyo komatu ndikudandaulilaninokha tsiku ndi tsiku pamen pachedwa lero, kuti angaumitsidwe wina wa inundi chenjelero la uchimo pakuti takhala ife olandilana ndi Kristu ngatitutigwiritsa chiyambi chakutama kwathu kuchigwira kufikira chitsirizilo.Dziwani chimene malembo awa akunena - ichi ndi chochokera kwaMulungu. Mulungu wamphamvu zonse akunena kwa inu ndi ine kutitiyenera tsiku liri lonse kuchenjezana wina ndi mnzake ndi kuthandizanawina ndi mnzake tsiku liri lonse. Mzimu Oyera udasankha kuti unene kuti“tsiku liri lonse”. Iwo siudanene kuti Lamulungu ndi la Chitatu liri lonseayi. Iwo siudanene ngakhale kuti misonkhano mokha, iwo adati tikhale pamuyeso wa choonadi mo moyo wa wina ndi mnzake tsiku liri lonse. Ngatiena ali opezeka kapena akhonza kupezeka, ndipo inu simufuna kukhalanao kapena kukhudzidwa chifukwa cha moyo wanu, kapena kunyada,kapena kudzikonda, kapena chisankho chimene mungakhalire, Mulunguadati monga iye amvera. Inu mudzapusisidwa mu kuganiza kuti mumadzi.Chimene chili choona pamene inu simudziwa. Icho ndi chimene malemboakunena mwatchuchutchu! Iye adangoti kuchipanga ichi, iye adati ngatisimupanga ichi, chidzakuvulazani kwambiri. Ngati ine ndilibe m’baleondiyankhula ine tsiku liri lonse zokhudza moyo wanga. Tsiku liri lonse inendidzasanduka olimba. Ine ndidzapusitsidwa. Inu mukhonza kunena kuti,“Koma ndimawerenga Baibulo tsiku liri lonse!” “Koma ndimapempheratsiku liri lonse! “Mkazi wanga ndi Mkhristu ndipo ndimamuona iye tsiku lirilonse!” Icho sichimene Mulungu akunena, mukhonza kuwerenga baibulondi kupemphera tsiku liri lonse, koma ngati simufuna kukhala mu moyowa wina ndi mnzake tsiku lili lonse, inu mudzakhala mukuwumila umilabendi kupusitsidwa pusitsidwabe. Mulungu adanena ichi mu Ahebri 3:12-14.Kodi mumakhulupirira baibulo? Kodi mumakhulupirira Mulungu?Kodi adalemba baibulo ndani? Mulungu! Mulungu adanena kuti ifetiyenera kukhala mo moyo wa wina ndi mnzake tsiku liri lonse. Ngatimuwona ine ndikudzikonda, mufunika kumbwera kwa ine ndi kunena,“m’bale, osakhala odzikonda. Ichi chipangitsa <strong>Yesu</strong> kukhumudwa.” Inumukandiona ine ndikunyada, chonde bwerani ndi kundikumbutsa ine108 109


kuti Mulungu amatsutsana ndi onyada. Ine sindifuna kuti Mulungu adanenane! Inu muyenera kuthandiza ine, chifukwa ine singingaone ichi nthawizonse. Palibe amene angahe. “Dandaulilani wina ndi mnzake, tsiku ndi tsikukuti ali yense wa inu asadzimitsidwe mtim kapena kupisitsidwa” Ichi ndimbali yofunikira (ndipo siyimveredwa pafupi pafupi dziko lonse. Iyi ndinjira ya chifungulo imodzi yokhalira ansembe pogwirista ntchito mphatso,ndiponso “akazembe a Khristu, monga ngati Mulungu amabweretsa chofunachake kudzera mwa inu.”Choonadi Chachinayi: MisonkhanoKwa zaka 1700, mudziko la chikristu mudali chosokonezo pa nkhaniyokhudza kuti Mkhristu ndi ndani …… mtsogoleri ndi ndani ………kodi moyo wa tsiku ndi tsiku uyenera kuoneka bwanji, maziko achinayiamakhudzana ndi misonkhano ya chikristu chakhala chosamvekakuchokera mu zaka 1700 ndipo kodi misonkhano iyenera kuoneka bwanji?Atate athu akufuna kubwezeretsa zinthu izi kwa inu mu moyo wanutsopano. Monga ngati mau a Mulungu adatayidwira mu matsiku a MfumuYosiya, ndipo choonandi chinakwiliridwa mu makhalidwe a ufumu ndimiyambo ya anthu, chonchonso lero Choonadi cha Mulungu, chakanidwa(koma chikadalibe mu Baibulo) koma chikhonza kumasula anthu muufulu. Mulungu adzasintha moyo wanu modabwitsa ndi kusinthanso aliyense ozungulira inu motsatira mwake. Ichi ndi choonadi champhamvundi cha mtengo wapadera. kaya muli anthu ambiri kapena ochepa m’mudziwanuwo, monga Yonatani, bwenzi la pafupi la davide adanenera, “Mulungusiali okanizidwa kupulumutsa kudzera mu ambiri kapena ochepa.” “Iyeamene wagwirizitsidwa oyenera kuonetsa kukhulupirika” Ife tiyenerakukhala ndi kulimbika mtima kuti tipangepo china chake chokhudzandi chilungamo chomwe chanyalanyazidwa kapena kusamveredwa kumbuyo kwapitaku. Ndi iye mwini wake adzakhala m’busa wanu, lingalanu ndiponso mulonda wanu ngati mukhala molimba mwa Iye.Ife tiyenera kukhala ndi kulimbika mtima, kukhala ndi misonkhanomonga mafotokozedwe a Baibulo mu Akorinto Oyamba 14, “pamenemubwera pamodzo, abale, wina aliyense ali ndi mau achilangizo, salimo,bvumbulutso” Palibe wina olamulira kupatula <strong>Yesu</strong> yekha. Ife timasonkhapamodzi poganizira m’mene “tingasulirane win andi mnzake ku chikondindi ntchito zabwino” (Ahebri 10:24-26). Ife tiyenera kuganizira ndikupempherera pamene tingathandizirane wina ndi mnzake pamenetibwera pamodzi, ndipo wina ali yense wa ife atengepo udindo kukhalachonyamulira cha Mau a Mulungu ndi chikondi cha Mulungu. Ife tili ndiali yense” kuganizira m’mene tingasulirane wina ndi mnzake ku chikondindi ntchito zabwino.” Ichi ndi icho chili mu Ahebri 10, chonde khalaniotsimikizika ndipo yang’anani pa malemba amenewa! ichi ndi cha tonse aife, ngakhale “mumisonkhano!”Akorinto Oyamba 14 akunena kuti, “pamene bvumbulutso libwera kwawachiwiri, siyani oyambayo akhale pansi.” Ichi ndi chimene baibulolinena. Nchifukwa chiyani sitichita chimene Baibulo limanena? Pasakhale“munthu wapadera” amene “mwachidziwikire” adziyembekezera kupangachili chonse kupatula kumvetsera ndi kuyankha kwa Mulungu mongawina ali yense. Ngati wina wake abweretsa chiphunzitso kuchokera kwa<strong>Yesu</strong> ndipo ena abwera ndi mau a chilangizo kapena salimo kapenabvumbulutso; ngati m’bale ameneyu kapena mlongo ameneyu akugawananafe chinthu china, chomwe <strong>Yesu</strong> waonetsa kwa iye ndipo bvumbulutsolabwera kwa wachiwiriyo, oyambayo akhale pansi - ngati tikumveralamulo la Mulungu, koposa miyambo ya anthu. MOnga m’mene baibulolimanenera nthawi zonse.Nchifukwa chiyani sitichita izi? Ndi chifukwa choti ife tatengerakatundu olemetsa wa miyambo wochokera ku katolika ndi kuchokeraku “maprotestant” ndiponso ku “dzipembedzo” ndi makolo athuopembedza mafano. “Ansembe” kapena “abusa” kapena “audindo” enaonse ali kutsogolo, kuyankhula kwa wofunikira “pang’ono”, anthu osaukaonse , anthu owonerera onse - atangokhala ndi kumamvera chabe. Ichimwachidziwikire ndi machitidwe ndi miyambo imene <strong>Yesu</strong> adati amadananayo, miyambo ya “Antikolatia” (kutanthauziridwa monga anthu amene‘agonjetsa anthu ake’) Koma Mulungu eti adanena kale kuti zonse iziziyenera kusintha chifukwa cha Iye ndi cha ife.M’malo mwake <strong>Yesu</strong> adanena kwa “bwalo lokhalo momuzungulira Iye”kuti ali yense ali ndi liu la chilangizo, salimo, bvumbulutso. Ife tonse tiliabale ndi alongo ndi zogowa zosiyana siyana othiridwa mwa <strong>Yesu</strong> ngatimwa m’modzi ndim’modzi pa chabwino chimodzi. Ndi chodabwitsandi chozizwitsa bwanji ichi! Iye AKUTIMASULA ife kuchokera ku110 111


“miyambo yopanda kanthu yomwe tidalandila kuchokera ku makoloathu” pamodzi ndi utsogoleri wa mpingo ndi miyambo. Iye akutimasuliraife ku dziko “loopsya” la kumukhulupirira ndi kumukonda IYE mongazonse mu zonse wathu! Ndipo sikukhala chiwawa kumeneko, chifukwaIye amadzitcha yekha, “Mulungu wa Mtendere” ndi “dongosolo” Ili ndidongosolo lake chabe, osati kutengerapo mwai kwa Iye.Madziko a kusinthaIchi ndi chosiyana kuchokera pazimene tidazolowera kodi? Kodi tili nakokulimbika mtima kumanga m’njira ya Mulungu? Kodi ndizopatsa mantha?Kodi zikumveka mosekesa: Kodi ndi chosangalatsa? Anthu ena amene tiligawo la Mpingo tidali mbali ya amene adakhala ali a Khristu kwa zakamakumi awiri koma akadalidi makanda. Koma pamene adadziwa njira izindi kuyamba kugwira ntchito ngati ansembe! Adakula kukula kofunikazaa khumi pa chaka chimodzi. Alleluya! Ena adakhala “atsogoleri”m’mipingo imene idali ndi anthu mazana ndi zikwi. Iwo adapeza kuti muuzimu akadali makanda! Iwo amaganiza kuti ndi atsogoleri, koma adapezakuti ana ndi amai ambiri adali a uzimu koposa iwe. Iwo amayenera kukulakuchokera kukhala khanda, ndipo adakula! Zonse izi ndi zopatsa manthakwambiri, komanso ndo zosangalatsa kwambiri.Ngati muika choonadi ichi chimene chakhala mu Baibulo nthawi zonsemudzakhala odabwa mmene mudzakhalire pafupi ndi <strong>Yesu</strong> zaka ziwirikuchokera pano. “Khalani limodzi tsiku ndi tsiku”. Monga pamodzi ndi anaanu, mabanja anu ndi kuntchito kwanu tsiku lililonse. Pitani kumeneko!Ndipo chokani kumalo kumene muli ndikuchita zimene simunachitepoinde ndikulankhulala ndi inu, chitani izi kwa <strong>Yesu</strong>. Lankhulani mauake monga mau a Mulungu kwa miyoyo yanu mwachitsanzo kundananimunzeru yabwino tsiku lonse. Pamene mubwera limodzi abale wina alindi kanthu nyimbo kapena vumbulutso. Pamene vumbulutso libwerakwa wachiwiri, woyambayo akhale pansi. Mukachita izi mudzapeza kutiena sakukonda <strong>Yesu</strong> ngati mmene mumaganizira. Ndipo ena amenemumawaganizira kuti ndiwofooka adzakhala amphamvu ndi a nzerukusiyana ndi mmene mumaganizira. Njira ya Mulungu imaonetserazinthu zopanda pake ndikukhazikitsa zofooka kukhala zamphamvu.Atamandike Mulungu!Chuma ichi chapatsidwa kwa inu muchigwiritse ntchito mokomera <strong>Yesu</strong>miyala imeneyi ndiye maziko mueyenera kuonetsera kuti Khristu ndindani monga <strong>Yesu</strong> ananenera. Mueyenera kudziwa utsogoleri umakhalaotani, khalani miyoyo yanu tsiku lonse, pamodzi limbikitsanani winandi mnzake manganani wina ndi mnzake, thandizanani kukula kukulandi kukonda <strong>Yesu</strong> kopitirira masana ano ndi madzaulo ano. Bweranindikukumanana pamodzi mozungulira Mfumu <strong>Yesu</strong>.Ngati mukonda<strong>Yesu</strong> ndikumanga njira yoeyenera, malinga andendesadzapambana ayi, uchimo udzawonongedwa, kufooka ndi matendakudzachiritsidwa. Uchimo udzakhululukidwa. Kukoma mtimakudzatitengera kukulapa. Ubale udzamangindwanso ndi kukonzedwansomopitirira mmene mumaganizira mumaloto anu abwino. Muzakhalaowala monga nyenyezi zakumwamba kuonetsera ubwino wa Mulungu.Ndi mkwatibwi, mpingo wake adzadzikonzekeretsa ndipo konzekeranipamene mkwati abwera. Amen112 113


Kubowoleza Kwa UlemereroOctober 3, 1999, Salima, Africa.Ngati tikumanga chomanga mwani nyumba uzakhumbila katundu;chochekela nyundo, misomali chomangila, chonenetsa mu nyumba yaMulungu. Pamakhala katundu wina wofunikila. Ngakhale zili chonchompingo onenetsa wa <strong>Yesu</strong> siukhuzidwa mu misonkhano, nthawi zinamisonkhano ndi yofunika monga zina zogwilira ntchito, ngati timayimbapamodzi mwa <strong>Yesu</strong>, pamakhala zinthu zina zimene timaphunzirakuchokera kwa abale ndi alongo. Ngati unapitako ku bwalo la milandundi kulakhulapo ndi iwo ngati amawona nthawi ya pa mkono, ndi kupitsamu thumba mwina kulankhula ndi ena. Oweruza safuna choncho ngatiukuyankhula ndi iyeyo utha kugona kusinza kapenanso kungozisiyachoncho kapena kusayankhulapo kanthu, akhoza kunena kwa inu.“tulukani mupite mukachite zenizeni. Mukakonzeka kumvera ineyo, muthakubweranso. Muntha kuchoka pokhapokha mutazikonzekelatsatso.Mulungu chimodzimodzi. Tikamayimbira <strong>Yesu</strong>, ngati timuyimbira muchoonadi <strong>Yesu</strong>, mitima yathu yimalumikizana naye. Maonekedwe ankhope yanu, kapenyedwe ka maso anu, mphamvu ya liu lanu kuthekerakwa kukhalabe mumaonekedwe izi ndi zinthu zonse zimene zili mbali yachiyanjano ndi mfumu ya mafumu. Msonkhano umakhala waphindu, ndipotsopano ndikupatsani chida misonkhano yimakhala ndi gawo lochepakusiya ndi moyo wathu mwa <strong>Yesu</strong>. Momwe tingathandizire abale ndi alongomonga a nsembe. Ngati pali munthu wina wayima pafupi ndi inu pamenemukuyimba pamodzi iye ndi kutaya chidwi mukuyimba, ndi chizindikilekuti akufuna kuthandizidwa. Kuti bvuto lake ndi chiyani. Mumayimbidweosangalatsa. Kuyimba ndi kulumikizana – kuyimbila mfumu ya ulemelero.Kwa nthawi zimalankhulidwa mu nyimbo yina, za mubuku na nyimboza uzimu ngati ndimalankhula ndi Yoswa ndi kusiya mwina kupenyamu mwamba kuona kusagwilizana ndi iye. Ndi pamene pakhala chidachothandiza kumanga nyumba ya Mulungu. Momwe Paulo anenera,“mukangano wa aliyense kuzionetsera kukwanilitsa, mwina kuziyeretsamwa khristu. Wansembe mwina ansembeyo ayenera kukanganirakuwoneka kwa aliyense moyera mwina kukwanilitsa mwa Khristu. Iyi ndi115


ntchito yanu mu nyumba ya Mulungu. Osati kukhala ndi kumvela, osatikuyimba kokha, koma baibolo likuti “tiyanganire kwa kuzionetsera mwaaliyense kulungama mwa Khristu”Ngati wina mwa inuyo ali ndi uchimo mwa mtima wosakhulupira.nde palizida kukuthandizani kuchita ichi. Ngati muli pamozi ndi aliyense kuimba,mutha kuwona nkhope zina, kuyera? Mutha kugwira chokhacho muonakumbuyo kwa mutu wawo. Koma tsopano tili banja ndipo tingaonanewina ndi mzake ngati ndili kuimba nyimbo kwa inu ndingathe kuona kwainu ndi kumwetulira ndi kuimba nyimbo ngati monga ndilankhula ndiinu. Ngati ndili ndi mtima wanga ndi kuyimba ngati kuti ndili kulankhulandi wina wake amene ndili ine. Ngati ndili kuyimba koma osakhudzidwandikugwedeza mutu wanga osalabadira ndi kumangoyang’ana uku ndi uko– ndiye uyenera kufunsa iwe kuti zili bwanji ine ndi ubale wanga ndi <strong>Yesu</strong>.Chodziwika ndi choti pali mabvuto amene ali ndi mgwilizano wanga ndi<strong>Yesu</strong> ngati ndili kulingalira zina pamene ndili kulankhula ndi iye.Baibulo limati aKristu wowona monga omwa mkaka, amafuna mkakawa uzimu wa mau a Mulungu Akristo wowona amafuna chiyanjano ndi<strong>Yesu</strong> monga mmene makanda afunira mkaka. <strong>Yesu</strong> anati kuti amene aliake chilakolako cha nyumba ta Atate chimatidya monga moto kunyeketsachitsulo. Tili ndi moto mu mafupa amane sangazimitsidwe. Ndipo ngatimuona wina amene ali chitsulo chonyowa ndipo moto sikunyeketsa,monga utsi, ndiye pafupi ka kuwathandiza iwowo.Chimodzi cha zida zothandizira kumanga nyumba ya Mulungu zimenezingakupatseni ngati chida chabwino ndi kukweza miyoyo yathu kwaMulungu. Ngati mungaone anthu amene Sali okhudzidwa kapenakuzichotsera kapena osasamalira kapena kukhala ongosangalala ndi za <strong>Yesu</strong>.Ganizani za izi ndipo pemphelani za iwo. Mwina pitani ku nyumba zawotsiku lililonse. Afunseni mmene ali kumvera, ndipo amene ali kumverazinthuzo. Nenani “ndaona kuti muli kulalikira naye <strong>Yesu</strong> ndipo simulinsokuonetsera chikondi kwa iye. Simunali kuika mtima wanu kwa zinthu izi.ndipo ndili odabwa ngati muli ndi mkwiyo pa zinthu zina. Ndi chiti chimenechilli chopambana pa moyo wanu koposa <strong>Yesu</strong>? Kodi mwalankhura munthawi yabwino ndi <strong>Yesu</strong> mukupemphera kwanu kwapadera? Kapena mulikupezeka chabe mu msonkhano pamene chiyangano ndi iye. Sichili bwino?Choncho ichi ndi njira imodzi imene mungathandizilane nonse pamodzikukhala mwa <strong>Yesu</strong> ndikukhala tcheru ndi anthu nonse pamodzi pa maloamodzi. Iyi ndi nira imodzi imene ife ansembe osati ongoonera chabe.Zimene anthu oipa amanenaPanali munthu oipa tsiku lina otchedwa Kaini mukumbuka Kaini,mwana wa Adamu. Anali oip china chimene ananena ndi choti. Saliosamalira mbale wake. Anthu oipa matero ndithu ife ndife osunga mbalewathu. Timakondana wina ndi mzake kuchokera mu mtima wakuya.Timalimbana kudzipeleka wina ndi nzake molungama kapena watunthumwa <strong>Yesu</strong>. Tidali mu zowawa mkubadwa kwithu mpaka <strong>Yesu</strong> wakhalamomwa abale ndi alongo. Izi ndi zimene tinena kwa inu. Nchifukwa chaketabwera kuchokera ma dela onse osiyana a dziko kudzakuwuzani zinthu izi;Tabwera kudzayetsetsa kudzalengeza kwa inu za chilungamo mwa <strong>Yesu</strong>.Ndipo muyenera kuchita ichi kwa wina ndi nzake mchilungamo mwa<strong>Yesu</strong>. Si inu ndi chiyanjano chanu ndi Mulungu. Ndife ambiri koma ndifeamodzi mwa <strong>Yesu</strong>, bukhu loyera likutero. Ngati chala chanu chikudwalakapena chilli ndi vuto lina lake, mumayamba kumva mutu kupweteka,mumamva kuzizira – thupi lanu lonse limaphwanya. Ndizowonansondi thupi la <strong>Yesu</strong>, ngati mmodzi wa ife wavulala mu uzimu tonsetimakhudzidwa mu uzimu.Ndife anthu osunga abale, ngati muwona wina wake amene ali ndi vuto ndichiyanjano chake ndi Mulungu mkupembedza kapena mukaleledwe kaana kapena munjila ina, tiyenela kuthandizana wina ndi nzake. Ife mmenetili ambiri ndife amodzi. Ndife amodzi wina ndi mzake kupyola mtunda,kupyolanso zaka. Ndife amodzi ndipo timafanana wina ndi nzake. Ndipotimakondana pothandizana wina ndi mzake kukula mu uzimu.Ndiye chida mmanja mawanu pakumanga kachisi wa Mulungu ndikumvetetsana wina ndi mzake – tikakhala malo amodzi. Ndipongati muwona wina wake safuna kulowa mwa Mulungu ndi mwaanthu ena.(ali pano potha chabe nthawi) ndipo ndiowonangedwa, ndiye muyendakulowa mmiyoyo mwawo ndi mmakomo mwawa ndikuwatenga iwo ndidzanja ndi kuwathandiza kumukonda <strong>Yesu</strong> kwambiri. Ndinu woyanganila116 117


mbale wanu. Tiyenela kuthandizana wina ndi mnzake. Timvetetsane winandi mzake.Pamene tinayimba nyimbo yotsiliza kodi mudalumikizana ndi mtima waMulungu? Ndipo kodi mudayamba mwayangana malo okuzungulilaningati alipo akuvutika? Ena amene alibe chidwa? Ena amane awukiraMulungu ndipo akufuna machilitso enei eni?Ena amene ndi ofowoka ndiye sakumvetsetsa bwino, zilipo zina pang’onomwa zinthu zimenezi. Chifukwa takhala womangidwa ntahwi yayitali,sitinathe kupeleka chidwi ku zinthu izi. ino ndi nthawi imene tiyenelakukula ndi kutengapo gawo mu nyumba ya Mulungu. Tsopano zilim’mznja mwathu pamodzi kutumikila zolinga za Mulungu mu mbadwowathu. Amen?Pamene zili zowona kuti zinthu izi zingathe kudzetsa kugawikana, zithakuwonetsa poyela za mkati mwathu zobisika pamene tinkavina ndikulambila. Anthu ena amakonda kuwala ndipo ena amadana ndi kuwala.Tsono kukhala koteleku kudzetsa kugawinikana chifukwa ena amakukondakuwala ndipo ena amadana ndi kuwala. <strong>Yesu</strong>anati sindinadze kubweretsaMtendere koma lupanga. Nthawi zina zitha kugawanitsa anthu ambanjawina ndi mzake.Uthenga WabwinoIfe tomwe tili ndi mipatuko. Muyenda munjila kumene mwalowela,muwona mtundu yonse ya kugawikana. Mpingo wa <strong>Yesu</strong>, Nazarene,Lutheran, katolika. Pali kugawinikana kwakukulu. Koma, pano pali uthengawabwino. Ngati mukhala ngati ufumu wa Mulungu monga chipembedzochimodzi, ngati mulalika za <strong>Yesu</strong> lalikani osati chipembedzo, ngati mufumamuthandiza anthu ena – kukonda <strong>Yesu</strong> kuti tichotse chimo, ndi kukhalaabwenzi a Babasiti. Alutherani ndi ena otere, aliyense adzayamba kusiyazizindikiro, ndi zimene zidzachitika muno mu Salima? Pamene aliyenseadzabwera ndi kudziwa mabvumbulutso ndi kumamvera iwo uku ndiuko mu misewu. Sipadzakhalanso kusiyana. Koma kusiyana kudzakhalapakati pa ofuna kukonda <strong>Yesu</strong> ndi amene safuna kukonda <strong>Yesu</strong> ndikumvera <strong>Yesu</strong>. Mmalo mwa zopusa zimene zili zimene tili nazo tsopanokusiyana kudzakhala mu kukondana ndi kumvera ndi osati miyamboyathu, ndipo <strong>Yesu</strong> adzakhala ndi umboni mu mzinda uno mu umodziumene sunalipo ndi kale lomwe. Ndi chifukwa chake ndi chofunika kutimumange mu njira imene tili kulankhura kwa inu lero fikirani miyoyowanu kwa okhulupilira mu mzinda uno ndi kuthandiza kumanga munjira imeneyi. Potere sipadzakhalanso kusiyana ndi mayina kusiyana kwaamene akufuna kukonda ndi kumvera <strong>Yesu</strong> ndi amene angofuna kusewerandi “chipembedzo” siuthenga wabwino kodi?Ngati tingaphunzire kukhala motere, miyoyo wa anthu idzasintha. Anthuadzaoneka monga <strong>Yesu</strong>. Padzakhala wina amene muli kumusamalirakwambiri ndi inu ndi ena onse pamodzi mudzalimbika kuti mumuonetserewatunthu kwa <strong>Kristo</strong>. Mudzamuona munthu ameneyu kupanga chiganizochomvera <strong>Yesu</strong> ndikuona kusinthika mu moyo wa munthuyo. Kodimukudziwa kuti mudzakwanitsa ngati muli nonse pamodzi ndi abalendi alongo? Mudzaimba mokweza chifukwa mudzakhala mukuyamikaMulungu pazimene ali kuchita. Simudzaganizo inde, ndiyimbe mokwezaine ndine wa “Pentekositi” mudzayamba kuganiza kuti <strong>Yesu</strong> wapangazinthu zopambana moyo wanu. “ndifuna kumuyamika iye.” Zimenetikulankhula lero lino pano – zimene miyoyo wa anthu idzasintha,mmene <strong>Yesu</strong> adzabwera kwa anthu ake. Ndizimene tidzaimbira nyimbo!Ndizimene tizayamika nazo Mulungu koposa!Satana adzaonongedwa mu miyoyo yathu ndi zimene tidzayamike nazoMulungu koposa!Ndikukuuzani kuti pamene tinayamba kuyenda mu zinthu izi zaka khumindi zisanu zapitazo zinali zomvetsa mantha ndi zolimbikitsa kodi muli ndimantha otere?Mukuoneka olimbika koposa mmene ine ndinalili chifukwa zinali zobvutakwa ine poyamba. Koma patapita zaka khumi ndi zisanu ndi zikwi za anthumu dziko lonse lapansi amene anayamba kuyenda mi zinthu zimenezi ndizabwino ndipo mantha anatha,choncho Mulungu adzatsinjiliza mu nzerundi chikondi pamene mupita patsogolo mu zinthu izi. adzatipatsa zosowazathu monga mwa kuchulukwa mu ulemerero wake. Zizakhala bwino,adzakhala Atate kwa ife. Adzakhala mphunzitsi ndi otikonda miyoyoyathu. Ndipo tidzapitilira mu njira zobvuta zambiri. <strong>Yesu</strong> adzapambana mumsewu ndi mzinda yonse uno, adzapambana mu mitima yathu. Pamene118 119


mantha, kuzikonda, ndi kunyada zimakhala. Adzatichapa ife ndikumangaife odzadza ndi afulu mu njira pa zimene sitingafunse kapena kuganizira.Zinthu izi ndi zoona ndipo mudzakhala mu zimenezi ngati mudzatsegulemoyo wanu ndi kupita patsogolo.Pamene Yoshua anapita mu dziko lalonjezo Mulungu anati “osachitemantha” ndipo pamene ansembe anayamba kulowa mu mtsinje kunalikobvuta kwa iwo pang’ono, Baibulo limati sanayendepo njira imeneyimbuyomu ndipo Mulungu anati “chabwino” ndidzakhala nawe” ndipozinthu izi ndi zoona kwa inunso. Osati pa malo pano pokha ndi maloozungulirz mzinda uno. Mulungu adzakhala ndi inu pamane mudzapitapatsogolo ndi mau ake. Khalani ndi mphamvu ndi kulimbika! Mulunguakuti “monga ndinali ndi Mose monganso ndinakhala ndi iwe mu nthawiyapitayi choncho ndidzakhala ndi iwenso monga mmene uli kupitirachitsogolo osaopa ai”Abale ena atalankhulanso popeleka miyoyo yawo.Abale ndi alongo mwaona zimene zikuchitika pano lero? Tayamba kuonaufumu wa Ansembe. Pamene bvumbulutso libwera kwa wina okhalapo.Woyambayo akhale pansi. Ndipo pamene bvumbulutso lafika kwawinanso ndi winanso!! (kunali kukuwa pokweza mau)Mipando IsanuLachiwiri Masana Salima, Malawi October 5,1999Mwachisomo cha Mulungu, ndifuna ndiyikize kwa inu zida zina zakuvetsetsa ndi kuzindikira makhalidwe a anthu. Tingoyezera, kwakanyengo kamene tili nako pano ife, mipando isanu. Ndipo akukhalamipando isanu imeneyi ndi anthu asanu kuyimirira mitundu isanu yaanthu amene inu mwachidziwikire mukumane nayo pa ulendo wanupadziko lapansi.Mipando iwiri yoyambaMu mpando oyamba, tili ndi osakhulupirira kapena wamafano wina wakesakhudzidwa ndi zotsata <strong>Yesu</strong> ndi pang’ono pomwe. Mwina munthuameneyu ndi msilamu kapena Mhindu. Munthu uyu samazitcha kukhalaMkhristu .Mu mpando wa chiwiri, ngakhale,tili ndi munthu amene amazitcha kutiamasatira <strong>Yesu</strong>, koma munthu uyu samvera <strong>Yesu</strong>. Pa misonkhano, munthuuyu amaoneka ngati okonda<strong>Yesu</strong>, koma iye samkonda zenizeni chifukwa samvera iye. Mu Mateyo7, <strong>Yesu</strong> adati padzakhala ambiri amene adzanene “Ambuye, ambuyepadzakhala ambiri amene adzagwire ncthito yotamandika mu dzina lake,koma ku amene iye adzanena “Ndichokereni ine, ine sindikudziwani inu”Aliyense akudziwa kuti munthu wa mpando woyamba sali owomboledwachifukwa munthuyu sazitcha ngakhale pang’ono kuti amasatira <strong>Yesu</strong>.Ife timadziwa kuti pokhapokha ngati uli ndi mwana, siungakhale ndiAtate. Pokhapokha ngati ukhulupira mumtima wako kuti mulunguadaukitsa <strong>Yesu</strong> kwa kufa, Mwazi siudzatsuka tchimo lako. Munthuuyu sangapulumutsidwe chifukwa iye sakhulupirira mwa <strong>Yesu</strong>. Mwaziwa <strong>Yesu</strong> siutsuka machimo amunthu otereyo. Kufikira munthu wapampando woyamba uyu atadzipereka kwa <strong>Yesu</strong>, iye sangapulumutsidwe.Iye akhoza katengedwa kukhala munthu wodabwitsa ndi tate wa bwinondiponso wacthito wabwino, koma iye sangapulumutsidwe kopandakuyeletsedwa ndi mwazi wa <strong>Yesu</strong>.120 121


Kumbali yinayi, munthu wa mpando wachiwiri anena “ine ndine mkhristu”koma makhalidwe amunthu ameneyo ndi oyipa, ngakhale kuti munthu uyuakhoza kupanga ncthito zabwino zowoneka mzina la <strong>Yesu</strong>. Mu uthengawabwino wa Luka, <strong>Yesu</strong> adati kuti pa tsiku la chiwerunzo, anthu ngatiuyu adzanena, “<strong>Yesu</strong>, mudaphunzitsa makwalala athu. Mudadya magomeathu. Ife tidapanga zozizitswa mu dzina lanu. Tidapereka chuma chathukwa osauka”, koma <strong>Yesu</strong> amanena kwa anthu awa mu mateyo 7:21. “inusimudamvere ine inu simudapange funiro la atate. ine sindidakuziweniinu. <strong>Yesu</strong> akuonetsa apa kuti anthu ambiri amene mazictha a khristundi mpakaso amapanga nchito za mphavu mun dzina lake ali munjira yachikulu yomwe imasogolera ku chionongeko. Anthu awa amanamizirakukhala a khristu, amanamiziran kuti ali ndi mamembala a mpingo, komamzenizeni saali choncho.Munthu wa mpando woyamba siali opulumusidwa chifukwa chakusakhulupirira. Munthu mumpando wachiwiriwo siali opulumusidwachifukwa chakusamvera, kumene Baibulo limanena kuti ndiosakhulupiriranso.Mipando itatu inayoTsopano anthu amipando atatu yotsaklayo ayimirira choonadi. Otsatira a<strong>Yesu</strong> ogulidwa ndi mwazi . Atatu awa ndiwo a khristu koma ndifuna kuunikakuti pasakhale chisokonezo ndi munthu wampando wachiwiriwo.Muli ndime zogwirizika kwambiri mu Yohane oyamba 2 imeneimaonetsera ndikuzindikiritsa anthu amenewa amene tili nawo mmipandoitatu yomalizayi. Yohane adati “Ndikulembera kwa inu ana ang’ono,azibambo ndi kwa inu achinyamata” Tsopano mmganizo athu a nthawizonse mudongosolo la zinthu ndi ana ang;ono, achinyamata ndiponsoazibambo sichoncho. Koma Mulungu akupereka dongosolo ili, “ana,abambo, achinyamata”Ana, abambo, achinyamata awa ndi anthu opulumusidwa. Awa ndi anthuamene amakhulupirira kuti <strong>Yesu</strong> ndi mwana wa mulungu, ndipo machimoawo ndi wokhululukiridwa ndipo ndi osambitsidwa ndi mwazi wake.Mpando wachitatu uyimira ana, mpando wachinayi uyimira abambo ndipompando wachisanu uyimira achimata. Inu mukhoza kuganizira iwo mongamakanda , anthu okhwima kapena akuthekera ndipo kenako chinthuchimene ndikufuna kuti ndionetsere bwinobwino ndi chakuti nthawizina makhalidwe a ana ngakhale kuti iwo ali opulumutsidwa, amaonekangati makhalidwe a anthu asapulumutsidwa (ngati munthu wa mpandowa chiwiri). Koma munthu wa mpando wa chitatu (Mwana weniweni)ndi osambitsidwa ndi mwazi wa <strong>Yesu</strong>. Munthu uyu wa mpando wa chiwiriakhoza kuzitcha kuti anasambitsidwa m’mwazi wa <strong>Yesu</strong>. Munthu ameneyoakhoza ngakhale kuimba nyimbo zokhudza Mwazi <strong>Yesu</strong> kuwapulumutsaiwo , koma chifukwa munthu uyu akhoza pang’ono ndi pang’onoKupita mpaka kupandukako kwa <strong>Yesu</strong>, munthu uyu siotsatira wa<strong>Yesu</strong> weniweni. Aliyense amene amazitcha kuti ali mwa iye , ayenerakuyenda m’mene <strong>Yesu</strong> adayendera. Aliyense amene sadzamvera kwa<strong>Yesu</strong> adzadulidwa kuchokera pakati pa anthu “Aliyense amene ali ndichiyembezo ichi adziyeretsa yekha monga iye ali woyera. Palibe ameneadabadwadi kwa mulungu amene adzapitilira kuchimwa chifukwa mbewuya mulungu imakhalira mwa iye, iye sangapitirire kuchimwa chifukwa iyeali obadwa mwa mulungu.Njakata ya mpando wachiwiri/Mpando wachitatuNthawi zina khalidwe la munthu wa mpando wachiwiri likhonza ngakhalelukhalako labwino kuposa khalidwe la munthu wa mpando wachitatu.Koma pali chinthu china chimene muyenera kumvetsetsa chokhudzanandi uthenga wabwino wa <strong>Yesu</strong>. Munthu wampando wachitatu ndikufunafuna kuyeretsedwa mu Mwazi wake. Mu Aefeso I ndi Agalatiya3 Mulungu adati kuti pamene munthu akhulupirira mu mtima mwake(osati mmutu mwake) mwa <strong>Yesu</strong> khristu kuti amapatsa munthu ameneyoMphatsoYa Mzimu oyera kuti ikhale mkati mwake. Mzimu oyeraumapatsidwa kwa aliyense amene akhulupirira moona ndipo akhulupiriramwa <strong>Yesu</strong> kuchokera mu mtimaTsopano muli mu njakata. Ngati inu mukungoweruza kudzeramumakhalidwe , ungadziwe bwanji mmene ungachitire? Nangabwanji utakumana ndi mkhristu wa chimwana amene ali ndikhalidwelosasangalatsa , ndipo muli ndi osakhulupirira amene amazitcha m’khristukoma pa zonse mungaone , mungaone mwina ali ndi khalidwe la bwinoko?122 123


Chabwino kodi alipo wina amene adapulumutsidwa ku machimochifukwa cha khalidwe la bwino? Kodi ichi ndicho uthega wa bwino wa<strong>Yesu</strong>? Kodi uthenga wa bwino ndiwoti kupulumusidwa ndi makhalidweathu abwino? Ayi sichoncho! Ife tapulumutsidwa ndi mwazi wa <strong>Yesu</strong>. Ifetapulumutsidwa ku machimo athu ambuyomu, ndipo tapulumutsidwa kumachimo obwera mtsogolo ndi Mwazi wa <strong>Yesu</strong> khristu.Tsono kenako, nchifukwa kumanenedwa mbaibulo mbuku la Agalatiyakuti aliyense amene akhala ngati wochimwa sadzalowa mu ufumu wamulungu? Ichi chikumveka kuti chipulumutso chathu ndichokhuzidwandi makhalidwe athu. Koma ife timadziwa kuti ichi sichingakhalechoona ife tinapulumutsidwa ndi mwazi wa <strong>Yesu</strong>, osati makhalidweathu. Tsono keneko nchifukwa chayani Baibulo limanena kuti aliyenseakhala mmachimo sangalowe mu ufumu wa mulungu ndipo sadzapitakumwamba? Nchifukwa chiyani <strong>Yesu</strong> amati, “Nkhosa ndi amene achitachifuniro changa ndi kundimvera ine, ndipo Mbuzi ndi amene sandimveraine? <strong>Yesu</strong> adati nkhosa zikupita kumwamba ndipo Mbuzi zikupita kuGahena. Ndipo <strong>Yesu</strong> adati mudzidziwa nkhosa kudzera mu zi ntchitozawo. Ichi chikumveka ngati tinapulumutsidwa ndi makhalidwe athu.Koma ife tidziwa izi sizoona.Kuthana ndi njakataKodi uthenga ndi chiyani apa? Kodi timamveka bwanji mbali iyi ya uthengawabwino? Chabwino ichi ndi chisisi cha uthenga wa bwino wa <strong>Yesu</strong>.Aliwonse amene amapereka mitima yawo kwa <strong>Yesu</strong> ndipo atembenuka kumachimo ndikusiya zammbuyo mwawo amapatsidwa Mphatso ya mzimuoyera. Ife timawerenga mu buku la Yohane Oyamba kuti pali zizindikirozambiri zimene mzimu wakukhala mkati umaoneka ngati moyo waumunthu. Pali ambiri amene adzanena “Ambuye,Ambuye” koma adzamva<strong>Yesu</strong> akuti” sindikukudziwani ndi pang’ono pomwe” Tsono ife tikudziwakuti munthu saali mkhristu chifukwa choti munthuyo amazitcha kukhalakapena amachita zinthu zooneka zodabwitsa mzina la<strong>Yesu</strong>.Buku la Yohane Oyamba lidalembedwa mu zaka zokwana makumiasanu ndi limodzi patangotha pentekosti. Mtumwi Yohane mwina adalindi zaka makumi asanu ndi atatu ndi mphambu zisanu kapena makumiasanu ndi anayi. Yohane adali ndi zaka zambiri kuti aganize kapena kutiapemphere zokhudzana ndi chikhristu chimaonekera. Pa nthawi imeneyi,zaka makumi asanu ndi limodzi patatha masiku a Pentekosti, padali anthuambiri omwe adali atakula mpingo. Padali makanda atsopano obadwaamene adakula ndipo adali ndi ana awo nawonso pa nthawi imaeneyi.Tsono pamene anthu amene adakula akunena mau olondola chifukwamakolo awo adanena mawu olondola pa nthawi imeneyi, padali anthuambiri amene “adakulira mumpingo” ndipo mwachoncho adadziwanyimbo ndi akhonza kuomba mmanja ndi kuimba ndi kunena mawu onseolondola. Koma Yohane adadziwa kuti ngakhale ana akhonza kuoneka akhristu, iwo akhonza kukhala asanadzipereke miyoyo yawo moonadi kwa<strong>Yesu</strong>. Munthu si mu khristu chifukwa choti mmalingaliro amakhululupirirazinthu zoona. Munthu, kutengera pa <strong>Yesu</strong>, sim khristu mkhristu chifukwachopanga zinthu zozizwa mu dzina lake. Padzakhala anthu pa tsikulo,amene adapanga zozizwa mu dzina lake, ndipo iye adzawauza iwo“Ndichokereni ine kunka kunja ku mdima. Ine sindidadziweni inu.”Gawo la mzimu woyeraMonga ndidanena buku la Yohane Oyamba adalembedwa zaka makumiasanu ndi limodzi patatha pentekosti. Yohane amayankha ambiri mwamafunso amenewa amene mwa chidziwikire iye adayenera kukumananawonso.Yohane adalemba zinthu zosiyana zambiri mu buku la YohaneOyamba zimafotokoza chimene mkhristu weniweni amaoneka ngati.Nthawi ndi nthawi iye amalongosola chimene chimaoneka ngati winawake ali ndi umboni wa Mphatso yakukhala mkati ya mzimu oyera.Baibulo limati kuti aliyense amene ali mkhristu oona ali ndi gawo kapenagawo la malipiro otchedwa mzimu Oyera.Pamene munthu akugula nyumba kapena galimoto, nthawi zinaamapereka mbali ya malipiro kapena malipiro oyamba gawo limenelo.Kapena mbali ya malipiro oyambawo amakhala ngati chikole kutimalipiro onse adzabwera. Baibulo limati kuti Mulungu, monga mbaliya malipiro , adapereka mzimu woyera kwa aliyense okhulupirira. Ichindi chitsimikizo kwa ife kuti ife tidzatenga moyo kwamyaya. Ngati winawake akusoweka mbali ya malipiro imeneyi, gawo la Mzimu woyera, ndichidzindikiro kuti pakhala popanda pangano kapena mgwirizano pati pamunthuyo ndi <strong>Yesu</strong>.124 125


Ichi ndi chifukwa chake Yohane, mtumwi adati kuti kusiyana kwaMkhristu ndi osakhulupirira sikulapa kwa ngati amapanga zozizwitsa,kapena ngati amakhulupirira zinthu zolonda, koma ngati ali ndi mzimuwoyera . Ndipo chimaoneka bwanji pamene munthu moonadi ali ndimzimu woyera ? Kodi ndikupanga zozizwa ? Kodi ndikuyimba ndikukhala nawo misonkhano ? Ayi izi siziwonetsera zimene zimathandizaife kumvetsetsa amene ali ndi mzimu ndiponso amene alibe . Munthuwampando wachitatuwo , amene ali mwana wachikhulupiriro, akhozaakhonza kukhala kuti adanzipereka kwa <strong>Yesu</strong> kuchokera mtima, komaakhoza kuonetsa khalidwe loipa nthawi zina.Ena anakonda kuwalaYohane ndi <strong>Yesu</strong> anapereka kwa ife yesero lofinika kwambiri kutithandizaife kutolapo kanthu pa chisokonezo ichi. <strong>Yesu</strong> anachiyika choncho, “Enaanakonda kuwala ndipo ena amadana ndi kuwala” (Yohane 3) Yohane adati“Ngati ife tikhonza kupitiriza kuchimwa, ndiye kuti Sitidziwa . Mulungu.,ndipo ife tawonetsera kuti ife tilibe Mzimu Oyera.” (1 Yohane 1:4).<strong>Yesu</strong> adati “Ena anakonda kuwala, ndipo ena anadana ndi kuwala.”Makhalidwe a munthu uyu opulumutsidwa akhoza kusakhala wabwinonthawi zina, koma chifukwa munthu uyu ali ndi Mzimu Oyera mmoyowake, munthu uyu adzakonda kuwala ndi choonadi. Monga khandalobadwa kumene, munthu uyu adzakakamira pa mkaka wa uzimu waMau. Pamene mudzayandikira munthu uyu ndi kunena , “khalidwelako ku nchito, kapena ndi mkazi wako ndi losakhutitsa m’bale. Kodiukudziwa kuti pamene uchita zinthu izi wukuwawitsa mtima anthuambiri kuphatikizirapo <strong>Yesu</strong>?” Munthu wa mpando wa chitatu uyu akhozakuyamba kulira ndipo nati “ukunena zoona. Ndikudziwa kuti ukunenachilungano. Mu mtima mwanga ndine odandaula mmene ndawachitiraakazi anga. Zikomo pakubwera kwako kudzandiuza . Ine ndikufuna iweundiuze zinthu zimenezi. Ndikufuna thandizo lako.” Uwu ndi umboniwaukulu kuti munthu uyu ali ndi Mzimu Oyera ndipo ali oomboledwa.Mwina makhalidwe a munthu uyu siabwino ku nyumba kapena kunchitopoyamba, koma Baibolo likunena kuti ngati wina ndi opulumutsidwa,Mzimu Oyera udzadzionetsera Okha ndi chikondi pakuwala ndichoonadi. Munthu uyu adzati, “ndipempherere ine! Umufunse <strong>Yesu</strong>adzandithandize! Chonde Iwe ndithandize ine? Ndikuyitanira iwekulankhula mau ndi nzeru za <strong>Yesu</strong> kwa ine nthawi zonse. Ndidzatsegulamtima wanga ndipo ndidzalandira kuwala ndi choonadi ndi Unsembewake wa okhulupilira onse.”Kodi munthu wampando wachiwiri anganene chiyani? Munthu uyu alibeMzimu Oyera. Munthu uyu akhonza kuwoneka kuchita zozizwa mu dzinala <strong>Yesu</strong>. Munthu akhonza kuyimba ndi kuvina ndipo ngakhale kulalika,komabe alibe Mzimu Oyera. Kodi mukudziwa kuti munthu uyu alibendipo ndiosapulumutsidwa kwenikweni? Chifukwa pamene mupita kwamunthu uyu ndi kunena, “khalidwe lako silabwino m’mene uchitira mkaziwako,” munthu uyu amanena, “kodi ukundiweruza ine! Chotsa chipikachakocho pamaso anga! Ukhala walamulo iwe! Samala za machitidweako! Kodi ukuwona ngati ndiwe ndani ukandiyankhule ine choncho?Usakhudze ozozedwa wa Mulungu!” Munthu uyu siopulumutsidwachifukwa munthu uyu sakonda kuwala. Pali umboni wa mphamvu kutimunthu uyu alibe Mzimu Oyera, chifukwa munthu uyu sakonda kuwala.Ena anakonda kuwala ndipo tsono ali opulumutsidwa. Ena anadanandi kuwala ndipo ali osapulumutsidwa (2 Atesa. 2:10). Ena anakondakuunika ndipo ena anadana ndi kuunika chifukwa cha zochita zawo ndizoipa (Yohane 3:19-21).Tsono ngati muweruza kudzera m’makhalidwe, mudzasokoneza. Nthawizina khalidwe la anthu ampando wachiwiri ndi wachitatu limaonekalofanana. Mu zoona, nthawi zina ampando wachiiriwu, amaoneka panthawi, kuti akupanga zinchito zabwino m’malo mwa <strong>Yesu</strong>. Koma <strong>Yesu</strong>mu Yohane 3, ndi Mtumwi Yohane mukukalata wa Yohane Oyambaanena khalidwe silimene munthu wungaweruzire. Inu mukhonzakumvetsetsa za amene ali ndi Mzimu. Ndipo chifunguro cha umbonichakuti Mzimu wukukhala mkati mwa munthu ndi m’mene munthuyoapangira ku kuwala.Pangano latsopanoNdidzapitanso kumbuyo mu Chipangano Chakale kuti ndionetseremfundo iyi. Uneneri okhudzana ndi kubwera kwa <strong>Yesu</strong> ku Chipangano126 127


Chatsopano ukhonza kupezeka mu Yeremiya 31 ndiponso mu Ezekiele 36.Mumalo onse awa, Iye adanena chinthu chimodzi chokhudzana kubwerakwa Pangano Latsopano. Mulungu adati kuti Mupangano Lakale munthuamanena kwa mzake, “Mudziweni Ambuye!” (Ife tayetsetsa kubwezeretsaPangano Lakalemu mpingo mfundo yolakwika).Pangano Latsopano, kutengera kwa onse Yeremiya ndi Ezekiyele,ntchito ngati izi: “Umboni oti ndakhululukira machimo awo ndiposindikukumbukanso zoyipanso zawo, umboni oti ndakhululukiradimachimo awo ndipo ndawapanga iwo akhristu oti ndidzayika Mzimuwanga mwa iwo ndipo ndidzapanga iwo kusunga lamulo langa.” Umboni otimunthu ndi mkhristu weniweni ndipo machimo awo ndi okhululukidwa,kutengera ndi uneneri wa zaka mazana asanu ndi limodzi pasanafikenthawi ya <strong>Yesu</strong>, ndilo kuti <strong>Yesu</strong> adzayika Mzimu wake mwa iwo ndipo Iyeadzatembenuza mitima yawo yamiyala ndi kukhala mitima ya mnofu. Iyeadzayika Mzimu mwa iwo ndi tsopano nkhosa zidzadziwa mau a m’busa.Umboni wa mzimu oyeraMkhristu, olengapo gawo la pangano latsopano, amakonda choonadi (2Atesa. 2:10) ndipo amakonda kuunika (Yohane 3:19-21) ndipo tsopanoali “otengapo gawo la chilengedwe CHAUZIMU” (2 Petro 1:4, Aroma6:1-14). Uwu ndiye umboni woti Mzimu umakhala mwa iwo kapenamwa wina aliyense wa ife. Ife sitiyenera mau a aliyense pakuti chifukwaakuti, “Ambuye, Ambuye! “Iyi ndi nkhani yabwino! Amafano kapenaazipembedzo zonyenga sangalamulirenso Mipingo! Ife tikhonza kumveratsopano, kuchokera mu ubale, ulamuliro oti “chotsani chotupitsa mumkate” wapanda kukhala “moweruza!” Ngati iwo samakonda kuunika kwakuonetsera chifukwa amakhumbitsitsa kukula mwa <strong>Yesu</strong>, koma koposaamathawa ndi kukana kutsekereza ena kudzera mkudzitchinjiriza, sialiopulumutsidwa, kutengera kwa <strong>Yesu</strong>, ndipo sangatengedwe kukhala gawola Mpingo Wake. Tsopano, kumbukirani: NDI CHIBALE CHATSIKUNDI TSIKU CHOKHA chimene mungadziwire ngati aliyense akondakuwala ndi choonadi ndipo potere ali mwana wa Mulungu. Misonakhanoyochepa pasabata sidzalola aliyense kudziwa ngati wina wake amakondakuunika ndipo ali chabe ofooka, kapena ngati iwo amadana ndi kuunikandipo potero siali opulumitsidwa. Ngati iwo sakonda choonadi ndikukhumbira icho ndi mitima yawo yonse (koposa kukana mchoonadindi kunyada ndi kudziteteza ndi kutsatsirana kulakwa). Kenako MzimuOyera amanena kuti iwo siopulumutsidwa konse. Ichi ndicho chothandizakwambiri kumvetsetsa: Ngati iwo ali opulumutsidwa, ADZAKHALAndi Mzimu Oyera (Aroma 8:9, Agalatiya 3, Aefeso 1). Ndipo UMBONIoti iwo ali ndi Mzimu Oyera mwa iwo (ngakhale nthawi yambiri bwanjiiwo akuuzani iwo “umboni” waukulu ndipo anena, “Ambuye, Ambuye!“Mateyu 7) ndi oti amakonda kumvera. Ali obadwa atsopano ndipoamakonda kuwala ndi kukonda choonadi, (2 Thess 2:10) ndipo mongamakanda amakonda mkaka ndi mau a Mulungu kuchitidwa mu moyowawo (1 Petro2).Mu Chipangano Chatsopano sitikakamiza munthu kudziwa Mulungu.Sitinena kuti “sintha makhalidwe ako kuti ukhale Mkhristu tsopanotinganene”. “Khalidwe lako silili ngati la <strong>Yesu</strong>”. Okhulupilira wowonamonga makanda akonda mkaka amati, “zoona” Mulungu andikhululukireine mungandikhlulukirenso ine 1 Akorinto 12 ndi Aefeso 4 amati ndilikufuna kuthandizidwa kuti ndikhale monga wa <strong>Yesu</strong>. Mungandithandizechonde mundipempherere ine ndipo ngati mungawonenso ndili kuchitachomwecho chonde bwerani kwa ine ndipo ngati sindili kumveranso inubwino, chonde tengani awirii kapena atatu bwerani ndi kulankhula ndi inemu njira imene Ambuye ndi okondedwa <strong>Yesu</strong> anatilamulira.Mukumbukira malembo mu Mateyu 18? Ngati mulankhula kwa mbalekapena mlongo ndipo poyamba sakumva ndi kudziwa bwino, <strong>Yesu</strong> amatitengani awiri kapena atatu kuti athandize kuti amvere. Ndiyenso ngatisamveranso ndikuti sakusintha yankhulani ndi mpingo wonse. SizimeneAmbuye athu anatiphunzitsa?Onani pa mtima, osati makhalidweMtima ndi choonera kuti Mzimu Woyera uli kukhalamkati mwa munthu.Mphatso ya Mzimu Woyera uli kukhala ndi dipo limene limatipatsacholowa chathu, ichi ndi chiweruziro chake amatero <strong>Yesu</strong> mu Yohane3. Ichi ndi chimene chimatisiyanitsa osalakwa ku chiweruzo. Osatialiyense ndi wabwino, koma amene machimo awo akhululukidwa onsendi kukonda “kuwunika”. Ali ndi mphatso ya Mzimu imene sanali nayo128 129


poyamba. Tsopano kuchokera pansi pa mitima yawo yowuma tsopanondiwofewa. Pansi pa mtima Mulungu ali kuwalamulira kusunga malamuloake. Kuchokera pansi pa mtima amasamala <strong>Yesu</strong> mau ake pa makhalidweawo. Pansi pa mtima mau a mbusa amadziwa chifukwa ali ndi Mzimuwa <strong>Yesu</strong> nkhosa imati! ndili kufuna <strong>Yesu</strong> nditsogolereni” Mbuzi zimatindisiyeni ndekha! Ndimachita zozizwa! Ndingapereke chuma changakwa aumphawi. Ndimadziwa zinthu. Ndiri wabwino koposa iwe ndiposindisamala pa zokamba zanu”.Kuwonera pa makhalidwe sinjira yabwino ku dziwa mtima ngati khalidwela munthu ndi loipa ndi chidziwitso choti pali bvuto. Koma ngatisimungalankhule kwa iwo chifukwa sakonda kuwala ndiye kuti mulindi bvuto lalikulu. Munthuyo ndi osapulumutsidwa ngati kumbali inamunthu ndi kutheka kuti ali choncho chifukwa choti ali khanda chabendipo khalidwe lokhalo ndi bvuto.Sakudziwa za izi bwino, koma amakonda kuunika ndipo ali kufunakuthandizidwa izi ndi zotheka kukoneka.Tisangoona pa bvuto la khalidwe lokha . anthu ambiri ali ndi mabvuto,chifukwa mwina makolo sanawalere bwino. Enanso mwina anali ndiabwenzi amene anali ndi magulu asanakhala otsatira A<strong>Yesu</strong>. Mwinaasanabwere kwa <strong>Yesu</strong> anali mu uchimo waukulu (mmene ndinali ndiinu nomwe) ndiye tinabwera mu ufumu ndi mukhalidwe ambiri oipa)ndibwelezenso, nkhani kodi timakonda kuunika.Mukumbukila chitsanzo cha malemba? Okhulupilira aku Akorinto analiakhristu oyamba kumene. Palibe amenen anali a khristu kwa zaka zoposazitatu kapena zinayi. Anali kukhala mu mzinda yoipitsitsa otchedwaAkorintho unali ndi zoipa, monga kugonana okha-okha amuna ndizinthu zina zambiri kulingana ndi kalata ya Paul okhupilira amenewa analiatachoka muzoipa zoipitsitsa komabe anali makandabe. Anali atapelekamiyoyo yawo kwa <strong>Yesu</strong>. Koma anali ndi zofooka ndi makhalidwe oipachoncho makhalkidwe awo sanali abwino koma mukudziwa zimene Pauloananena pamene anakomana ndi mabvuto amenewa? Anati, ndimadziwakuti mudzamvera.Mukalata ya chiwiri kwa Akorintho, mu mutu 7 Paulo anati, pamenemudalandira kalata yanga yoyamba munayankha ndi mphamvu ndi kulapakwakukulu. Munaopsedwe ndi uchimo umene unalipo mu miyoyo yawo.Munakhudzidwa ndi uchoyo ndipo mudakonzekera kuuchotsa Pauloanati ndinamuuza Taitasi kuti timadziwaKuti pamene mulandila kalata yanga kuti mudzalapa ndi zimene Akorinto2:7 amanena.Makhalidwe awo anali oipa mu mpingo wa Akorintho Paulo analembakalata yoyamba kwa iwo ndikuthandiza za uchimo wosiyanasiyana.Koma ndithu anali woomboledwa ndipo Paulo amadziwa kuti analiopulumutsidwa ndiye anali oyera choncho ndimadziwa kuti mudzalapandipo ndinamuuza Taitasi kuti walapa. Choncho tsopano Taitasiwabwera kwa ine ndi kundibweretsera uthenga wachikondi ndipochabweretsa chimwemwe mu mtima mwanga kuti mwalapa mongammene ndinamuuzira. Aliyense amene ali ndi mzimu woyera amalandirakalata yochokera kwa mbale yomuthandiza. Amamfuna kuthandizidwa.Uthenga wabwino ndi woti <strong>Yesu</strong> Khristu ndi oti tinatchulidwa ndimwazi ndi kuti machimo athu onse anakhululukidwa chifukwa tinaikachikhulupiliro chathu chonse mwa <strong>Yesu</strong> monga mpulumutsi. Chitsimikizochoti tachita zimenezi kuchokera mu mtima, ndipo omwe amasindikiza zacholowa zathu, ndikuti mzimu woyera waperekedwa kwa aliyense ameneali woona mtima ngati munthu ali ndi mzimu oyera adzakonda kuwalandi kukonda chowonadi…. Ndiye kenaka khalidwe lawo lidzasintha.Amalapa pa zimene alikuchitira ndi amuna awo kapena akazi awo ndikusintha. Amalapa mmene amakhalira ndi ogwira nawo ntchito, kapenaana awo kapenanso ozungulira nyumba zawo ndipo makhalidwenso oipandi kusintha ndi kukhala akulu msinkhu.Chikonzero cha Mulungu kuti ife tikule tsopanoMukuwona m’mene mpingo umakhudzidwira ndi nkhaniyi? Chikonzerondi chuma chobiisika pansi pa nthaka. Chikonzero cha Mulungu ndichoti unsembe ya okhulupilira. Pulani ya Mulungu ndi kwa anthu akendi kumangilirana wina ndi mzake tsiku ndi tsiku monga timakhaliramoona ndi tonse pamodzi choyamba chopindulitsa ndi chakuti onseamene ali ana a Mulungu amakula ndi makhalidwe abwino. Zabwinonsozimene zimakhala poyenda pamodzi ndi Mulungu ndi choti, ngati wina130 131


sakonda kuwala, amawonekera kuti ndi onama chabe. Ngati ndi wosafunakukonzeka, ngati sasamala pazimene <strong>Yesu</strong> ananena pa zinthu izi ngatiamakwiya ndi kupsya mtima pamemepo amaonetseredwa ngati a khristuonyenga. Zimawonekera kuti sanapeleke moyo wawo kwa <strong>Yesu</strong> chifukwaalibe choonadi ndiye satha sangakhale ndi Mzimu Woyera ndiye kukhalaosakonda kuwala (Yohane 3, 1 Yohane 1, 3).Choncho ngati mpingo ndi mpingo woona, ndiye ngati ansembe tonsetidzathandiza kuti tikhale ndimakhalidwe abwino. Tidzakhala tonsekuwala ndi moyo wina ndi mzake. Tidzathandizana wina ndi mzakekuwona zinthu zimene sitingathe kuona tokha. Ngati ndili wodzikonda,sindingathe kuona kudzikonda kwanga. Kudzikonda kwanga kulikuwawitsa <strong>Yesu</strong>. Kudzikonda kwanga kuli kuononga kuthekera kwangakukonda <strong>Yesu</strong>. Ngati ndili ndi kudzikonda zili kuwononga kudalitsikakwanga kwa Mulungu chifukwa Mulungu safuna kudalitsa kuzikondakwanga. Zimawononganso umboni wanga wa <strong>Yesu</strong> ngati ndiliwozikonda motero cholinga cha unsembe ndikuthandizana kudziwaMulungu bwino tsiku ndi tsiku. Mu msika, ku nyumba zathu pamaloathu mu mpingo. Ndingakule kuchoka mu mkanda la kuzikonda ndikukhala munthu wa Mulungu.Paulo anati, 1 Akorintho 3) kuti anthu ambiri amene anapulumukaamakhala atachoka mu lawi la moto. Anthu awa amapita kumwamba komaatadutsa mu Malawi a moto pofika kumeneko. Werengani 1 Akorintho3 nokha. Baibulo limati anthu ena anapulumutsidwa koma atadutsa mumalawi a moto koma ichi sicholinga cha Mulungu. Sizimene Mulunguamafuna kuti ife tikalowe kumwamba. Cholinga cha Mulungu ndikutiosati kuti tikhale makanda ndi uchimo kenaka ndi kupita kumwamba.Cholinga cha Mulungu ndikuti ndife mudzi oikidwa pa mwamba paphiri umene sungabisidwe cholinga cha Mulungu tikhale oikidwa mongamfumu pa mapiri. cholinga cha mulungu ndi choti kuti mkwatibwi amenewakonzekera kale. Cholinga cha Mulungu ndi choti ndife wowengeka,omanga banja ndi mkwatibwi omanga uchimo. Cholinga cha Mulungundikuti mpingo ukhale okonzeka mwana wa Mulungu pamene abweransokwa mkwatibwi.Aliyense ndi wololedwa kwa Mulungu kukhalamu mpingo amene akondakuwala. Ena aife tikhonza kukhala aang`ono. Ena a ife tingakhale ndikhalidwe loipa kwa nthawi zina koma ngati tili ndi mzimu wa Mulungungati tili ndi akhristu osati akhristu onyenga – ndiye kuti tili kukondakuwala. kukonda kuwala pamodzi ndi abale ndi alongo. Tidzakwanitsakuthandizana wina ndi mzake kukula. Ndiye kuti aliyense adzakulandi mphamvu ndi mphamvu ndi nzeru . Tingakhale okonda <strong>Yesu</strong> ndimphamvu zambiri ndi moyo wathu. Umboni wa <strong>Yesu</strong> ukhonza kukhalawa mphamvu koposa ndi kuononga mdaniwo sipazakhala ana okha okhandi makhalidwe oipa amene angaoneke osati ngati <strong>Yesu</strong>.Ana ambiri ang’ono ndi a makhalidwe oipa sizakondweletsa kwa makomoa ndende. Ana ambiri ang’ono ndi amakhalidwe oipa sizodzathandizaosakhulupilira kuti atsate <strong>Yesu</strong>.Ngati tili mpingo wa amuna ndi akazi a Mulungu amene ali okhwima ndikumaoneka ngati <strong>Yesu</strong> ndi moyo wathu ngati mpingo ndi wopambana,nzeru, mkwatibwi wopambana wa <strong>Yesu</strong> ndi mphamvu ya Mulungu ndikhalidwe la Mulungu mu moyo wathu ndiye anthu adzakhala okondwandi <strong>Yesu</strong> ndipo adzafuna kubwera kuti adziwe <strong>Yesu</strong>.Choncho lingalirani za Chikhristu chonyenga mpando wa chiwiri) ndikuti Mkhristu weniweni (mpando wachitatu, wachinayi ndi wachisanu)Lingalirani kuti khalidwe loipa sizoti kuti ndiye sanasambitsidwe ndi mwaziwa <strong>Yesu</strong>. Nkhani yeni yeni monga mu Yobu 3, Yohane 1, 2 Atesalonika 2ndi Petro 2 ndi yoti Mkhristu woona ali ndi Mzimu wa Mulungu. Indemakhalidwe ake angakhale oipa monga mwana pa makhalidwe akesakhala abwino koma ngati anabadwa kachiwiri ndi Mzimu ndipo mongamakanda adzakhala akumwa mkaka adzakula mu choonandi ndi kuunika.Cholinga cha mpingo ndi kuthandiza munthu ameneyo wa makhalidweoipa amene amakonda chowonadi kuti akhale ndi nzeru ndi kulimbikamtima poopa <strong>Yesu</strong> ndi kukula msinkhu.Choncho tiyenera kumasulira Mkhristu motere ndiponso tiyenera kukhalamonga mpingo uyenera kukhalira. Kuthandizana wina ndi mzake tsiku nditsiku kuti wina asaumitsidwe kapena kunamizidwa ndi uchimo. Tiyenerakukhala ngati ansembe. Ndipo ana ang’ono adzakula ndi mphamvu.<strong>Yesu</strong> adzakhala ndi umboni:- Mkwatibwi adzazidwa ndi Mzimu ndimawonekedwe ake. <strong>Yesu</strong> adzakhala ndi mpingo umene makomo andendesadzatha kugonjetsa. Motero kukongola kwa <strong>Yesu</strong> kudzakhala kwa Isilamu132 133


onse ndi kuchita uHindu kuti onse awona kuno konse. Tisakhale makandachabe amene amanena bwino zinthu. Koma osakhala monga <strong>Yesu</strong> ndipoMpingo sikupeza anthu onyengezera chabe amene amakhala bwinochabe koma alibe Mzimu wa <strong>Yesu</strong> okhala mwa iwo monga munthu. Komatikhonza kukhala opambana namwali wa <strong>Yesu</strong> uwu ndi uthenga wa bwinowa ufumu wa Mulungu.Mphamvu chosintha, mphamvu yowonetseraTsopano tibwererenso ku machitidwe a mipando isanu ija, Anthu ameneangakhale mu mipando wa chiwiri, wachitatu, wachinayi ndi wachisanuali opezeka ku Bapatisiti, Nazarene, Methodis ndi ma Pentekositi mumisonkhano awo. Chifukwa tamanga molakwika mpingo ndipo anthuonsewa ali pamodzi. Mipando isanu yafanizira ija. Kuphatikizira ndimpando wa chiwiri umene suloledwa mu mpingo ngati mamembalakoma posowa chilungamo, chiyanjano mu tsiku ndi tsiku mu unsembe(monga Mulungu amafanizira ndi kulamulira) wa pa mpando wachiwiriamaloledwa (mukusamvera kwa Ambuye) 1 Akorinto 5). Monga alioipa ndipo wa mu mpando wachitatu nthawi zone amakandira kapenaosafunidwa, zoona zake ndi zoti 85% ambiri amene amaloledwa mumpingo kuli konse ndi mpando wachiwiri kapena wachitatu. Uku ndizomvetsa chisoni ndi zosafunikanso ngati tili kumanga mu njira ya<strong>Yesu</strong>. Posakhalitsa tidzakhala ndi Chisilamu kapena mu Hindu amenetidziganiza kuti ali chiwalo cha mpingo.Koma chimbedzo kungokhala mwa mpingo wa chipembedzo (siumenempingo umene mulungu amafuna kuthandinzira) umene uli ndi onseinali ya anthu pamodzi. Mukuvetsa zimenezi?Ngati tikhala mnjira imene <strong>Yesu</strong> ananena ndi kuyamba kumanganjira imene mpingo uyenera kumangidwira, ndiye tikhonza kudziwaamene ali ongonama chabe kapena amene ali opanda mphamvu ndipotingawathandize. Ngati mpingo ungamangidwe pozungulira mumgwirizano mmalo mwa msonkhano wa lamulungu ndiye onse anthuamitundu inayi idzakhala ndi kulumikizidwa tsiku ndi tsiku. Onamandi ana enieni. Atate ndi anyamata adzakhala mu mgwirizano ndi winandi mzake Kukonda wina, kuthandizana ndi wina zobvuta kukwaniritsalamulo la khristu. Ngati mmenemu ndi mmene mpingo ungaonekere,ndiye muli ndi mphamvu zosintha zinthu ndi kuzionetsa poyera.Mukukumbukira mu Machitidwe 2:42-47 kuchokera tsiku loyambachikhristu onse ali pamodzi okhulupira ndipo anali ndi zofanana? Izisizinali chifukwa cha “chikhalidwe” kapena zochita – zidali anthu okhalamu moyo ndi chipulumutso cha <strong>Yesu</strong>. Anthu lero amakhala kumbuyo kwazokangana za chikhalidwe kuonetsera kuti amakonda dziko ndi zinthu zamziko ndi kufuna mulungu wa la mulungu mmawa ndi lachitatu usiku ndimagulu okumana lachisanu. Koma anthu a mulungu obadwa kuchokeraku mwamba ndi <strong>Yesu</strong>, poyamba ndi zofunika tsiku ndi tsiku ndikukhalaonse pamodzi nyumba ndi nyumba. Anali onse tsiku ndi tsiku kukhalamu chiphunzitso cha Atumwi, kukhala mu chiyanjano kunyema mkate,kupemphera. Sanali ongofanana mu zinthu zina Mach 5.4.5 koma moyowatsopano kuchokera mwa iwo monga <strong>Yesu</strong> analamulira kuti zinthu zonsesizinali zawo zawo. Baibulo limati anali anthu alukana pamodzi mongamithempha ukhalira. Uwu ndiwo mpingo wa chipangano chatsopano-Tsiku lililonse. Mgwirizano wawo, aliyense wa iwo anali ndi amayi ambiri,abale, ndi alongo ngati ndi m’mene tingamangire pali mphamvu yamulungu wosintha mphamvu yoonetsedwa ndi kuchotsa malinga a satanamu moyo wathu.Tiyenera kumanga mu njira ya mulunguNgati tikumanga mu njira imene anthu anamangira ndi miyambo ya anthupokhala ndi mmawa wa la Mulungu ndi ulaliki ndiye anthu awa amene alimu mpando wa chiwiri umene amangosoneyeza anthu odzangowonererachabe tsopano 1 Akorinto 5 limanena kuchotsa chotuopitsa. Baibololimanena kuti ngati pali ojedana pakati panu, achiwerewere, odzikonda,opembedza mafano kapena anthu amene amakonda dziko lapansi tiyenerakuwachotsa mu msonkhano. Mau a Mulungu amati ngakhale osadya nawopamodzi amene amati ndi .okhulupilira koma osakhala nawo mu njiraya Mulungu. Tisakhale nawo pamodzi kapenanso kukhala abwenzi athu.<strong>Yesu</strong> anati tiyenera kuwathamangitsa. Baibolo limati aliyense amane amatindi mbale koma amakhala mu uchimo ayenera kuchotsedwa pakati pamsonkhano. Tsopano, mungachite bwanji zimenezi ngati ndi lamulungummawa. Kapena ndi moyo wokha womwe ndi wowonekera mmawa okha.134 135


Amayankha, “Ai sichoncho. Sizikukukhudzani ai. Ndipo mukatichabwino chifukwa chiyani mukutero? Ndingadziwe chifukwa chache.Sizikukukhudzani ai. Chotsani chisoso chanu mmaso anu. Bwanjimuli oweluza ine motero ndimalamulo. Chabwino, ndamva kumenemukuchokera ndipo ndikukupemphani kuti mufewetse mitima! Mwinadipalibe chobvuta koma timangofuna kufunsa, chifukwa ndikukhuzidwandi mtima wanga koma simungalire kuti tilankhulanabe kuti ndidziwe?Ai samalani zanu.Chabwino choncho ndiyenera kuchita zimene <strong>Yesu</strong> ananena kutitizichita mu zinthu ngati izi ndipo tiganize kuyitana abale ena kutitipitilize kulankhulana pa nkhani imeneyi aliyense amene mungaganizaamene tonse tinagulitsidwa kwa <strong>Yesu</strong> ndipo ndiwozindikira zinthu? <strong>Yesu</strong>anandilamula ine kutenga enga awiri kapena atatu ena kuti tilankhule zazinthu izi chifukwa choti ndiotsatira ake a <strong>Yesu</strong> muyenera ,kumvera <strong>Yesu</strong>pobweretsa ena awiri kapena atatu ndipo tikhale pansi ndikulankhulana zaizi, akanena kuti sindifuna kuti ndilankhulane ndi ena abale awiri kapenaatatu ndikuti musamale zanu osati za ineNdiye mumadziwa kuti ooh tili ndi mavuto akulu pano ngati sizisintha,ndiye kuti safuna kukonda kuwala kapena kukonda chowonadi,ndichitsimikizo choti ndichotupitsa chimene ndichofunika kuchoka pampingo ngati palibe kulapa.Tsopano tingadziwe bwanji kuti tili ndi zobvuta m’banja? Munthu uyuanali wa mphamvu pa la mulungu mmawa ndingadziwe bwanji za munthuonyenga amene ali ndi miyoyo yiwiri? Tikadziwe ngati tingapite kwawola chinayi madzulo. Pomaliza, timadziwa kuti mbale uyu sanali kukondakuwala chifukwa sanali kukonda kuwala ndi mboni yoti analibe mzimuwa <strong>Yesu</strong>. Safuna kusintha, sasamalira pamaganizo athu. 1 Akorinto 5limati ngati wina azitcha yekha mbale koma kukhala mu uchimo osadyanaye, osakhala naye pamodzi ngati bwenzi ndipo achotsedwe pakati paabale. Ngati tingamange mmene anthu amangira ndipo sitidzadziwakuti pali vuto ndi munthu mumoyo wake ndiye chikumbumtima chakendichoumitsidwa. Koma ngati tingamange mnjira imene <strong>Yesu</strong> ananenakuti timange potengerana zothobwitsa, wina ndi mzake tsiku ndi tsikumwina munthu uyu adzakhala munthu wodalilika.Wonani abale kuti kapena ukhale mwa wina wa inu mtima wiopaosakhulupilira, wakulekana ndi Mulungu wa moyo komatu dandaulirananinokha tsiku ndi tsiku pamene pachedwa lero kuti angaumitsidwe wina wainu ndi chenjero la uchimo. Pakuti takhala wolandirana ndi khristu ngatitutigwiritsa chiyambi chakutama kwathu kuchigwira kufikira chitsiriziro.(Aheberi 3:12-14).Ngati tingamange mu miambo ya anthu ndi kulalikira kwa lamulungundingaganize kuti munthu uyu ndi mkhristu koma Mulungu akuti“Sindimudziwa iye” Tingamuthandize bwanji ku uchimo ndi kuwukirakapenanso kukonda dziko ngati sanawonekere?Nthawi zina kulalikira kumachitika pakati pa miambo ya anthu kwa anthuamene amaganiza kuti ndi akhristu?Ngati mungamange mnjira yabwino tsiku nkdi tsiku kuchokera muzinyumba ndi zinyumba ndiye kuti uchimo udzawonekera ndipo tidzawonangati ena li kukonda kuwunika ngati sakonda kuwunika ndiye timawayikakumene ayenera kukhala monga mmene Mulungu amanenera, “Achotsenipakati pa abale ndipo munthu uyu sakhalanso otchukanso ayi adzayambakuganiza za moyo wake chifukwa sakhalanso monga mmene analiri kaleai mwaina tsopano ndi mmene angakhale mkhristu weni-weni.Kapenanso mukumanga munjira ya Mulungu tinapeza chumachimene siitinachidziwe ngati tili monga mmene Mulungu analamulirakukhudzidwa ndi miyoyo ya mabanja ndi zodabwitsa zizawoneka zimenesiziwoneka ku magule ena kapena lamulungu mmawa. Ngati tidzakhalamonga Mulungu afunira wokhala tonse ndi chikhulupiliro chimodzitonse ngati munthu mmodzi ndipo wokhlupilira onse anali pamodzindipo zodabwitsa zidzakhalanso. Koma kufuna ufumu osati kukhalawodzidalira tokha kuchotsa miyolyo yathu kuchokera muthupi ndi mwazikoma mukubadwando mu mzimu.Mbiri ya dziko yasonyeza kuti anthu amene mu mpando wa chiwirindamene ali atsogoleri koma ndiosapulumutsidwa! Kodi munamvaza munthu wotchedwa Charles Finney? Monga munthu wa mkuluanali mtgsogoleri wa woyimba koma adazindikira kuti sadali mkhristundipo anabadwanso ndikukhala munthu wa Mulungu. Charles Finneyanabweretsa anthu 500 000 kwa <strong>Yesu</strong> mu nthawi ya moyo wake mukudziwa138 139


kuti iye anali wodzikpereka ndi wachipembedzo mukukula kwake komaanadziwa kuti sanali mkhristu ai ndipo anasinthika mu mtima ndikukhalamunthu wa Mulungu ndingatchule ambiri ena amene timawadziwa kutindi anthu amphamvu a Mulungu kuchokera mu mbiri anali atsogoleri muchikhristu koma anazindikira kuti sanali akhristu ai.Mbiri ya dziko yasonyeza kuti anthu amene mu mpando wa chiwirindamene ali atsogoleri koma ndiosapulumutsidwa! Kodi munamvaza munthu wotchedwa Charles Finney? Monga munthu wa mkuluanali mtgsogoleri wa woyimba koma adazindikira kuti sadali mkhristundipo anabadwanso ndikukhala munthu wa Mulungu. Charles Finneyanabweretsa anthu 500 000 kwa <strong>Yesu</strong> mu nthawi ya moyo wake mukudziwakuti iye anali wodzikpereka ndi wachipembedzo mukukula kwake komaanadziwa kuti sanali mkhristu ai ndipo anasinthika mu mtima ndikukhalamunthu wa Mulungu ndingatchule ambiri ena amene timawadziwa kutindi anthu amphamvu a Mulungu kuchokera mu mbiri anali atsogoleri muchikhristu koma anazindikira kuti sanali akhristu ai.Choncho chinthu chabwino chimene tingachite ndi munthu amenesakonda kuwala ndi kumvera zimene <strong>Yesu</strong> ananena ndi zimenePaulo ananena “pitani kwa iwo okha” ndikuyesa kuwapindulangati apitilira mu uchimo ndipo safuna kumva ndiye tengani awirikapena atatu ena ngati sakonda kuwunika ndi kusasamala ndiyetiyenera kumvera Mulungu ndikuwachotsa iwo mu mpingo mwinamoyo wawo wungapulumutsidwe chifukwa tagwiritsa chidachimene Mulungu anatipatsa ife kuti achenjezedwe. Sitichita izi mumkwiyo ,kapena mu kuziyenereza tokha oyera. TimachitaIzi mukumvera Mulungu .Timakonda iwo. Timafuna kuti asinthike mtima moona ndithu Osatikunyengedwa chabe kwa mtima. Ichi ndi chida chimene mulungu waperekakwa ife potandiza anthu kuti azindikire amene ali mu chipembezo komaonamizidwa.Mpaka titathandizana wina ndi mzake tsiku lililonse ndi kukhalandi mgwirizano weni weni tsiku ndi tsiku munthu mu zochita zakezenizeni sizingatheke kudziwika baibulo limati chotupitsa pang’onochimatupitsa mtanda wonse, choncho ngati munthu ali ndi chinsinsi chauchimo mu umoyo wake ndipo sanathane nazo ndiye kuti anthu onsea mulungu amapwetekeka chifukwa cha chimenechi. Anthu a mulunguanagonjetsedwa Kwambriri Ai chifukwa mmodzi wa iwo (Akani)anakwirira choipa mu nyumba yake. Mulungu anachita ndi anthu akepankhani monga mudziwira. Tiyenera kumanga mpingo mu njiraimene iyenera kumangidwira kuti tisakhale ndi nyumba yoonengedwa.Pamenepo pokha pamene anthu angochokere mu mpando wachiri kufikadu mpando wachisanu.Tithandizane ena kuti akuleTsopano palinso fundo ina imene tiyenera kuti timango bwino. Izizimakhuzana ndi (wampondo wachitatu) munthu wofooka, amenemakhalidwe ake Sali abwino koma anapulumutsidwa. Ngati tingamangemmene anthu anamangira miyambo ya anthu ndiye tingampaste uthengakwa munthuyu. Tikuyetsesa kuti akhale mu zochita zathu. Komangati timange mmene anthu a dziko ndiye kuti zochita za munthuyosizingadziwike ayi mwina ali kulira ndi chimo pamene agona usikuchifukwa mbusa amamva kulira kwa nkhosa ndipo ndi mkhristu woonaokhala ndi mtima woona ndi mtima wofewa munthuyo safuna kukhalawogonjetsedwa. Ali kulankhulana ndi ndi <strong>Yesu</strong> za uchimowu, komamu miambo ya anthu sathandizidwa ai amangomva uthenga ndipoamangoyetsa kwambiri koma nthawi zonse, uchimo umapititita kwa zakampaka amangosiya.Pa dzanja lina, ngati tingamanga mnjira ya mulungu yimene iye anatiuzapali ndithu chiyembekezo. Mu nyumba ya mulunga munthu yemweyupa nthawi yockepa pa sabata imodzi mwa mkhristu adzakhala ndi abableanayi kapena asanu amene ali kumuthandiza mu kufooka kwake. Alikupemphera limodzi, ali kulankhula limodzi, ali kulankhula pamodzimawu a <strong>Yesu</strong>. Ali kuulura machimo ake kwa anzake. Okhulupirira awa alikuchengetana wina ndi mzake tsiku ndi tsiku ndi kubweretsa mphatsomu umoyo wa munthuyo. Choncho mmalo mwa kumva zowawa yekha,munthu wan’gono ameneyo ali ndi anthu amene ali okhudzidwa ndimoyo wake tsiku ndi tsiku kumuthandiza kusintha Palibe ali ndi chinsinsimu umoyo wake kapena kutsiyanitsa moyo usadziwike ndi iwo ameneamudziwa <strong>Yesu</strong> ndi kulumikizidwa kwa iye “kubatizidwa ndi mzimu140 141


umodzi, mu thupi limodzi” Timathandizana mu zofooka sathu (monga ifetili nazo) palibe otchuka. Tikuthandizana wina ndi mzake monga mbalepakati pa abale.Choncho tiyeni tinene za munthu amene ali mkhristu kwa sabataimodzi. Ali ndi chikhulupiriro mwa <strong>Yesu</strong> monga Messiah Baibulo limatimachimo ake anasambitsidwa. Baibulo limati machimo ake awululikakwa iye mulungu ndi wokhulupirika ndi olungama ndi mwazi umapitirirakutitsuka. Chingachitike ndi chiyani ngati munthuyo atafa asanagonjetseuchimo mu moyo wake? Munthu uyu ndi opulumutsidwa ndi <strong>Yesu</strong> mongaPaul wa Taitus ndi mwazi wa <strong>Yesu</strong> khristu munthu ndi wonulumutsidwamonga unatipulumutsa ife ku uchimo! Okhulupirira amakonda choonadiamafuna kusintha ndiye ndi opulumutsidwa, osati kungonamizira chabe.Ichi ndi chipulumutso chimene tili nacho abalendi alongo.Uthenga wa bwino wa ufumuTikupatseni malembo amodzi amene amabweretsa zinthu zonsezipamodzi mu buku la Ahebre Baibulo limati timakonzedwanso ndikukhalawoyera. Ndinakonzedwanso-zinachitika pamene tinapeleka moyowathu kwa <strong>Yesu</strong>. Kukonzedwa ndi kukhala woyera mawu oti “woyera”amatanthauza mbee ndikukhala wofunika kwa mulungu. Atate akondamwana ndi onse amapeleka moyo kwa <strong>Yesu</strong> kuchokera mu mtima aikakhristu ndi kubvala chikhristu .Mwachocho mwana watsopano ndi mkhristu wakale onse ndiopulumutsidwa chimodzimodzi chifukwa atate anaombola mwana, <strong>Yesu</strong>ndiye pamene atate ayang’ana pansi ndi kuona anthu amene asambitsidwandi mwazi wa nkhosa. Angelo a imfa amapitirira ndipo sawakhudza aimwazi wa <strong>Yesu</strong> wakhala wa thunthu kwa iye mu chionetsero cha mipandoisanu amene anali mpando wachitatu, wachinayi ndi wachisanu. (Ana,atate ndi anyamata) onse ndi opulumutsidwa kwatunthu.Ndi <strong>Yesu</strong> yekha amene ali wangwiro, mwamva? Ndiye pamene tabvala<strong>Yesu</strong> timakhala wangwiro ngati iye ali popitirira ndi chipulumutso chathutimakhala a ngwiro monga <strong>Yesu</strong> ali. Takhala a ngwiro ndi woyera ndi mmenemalembo amatiphunzitsira. Ngati muli ndi mzimu mkati mwanu pamenemuli opulumutsidwa kwenikweni ndiye mwakonzedwa mu ungwiro monga<strong>Yesu</strong> ali.Ndipo machimo anu akhululukidwa ndipo dipo laperekedwa pamachimo anu onse ndipo ndinu okonzedwa mu mzimu wa <strong>Yesu</strong>.Tsopano nkhani imene tikulankhula kulumukiza ndi mpingo mumaonekedwe osati kukhala wangwiro kokha komanso kukhala woyerachidachothandiza mu nyumba ya mulungu ngati mpingo umangidwamu njira ya mulungu monga ngati uyenera kumangidwira ndipo ndifeokhunzidwa ndi ubale wa wina ndi mzake akhale wa ngwiro monga pakutiali kale a ngwiro pa mwazi wa <strong>Yesu</strong> koma tidzawathandiza kuti akhalechida potumikira mulungu. Tidzawapanga a mphamvu mwa khristu.Tidzawapanga kuti akhale pa ubwenzi ndi <strong>Yesu</strong> ndipo ife sitidzapedzachipulumutso chokha kwa <strong>Yesu</strong> koma <strong>Yesu</strong> adzapenzanso kanthu kwa ife!Ana ang’ono kupedza kanthu kuchokera kwa <strong>Yesu</strong> Abambo ndi anyamataadzapereka kanthu kwa <strong>Yesu</strong>! Mwana wa nkhosa wa mulungu adzapedzaphindu mzowawa zake.Mpingo omwe <strong>Yesu</strong> akumanga ndi njira ya onse amene ali wokula msinkhu.Ngati timanga ndi miambo ya anthu, anthu ambiri amakhala makanda kwanthawi yayitali. Izi ndi zokhumudwitsa <strong>Yesu</strong> mmalo mwa chisangalalo.Tikamanga monga mwa pulani ya mulungu ndi maonekedwe ake ndipomakandawo adzasanduka Asitifano, Paulo ndi a Yohane ndipo kuyambirawang’ono mpaka wamkulu adzakahala monga <strong>Yesu</strong> pamodzi ndipompingo udzakhala monga mzinda oikidwa pa mwamba pa phiri umenesungabisike. Pamodzi tonse monga mwa Paulo tidzakhala malo okhalamomulungu mwa mzimu osati kungopedza mphoto ya chipulumutso chokha,koma tsopano pomalizira<strong>Yesu</strong> adzapedza phindu la mpingo woona! Uwu ndiwo uthenga wabwinowa ufumu. Kukonzedwa ungwiro ndi kukhala woyera.“Mulungu ndiye kuunika ndipo mwa iye monse mulibe mdima. Tikati tiyanjanendi iye ndipo tiyenda mumdima, tinama, ndipo sitichita choonadi koma ngatitiyenda mkuunika monga iye ali, tiyanjana wina ndi mzake ndipo mwazi wa<strong>Yesu</strong> mwana wake utitsambitsa kutichotsa uchimo wonse”.“Tikati kuti tilibe uchimo tizinyenga tokha ndipo mwa ife mulibe choonadi.Ngati tibvomereza machimo athu ali wokhulupirika ndi wolungama iye kutiatikhululukire machimo athu ndi kutisambitsa kutichotsa chosalungama chirichonse.” (1 Yohane1:5-9)142 143


Alipo munthu amene akonda kuunika, ndipo wina amene amati alibeuchimo, koma akonda mdima kuchokera pa tsamba ili kuti mulunguamaona mosiyana.“Ndikulemberani tiana popeza machismo akhululukidwa kwa inu mwa dzinalache. Ndikulemberani Atate, popeza mwamuzindikira amene ali kuyambirapachiyambi. Ndikulemberani anyamata popeza mwamulaka oyipayondikulemberani, ana, popeza mwazindikira Atate.” (1 Yohane 2:12-13)Ngati timanga mu njira ya mulungu idzakhala yobveka bwino kwa iwookonda kuunika adzachoka ku mwana kukhala atate ndi ku anyamata.Uwu ndi uthenga wodabwitsa!!Kudzadzidwa Ndi MzimuWoyera Pamodzi!!!Lachiwiri la m’mawa a pa 5th October,1999Panthawi yokhala pamodzi mu Africa, kuthandizira m’chichewa, kutsiyanakwa malingaliro ndi zakumitima kwa abale.Panopa, mbale amakamba za kukhonza kumva mau a <strong>Yesu</strong> abwinowokhala ndi <strong>Yesu</strong> kuti tikakhale akumva mau ake. Izi zili ndi zambirizochita ndi ife pokhala kachisi wa Mulungu, pa idzi makhomo aku gehenasangatsekuke.Baibulo likutiuza zakudzazidwa ndi mzimu woyela. Mzimu wa Yehovakukhala mwa ife ndi kutidzadza mpaka pa mathero. Ili ndi lamulo laMulungu. Izi zithandauza kuti titha kumvera lamulo kapena ayi kutitidzazidwe ndi mzimu. Tikudziwa pokhala mkhristu, tayenera kukhalamwa Khristu, ndi kuti Khristu akhale mw aife. Amen? Chonchonkotheka kukhala mwa khristu, koma otsazazidwa ndi Khristu. Chonchonkotheka kutsamulingalira <strong>Yesu</strong> kapena kumumvela momwe tayenerakuchitira. Mwatsoka, ili ndi vuto la a Kristu ambiri lero. Koma palivumbulutso lochokera kwa Mulungu za momwe izi zingatsithire. Njirayake ndi yokhuzana ndi kumanga mpingo bwino, “makomo a ku gehenatsangatsekuke,” tayenera kumanga miyoyo yathu kuti anthu a Mulungu,kuyamba kuchiyambi mpaka kumathero, kudzazika ndi Mzimu – osatitsogoleri awiri kapena m’modzi, koma anthu onse a Mulungu adzazidwendi Mzimu.KuzamilatuNdingokuyambirani chinthuzi cha mfundo imeneyi. Tiyerekeze mulindi ndowa ya madzi. Tinene kuti pokhala ndi ndowa ya madzi kapu yamadzi ili ndi chivindikiro pamwamba pake. Kapu ili ngati munthu yemweali ndi <strong>Yesu</strong> mkati mwake. Kwa munthu ameneyu kukhala mukhristu,wayenera kukhala mwa <strong>Yesu</strong>. Ndiye kapu yozaza ikhale mu ndowa. Ngatimunthu ali wozazidwa ndi Mzimu, adzakhaliratu mwa Khristu, ngati144 145


muli mphyeya mu kapu, idzakhala pa mwamba. Ngati sitili odzazidwandi Mzimu Woyera, ngati munthu, tayenera kukhala mwa Khristu ndikupulumutsidwa, koma sitingaze mene mwa <strong>Yesu</strong>. Paulo alemberaku mpingo wa ku Agalatiya (Ch4), “Ndili mukuwawa wa kuberekamwana, pamene ndili pafupi kukhala ndi mwana. Ndikumva kuwawakwa kubereka <strong>Yesu</strong> apangidwa.” Amalembera kwa anthu amu mpingowaku Galatiya amene adali wopulumutsidwa kale (zikunena za izi muchapter 3:. Mudali kufooka kwakukulu mu mpingomu, choncho. Tsadalikhristu wokhazikika mwa iwo. Adali ndi mphyeya mwa iwo, pweya wadziko, koma osati khristu. Sono adayanjana pamwamba. Iwo tsadazamemu mzimu wa Khristu. Chifukwa tsadali pawokha, wozazika ndi Khristu,tsadamire mwa Khristu.Aroma 12:1-2 akutsindika kuti mwa kudziwa zabwino, chifuniro chabwinondi changwiro cha Mulungu kuti timumve Mulungu ngati munthu,tidzazidwe “Pantchito za dziko.” Titsakonde zomwe dziko limakonda.Titsakhale ndi malingaliro a dziko kapena kukhula monga momwearankhulira. Tisinthe manja athu mosiyana ndi a dziko. Timwaze ndalamamosiyana ndi momwe a dziko amamwazila nthawi yawo ndi ndalama.Mulungu anati kupembedza kwithu kwa uzimu kutsakhale ngati kwadziko mu zovuta zilizonse. Mulungu adati kuti tikhale akusandulika, ngatikuchokera ku caterpillar kupita ku butterfly, mwa mau a Mulungu. Ndiyetikhoza kumva Mulungu “Ndiye tikhoza kudziwa zabwino chifunirochabwino ndi changwiro cha Mulungu.” Ngati tili ndi zina zamudzikomwa ife, m’malo mwa kusandulika kwa mau a Mulungu, tidzayanjanapamwamba. Ngakhale tingakhale mwa Kristu ndi ku pulumutsidwa, sitiliozama mu cholinga cha Mulungu.Tikufuna M’modzi ndi NzakeCholinga cha mpingo ndi chothandiza aliyense kudzazidwa ndi MzimuWoyera, sono tikhoza kuthandizana kuchotsa dza mudziko mu miyoyoyathu. Ku Hebrews 3 akuti, “Tayenera kuuzana ndi kuthandiza ndikuchenjezana wina ndi mzache tsiku lililonse kuti patsakhale modzimwa ife amene adzachite manyazi ndi kukanidwa. Baibulo likuti tiyenerakuthandizana tsiku ndi tsiku. Tichoke mumanyumba mwathu ndikulowa mumiyoyo ya ena, mu malo ogwilila ntchito ndi mu ma nyumbamwa azizathu. Tayenera kuthandizana kuti tisakhale adzichito chito zadziko. Anthu ena mati, “ndili ndi ubale wawo ndi Mulungu wawo.” Izisizomwe Baibulo likunena. Baibulo likuti “langidzanani wina ndi zachekuti pasadzakhale okanidwa ndi wotsalandilidwa.” Baibulo likuti ndife ansembe awokhulupirira ndipo tayenera kuthandizana wina ndi nzake kutitikazazidwe ndi Mzimu Woyera. Timagwiritsa ntchito mphatso zomwe zilimkati mwa ife kuthandiza ena kuti adzaze ndi Mzimu Woyera. Membalawina aliyense wa mpingo athandize membala nzake kumpingo.Izi ndi zinthu zosiyana momwe Anthu ambiri pa dziko lapansi amangairapamodzi cikhristu. M’mayiko ambiri, anthu amabwwera pamodzi patsiku la sabata ndi pa misonkhano. Momo amakhala ndi “Mumpingoyambiri padziko la pansi kulibe kuti dziko liti, Anthu amabwera pamodzipa sabata ndikukhala mumizele. Ndiye akulu .--- akulu (anthu oyera)amabwera kumbuyo kwa anthu ndi kuyambitsa mapologalamu. Koma izizisimomwe Baibulo limanenera ayi kuti cikhristu cimakhalira choncho. Tilinayo, mmayiko yosiyana siyana, momwe tamangira mpingo molakwikamudzankha zoposa tusauzande (2000) mdzaka zapitazo.Chifukwa chiyani tamanga molakwika mpingo chonchi? Chifukwamamangidwe ache amangidwa ngati a chipangano cha kale, momwe akulua sembe ali momo ndipo anthu ambiri ali momo kuwonerera. A Levi(wasembe) amapeleka sembe za anthu onse. Iyeyo amakhala mu nyumbaya Mulungu wa padera dera amene amawathandiza anthu kuti amudziweMulungu. Ichi ndi chabwino ngati inuyo munakhalapo zaka thusauzande(2000) kumbuyoku ngati ife tifuna kukhala a Kristu osati Ayuda, ndiyetimange ngati Akhristu AMEN? Tamanga molakwika chikristu mumayikowosiyanasiyana koma, Mulungu alikubwezeretsa tsopano mpangano latsopano Mchikristu mudziko lonse la pansi.Ufumu wa AnsembeMpangano la tsopano anthu onse a Mulungu aynera kukhala a sembekwa wina ndi mzake. Chikumbu kumbu cha Mulungu si cha kuti munthuozozedwa modzi azilamulira mapologalamu ayi. Mawu a Mulungu akunenakuti <strong>Yesu</strong> anakwera kumwamba mwamba ndipo anapeleka zipatso pa anthuake, anapanga ufumu wa ansembe. Iye anayika gawo limodzi la iyi mwinipa anthu ake kuti iwo ndi woona osandulika ang’ono ndi akulu.146 147


Ndi chifukwa chake amafuna mphatso ya wina ndi mzake. Timafunamphatso zonse <strong>Yesu</strong>. Pali mphatso zambiri – mbiri chifukwa zonse <strong>Yesu</strong>anadzithira pa banja lake (mpingo). Ichi ndi chifukwa chake <strong>Yesu</strong> anati,tonse tili a mbale wina ndi mzake sitifuna ife, mtundu modzi kapenamphatso yimodzi yizimilira patsogolo pathu nthawi zonse. Izizi sitizalorakuchitika pakati pathu. Onse amene osindidwa oona ake ndipo okhalamkati amakhala a kulimbika mmoyo wawo nthawi zonse kwa wina ndimzake ndipo kuwonesetsa (Aheb 3:12-14) kuti onse ndi a sembe.Mtima wa Mulungu, mpatso yanu yikale yanga komanso mpatso yangayikhale yanu. <strong>Yesu</strong> amatero, “Musamuche wina mw ainu wamkulu,Revelande, Mbusa, kapena wasembe” ngakhale kwa ophunzira ake ajaasanu ndi awiri, iye anati “inu nonse muli a mbale,” ngati chiri choonakwa Petulo ndi Yohani nditi ndi choonadi kwa ife tonse Ameni. Mphatsozimene zili mkati mwa ambale ndidzo gawo la <strong>Yesu</strong>. Ngakhale ana alinadzo mphatso zimeneso ndi gawo la <strong>Yesu</strong>. Mphatso zonse zimafunika pamoyo wathu. Ife tonse ndife ambale. Izi ndi zomwe Baibulo limanena.“Inde lero a mbale, ngati mumbwera pamodzi, pali wina ali mawuachiziwiso, yimbo, kapena vumbulutso,” izizi ndi zomwe kawiri kawirimawu a Mulungu amanena ku 1 Akorinto 14, “Ngati mumbwerapamodzi, ambale, aliyense ali ndi mawu a chiziwitso, yimbo, vumbulutsokapena uneneri.”Ngati timakhala choncho, ngakhale osakhulupirira amagwera pamasopake ndi kulira, nanena, “Mulungu ali pakati panu.” “Ngati vumbulutsolavumbuluka kwa munthu wa chiwiri ndiye WOYAMBA ASIYE NDIKUKHALA PANSI!” Ichi chi ndi chimene chimathandauza ku 1 Akorinto14. izi zisimaoneka kawiri kawiri ndi amanena “amakonda kukhalaoyamba, amakonda kukhala olamulira komanso kuonesetsa ngati “iwondi auzimu eni eni. Ndi kutenga ndalama za oyera mtima.Ife tiyenera kukhala ufumu wa a sembe. Ife tiyenera kumangilidwawina ndi mzake tsiku liri lonse. Ngati sitimangirilana, Baibulolikuti tizaumitsidwa ndi kunamidzidwa. Chikumbu kumbu chathuchizamangiriridwa. Ife tidzazakhala kuyerekedza! Kutengeka ndizinthu zonse zimene zimaoneka zochimwa kumoyo wanthu. Ngatisindingapeze anthu ambiri ozipeleka otsatira a <strong>Yesu</strong> kukhudziwa ndimoyo wanga tsiku ndi tsiku ndi ena Sali okhudzidwa ndi moyo wangandiye kuti tidzakhala ounotsidwa mitima ndipo sitidzadzidwa choonadi.Izi ndi zimene Baibulo limanena nthawi zonse. Tiyenera kukhala mumoyo pamodzi kuthandizana tsiku ndi tsiku. Ngati mukufuna kutsutsabaibulo ndi kunena kuti siloona, ndiye kuti mudzayamba chipembedzochanu. Anthu ambiri ali mu chipembedzo chotero. Koma nonse a inumwasonyeza pa kuzipeleka kuti muchita chilichonse cha <strong>Yesu</strong>. Chonchotiyeni tipite kukwera pamodzi ndi iye tsopano!Tsiku Lililonse<strong>Yesu</strong> akumanga mpingo wake umene makomo a ndende sadzaulaka. <strong>Yesu</strong>akubweletsa mphatso kuchokera kwa anthu ake ndikulora iwo kuti akhaleansembe tsopano – osati msonkhano, koma tsiku ndi tsiku. Baibulolimati ululani machimo kwa wina ndi mzake ndi kupemphererana winandi mzake kuti muchilitsidwe. Tadikilani kodi anthu onse a Mulunguamachita zimenezi? Ndi liti lomaliza kuwulura machimo anu kwambale kapena mulongo. Kodi mukufuna kuchilitsidwa? Kodi mukufunamphamvu ya Mulungu mu moyo wanu? Baibulo limati lapani machimoanu kwa wina ndi mzake. Chifukwa chiani sitipanga? Sitipanga izi kwanthawi zonse chifukwa timaopa. Sitipanga chifukwa cha miyambo yaanthu imene yatimeza ife. Taleka kukhala woyenerera chifukwa chakuzikonda. Mulungu akuti kwa inu ndi ine. Titsegule mitima yathu kukhalaozichepetsa ndi wofewa. Kuwulura machimo kwa wina ndi mzake tsikundi tsiku ndi kupemphereeana kuti tichiritsidwe.Iyi ndi imodzi imene timathandizira wina ndi mzake kudzazidwa ndiMzimu Woyera. Timatsegula mitima yathu kuchengetana wina ndimzake tsiku lililonse. Tsiku ndi tsiku kuti pasaoneke wowumitsa mitimakapena kunyengedwa. Atero Ambuye, Mulungu wanena kuti tiyenerakutsegula moyo wathu kwa wina tsiku ndi tsiku, tsiku lililonse ngatitizamanga munjira yotere yokumanirana pa Mulungu ndiye kenakatipita ku nyumba zathu ndi kukhala mosiyana ndi mabanja. Tidzakhalaosamvera Mulungu.Mulungu walankhura momveka bwino pamene tingayendere pamodzi ndikuthandiza wina ndi mzake kudzozedwa ndi Mzimu Woyera. Mulungu148 149


anati, “thandizanani wina ndi mzake tsiku ndi tsiku.” Mulungu anati,“Tikuika mzimu wanga ndi mphatso mkati mwa inu ndiye taya moyo wakochifukwa abale tsiku ndi tsiku.” Mulungu anati, “lapitsanani machimoanu kwa wina ndi mzake tsiku ndi tsiku.” Mulungu anati, “Tengelelanizothobwetsa ndi kukwaniritsa lamulo la Kristu.”Muntha kuona kuti ndi chinthu chochitika tsiku ndi tsiku. Mungatengebwanji zobvuta za munthu wina mu msonkhano kukwaniritsa lamulo laAmbuye tiyenera kutengelana zobvuta za munthu wina. Nanga zothodwazimenezi zili kuti? Kodi zili ku misonkhano wa Mulungu? Ai, zobvutazamoyo zimapezeka ndi ana athu, ndi akazi athu ndi amuna athunsomu zintchito zathu. Zobvuta zamoyo ndi pamene chisilamu kapenachipembedzo chonama ndi mabanja athu a thupi atida ife chifukwachoti tabwera kwa <strong>Yesu</strong>. Amaswa moyo wathu ndipo sitidziwa chimenetingachite. Tikufuna inu kuti mundithandize mabvuto anga pamenemwana ali odwala. Sindifuna kumva uthenga wako lamulungu singapitekumeneko pamene mwana wanga adwala. Sindifuna kumva nzeru wakoyozama ndi kulankhura kozama ngati sungathe kundithandiza pamenendili ndi mabvuto ndi mkazi wanga. Ndi chochitika tsiku ndi tsikusizokhudza misonkhano ai. Kutengelana zothobwetsa tsiku ndi tsiku ndikukwaniritsa lamulo la <strong>Kristo</strong>.Tamanga molakwika mpingo mu mayiko ambiri kwa zakanso zambiri.Mulungu ali kuitana tsopano anthu amene ali ndi kulimbika ndikuzichepetsa ndi kuzipeleka yekha kuti imangidwe bwino. Ngatitidzamanga nyumba ya Mulungu kusata maonekedwe amene anaikidwa.Makomo a ku Hade imene ndagwira. Mudzachita, Atero Ambuye.Tikaona monga <strong>Yesu</strong> pamene adali kuno. <strong>Yesu</strong> sanangokamba chabe ai.Anakhala moyo Yohane 1 amatero “Moyo ndipo unasanduka kuunika kwaanthu.” Ndi chonchoso mpaka lero moyo wa tsiku unasanduka kuunikakwa anthu. Ngati tikufuna anthu kuti aone chikondi cha Mulungu ndipongati tifuna kuti abwere kwa <strong>Yesu</strong> mmalo mwa ndalama ndi mphamvuya chisilamu, ngati tikufuna kuona anthu ndi kunyada kwawo. Tiyenerakukhala mu moyo wa <strong>Yesu</strong> pamodzi tsiku ndi tsiku.Mbali ya AliyenseTalankhula zokhala ngati kapu ya madzi yodzadza ndi kulowa mwa <strong>Yesu</strong>.Tingalankhulenso za chinthu mpika wa mbatata ndinso mapika wachimanga chosatongola umu ndi mmene tamangira mpingo kwa zaka2000 zapitazi anthu amabwera onse pa lasabata monga anthu okhalangati mbatata kapenanso monga chimanga mtima wa Mulungu suli mumphaka wa mbatat kapenanso aliyense payenkha mu mphaka pamodzikwa masiku awiri limodzi, kapena atatu pasabata. Pokhala mu nyumbamnalowa chipembedzo mopembedzelamo si mwabwino ngati sitingathemitima yathu ndi mmene tingagwirile wina ndi mzake tsiku ndi tsiku.Msonkhano pawokha sumangitsa kuti ndi mpingo wa mbaibulo ai. Ukundi kumene mbaibulo amati malo ophunzitsilamo mphika wa mbatata payekha payenkha si mpingo. Mungathe kuponya mbatata zonse kapenansozimanga zonse mu mphika lamulungu lililonse komabe sukhala mpingosimpingo ai. Mpingo woona umafanana ndi mphika wa mbatata zosendandi chimanga chosendedwa ndipo simakhala zofanana. Monga zimodzimongaso okhala amodzi mu chikhulupiriro. “Mtima umodzi moyoumodzi, onse pamodzi ndi machitidwe amodzinso. Angakhale ndifeambiri koma ndife mmodzi kubatizidwa ndi Mzimu mu thupi limodzipamene wina sanganene kwa mzake sindifuna iwe mpaka nthawi yinasabata ya mawa.Mphika wa mbatata yosenda kapenanso chimanga ndi moyo wanukukhala mbali ya mbali ya ine ndi moyo wanga kukhala wa ine. Pamene tilamodzi monga <strong>Yesu</strong> ndi Atate ali – pamenepo ndiye mpingo wowona enaangapulumutsidwe inde popanda moyo umenewu koma sakupindula kwa<strong>Yesu</strong> pa msonkhano. Powonetsera kudziko za mphamvu yake ndi moyo.Ndidzamanga mpingo umene makomo a ndende. Sangathe kuwononga!Pokula msinkhu, kwa ana ndi akazi anu ndinso okhala nawo pafupi ndiena olumikizidwa ndi kulukidwa pamodzi. Umenewu ndi mpingo mupulani ya Mulungu.Pamene moyo wanu uli mbali ya moyo watsiku ndi tsiku pamene mphatsoyanu uli mbali ya ine ndi mphatso yanga ndi mbali yanu tsiku ndi tsiku.Pamene ndiulura machimo kwa inu ndipo mukuulura machimo kwaine ndipo tipemphererana wina ndi mzake kuti tichilitsidwe. Pamenemundidziwa ine koposa choncho mungathe kuwona kuchokera mu maso150 151


anga kuti ndawaidwa moyo ndipo muli kunditengera zothodwa – Ndipamene mpingo udzayamba kukhala mpingo wa <strong>Yesu</strong>. <strong>Yesu</strong> anati umundi mmene (Asilamu, Amboni za Yehova, Amarmori ndi onse woofookandi othentha chabe mu chipembedzo) adzadziwa kuti chikristu ndichochokera ndithu kumwamba. Onse adziko adzadziwa kuti tili a iyepamene tikondanilanaMungathe kunena za mwazi wa <strong>Yesu</strong> ndi mau a Mulungu koma mpakamutayamba kukhala ndi moyo wokondana wina ndi mzake ndiye kutiodzangokhala mau chabe. Ngati dziko lidzaona ife kukondana wina ndimzake chifukwa choti moyo wathu wataika pothandiza wina ndi mzakendiye kuti moyo wa Mulungu ndi mphamvu idzakhala ya mphamvukoposa. Mukumizidwa ndi mu mphamvu (ndipo tidzapachitikidwa ndikudedwa, kunamizidwa monga mwa <strong>Yesu</strong> analankhulira!).Atate akonda mwana ndipo tidzayamba kuoneka monga mwana kuwalamonga nyenyezi zakumwamba. Mudziyikidwa pamwamba pa Phiri umenesangathe kubisika. Ameneyo ndiye <strong>Yesu</strong> ndi cholinga cha mkwatibwiwake, mpingo sitingoyenera kukhala owonera chipembedzo ndi kunenamau ena tiyenera kusiya kukhala mu mipando monga zidoli kumvetserakwa wina ali kulankhura. Tiyenera kuti tikhudzidwe kwatunthu mumiyoyo mozama ya azanthu tsiku ndi tsiku abale pakati pa abale. Izisimsonkhano okha koma kupeleka mitulo kwa ine ndiponso ine kwa inutsiku lililonse mu zinyumba zathu ndi muzintchito kumunda ndi kubanjaathu izi zimafunika kusintha mmene mumagwilitsira nthawi yanu ndipomusinthe zinthu zimene munazitenga kuti ndi zoyambilira mu moyowanu ndi kutero “Thangani mwapeza ufumu wa Mulungu.”Banja Lenileni!!<strong>Yesu</strong> anati ngati mupeleka moyo wanu ndi kukhala mkristo mudzakhalandi amai ambiri abale ambiri ndi alongo ochuluka kuthandauza kutimgwilizano wopambana ndi zimene baibulo limathandauza za chikristo!Mudzakhala ndi chiyanjano amene ali pafupi monga mai ndi mwana kapenambale ndi mlongo pamodzi pafupi – pafupi molumikizana chibale. Sanatiabwenzi ambiri kapena otizungulira ambiri <strong>Yesu</strong> anati mpingo ndiwo zanala mgwilizano umene uli olumikizana monga mai kwa mwana wake.Mai wabwino amamva kulira kwa mwana wake ndipo amamva kulirakwa mwanayo pamene wabvulala kapena pamene ali ndi njala. Awandi kulira kosiyana amadziwa kulira kwa mwana wake molumikiza– zonse zokhudza za mwana wakeyo. <strong>Yesu</strong> anati mu mpingo wangawoona mudzakhala ndi ubale ochuluka “wolumikizana mongaamaindi mwana mudzatha kuwona mu maso anga, ndinso ndizatha kuwonammaso mwanu pamene mwatopa muli ndi njala, mwakwiya ndi pameneodandaula izi siza msonkhano ai sichoncho kodi? Siza lamulungu mmawamukulalikira, sinchoncho kodi? Simsokhano wolalikidwa lamulungumwamva kodi? Koma moyo wa tsiku ndi tsiku pamodzi monga amai ndimwana wake.Mai kodi angakhale ndi mwana wake lamulungu lokha basi akhozakukhala mai oipa, sichomwecho? Chidzachitike ndi chiani ndi mwanayo?Mwanayo adzafa. Izo ndi zimene zachitika ndi akristu ambiri tamangamolakwika kwa nthawi yaitali ndi munthu olalikira ndipo ena tonsekumangomvetsera ndi kumaimba ndi kuvina ndi kupita kumudzindikukhala ndi moyo wosiyana chifukwa cha ichi ana ambiri afa ndipoamai ambiri asweka mitima yawo.Cholinga cha <strong>Yesu</strong> pa mpingo wake ndi kukhala amai ambiri abale ambirindi alongo ochulukanso. Malo athu ndi zokhala nazo ndi nthawi ndindalama sizathu ayi, ifenso si a ife tokha. Tinagulidwa ndi mtengo wamkulundi mwazi wa <strong>Yesu</strong> ndiye timapanga chiganizo kuti tisankhalenso ndimoyo wathu pokhala mu moyo wa wina ndi mzake tsiku ndi tsiku AAHndatopa ndikuganiza zopita kukagona Ai pita kukakumana ndi kukondaambale ako gwira ntchito pamene kuli masana usiku ubwera ndipo palibechochita. Ndikuganiza zochita zimene ine ndizikonda. Bweletsani mbalekwa ine ndi abale enanso ambiri chitani ndi anthu ena chabwino tiyenerakupita ku msika. Ndilibe nthawi yokhalira ndi abale kapena alongoatengeni onsewo. Ndipo chitani nonse pamodzi ndipo mumodzi. Ndiponjiramo mudztha kudziwa zosowa za zimene afuna ndi zinthu zimenezili zofunika kwa iwowo chifukwa ndinu okhuzidwa ndi moyo wanundipo sika ndi muzochita osati mphatso yathu yokha imene ili yokhayokha.TONSE tili ndi mphatso ya <strong>Yesu</strong> ndikuonetsera moyo wake.mngelo anati “pitani nonse ku misika ndi kuuza wina aliyense za moyowa TSOPANOwu umene muli nawo wa <strong>Yesu</strong>! Izi ndi zimene anthu onse152 153


adzadziwa. Pakuona kuti muli KUKONDANA WINA NDI MZAKE!”moyo unakhala (ndipo unakhala) kuunika kwa anthu.Ngati tidikira mpaka kutha ntchito yathu yonse ithe kuti tikhale banja,sitidzakhala banja. Banja limapanga zinthu zonse pamodzi. Kuchapazobvala zathu pamodzi ndi kupita ku msika pamodzi. Kuyendapamodzi ndi kulankhura machimo kwa anthu za <strong>Yesu</strong>. Pamene tili tonsepamodzi timaulura machimo kwa azanthu timati, mlongo mungathekundipemphelera? Ndili wotopa ndi ana anga ang’ono ndiponsondakwiya ndi mwana wanga wa ng’ono dzulo. Ndafunsa Mulungukuti andikhululukire komanso ndikufuna kuti andikhululukirensokapena mb’ale kodi mungakhululukire di kundipemphelera ndinaliku ntchito ndipo ndinakwiya ndi wina amene amafuna kundinamizandipo ndinalankhura mau oipa kwa iye. Ndinapita ndikumufunsa kutiandikhululukire ndipo ndili kuwulura machimo anga pa iwe. Choondemungathe kundikhulukira ndi kundipempherera ndikuti ndingakhaleolimba zonse. Inde ilipo nthawi imene timafunika kukhala patokha ndikupemphera mu seri ndi kukhala ndi nthawi ya wekha ndi zinthu zina.Koma pena pake tataya moyo wa <strong>Yesu</strong> umene umatikhalitsa pamodzi.Mphaka <strong>Yesu</strong> anatenga abale atatu ndi iye pamene anapita ku Geshemanemmunda uja pa nthawi yowawitsa ya moyo wake. ndi ifenso tichitechoncho. Aliyense amene amati ndi wake wa iye ayenera kuyenda mongaiye anayendera ndi chabwino ndi chopambana chimene chataika mu njiraya makona mu nyengo ya kutanganidwa Nu Clear. Kuzikonda ulesi ndikunyada. Tiyeni tilengeze <strong>Yesu</strong> kuti dziko lidziwe ndikuti tikule msikhu.Titsegule Mitima YathuIchi ndicho chifungulo chenicheni. Ife tiyenera kutsegula mitimayathu ndikulora anthu ena alowe m’mitima yathu. Ichi ndi chofunikirakwambiri. Palibe njira ina yozungulira ichi. Ife tiyenera kutsegula mitimayathu kwa wina ndi mnzake kuti <strong>Yesu</strong> akhonze kulowamo ndipo abale ndialongo athu akhonze kulowamo. “Ufumu wa Mulungu siuli pano kapenaapo,” <strong>Yesu</strong> adatero “Ufumu wa Mulungu uli mwa inu.” Ngati inu ndithudimufuna Ufumu wa Mulungu, sikungokhudza kukhulupirira zinthu zoonakapena kupita ku misonkhano. “Ufumu wa Mulungu siuli pano kapenaapo; uli mwa inu.” Ichi chitanthauza kuti ine ndifuna Ufumu wa Mulungu,ndiyenera kulowa mwa inu ndi mmene Ufumu wa Mulungu uli. Ichichitengera kulimbika mtima, kudzichepetsa ndi kumvera. AMEN? Ifetiyenera kukhala osakanizana osati osiyana. Ife tiyenera kukhala zana laamai, alongo ndi abale – osangoti zana la abwenzi abwino.Ngati ife tidzayamba kukhala munjira iyi kwambiri ndi kwambiri tsikulililonse pamodzi -------- ngati ife tidzatuluka m’nyumba zathu ndi kulowamumitima ndi miyoyo ya anthu ndi kuwalandila iwo m’mitima ndi miyoyo,ndiye kuti ife tidzaona mpingo moti makomo a ndende sadzaulakansokonse ayi! Ife sitidzafuna zigawo zonse zongopangilapozi za Baptist,Pentekositi kapena Nazarene. Ife sitidzafuna zigawo zonse ayi chifukwa <strong>Yesu</strong>adzadzadza ife! Ife tidzaona ulemerero wa Mulungu ukutsika mu miyoyoyathu munjira yodabwitsa. Ife sitifuna zizindikiro zonse izi tsopano.Tsopano anthu adzadzidwa ndi mzimu Oyera onse a iwo, ndipo ifetidzamizidwa pamodzi mwa Khristu.Ife taona zotsekeredza izi zikugwetsedwa pansi mu malo ambiri.Mpingo umene ife tili mbali uli ndi anthu ochokera kwambiri za umoyozosiyanasiyana zambiri amene ayika mbirizo pambali chifukwa chotiagwa m’chikondi ndi <strong>Yesu</strong>, pamodzi, ndipo ife tili kuthandizana wina ndimnzake kukula kukhala ngati iye tsiku lirilonse. Khalani ndi masomphenyaawa pa mzinda wanu. <strong>Yesu</strong> afuna anthu AKE kuti akhale AMODZI. Ifesitikhala amodzi chifukwa tapanga chisankho kutaya ziphunzitso zathu.Ife tidzakhala amodzi pokhapokha pamene tapanga chisankho kutayamachimo athu. Sikuti ndi aliyense AFUNA ichi – koma INU mukhonzakukhala kapena kufa chifukwa cha icho!Ufumu Kulandidwa Zida?Tangoyeserani padali mafumu awiri – mfumu yabwino ndi mfumu yoyipa.Mfumu yabwinoyo idali ndi mphamvu kwambiri kuposa mfumu yoipayo.Ankhondo a mfumu yabwino adali ndi zida zimene zikadagonjetsa mfumuyoipayo. Zida izi zidali za mphamvu yoposera. Mfumu yoipayo idadziwakuti siyingaime kulimbana ndi mfumu yabwinoyo. Tsono mfumu yoipayoidaitanitsa msonkhano wa akulu ankhondo ake.Iye adati, “ine ndili ndi njira zitatu.” Ife sitingalimbane ndi zida izi, tsonotiyeni choyamba tinyengerere gulu la nkhondo la mfumu yabwino kuti154 155


iwo safunika kuphunzira kumenya nkhondo ndi zida zao. Tiyeni tipangeiwo azingokumana pamodzi ndi kungoyankhula zokhudza zida zao.Atsogoleri awo akhonza kuyankhula zokhudzana ndi kudabwitsa kwazida zao. Iwo azimva bwino zokhudzana ndi zida, koma iwo ayiwala zammene angadzigwiritsire ntchito izo.”“Nayi njira yanga ya chiwiri. Ife tidzagawa gulu la nkhondo la mfumuyabwinoyo. Ife tidzazala mbeu ya chigawanikano pakati pao. Tsonokenako, mmalo mwa gulu la nkhondo limodzi, iwo adzakhala ndi timagulutating’ono tokwana zana limodzi. Iwo sadzadziwa m’mene angamenyerenkhondo pamodzi. Ife tidzawagawa iwo ndi kuwagonjetsa iwo.”“Nayi nira yachitatu. Ife tidzanyengerera gulu lankhondo la mfumuyikuti alore wina aliyense kulowa nawo gululo. Ife tidawauza kuti gulu lankhondo lalikulu ndi laulemerero ndikuti aliyense amane ali ovomerakuvala uniform akhonza kulowa nao. Ife mwachinsinsi tidzatumidzaena mwa asilikali kukalowa nawo gululo. Motero, iwo adzakhala ndizida zamphamvu koma sadzadziwa kugwiritsa ntchito iwo adzakhalaogawikana pa wina ndi mnzake. Ndipo gulu lao lidzadzaza ndi anthuamene ali opereka ulemu kwa ine, mdani wao.” Munjira iyi, mfumu yoyipaidali ndi kuthekera kolimbana ndi mfumu yabwino.Umu ndi mmene zachitikira mu mpingo. Nyimbo zili bwino, monga momwetayimbira – Mwazi wa <strong>Yesu</strong> siudzataya mphamvu zake. Mau a <strong>Yesu</strong> sadzatayamphamvu zake. Dzina la <strong>Yesu</strong> silidzataya mphamvu zake. Izi ndizo zida zathu.Satana angayime kulimbana ndi Dzina, mwazi ndiponso Mau a <strong>Yesu</strong>. Komampingo wa <strong>Yesu</strong> wataya mphamvu zake. Mmalo mwakukhala akhulupiriraa unsembe, ife tasanduka omvera ndi ochita a ndondomeko (pologramu).Ife tayiwala mmene tingagwiritsire ntchito Dzina la <strong>Yesu</strong>, Mwazi wa <strong>Yesu</strong>ndiponso Mau a <strong>Yesu</strong>. Ife tili okhutitsidwa ndikungokhala pamodzi ndikumamvera kwa wina wake akuyankhula zokhudza zinthu izi. ife tilinsoogawikana wina ndi mnzake. Pali mazana a mipingo, wina uliwonse ndimiyambo. Ife talola migawanikano iyi kuima mnjira yathu ife tisagwirizanepamodzi ndi kumenya nkhondo ndi mdani. Ife takhalanso auchisayero.Anthu ambiri mmabwalo achipembedzo samudziwa ngakhale <strong>Yesu</strong> mongaMpulumutsi ndi Mbuye wawo. Iwo ali osokonezeka. Iwo akuganiza kutiamamudziwa <strong>Yesu</strong>, koma iwo siali choncho ngakhale pang’ono, chifukwaiwo sadapereke moonadi miyoyo yawo kwa iye.Umboni Wa Moyo Wa <strong>Yesu</strong>Tsono mu mnjira zonse izi mpingo watwya mphamvu zake koma <strong>Yesu</strong>adanana kuti mpingo umene iye amangaudzakhala wakutheker kugonjetsamakomo a ndende. Chimene ife takhala tikuyankhula lero ndi yankhola vuto ili. Ngati ife timanga mnjira ya Mulungu, ife tidzakhala woyera.Osati chifukwaife tili a bwino, koma chifukwa anthu ambiri akutithandiaife tsiku lililonse. Iyi ndiyo njira ya Mulungu, Ngati ife timanga mnjiraimeneyi , ife tidzayanjanitsidwa mu umodzi. Ndipo ngati timanga mnjiraiyi, membala aliyense adzagwiritsa mphatso yake pochitira ubwinoonse. Ife sitikhala womvera chabe, ife tidzakhala asilikali, ndipo Banja lachikondi. Banja loona, kutengera kwa <strong>Yesu</strong> mu Marko 3:33-35 iyi ndiyonjira imene mpingo wa <strong>Yesu</strong> ukhonza kutengeranso mphamvu zake.Ife tinakwera kuno mumatola mmawa uno. Oyendetsayo aamanena,mukuwawa, kuti chisilamu chakhala chikutenga mphamvu mu dziko muno.Chabwino, ine ndekha sinditsamala kuti wina ali ndi nambala yambiri.Chimene ine nditsamal ndi choti, padzakhala umboni wa <strong>Yesu</strong> khristu padziko ili. Umboni womwe ndi woyera, umene ndi wa mphamvu ndi umeneuli ndi mphamvu yogonjetsa satana mmiyoyo ya abambo,amayi ndi ana.Ichi chikhonza kuchitika pokhapokha ngati mpingo wa <strong>Yesu</strong> ungatengesomphamvu zake.Ife tiyenera kuthandizana wina ndi mzake. Ife tiyenerakumanga miyoyo yathu pamodzi, tsiku lililonse. Ngati ife tizakhala mnjiraiyi, diye kuti dzina la <strong>Yesu</strong> lidzatengedwa mu ulemu wa pamwamba.Anthuadzayamba kunena kwa ife, “Tiudzeni ife za <strong>Yesu</strong> ameneyu amene inumumudziwa”. Apa ndipo pothera pathu, ngati ife tidzakhala ndi kulimbikamtima kuti tiumange njira iyi. Ameni?Chotsani Dengu Pa ChomeraAheberi 3 amanene kuti ife tiyenera kulimbikitsana wina ndi mzaketsiku lilonso. Ife tiyenera kuchenjedzana wina ndi mzake tsiku lilonse.Ife tiyenera kuthandidzna wina ndi mzake tsiku lilonse ndi ana athu aniakazi athu ndi ntchito zathu mminad mmisika----kutithandizana winwndi mzake siku lilonnse. Aheberi 3 amatiamapitilira kunena kuti ngati ifesitipanga achi, ndiye kiti dzinthu ziwiri zichititka. Ife tidzasanduka ouma,ndipo ife tidzaputsisidwa. Ngati inu muli ndi chikho cha madzi ndipomukuthira madziwa pa nthaka yofewa, nthaka yofewayo imamwerera156 157


madziwo. Koma mukathira pa mwala youma madziwo amangoyendererapa mwamba. Nthaka ndi yofewa ,mwala ndi wouma. Mwala ndi woumasungalandire. Ngati ife sitikhalirana ndi wina ndi mzake tsiku lilonsemonga Aheberi 3 afotokonzera, ife timauma. Mau a mulungu, sangalowemmtima yathu, iwo sangalowerere. Mtima wathu watsanduka ouma.Ife tidali chabe mdzinda wina wamtunda wokwana milingo zana limodzikuchoka pano, pafupi ndi nyanja. Nthaka ya mfupi ndi nyanjayo ndiyofewa, chifikwa madzi nthawi zonse ali pa iyo. Kutali ndi nyanjayi,nthakayi siiyandira mvula yambiri ndi youma. Ife tiyenera kukhala mwawina ndi mzake tsiku lililonse kapena ife tiuma. Ife sitingamve Mulungu.Ife sitingakule. Ngati inu mutenga chomera ndikuyika pansi pa dengu,chomeracho chidzafa. Chomera chimafuna kuwala. Monganso ife!nkuwerenga ma Baibulo sikokwanira. Kukhala nawo mitsonkhano pa sabatasikokwanira. Monga mbewu pansi pa dengu, ife tikhodza kufa. Timafunakuwala. Pamodzi tikhala mnjira iyi. Ife timagawirana kuwala pa wina ndimnzake. Popanda kuwala kumeneku, tifa. Popanda kuwala kwa wina ndimnzake mu miyoyo athu tsiku lirilonse, ife timauma.Chinthu chachiwiri chimene chimachitika ndichakuti, ife timaputsitsidwa.Ichi chitanthauza kuti sitidziwa kuti ife ndiouma. Ife taputsitsidwa. Ifetikuganiza kuti tili ofewa, koma ndife ouma. Ife timakonda kuyimba ndipotimakonda nthano za mBaibulo. Ife tikhozanso kukonda kuyankhulazambiri zokhudza <strong>Yesu</strong>. Koma ife tili ouma ndipo ife sitikudziwa ichi,chifukwa abale samatithandiza ife kukhala ofewa tsiku lirilonse. Ichi ndichoopsa kwambiri! Ngati munthu ali wakhungu, koma iye aganoza kutindi ondetsa wabwino wa basi, sichoncho?! Icho ndi choopsa!Munjira yomweyo, ife tikhoza kuputsitsidwa. Popanda kuwala kwa anthua Mulungu mu miyoyo yathu tsuku lirilonse, sikuti tidzangouma kokhaayi ife tidzaputsitsidwa. Ife sitidzaona mbali immene ili mwa ife imenesiili ngati<strong>Yesu</strong>. Malingaliro athu adzaputsitsidwa. Awa ndi malo oipakukhalapo. Kuwala kwa Mulungu sikungalowe, ndipo zinthu zoipazosidzingachuluke. Ife sitidzawadziwanso kuti zinthu zoipazo zilimo,chifukwa ife taputsitsidwa. Ngati inusimukhalira tsiku liri lonse pamodzindi wina ndi mnzake mu njira imene Baibulo limafotokozera, ndiye kutiinu ndi ouma ndi oputsitsidwa. Ichi ndicho Baibulo linena. Mulungusanama ayi. Aliyense amene sakumanga tsiku ndi tsiku pamodzi ndianthu ena, ndi mau a Mulungu, amauma ndi kuputsitsidwa. Ngati ifetidzadandaulirana ndi kulimbikitsana wina ndi mnzake tsiku ndi tsiku,mitima yathu iodzafewa ndipo Ife tidzamva Mulungu bwino lomwekudzera ku abale ndi alongo, ndi ngakhale kudzera mmalemba pamaenetiwerenga. Pamene ife tikhala mnjira ya Mulungu, ife timafewa. Kuwalakwa Mulungu kulowa. Mvula ya Mulungu ibwera ndi kumaliza kudzadzaife, ndi kuchotsa mphepo zoipa mwa ife. Pali chiyembekezo chambiri ngatiife tikhala mu njira ya Mulungu! Palibe chiyembekezo ngati ife sitikhalamnjira ya Mulungu.Ife tamanga munjira yolakwikwa kwa zaka zambiri. Mipingo yambirikuzungulira padziko lapansi ili ngati chomera pansi padengu. Iwoakhza kumva ziphunzitso zabwino, koma iwo alibe kuwala kwambirimuniyoyo yawo. Ambiiri ndi akufa, ena ndi okhinimbira. Ife tifunikakuchotsa dengu ili pachomera. Njira yaikulu yimodzi yochitira ichindi kulowerana mwa pamtima ndi wina ndi mnzake, kuthandizana ndiwina ndi mnzake, kulimbikitsana wina ndi mnzake, kukondana wina ndi,mnzake tsiku lirilonse.Iye akumanga anthu a MphamvuIye akumanga anthu kulamandaIwo akuyenda pamodzi ndi MulunguNdipo iwo akukula ndi Dzina Lake LopambanaMangani Mpingo Wanu, Mbuye,Tipangeni ife amodzi Mbuye,Mu Ufumu wa Mwana wanu,Mangani Mpingo Wanu MbuyeTipangeni ife amodzi, Mbuye,Mu Ufumu wa Mwana Wanu.Yendani UlendoBaibulo ndi loona mnjira iliyonse. Izi ndi zokhudza <strong>Yesu</strong> ndiomutsatira ake. Izi ndi nkhani za m’mene amawawidwira mtima ndi158 159


mmene amaphunzirira kudzera mmakhalidwe awo ndi Mulungu. Ifetikhonza kuphunzira kuchokera munkhani zawo, koma tikhonzansokuphunzira: pakukumana ndi kuonana ndi Mulungu pamodzipamoyo wathu wa tsiku ndi tsiku. Mu ichi nafe tili “malembo amoyo.”Zolembedwa zonse mu dziko lapansi sizinganthe ife monga m’menemoyo wapamodzi ungatisinthire ife. Zinthu zakuya zomwe tizifunasizidzafika pansi pa mitima yathu pamene zingawerengedwa kuchokerapa pepala chabe. Pamene tikonza zinthu pamodzi tsiku lirilonse, <strong>Yesu</strong>aliphunzitsa ife ziphunzitso zakuya zamoyo zomwe sitingaziphunzirekuchokera m’Baibulo, “ngakhale zoonadi ndi eklezia—mpingo.”“MOYO umasanduka kuunika kwa anthu.”Moyo siunapangidwe kukhala ngati sukulu ya galamala yomwetimakaphunzirako mfundo zina ndipo kenako kukhulupirirandondomeko ina kapena zinthu. Malo mwake Mulungu watiyitana ifekukhala amuna ndi akazi a Mulungu chimodzimodzi monga omweadaliko pasadabwere ife—olumikizidwa kwa Mulungu yemweyo ameneiwo adalumikizana naye—okhala m’chikondi chozama monga iwoadaliri. Kuti chimene tichichite kapena kuchikwanitsa, ife tiyenera osatikudziwa momwe iwo amadziwa zokha. Koma tiyenera kumva chimeneiwo amamvera, Mulungu ayenera kuti—tenga paulendo onga ngatiwawo. Tsono ife titenga ulendo umenewu mukugwiritsa ntchito Mau aMulungu kumodzi ndi moyo wathu. Ife tiyenda ulendowu ndi misozim’maso mwathu, ndikuthandizana wina ndi mnzake—mu nthawiyoipa ndi nthawi yabwino—ndi maso athu pa chiyembekezo chathu,Messiah wathu. Ife tikupita chitsogolo, kukhulupilira kuti Mulunguakhala otipatsa wathu, kutithandiza pomwe tikhala pamodzi.Kudzodza Kwa Wonse <strong>Yesu</strong>Ndiye BanjaMzuzu, Malawi Afirika 1996Kuti ukathe kuyankhula mawu a Mulungu munthu uyenera kudzodzedwa.Kodi izi ndizo inu nonsenu mumaganizira maganizo anu? Ndili ndiuthenga wabwino wochokela kwa <strong>Yesu</strong> kunza kwa inu okhudza zazimenezi. Izi zikulankhuliridwa kuchokela kwa buku la Yohane woyambachapter 2 (okhululupira) kuti muli nako kunzodza pa inu koona osatikwachinyengo. Mzimu wa Mulungu, <strong>Yesu</strong> amene anali mphunzitsiwamkulu akhala mwa inu. <strong>Yesu</strong> ndi mphunzitsi wamkulu, wodabwitsakomanso wamphungu. Paulo adanena kuti ngati mulibe mzimu wa <strong>Yesu</strong>mwa inu ndiye kuti simuli aiye. Ngati inu muli mkhristu, ndiye kuti<strong>Yesu</strong> khristu adali munthu odzodzedwa kuposa munthu wina ali yenseadakhalapo-Iyeyo akhala mwa inu. Uku ndiko kunena kuti ngati muliMkhristu, ndinu wodzodzedwa. Alleluya!Osakhala ndi udindo kapena dzina –Koma ntchito yochita.Pali nthawi zina pakati pa anthu okhulupirira pamapezeka ntchitoyoyenera kuchita. Pamakhala ntchito ngati kusamalira ana, kugawachakudwa, kusamalira chuma, kusamalira amai amasiye komanso anaamasiye, kuthandiza kusamalira zinthu kapenanso nyumba za anthu,kukonza mapaipi odutsira madzi a zimbudzi, kuikira magesi, kusoka zovalakapenanso kunthandidzana kulima munda. Pali ntchito zambiri muthupila <strong>Yesu</strong>. M’buku la Machitidwe makamaka mutu wa 6 padali ntchitoyoyenera kuchitidwa. Mchitidwe amu (malembo) m’mawu a mulungusizimanena “zokhudza kudzodza kokhala m’busa yekha ayi.” Anthu asanundi awiri omwe akufotokozedwa mukhaniyi adali anthu wamba chabeamene adadzadzidwa ndi mphamvu ya mzimu woyera komanso nzeru.Iwo chikhalilecho adali (akutumikira) akugwira ntchito yabwino ya <strong>Yesu</strong>.Petro adakana <strong>Yesu</strong> atayenda ndi Iye kwa zaka zitatu, koma pameneiye adamva tambala atalira, zidamuswa mtima wake. Ndipo pomwepoiye adabwererapamodzi ndi mbale wake Yohane. Ichi ndi chimodzimodzindi ife. Pali nthawi imene ife tidzapanga zinthu zoipa ndi nthawipamene ifee tidzapanga zinthu zabwino. Koma chili chonse tipange,ife tiyenera kupangira pamodzi ndi maso athu pamodzi ndi <strong>Yesu</strong> ndikulola Iye atipange ife akuya mukudalira pa Iye pamene masiku akupita.Moyoudakhala luwala kwa anthu.” Ife tiyenera kuphunzira kwambirizakhudza <strong>Yesu</strong> kudzera mukukhala pamodzi ndi kuthandizana wina ndimnzake- Mulungu, tithandizeni kutsegula maso athu.160 161


Adali ndi mbiri yabwino yokhudza khalidwe lawo lodzichepesa ngatiatumiki a <strong>Yesu</strong>. Koma padali ntchito yofunika kudyetsa amai amasiye. Ndichifukwa chake mubuku la Machitidwe mutu 6 likufotokoza za kuika kwamanja osati ngati kupemphera kwa <strong>Yesu</strong> koma kugwira ntchito.Monga molingana ndi Baibulo anthuwa sadali madikoni ngati mmenetingaganizire ambiri aife. Monga mmene iwo adalili adali oposa udikoni.Timamva tikawerenga mbuku loyamba la Timoteyo mutu wachitatu(3) timawerenga kuti dikoni ayenera kukhala mwamuna (wokwatira)wapabanja, koma monga mmene tikudziwira bwino ife tonse, anthu awasadali okwatira kapena adali ndi ana ayi.Tikumva nkhani inayake mmbuyomo, Paulo adapita kukaona Filipo,amene adali mmodzi wa madikoni asanu ndi awiri. Kodi mukukumbukilakuti Filipo adali ndi ana a kazi anai amene nawo amene adachitapo ulosi?Mzimu woyera umafotokoza bwino lomwe za Filipo ngati “m’modzi mwaanthu asanu ndi awiri,” osati “modzi wa madikoni asanu ndi awiri.” Kudalimadikoni ambiri m’mipingo yochuluka ya m’nthawi imeneyo komamzimu woyera siukutiuza kuti, Filipo, adali m’modzi wa madikoni asanundi modzi.” Koma mzimu woyera ukutiuza kuti Filipo m’modzi wa anthuasanu ndi awiri. Iyi ndi fundo yofunika kwambiri. Pali kusiyana pakati paDikoni ndi munthu wina amene adasankhidwa ku utumiki.Dikoni amakhala ndi ntchito yopitilira, Koma anthu asanu ndi awiri omweadasankhidwa mabuku la Machitidwe Atumwi mutu wa chisasnu ndichimodzi (6) tikumva kuti adasankhidwa ku utumiki wapadera. Ndipotonse tikuntha kuona kuti ntchito ya utumiki wawo idasintha pomwezinthu zidayamba kusintha mu Yelusalemu. Filipo adapita ku Samaliya,Stefano adanka naralikira masunagogi kumene tikumva kuti adaponyedwamiyala naphedwa koma sitikumvanso kuti iwo adapitiriza kuperekachakudya kwa akazi amasiye. Nthawi zina timayenera kuyika manja paanthu okhulupirira kuti Mulungu awatume ku ntchito yapaderadera,koma ngati ntchitoyo yomwe adasankhidwira yatha sapitirizanso kukhalamaudindo omwe kalero adasankhidwira. Pano pali mbali yosiyana,ngakhale, thawi zina pamene Mpingo wakula kwambiri, kuti ukhale ndimadikoni ndi akulu a Mpingo. Izi zimangokhala ntchito zopitiriza-pitirizaimene imalira zinthu zambiri monga mwa udindo kuti ukathe kuthandizamunjira zambiri.Pamene mudzatchedwa mkhristu, <strong>Yesu</strong> adzakusanjikani manja ndipopomwepo mudzakhala wansembe. Mudzakhala olankhula koma okondamawu a Mulungu. Pamene mpingo ukukula komanso kusintha, pamakhalantchito yoyenera kuichita kapena kuti mpingo umasankha mwa anthu akeamene alipo ena monga awiri kapena anai amene ali odzala ndi Mzimuwoyera ndi nzeru. Kapenso ngati ntchitoyo ioneka kuti ndiyaikuluamasankhirapo anthu ena asanu ndi awiri wodzala ndi mzimu woyerandi nzeru kudzaika manja pa iwo pamodzi komanso kuwasankha iwo kuutumiki. Koma izi zimakhala choncho ngati pokhapokha pali ntchito apobi ayi, anthuwo amakhaladi okhulupirika ndi omvera ku ntchitoyo ndipoadzakhaladi ndi udindowo, koma ngati kudzaoneka kuti sali okhulupirikapa udindowo, udindowo udzachotsedwa kwa iwo. Koma ngati alibeokhulupirika adzagwira ntchito paudindowo kufikira ntchito yomweadasankhidwira yachitika. Pamene tikamanena za Madikoni ndi Akulu aMpingo, iyi simakhalanso ntchito. Komanso ndi zoona kuti mwina nthawizina zimatha kutheka kuti ngati akhala anthu osakhulupirika amathakuwachotsa pa udindo wawonso.Mphatso ya MtumwiMtumwi Paulo adanena kuti iye ndi kapolo wosankhidwa ndi Mulungu.Sichinali kuti adali munthu wapaderadera ayinso, koma kuti Mulunguadali kufuna kuonetsera chifundo chake. Izi zidali chomwecho ndi atumwionse. Iwo sadasankhidwe chifukwa adali anthu apaderadera ayi. Iwoadasankhidwa pa mpikisano wa chifundo cha Mulungu. Paulo adanenazimenezi kwa akhristu aku Mpingo wa ku Korinto kuti ngati sangachitentchito yomwe Mulungu adamuitanira ndiye kuti chinthu china chakechikhodza kuchitika monga ngati matembelero. Paulo adanena kuti udindowa mphatso ya utumwi ndiwo nthawi zonse ayenera kukhala munthuwokhulupirika ngati kapolo kuti ukathe kuwauza anthu ena za ukulu waulemerero wa <strong>Yesu</strong>. Choncho adakhala kapolo wa uthenga wabwino wa<strong>Yesu</strong>, ndipo m’malo mwake adapereka moyo wake pa mtengo uli wonseomwe akadayenera kupereka, kuti akathe kukwanitsa kuwauza anthu enaza uthenga wabwino wa <strong>Yesu</strong>.Pali mphatso zambiri muthupi la <strong>Yesu</strong> khristu ndipo mphatso iliyonseili ndi kufunikira kwake. Paulo adanena kuti mphatso zomwe aliyense162 163


adali nazo zinali zofunikira mwapadera, kuti aliyense athe kutumikirangati wansembe kuti akathe kuwauza anthu ena za <strong>Yesu</strong> Khristu. Iyeadanenanso kuti anthu ena omwe amanena za <strong>Yesu</strong> adzalandira mphoto.Koma mtumwi Paulo adanena kuti, ali otemberereka ngati sangawauzeanthu ena zokhudza <strong>Yesu</strong>. Mphatso ya utumwi ndi ubwino wake ndiumodzi komanso yapaderadera komanso yosowa kwambiri. Komansoili ndi zopereka mtengo wache zambiri, monga kulankhula kwa Paulo.Atumwi ali ngati mizati m’nyumba ya Yehova. M’buku la Aefeso mutu3, Paulo akulankhula za zinthu ziwiri zomwe iye amayenera kuchita paudindo wake ngati mtumwi. Adanena chinthu chimodzi pa (versi la 8)ndiko kuuza anthu ena za chuma ulemerero wa <strong>Yesu</strong>. Mundime la a Pauloakunena za chinthu chachiwiri chimene iye adaitanidwira, ndiko kutiakathe kuwafotokozera anthu momveka bwino m’mene angakhalire muulemerero odabwitsa wa <strong>Yesu</strong> Khristu. Iye adanena kuti adzawaphunzitsam’mene angakhalire ndi moyo wodabwitsa wa <strong>Yesu</strong> komanso m’meneangasanthulire moyo wodabwitsawu wa <strong>Yesu</strong> m’moyo wawo.Mubuku loyamba la ku Akorinto mutu wa 3, Paulo akudzitcha yekha womangawaluntha. Iye sadanene chinthuchi chifukwa adali onyada koma Mulunguadachiika chinthuchi m’mafupa ache. Mulungu adampatsa iye chifundokomanso kumkomera mtima pomupatula iye mwapadera kuti akhale nayomphamvu yotha kuona zinthu zimene ena samakwanitsa kuona. Mu bukhula Akorinto loyamba mutu wa 15: ndime ya 10, Paulo adanena kuti iye adalichigawenga koma Mulungu sadamukhululukire kokha koma adamupatsamphatso yapadera. <strong>Yesu</strong> amapereka mphatso zambiri, zosiyanasiyana.Muzinthu zonse zomwe <strong>Yesu</strong> adali ziwalo zake zonse, adazipereka ku Thupilake. Mukunena kwa tchutchutchu mphatso zonsezi ndi zofanana chifukwazonsezi ndiye <strong>Yesu</strong>yo. Koma mphatso yomwe Mulungu adamupatsaPaulo idali ya utumwi. Paulo adanena kuti iye “sadali munthu oyenerakukhululukidwa machimo ake. Koma chifukwa adamukhululukira machismoake ndikumupatsa mphatso, iye adzagwira ntchito modzipereka kwambiringati njira imodzi yonenera zikomo Inu Mbuye <strong>Yesu</strong> pondikhululukiramachimo anga.” Mphatso imeneyi idali kuti akathe kuwafotokozera anthuena za chuma cha mtengo wache wapatali cha <strong>Yesu</strong>.Chifukwa kuti Paulo adali ndi mphatso yamtengo wapatali yoona zinthuzomwe anzake sankaziona, iye adafunitsitsa kuthandiza anthu onse aMulungu kuti athe kuona m’mene angayendere pamodzi. Umu ndi m’menemphato ya utumwi ilili, n’chifukwa chake mphatso imeneyi ili yofunikakwabasi mumpingo pa dziko lonse loti zungulira. Tayerekazani mutayikaakhristu odzipereka okwana zana limodzi pamalo amodzi, onsewo adzakonda<strong>Yesu</strong> ndi mitima yawo ndipo kudzakhala kufuna kwawo kuti amumvere<strong>Yesu</strong>. Koma kopanda chiyanjano ndi mtumwi nthawi zina zimakhalazovuta kudziwa m’mene angayendere pamodzi. Angadziperekere, akhristuokondana angamavulazane wina ndi mnzake, koma mphatso yomwe <strong>Yesu</strong>amapereka kwa iwo ya utumwi imawathandiza kuti agwire ntchito limodzi.Kuika Ziwalo Zonse PamodziTikhoza kutenga ziwalo zonse za galimoto – chowongolero, bampala,mota, chitseko – ndikuziunjika munyumba imodzi. Zonsezo zikhozaokukhala ziwalo zodabwitsa, koma m’malo mwake simungathe kuyendetsamtunda wautali ngati zidutswa zonse za galimoto sizinaikidwe pamodzi.Zoonadi zeni zeni pa nkhaniyi ndi yakuti mukhoza kupita kuli konse ndigalimoto imeneyi. Mphatso ya utumwi ndiyo imasonkhanitsa mphatsozonse pamodzi. Mumpingo tikufuna mphatso yomwe ingapangitse kutizidutswa za galimoto zikhale pamodzi. Izi ndi zimene Paulo amanena pabuku la Aefeso 3. Iye amawauza anthu za ukulu wa dzina la <strong>Yesu</strong> limenelimathandiza kuika mpingo pamodzi. Paulo adafuna kuika mpingopamodzi kuti itchedwe nyumba ya Mulungu. Mphatso zonse komansoakhristu onse odzipereka amafuna mphatso ya utumwi kuti iwathandizekuika nyumba pamodzi.Mubuku la Aefeso mutu 4, Paulo adanena kuti Mulungu amaperekamphatso kwa mpingo – mtumwi, mneneri ndi mphatso zina kutipamenepo tikakule tonse pamodzi. Imatiphunzitsa kuti tisakhalensomakanda, imatithandiza kuti tikule kufikira muuphumphu wonse wa<strong>Yesu</strong> Khristu, kutithandizira kuti tikaumbike pamodzi. Paulo adanenaza kufunikira kwa mphatso ku mpingo kuthandizira anthu abwino kutiamangirirane pamodzi.Makalata ambiri a Paulo amalankhula za ntchito zochitika zenizeni. Iyesadakambe zambiri za <strong>Yesu</strong> Khristu, koma makamaka zinalimbikitsaokhulupirira m’mene angakhalire pamodzi kwa wina ndi mzake. Iye164 165


adawaphunzitsa iwo ndi zinthu zochitika zeni zeni kuyambira ndalama,ukwati, ana ndi akazi amasiye, komanso m’mene angamangiriranemumpingo mokhudzana ndi ulamuliro. Iye adawaphunzitsa zokhudzanandi kupembedza kwawo pamodzi, misonkhano, komanso m’meneangamangirirane pa zinthu zosowa zawo wina ndi mnzake.Chiphunzitso cha zidutswa zabwino za galimoto (kuti m’mene zikhaliregalimoto) izi ndi zimene mtumwi Paulo amachita ndi mphatso yache iyeamafuna kuwaphunzitsa kuti akhale pamodzi ndi kupita kwina kwake,ifeyo sitikufuna kukhala ngati mkoko wanthochi omwe siungathe kupitakwina kuli konse. Ife tikufuna kukhala Basi ya <strong>Yesu</strong> yomwe ingakwanitsekupita kwina kulikonse. Tikufunika kumangika pamodzi kenako ndikuphinzira m’mene tingagwirire ntchito muchikondi.Paulo akutiuza kuti ndichinthu chabwino kukhala ndi mafunso a zinthuzochitika. Mubuku la Akorinto woyamba mutu 1, tikuwerenga za banjala Kloe lidayenda mtunda wokwana 100 milosi kuti akathe kumufunsamafunso Paulo. Amakamufunsa za magawano chomwe iwo mu mpingowakumeneko zokhudzana ndi mabanja, komanso chomwe iwo angachitetchimo likakhala liri pakati pawo. Chifukwa kuti mphatso yake idaliya utumwi adatha kuona chomwe iye angachite. Anthu a Mulunguadali kumufuna Paulo kuti athe kuona komanso kuwathandiza. Paulochonsecho sadali “opsa wina aliyense ayi.” Iye adali kudziwa bwino lomweza chifoko chake mumtima mwake, kuti tsiku lina iyenso adachitapouchimo asadatembenuke. Koma chifukwa Mulungu adamukonda Paulo,n’chifukwa amafuna kunena “kuti zikomo” pogwiritsa ntchito mphatsoyake kwa anthu a Mulungu.Mafunso Ofunsa Zinthu ZenizeniZokhudzana Ndi Udindo Wa Amuna Ndi AkaziKomanso ndikadakonda amai adzivala bwino modzilemekeza, osati nditsitsi langale zamtengo wapatali ngati golide, kapena zovala zamtengowapatali, akhale ndi makhalidwe abwino ovomere kwa akazi onsewopembedza Mulungu. Akazi ayenera kuphunzira mwakachetechete,koma sindilola ine akazi ayenera adzimveke okha ndi chovala choyenera,ndi manyanzi, ndi chidziletso, osati ndi tsitsi loluka, ndi golide kapenangale, kapena Malaya a mtengo wache wapatali, komatu; (umo mokomeraakazi akuvomereza kulemekeza Mulungu), mwa ntchito zabwino. Mkaziaphunzire akhale wachete m’kumvera konse. Koma sindiloloa ine kuti mkaziaphunzitse, kapena kulamulira mwamuna; komatu akhale chete. Adamuadali oyamba kulengedwa, pambuyo pake Eva. Adamu sindiye adayambakunyengedwa ndi chinjoka koma mkazi ndiyo. Mkazi adapulumutsidwamwakubala mwana ngati akhala n’chikhulupiriro, n’chikondi ndi n’chiyeretso.(1 Tim 2:9-15)Izi zikungofanana ndi mawu omwe akupezeka m’buku loyamba la 1Akorinto mutu 14, Paulo adalemba mawu onsewa ndi mzimu wa Mulungu.Ndiye n’chifukwa ndikufuna kuti timvetsere zomwe mzimu woyeraamaganiza komanso pamene iye amalemba zinthuzi. Mzimu woyera ndimunhu amakhala ndi maganizo komanso zokhumba, monganso mene inundi ine tili. Inuyo mukalankhula kanthu kwa ine ndiye kuti mukulingalirazinthunzo komanso muli ndi chikhumbitso chachikulu kuposa umomwalankhulira. N’chifukwa chake ndafuna kuti timvetsere zimene mzimuwoyera amamvera komanso kulingalira chifukwa mzimu woyera ndimunthu, osati mawu okha ayi.Mtima wake wa Mzimu Oyera umakonda mai kapena bamboochimodzimodzi. M’bukhu la Agalatiya mutu 3, iye amanena kuti palibemwamuna kapena mkazi tonse ndife amodzi mwa khristu. Palibe M’yudakaya Mheleni, palibe mkazi, palibe mwamuna, palibe wakuda, kapenawoyera, kapena wachikasu. Alleluya!! Koma tsopano tonse ndife a <strong>Yesu</strong>.Kodi <strong>Yesu</strong> adali ndi maonekedwe anji? Ndani akuchidziwa chinthuchi?Iye ndiye wodabwitsa! Chifukwa cha chimenechi, ndichifukwa chaketilinacho chikhulupirio mwa <strong>Yesu</strong> Khristu, tonse timavala <strong>Yesu</strong>, palibensoMyuda kapena Mheleni, kapolo kapena mfulu, mwamuna kapena mkazi.Izinso Mzimu Oyera adalankhula mubuku la Agalatiya mutu 3.Malingaliro A Mtengo Wapatali OkhudzaZa UlamuliroPali zinthu zambiri zomwe Mzimu Oyera amaganiza zokhudzana ndimkazi kapenanso mwamuna; zinthu zimenezi ndi zamtengo wapatalitiyenera kuzimvetsa pamodzi. Pamene tikulingalira za mwamuna kapena166 167


mkazi, tikuona kuti Atate ndi mutu wa Khristu. Khristu ndi mutu wamwamuna. Mwamuna ndiye mutu wa mkazi. Kodi <strong>Yesu</strong> sindiyenso mutuchimodzimodzi Atate wake? <strong>Yesu</strong> adanena, “Ine ndi Atate ndife amodzi.”Koma Atate ndiye wamkulu kuposa khristu, ngakhale ndiwo amodzi.Tomasi adanena ndi <strong>Yesu</strong>, “Ambuye wanga ndi Mulungu wanga.” Atatendi mwana ndiwo amodzi.Chachidziwikire kuti <strong>Yesu</strong> ndiye mutu wa mwamuna. Koma ngatitidavekedwa <strong>Yesu</strong> tili naye pamodzi <strong>Yesu</strong>yo. Apa tikuona kuti pali ulamuliropakati pa mwamuna ndi mkazi. Mwamuna aposa mkazi chimodzimodzi<strong>Yesu</strong> ali oposa mwamuna. Pamene mwamuna ndi mkazi ndiwo amodzimwa khristu. Choncho, kunena momveka bwino tikutathauza kutimwamuna ndi mkazi ndiwo amodzi (ofanana). Koma ngakhale zilichoncho pali ulamuliro pakati pa mwamuna ndi mkazi.Zinthu izi ndizo za mtengo wapatali ndipo muyenera kutchereza.Mwamuna angathe kutumikira mkazi ndi mtima wanu wonse. Mwamunaayenera kukonda mkazi kumuchengetera mozama. Mwamuna, munjiraina iliyonse ayenera kukhala kapolo kwa mkazi. Ngati chimodzimodzinsokhristu adabwera kudzatumikira mpingo. Ngakhale kuti <strong>Yesu</strong> angathekusambitsa mapazi athu ngati kapolo angachitire, komabe ali ndi ulamuliro.Chimodzimodzinso, mwamuna achengetere komanso akonde mkazi,mpakana adadziyesera yekha kapolo kwa iye munjira ina iliyonse, iye alinawo ulamuliro pa mkazi, ndipo mkaziyo ayenera kumvera ku zimenezi.Ngakhale kuti zili <strong>Yesu</strong> ali ndi okoma mtima kwa ife komanso kutikondaife sindicho chifukwa kuti ife tiyiwale ulamuliro wake, kodi sichoncho?Muli dongosolo mwa Mulungu la kachitidwe kazinthu. Muli ulamuliromwa Mulungu. Pamene Mzimu Oyera amalankhula nafe pa 1 Akorintomutu wa 14, ndiso 1 Timoteo mutu wa 2, izi sizikutanthauza kuti amunandi olamulira, kulamulira mkazi ndi nkhonya ya chitsulo. Komansomkazinso sikapolo kuti ayenera kuti adzithawira kukonda mumdima.Tiyenera tikondwerere mphatso adapereka kwa akazi athu, ngakhalebeamadzipereka pa mphatso zomwe Mulungu adawapatsa mitima mwawo.Koma akazi ayenerabe kuzindikira za ulamuliro umene Mulunguadauyika pa amuna. Choncho zinthu zonse ndi zamumtima. Zinthuzonse zotchedwa chi khristu zimakhudza mtima osati malamulo. <strong>Yesu</strong>sadatininkhe ife malamulo m’malo mwake adatipatsa ife mtima wake. Iyeadatiphunzitsa ife kuganiza monga momwe iye angaganizire. Chonchocholinga chathu chachikulu ndicho kukhala ndi mtima omwe iye amafunaife titakhalira monga mawu opezeka mabuku a 1 Akorinto 14, kudzanso1 Timoteo 2, Baibulo sindiyo Buku la malamulo lokha komanso m’menetimapezamo moyo. Kodi zimenezi zikuoneka bwanji m’moyo wathuwa tsiku ndi tsiku? Muchiyanjano chomwe chilipo pakati pa mwamunandi mkazi, mwamuna adzadyetsa, kusamalira, komanso adzachengetamkazi wake. Adzautaya moyo chifukwa cha mkazi munjira ina iliyonse,ngakhalenso kupitirira apo kukhala kapolo chifukwa cha Mpingo.Chimodzimodzi mkazi ayenera kukhala otchereza kwa mwamunachifukwa ndi mtima wake. Mtima wake wa mkazi ndi kutcherezamawu onse komanso kuchita zomwe mwamuna akufuna. Ili si lamulokoma m’mene <strong>Yesu</strong> amakondera kuti ife tizikhalira m’mtima mwathu.Mukuchulukira komwe mwamuna angakhale nayo nthawi yochitazomwe tatchula pamwambapa, mochulukira mwamuna adzamverakulankhula kwa Mulungu. Komanso mkazi akakhala ndi moyo womverakwa mwamuna, iyenso adzakhoza kumvera kulankhula kwa Mulungu.Mawu amanena kuti, “Anthu awiri adzayenda bwanji asanapanganiretu?”Ulamuliro Umatimasula Ife!Zinthu zonsezi tatchulazi, ndi zofunika. Ngati mpingo uli pamodzi,komanso ngati mitima yathu ndi maganizo zili zabwino, ndipo mwamunaadzakhala wochita ulemu komanso okonda akazi onse (am’menesadzasowa ngati mipando). Amuna adzayamba kukonda mphatso zomwezili mwa mai ndipo iwo sadzalola kuti mphatso zomwe zili mwa iwozikwiririke m’nthaka. Nawonso alongo adzayamba kulemekeza abale,pamene ali pachiyanjano cha oyera mtima, ndipo iwo ngati akazi adzathakudziwa ulamuliro wa amuna osafuna kukhala pamwamba pa ulamulirowa amuna. Paulo adanena, “Ine sindilola mkazi aphunzitse komansoakhale ndi ulamuliro pa mwamuna.” Ngakhale angathe kupereka mphatsozawo. Mwachitsanzo: Ngati mlongo wina ali ndi kanthu kena m’mtimamwake kofunika kulankhula, iye sayenera akwirire luntha lake. Iyesayenera kuti akwirire mphatso yomwe Mulungu adamupatsa mphatsoyomwe ili mwa iye. Ife timafuna zonse za <strong>Yesu</strong>. Choncho ngati mlongoali ndi kanthu komwe kakumutentha mumtima mwake kofunika168 169


kulankhulidwa, wayenera mlongoyu apemphe abale pofuna kulemekezaulamuliro oposa wake nthawi zonse. Ngati pali mwamuna wa ulamulirooposa wake, ayenera kumufunsa ngati koyenera kulankhula. Komansongati kungakhale kotheka mwamunayo angathe kufunsa mpingo ngatikuli koyenera kuti mlongoyo alankhule kapena ayi. Ngati kungakhale kutimwamunayo aona kuti ndi kosavomereza mlongoyo kulankhula komansompingo wawona kuti mkaziyo asalankhule panthawiyo, iye ayeneraakhale okondwa kukhala chete. Mkaziyo sayenera kuti akwiye chifukwaadakanizidwa kulankhula. Sayenera kunena taonani, “kuyambira lerosindidzalankhulanso kanthu pakati pa mpingo.”Umu ndi m’mene amai angakhalire a <strong>Yesu</strong> kwa aliyense, komansomwamuna pokhalabe ndi ulamuliro. Wamuna angathe kutengamphatsoyo, koma munthu wa mkazi samadziika yekha pamwamba pamwamuna. Pamene muwerenga ziphunzitso za mawu a Mulungu nonsepamodzi, chimene mungaone ndi chakuti Mulungu ali mtima wolunjikakwa amai. Mkazi sindiye mpando kapena gome m’chipinda. Mlongoyoali ndi moyo mwa <strong>Yesu</strong> ndipo tiyenera kukhala omufunitsits mlongoyo.Komanso mlongoyo ayenera kumvetsetsa za ulamuliro wa Mulungundipo sayenera kukhala onyada. Iye ayenera kukhala odzichepetsa kutiathe kudzipereka yekha nsembe. Iyi ndi dongosolo la Angelo, dongosolola Mulungu Atate ndi dongosolo la <strong>Yesu</strong> mwana, komanso dongosolola mwamuna ndi mkazi. Tonse ndife amodzi, koma pali ndondomekomwa Mulungu imene imathandiza kuti zinthu ziziyenda bwino. Ndifeofanana, komanso mphatso ya mkazi ikhoza kukhla yabwino koposapoyerekeza ndi ya mwamuna wake, koma Mulungu adamupanga kukhalawa mwamuna. Ichi n’chifukwa chake pali dongosolo. Komanso mwina iyesamayenera kukhala ndi ulamuliro. Koma Mulungu amasankha zinthuzimene tiyenera kuzilemekeza, choncho tonse pamodzi tiyenera kugwirantchito yobweretsa mphatso komanso kukonda ndondomeko yomweMulungu waika kuti tiyende pamodzi tonse.Kumene ndimakhala ine kuli amai ambiri omwe ali ndi mphatso. Mpingokumeneko ndi odalitsika kwambiri chifukwa uli ndi amai olimba kwambirimwa <strong>Yesu</strong>. Iwonso akhoza kukuuza za ndondomeko yomweyi mongangati chinthu choyendetsa zinthu mwa dongosolo la Mulungu – chinthuichi sichiwakanikiza iwo pansi; koma m’malo mwake chimawamasula. Paliufulu wambiri popeleka mphatso zawo ngati nsembe m’malo mongotengapotsatira ulamuliro. Ndi chinthu chamtengo wapatali kukhala munthuwodzipereka. Akazi pa iwo okha adzakhoza kukuuzani kuti ulamuliroumawamasula m’mitima yawo ndinso umawapanga iwo kuyimba nyimbom’kati mwawo pamene akupereka nsembe ya mphatso zawo koposakutsatira ndondomeko. Choncho pamene sitiri kufuna kupondereza pansimphatso zonse, mphatsozo zimabwera ngati zopereka kuchokera kwaalongo, izi ndi zoona makomo, komanso m’ziyanjano za oyeramtima. Uwundiwo mtima omwe <strong>Yesu</strong> amaufuna – mtima omwe iye angaudalitse.Kodi mukukumbuka zomwe Ambuye <strong>Yesu</strong> adanena kwa Kentuliyo,Msirikari wa Chiroma? Iye adanena kwa Kentuliyoyo kuti mwa iye,adaonamo chikhulupiriro chachikulu kuposa anthu onse M’Israeli.Chikhulupiriro chomwe <strong>Yesu</strong> adali asanachionepo chidapezeka mwamunthu mwamuna amene amadziwa kukhala pansi pa ulamulirokomanso ndikukhala ndi ulamuliro. Mlonda wachiroma adanenakuti Iye angathe kunena kwa watchito wake “Pita”, ndi iye adzapita.Adzanenanso kwa waichito wina “Bwera kuno”, ndipo iye adzatero.Iye adanenso kuti ndiye munthu odziwa ulamuliro ndiko kunena kutiPita ndinso Bwera ulamuliro wake. <strong>Yesu</strong> adanena kuiti uyu ndi munthuwachikhulupiliro Chachikulu yemwe <strong>Yesu</strong> adamuonapo chifukwaamadziwa kumvera ulamuliro. Ichi chinali chomwe chinamumasulaiye, osati chomwe chingamukanikize iye pansi.Pamene <strong>Yesu</strong> ali mutu wa Mwamuna, mwamuna amamasuka. <strong>Yesu</strong>adanena kuti ngati sitingathe kukhala kapolo wache tingathe kukhalakapolo wa tchimo. Ngati sitingathe kumulola <strong>Yesu</strong> kukhala Mbuye wathu,uchimo udzakhala mbuye wathu. Koma ngati mwana adzatiyesa ife mfulutidzakhala mfulu ndithu. Kodi mukutha kuona zinthu izi m’moyo mwanu?Mukangomumvera <strong>Yesu</strong>, inuyo mudzamasulidwa? Koma pamenemungakhale osamvera <strong>Yesu</strong> ndi osalungama m’mtima mwanu.Izi ndi m’mene zilili ndi mwamuna ndi mkazi. Ife tikatsalira ulamuliro waMulungu, sitikhalanso akapolo; ndife mfulu. Koma ngati sititsalira timakhalaakapolo ku zolakwika zathu. Mkazi yemwe Sali pansi pa ulamuliro ndiyeosalungama m’mtima mwake. Iye adzakhala okhumudwa ndi osakonzeka,Mulungu ndiye amapereka ulamuliro m’banja komanso m’mpingo – izisizitanthauza kuti pali munthu wina yemwe ali wabwino kwambiri kuposa170 171


wina ayi, kapena kuwafotokozera anzakenso kuti achite chiyani powalamulirachomwe angachite. Iye amapereka ndondomeko ndi ulamuliro kuti tonsetikhale omasuka kuchikondi ndi dongosolo la Mulungu.Kulankhula Ndi Atate Ngati BanjaChomwe tikufuna kulankhula apa ndi m’mene tingakhalire, osatim’mene tingakhalire ndi Chiyanjano. Kuyankha mafunso amoyo watsikundi tsiku ndikophweka poyerekeza m’mene zingaonekere pachiyambi.Pamene tidzathe kukhala ngati banja muchoonadi pomwepo zithuzidzayamba kumveka bwino. Anthu ambiri ali okodwa pakati pa banja ndichipembedzo ngati kabungwe. Gulu lina la anthu achabe a chipembedzondi banja. Pamene enanso akodwa pakati pongokhala opita kutchalitchindinso banja. Pamene chonsecho Mulungu akubweretsa Mpingo wakekuti ukhale ngati banja, pamenepo zinthu zimayamba kumveka bwino.Pamene tidzadziona pa ife tokha ngati banja, mayankho a mafunsoambiri omwe tingakhale nawo amayamba kupezeka. Chifukwatimayamba kukondana wina ndi mnzake mowirikiza, timagawanambali ina iliyonse ya moyo wathu umalukika pamodzi tsiku lili lonse,amuna amadziwa kukhala bwino ndi akazi komanso akazi nawoamadziwa m’mene angakhalire ndi amuna. Ngati tingadziwe m’menetingachitire m’makomo athu ndinso makwalala, tidzadziwa m’menetingachitire misonkhano.Mu zinthu zonse, tiyenera kuzindikira ndondomeko ya Mulungu,komanso tiyenera kusauzima Mzima. Tiyenera kuzindikira dongosolo,komanso sitiyenera kukwirira luntha lathu. Choncho, ngati Oyeramtima asonkhana pamodzi Mulungu amapereka pemphero mumtimawanga, ngati munthu wamwamuna ndine oyeneranso kufunsa ngati kulikoyenera kuti ndipemphere. Koma ngati amene akufuna kupempherandi wamkazi ndi chichidziwikire kuti ayenera apemphe kaye mwamunangati kuli koyenera kuti apemphere, mwamunayo naye ayenera afunseanthu onse osonkhanawo, “Kodi ndikoyenera ngati mlongoyo ayenerakupemphera?” Ngati mwamuna ndi msonkhano onse aganiza kutindikoyenera, mlongoyo ali pansi pa ulamuliro. Iye ndiwokutidwa ndiulamuliro ngati timulola iye kutero, koma ngati iye angachite zinthuzipayekha, izi zidzakhala kunja kwa ulamuliro (dongosolo). Koma ngati ifetonse tingamlole kuti apemphere mlongoyo ali pansi pa ulamuliro ndiponthawi yomweyo zinthu zili bwino. Zinthu izi nthawi ndizoona.Tiyenera kumvetsa zinthu zina zake zokhudza pemphero. Mawu oti‘Pemphero’ amamveka ngati achipembedzo ku makutu athu. Pamenetikhala ngati banja, mnjira yomwe tingagwirire tchito limodzi zimapangitsakuti zinthu ziyambe kumveka bwino pakusonkhana ife. Pamene tidzakhaleoyandikira kwambiri ndi Mulungu, mapemphero athu adzayambakumveka. Mudzipembedzo zonyenga nazonso, anthu amapempheramapemphero. Mwa <strong>Yesu</strong>, m’chikhristu, timakhala ndi chiyanjano ndiAtate athu okondedwa. Choncho, kunena kuti “Mapemphero okumanapamodzi amatanthauza chiyani?” Kodi zimatanthauza chiyani tikamanenakuti kukhala ndi banja la Mulungu pamodzi? Kodi mukutha kuonakusiyana” Wina ndi wachipembedzo, ndipo wina ndi wachiyanjano.Sitimanena kuti “mapemphero” koma m’malo mwake timanena kutikulankhulana ndi Atate – m’mene mwana amalankhulana ndi atateake. Kodi mwana angakonze mnsonkhano ndi atate ake, kodi angathekulankhulana ndi atate ake chifukwa amawakonda iwo? Tangoganiziranitiyana tating’ono titasonkhana m’kachipinda adzayenera kukonzamnsonkhano kuti akambirane ndi atate awo? Kodi adzapanga mnsonkhanoofuna kukumana ndi bambo wawoyo. Iyi sidzakhala mapempherookumana. Koma m’malo mwake idzakhala banja kukumana pamodzi ndiatate wawo.Tsopano ndiganiza mwayamba kuona mapemphero aumodzi amagwirirantchito. Siziyenda zinthuzi! Zimene timachita n’chakuti ngati m’baleakufuna kulankhulana ndi atate ngati iye atha kulankhula ine ndifunandilankhule nawo atatewo!” Umu ndi m’mene timapempherera pamodzipagulu. Umu ndi m’mene timalankhulirana ndi Mulungu pamodzi, pameneMulungu akutakasa mitima yathu. Mlongo wina akhoza kufunsa m’balewina, “Kodi chikhoza kukhala choyenera kulankhula ndi atate tsopano?”Iyeyo ali mudongosolo chifukwa ali pansi pa m’baleyo yemwe ali ndiulamuliro pa iye. Koma izi sizitanthauza kuti mlongoyo alibe ufulu akuthakulongosola za dongosolo loyenera. Umu ndi m’mene tingamachitiretikakhala ndi mapemphero, chiphunzitso, komanso tikamafuna kuyimbanyimbo, chifukwa tili ngati banja pamodzi ndi Atate wathu.172 173


Tikufuna tichotseretu miyambo ya anthu ndi chipembedzo-pembedzozichoke zituluke ndipo ife tingokhala ana wina ndi mnzake. Sitikufunakukhala achipembedzo, anthu oyera ndi Maina ndi zikhulupiriro zamiyambo ya anthu. Tikufuna tikhale ana okondedwa wina ndi mnzake,komanso ndi atate tsiku ndi tsiku. Kukumana kudzadzisamalira kokhachifukwa ife ngati ana komanso banja tingathe kukumana nthawi zonse.Timalankhula ndi adadi athu nthawi zonse. Timabweretsa chiphunzitso cha<strong>Yesu</strong> Khristu kwa wina ndi mnzake nthawi zonse. Ngati zingapangike kutitakumana pamodzi muchipinda chimodzi, zimakhala zinthu zamphamvu.Komanso izi sizitanthauza kuti zikhoza kukhala zosiyana mphindi makumiatatu zikatha.Funso Lokhudza AmaiFunso ndi ili: M’baibulo mawu a Mulungu amanena kuti pamene tisonkhanaAmuna ayenera akweze manja awo mwamba, koma akazi ayi. Kodi akazinsoakhoza kukwezanso manja awo mwamba? Kodi Izi zikhoza kukhalazabwino?Funso Labwino: 1 Timoteo 2:8-9 akunena kuti “ndikufuna amuna onsekulikonse akweze manja awo kumwamba akamapemphera, popandamkwiyo kapena kukangana kwina. Komanso ndikufuna amai adzivalamodzilemekeza, ndi moyenerera osati ndi tsitsi loluka kapena dzovala za pamwamba.Paulo sakutanthauza kuti, amai sayenera kukweza manja awo mwambapopemphera.” Komanso sakutanthauza kuti abambo sakuyenera kuvalamoyenera. Ngati m’bale angakwanitse kukweza manja, ayenera akwezemanja oyera. Mawu akulu pamenepa ndi “kuyera.” Ayenera kukwezamanja omwe ali odzipereka kutchito ya Mulungu komanso ofunitsitsakumutumikira pokhapokha amai akagwiritsa udyo ulamuliro, koma ali ndimanja ofunikira motumikira Mulungu, iye wayenera kukweza manja akemwamba. Mulungu sakutiuza kuti abambo sayenera kuvala modziyenerezakomanso sakutiuza kuti iwo sioyenera kukweza manja awo mwambapopemphera; kapena kuti ndi zabwino, ngati iwo ali ndi manja oyera,m’mene zilili zovomerezeka kwa amuna onse kuvala modzilemekeza.Ubatizo Wa <strong>Yesu</strong>September, 1996 Mzuzu MalawiKuzindikira UbatizoZimene Mulungu anaika kukhala chinthu cha bwino monga mphatsochakhala chinthu chochitira nkhonkho. Monga thupi la Kristu likamakulamonga ofanana ndi <strong>Yesu</strong> ndi zina. Tiyenera kudziwa kumasulira kwakuti ubatizo ndi chiyani? Timaona mu chipangano cha tsopano mmeneYohane Mbatizi anabwera kudzawabatiza anthu kuti machimo awoakhululukidwe. Panalibe malemba mu chipangano chatsopano zotiYohane adzabatiza anthu. Pamene Yohane anabwera anabviika anthu mumtsinje wa Yorodani zinali zodzbwitsa kwa anthu. Chifukwa panalibeuneneri wa ubatizo ndipo panalibe wina kale amene amadziwa mpakaYohane anabwera.Choncho kunali kosabvuta kuti Yohane ali kulakwa chifukwa panalibepamene Baibulo limanena kuti ndibatizidwe mu chipangano chatsopano?Koma chifukwa Yohane anali bwenzi wa Mulungu ndipo anatumidwa ndiMulungu ndi uthenga wabwino kwa anthu anabweletsanso ubatizo kwa iwo,ndipo amabwera kuchokera kumadera ndi m’midzi kuti kudzabatizidwa.Anthu ena amumpingo mu nthawi ya Yohane anati sitifuna ubatizo utiuzekuchokera mu ubatizo. Yohane kuti tibatizidwe Yohane sanathe kuwauzakuchokera mu Baibulo chifukwa munalibe chiphunzitso mu chipanganochakale. Koma Yohane anamvetsera kwa Mulungu ndi kumva mau aMulungu za ubatizo. Anthu ambiri ndi Afarisi anati. Ai ubatizo Baibulolimanena momveka bwino kuti anakana chifuniro cha Mulungu ku miyoyoyawo pokana ubatizo ndibwelezanso kuti mumvetse bwino Baibuli limatianthu amene anakana chifuniro cha Mulungu mu miyoyo yawo.Mwina sitidziwa bwino ubatizo mwina kunyowa konseko sitidziwa kutindi chiani kwa ife. Mwina sitingadziwe za izi koma ndi zofunika kwaMulungu mum moyo wathu. Mwina sitingadziwe kuti izi ndi chiani.Oma ndi zofunika kwa Mulungu ndiye ndizo funikanso kwa ifenso.174 175


Kufunika Kwa Ubatizo Kwa <strong>Yesu</strong>Mukuyangana mu chipangano chatsopano ndi chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong>zinthu zomalizira zimene <strong>Yesu</strong> analankhura asanapite kumwambamu mitambo zinali. Pitani ku dziko lonse ndipo pangani anthu kukhalaophunzira anga. Phunzitsani iwo mu njira zonse. Batizani iwo mu dzina laAtate, Mwana ndi Mzimu Woyera.Ngati ndikagona pakama mwina pafupi kufa ndipo ndili kukuuzani inukumakutu anu mwana ndi mau omalizira ndithu ndipo mau omaliziraamakhal ofunikira kwamabiri. Sichoncho? Mwa mau ena amenewaamene <strong>Yesu</strong> analankhula ndi kuti Akhale ophunzira anga abatizeni iwo.Aphunzitseni kuti amvere zonse zimene ndikuuzani ndi mau ofunikakwambiri kwa <strong>Yesu</strong> ndipo ayeneranso kukhala ofunikira kwa ifenso. Mauoti ubatizo mumau amu chigriki ndi ubatizo kuthandauza kumizidwakumira. Pamene anthu anamva <strong>Yesu</strong> ali kulanhkula sanamvetsetse. “pitaniakhale ophunzira anga abatizini mu chilankhuro chawo, anamva <strong>Yesu</strong>akuti . pitani akhale ophunzira anga abatizeni iwo kumizidwa mmadzi.Ubatizo sunali mau a chipembedzo nthawi imeneyo. Pamene timamvamau oti ubatizo tsopano timaganiza kuti ndi mau chipembedzo nthawiimeneyo. Pamene anthu amachapa nsalu amaika mmadzi ndi zobvalazozimakhala pansi pa madzi ndi kumachapa, ndipo akamatchuka ziwiyaamazikanso pansi pa madzi ndimazitchuka anali mau amene analipo kalendiye ubatizo sanali mau achipembedzo ndiye pamene <strong>Yesu</strong> amati pitaniakhale ophunzira anga ndiye amatiuza momveka bwino pazimene iyeamafuna kuti tidziwe.Pali mafunso ambiri pa maganizo anthu ambiri pankhani imeneyi komamau a <strong>Yesu</strong> ndi oti ndi ofunika tiyenera ngati sichoncho ndiye kutisitili okonzeka kubatizidwa. Timaika manda anthu akufa ndi pamenetimapeleka moyo wathu ndi pamene timauka ndi kuyenda mu moyowatsopano ubatizo ndi chikondwelero chopeleka moyo ndi kulandiramoyo wa <strong>Yesu</strong>.kuikidwa mmanda pamodzi ndi <strong>Yesu</strong> ndipo zinthu izi ndizofunika chifukwa <strong>Yesu</strong> anatero. Angabatizidwe ndi ndani? Ndi funsolabwino. Peturo anati ubatizo ndi kulira kwa munthu olungama mtimakwa Mulungu. Mtima umene amafuna kukhala mwa kulira kwa <strong>Yesu</strong> kwaMulungu kukhulupirira kuti <strong>Yesu</strong> ndi mwana wa Mulungu ndi kufuna kutimachimo awo akhululukidwe ndi kuchotsedwa akhonza kubatizidwa.Munthu amene sakhulupilira <strong>Yesu</strong> salira moyo wake kwa Mulungu ndiposanakhulupirire kuti akufuna kukhala mwa <strong>Yesu</strong> ndi mitima yawo kufikirakuthekera kwawo ndiye kuti Sali okonzeka kuti abatizidwe.Sitingathe kumvetsetsa bwino za ubatizo ndi kusamvetsatso bwinommene tingakhalire mwa <strong>Yesu</strong> koma kuti moyo uyenera ofuna kulondora<strong>Yesu</strong> ndi mmene tingadziwire. Tiyenera kudziwa kuti tinapachikidwapamodzi ndi <strong>Yesu</strong> pamodzi ndi machimo anga ndi kumva kupwetekakuti tinapha mwana wa Mulungu osalakwa. Tiyenera kufuna kunenakuti, pepani, chonde tengani moyowanga Aroma 6 amanena kuti tinafaku machimo athu tinafa naye pamodzi ndi <strong>Yesu</strong> ndi kuyenda mu moyowatsopano. Sitiyenera kukwirira munthu amene ali ndi moyo ndipokuikidwa mmanda ndi kwa anthu akufa. ndi zoona mu mzimu tiyenerakufuna kufa ku machimo athu ngati sichoncho ndiye kuti sitili okonzekakubatizidwa. Timaika mmanda anthu akufa ndi pamene timapeleka moyowathu ndi pamene timauka ndi kuyenda mu moyo watsopano ubatizo ndichikondwelero chopeleka moyo ndi kulandira moyo wa <strong>Yesu</strong>.Monga mwa zonse zochitika muchikristo ndi nkhani ya mtima osatizochitika kunja kwa thupi. Tikuthandauza kuti zofunika kwenikwenitiyenera kuti tikonde <strong>Yesu</strong> mwana wa Mulungu ndi kupeleka moyowathu kwa iye. Koposa mau amene amanenedwa a zaubatizo <strong>Yesu</strong>akufuna kutipatsa ife mzimu woyera ndi kukhululukidwa machimoathu. <strong>Yesu</strong> akufuna kuti tibatizidwe ndi mzimu umodzi kulowa muthupi limodzi akufuna kuti tikhale mu mbali ta Atate, mbali ya mwanandi mbali ya mzimu woyera. Kodi nanga tikhathe kunena zotero mongamwa chizolowezi kuti iye akwaniritse malonjezano ake?Yankho ndi loti simau amene timalankhura ndi mtima ndi moyo umenetimapeleka kwa Mulungu umene uli ofunika. Ngati tingadziwe ndikukhulupirira ndi mtima wathu kuti <strong>Yesu</strong> ndi mwana wa Mulungu ndi kuti<strong>Yesu</strong> anafa ndi kuti machimo athu okhululukidwa ndi kudziwa kuti tiyenerakukhala mwa <strong>Yesu</strong> osati mwa ife tokha ndiye timumvere ndi kupeleka miyoyoyathu kuti tibatizidwe ndiye kuti tili kumwamba ndi ngati kuti mkono wa<strong>Yesu</strong> watsitsidwa kuchokera kumwamba kufikira pa ife pamene tibatizidwa.Ubatizo ndi ofunika kwambiri pali ndi malonjezo ambiri amene ananenedwaokhunzana ndi ubatizo. Satana amatsutsa ubatizo amadana nawo.176 177


Tinaona izi India mwa chitsanzo, munthu anganene kuti ndikhonzakukhala mkristu ndipo anzake tikunena “chabwino” “chabwino” munthuoyamba anganene tifuna kubatizidwa ndipo mpaka wina amaotchanyumba yake satana amadana ndi ubatizo zili zonse zimene satanaamadana nazo, ine timazikonda.Ubatizo ndi malo amene Mulungu amakumana ndi munthu ndi lamoopatulika. Sichinthu chimene umangochichita. Sizingakhala ndi kukhalandi okhulupilira ena ndi zazikulu kuposa pamenepa. Mulungu ali muubatizo mu kupambana koposa ndi chifukwa chake <strong>Yesu</strong> ananena mamau ake omaliza ndi chifukwanso Peturo ananena kuyamba ku mpingoyoyamba uja “Mulungu waika <strong>Yesu</strong>, uwu amene munamupha. KukhalaAmbuye ndi <strong>Kristo</strong> chifukwa anali odulidwa mtima ananena kuti inde.Tidzachita chiani amuna inu abale? Peturo mwa Mzimu Woyera adatikuti, lowani mpingo Ai. Peturo mwa mzimu woyera anati lapani chotsanimachimo anu ndipo ena onse ainu lowani mmadzi ndipo mudzalandiramphamvu ya Mzimu Woyera ndi kukjulukidwa kwa machimo anu,angakhale kuti machimo anu ndi ofiira adzayeletsedwa monga matalalandipo mudzalandira Mzimu Woyera kukhala mkati mwa inu ndi lonjezoili lili kwa inu ndi ana anu ndi kwa iwo amene ali kuti kw aiwo ameneaitana padzina la Ambuye. Izi ndi zofunika ndithu ngati munthu wapelekamoyo wake kwa <strong>Yesu</strong> amamva chisoni ndi machimo ake ndipo amadziwakuti <strong>Yesu</strong> amakhulukira machimo ndi kufuna kuti akhale mukuzindikira<strong>Yesu</strong> ndiye mafuna kubatizidwa.Mu Machitidwe 8. Filipo anakumana ndi munthu pa njira ndipo analiwaudindo wake ku Ethiopia anali wa nzeru ndi ophunzira ndithu. Analikuwelenga mau a bukhu la Yesaya, Filipo anadza kwa iye nati, Kodimukudziwa zimene muli kuwelenga? Anali kuwelenga za Mpulumutsi ndiMessiah, <strong>Yesu</strong> ndipo munthuyo anati ndidzadziwa bwanji ngati pali winaondiuza? Ndipo Filipo anadza namuuza zonse za uthenga odabwitsa waMpulumutsi anamuuza za bwenzi lathu, ndinso Mfumu <strong>Yesu</strong>. Anamuuzaza <strong>Yesu</strong> amene anali kuyenda panyanja. za <strong>Yesu</strong> amene anali kuimitsanamodwe kukhala bata. Anamuuza za <strong>Yesu</strong> amene anali kuukitsa akufandi kuwonetsa akhungu kuwona. Anamuuza za <strong>Yesu</strong> amene amatengamiyoyo yosweka ndi kuyeletsanso. Ndipo pamene munthu uyu yochokeraku Ethiopia anamva mau amenewa za odabwitsa <strong>Yesu</strong>, anati siawa madzi.Batizani ine tsopano anadziwa kuti chiphunzitso cha <strong>Yesu</strong> ndi ubatizounali olumikizidwa ndipo sanafune kuti adikire kwa kamhpindi. “Siawamadzi” chonde letsa ine ndi chiani? Anatero. Ndipo anapita kumenekunali madzi Filipo anamuuza iye kwa <strong>Yesu</strong> ndipo anabvuuka mmadzi alindi chimwemwe koma kufuna kwa mtima wake unali kulumikizidwa ndi<strong>Yesu</strong> mu ubatizo.Panalinso usunga ndende ku mzinda otchedwa Filipo kumena abale athuena anatsekeredwa kunali chibvomelezi ndipo abale athuwa amasulidwandi mphamvu ya Mulungu. Wandende anaona kuti makomo anali otsegukandipo anafuna kuzipha yekha. Abalewa anamuuza kuti apulumutsidweangakhale kuti kunali pakati pa usiku, anafuna kuti abatizidwe nthawiyomweyo panali pakati pa usiku. Sikunali kotheka sikunali kophwekakoma mtima wake unafunitsitsa <strong>Yesu</strong> kuti ayenera kubatizidwa kumizidwangati tili ndi maganizo a Mulungu pa ubatizo tikhala okondwa pa zimenezimonga mmene munthu wa ku Ethiopia wosunga ndende wa ku Filipo ndizikwi zitali (3,000) za anthu aku Yerusalem, tsiku limodzi anali okondwandi ubatizo.Tsopano pali kusiyana kotani ubatizo wa Yohane ndi ubatizo wa <strong>Yesu</strong>?Ubatizo wa Yohane unali okhulukira machimo (Mari) ndipo ubatizo wa<strong>Yesu</strong> unalinso wokhulukira uchimo (Machitidwe 2) patapita nthawi mubukhu la Machitidwe a Paulo anakumana ndi anthu amene amafunika kutiabatizidwanso, chifukwa analandira uthenga wa ubatizo wa Yohane ndipoamafunika ubatizo wa <strong>Yesu</strong>. Choncho amafunika ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndiye kutiubatizo sikungonyowa konkha ai. Anthu awa ndi ubatizo wa Yohane analiachite ntchito yabwino ndi asachimwenso. Ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndikubweramu mzimu woyera wa <strong>Yesu</strong> ndi kukhala pamodzi ndi <strong>Yesu</strong> wa ku Nazarene.Ubatizo wa Yohane unali wa ntchito, ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndi wa chikhulupiriro mumwazi wa Mpulumutsi. Ubatizo wa Yohane unali kulonjeza za kwa Mulungundi kumvera Mulungu ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndi kulira kuti tidzaziwe <strong>Yesu</strong>, ubatizowa Yohane unali kuchita chilungamo, ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndi chikhulupiriromwa <strong>Yesu</strong> kutenga machimo athu ndikusinthana ndi chilungamo ndikuchitachinthu chabwino kwa <strong>Yesu</strong> osati ntchito zimene tigwira zathu.178 179


Atate akonde mwana wa Mulungu amene anachita pangano ndi Atatendi kumvera iye mu zilizonse ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndi kulira kwithu kw aMulungu kuti atibise ife kwa <strong>Yesu</strong>. Ichi ndi pangano lomwe Atate anachitandi mwana linakhala pangano lathu. Osati ndi ntchito zabwino, komachifukwa cha <strong>Yesu</strong>, uwu ndiwo uthenga wabwino, chifuwa ntchito yathuyabwino sizingathe kukondweletsa atate. Koma atate amakonda mwanandi iye, atate amakondwera mwa iye ndiye pamene okhulupirira abisalamwa ubatizo wa <strong>Yesu</strong>, chifukwa Atate akonda mwana motero akondweramwa iye uwu ndiwo ubatizo wa <strong>Yesu</strong>. Umene Atate anapeleka Mzimuwa mwana wake ndi kubveka ife mwana amene akondedwa uwu ndiwouthenga wabwino.Pali anthu amene abwera kwa ife kuti akhale mbali ya mpingo mwanisanabvikidwe mwina sanabvikidwe mwa <strong>Kristo</strong>, mwina amakhulupirira<strong>Yesu</strong> ndi mwana wa Mulungu ndi kuti ndinapeleka monga wanga kwa iye.Koma sanabatizidwe pali njira ziwiri zimene zingatsalidwe njira ina ndi yakunja kwa thupi monga mwa lamulo ndiye kunena kuti sitingayende kuti,“tikufuna iwe ukonde <strong>Yesu</strong>, ndi kuti upeleke moyo wako kwa iye ndipoubatizo ndiyo funika kw a<strong>Yesu</strong>. Pepani, nganizirani ndi kupemphera pazinthu izi. awa ndiyo chiphunzitso chochekera kwa Paulo, Petulo, Yohanendi kwa <strong>Yesu</strong>.Baibulo limati mu <strong>Kristo</strong> ndi amafuna mkaka wa uzimu wa mau a Mulungumonga mmene ana ang’ono khanda amafunira mkaka ndiye tinganenekuti sitingayende ndi iwe mpaka utabatizidwa? Kapena kuti tiyambekuwapanga mau a Mulungu kuti tione ngati akukonda chakudyachokapena ai izi zimatenga nthawi koma ngati akonda chakudyacho chimenesanamvepo ndikale lomwe. Ndiye kuti adzabatizidwa ngati sakonda maua Mulungu sizithandauza kanthu ngati abatizidwa. Sitingayende ndi winaaliyense amene sakonda mau a Mulungu ndipo chonyezera ndi osatisakubatizidwa koma ngati akukonda mau a Mulungu.Mu malembo woyera, ubatizo ndi chofunika ndithu kwa Mulungu ndikwa wina aliyense amene adziwa Mulungu monga kwa munthu wakuEthiopia pamene anamva ubatizo anafuna kuti nthawi yomweyo mongaanthu 3000 okhulupirira mu Machitidwe 2 mmene anamvera za ubatizoanachita ntahwi yomweyo wa ndende waku Filipo anachita nthawiyomweyo angakhale kunali pakati pa usiku sizinamukhudze kuti inalinthawi yanji? Zinali choncho bwanji? Zinali chonchi chifukwa onse analiokonda Mulungu pamene mukonda amuna anu kapena akazi anu ndikukufunsani zina zake zimene akufuna kuti muwapatse ngati mukonda<strong>Yesu</strong> ndiye kuti ubatizo ndi chinthu chopambana kwa iye ndiye kutimudzakonda kubatizidwa chifukwa <strong>Yesu</strong> amakonda ubatizo.Zimatenga ntahwi kuti mau a Mulungu afikire anthu koma tikhala tonsepamodzi ndi kulankhura zimatengera kuti ndi ubatizo ngati sadziwaubatizo tidzakhala nawo kwa nthawi yochepa chifukwa ngati akonda maundi Mulungu adzakula ndipo adzabatizidwa.Timakula mu zinthu zambiri sinchoncho? Kuyesa kwithu sikwazinthuzimene timadzidziwa kuyesedwa ndi kwa zinthu zimene zidzasinthidwetimakhala mmalo osiyana siyana kuyesedwa kwathu ndi ngati timakondamau a Mulungu ndikuti tili kufuna kusintha nthawi zina. Kusintha ndikobvuta ndiye tikobvuta pafunika kufatsa ndi kukondana wina ndi mzakengati wina sakonda mau a Mulungu ndiye bvuto ndithu. Koma akondamau a Mulungu koma zili kwa bvuta ndiye kuti tiyenera kwathandiza.Anthu A Mulungu Ndiwo BanjaNgati tiyenda pamodzi ngati banja tsiku ndi tsiku ndiye kuti tidzachitazonse pamodzi ngati mpingo ndi malo ongokumana pa sabata. Mmawa tilindi bvuto chifukwa tidzaona kuti amene Sali membara wathu kapena ai.Koma ngati ndi banja tsiku ndi tsiku, koma wina sakonda mau a Mulungundiye kuti adzadziwika. Tidzadziwa pakukhala kwithu kwa tsiku ndi tsikukuti ali kukonda mau a Mulungu.Ngati munthu adzati ndabatizidwa koma sakonda akazi awo kapena amunaawo uko ndiwo kuipa ndithu. Ngati tikhala banja tsiku ndi tsiku tidzadziwangati ali kukonda <strong>Yesu</strong> kapena ai. Ngati tikhala banja tsiku lirilonsetidzakhala ndi nthawi yolankhula za ubatizo. Sidzakhala uthenga wa ubatizo,udzakhala abwenzi kulankhura za ubatizo mwana wina sangathe kulankhurabwino za ubatizo asabweletsa wina amene angalankhule bwino za ubatizo.Pali mphatso zosiyana – siyana mu thupi la <strong>Kristo</strong> ndiye ena angalankhurebwino koposa ena. Pamene tikhala monga banja tingakwaniritse zinthuizi pamodzi tsiku lililonse. Zimasintha zinthu kukhala banja kusiyana ndikuonelera chipembedzo chifukwa takhala ndi nthawi yosintha zinthu ndi180 181


kudziwana wina ndi mzake. Pamene mubwera ku nyumba ya mapempherondiye kuti thandauzo la mpingo lili painu. Ndiye kuti tidzakhulupilirazinthu zonse panthawi yake kuti tonse tikhalepo.Koma ngati ife ndife banja tili ndi nthawi yokambilana za kusiyanakwithu. Chifukwa timakondana osati ndi uthenga koma kulankhulanamonga banja izi zimapangitsa chisangalalo ndi ufulu. Izi ndi zimeneBaibulo limati mpingo ndiyo maziko a choonadi ndi, chifukwa pamodzimonga banja tikhonza kupeza maganizo a Mulungu. Pamene mphatsozikukhalira pamodzi ndikugawana moyo wathu pamodzi. Mulunguwathu adzatithandiza kudziwa maganizo ake ku zinthu zosiyana mu derala choonadi.Tonse Timapeza MayankhoIzi ndi zabwino chifukwa palibe wa ife amene ali ndi maganizo abwino.Ambiri amasiyana ophunzira bwino za mbali ina ambiri Sali ku mbali yampingo wa moyo. Amapita ku mpingo la Mulungu mmawa basi zatherapamenepo. Sakhala ndi nthawi yoti mphatso ina isinthe moyo, ndiye alindi nzeru zochepa ayi akhale ndi malingaliro okhudzana ndi zophunzirazawo. Koma maganizo awo ndi osiyana ndi anzawo ndiye ali okonza ndani?Mulungu akuti maziko a choonadi ndiwo choonadi cha mpingo wa moyo.Tonse tidzapeza mayankho mu Machitidwe 15 ophunzira sanadziwe kutiokhulupirira ayenera kudulidwa kapena ai. Ndiye amabwera pamodzikudzithetsa bvutoli. Mmodzi anati ndili kukumbukira zimene mneneriAmosi analankhura mu malemba woyera. Anali kuchitira zinthu pamodzimonga anthu a Mulungu monganso banja la Mulungu kupeza mayankhokwa Mulungu. Anachita zonse pamodzi kupeza mayankho a Mulungupopanda otchuka okhala ndi maganizo apamwamba koma linali banja laMulungu kugwilira ntchito pamodzi ndiye Yakobo anati. Ndi chabwinokwa ife ndi mzimu woyera kuti iyi ndilo mayankho. Mpingo ndi mizatia choonadi. Tonse tikhoza kupeza mayankho. Sipofunika kukhala wanzeru koposa kuti mukhale kuti Mulungu akugwiritsireni ntchito mu njiraimeneyi.Ubatizo Wa <strong>Yesu</strong> - Lonjezo La TsopanoMonga ubatizo watsopano umene Yohane amaphunzitsa Machitidwe 2.limanena kuti ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndi kukhulukiranso machimo kusiyana kwaubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndi wa Yohane ndiye kuti ubatizo wa <strong>Yesu</strong> ndi ubatizoupita ku mzimu woyera ndi kuitanira kwa Messiah.Yohane ali kubatiza <strong>Yesu</strong> asnapachikidwe pa mtanda mwazi wa <strong>Yesu</strong>usanakhetsedwe ndiye kuti Yohane anali mu chipangano chakale analikuchita monga mwa lamulo la Alevi. Pamene anali kubatiza unali mwaziwa ng’ombe ndi mbuzi zimene zinali kukhululukira machimo ubatizowa Yohane unatha pamene <strong>Yesu</strong> anafa pa mtanda. Yohane anadulidwatuAmbuye <strong>Yesu</strong> asanafe pa mtanda koma pano pamene <strong>Yesu</strong> ali ndi moyo alikubatizidwa ife ndi lonjezo latsopano.Peturo anatero mu Machitidwe 2 kuti pangago latsopano machimo anthuakhululukidwa mu ubatizo, lapani, batizani iwo wina aliyense ndipomachimo anu adzakhululukidwa ndiye mbali yopeleka moyo wathukwa <strong>Yesu</strong> imakhudzana ndi kukhulukidwa kwa machimo athu. Komapali chinthu china chimene Yohane sanakatha kutipatsa ife chimene<strong>Yesu</strong> anatipatsa. <strong>Yesu</strong> amatibatizanso ife ndi Mzimu woyera “ndipomudzalandira mphatso ya mzimu woyera” mu Machitidwe 19, amunaanali kubatizidwanso kachiwiri. Paulo amawafunsa iwo ngati analandiramzimu woyera ndiye anati sitidziwa ngati mzimu woyera unapelekedwandipo ndi chiani? Izi ndi zimene zinapangitse kuti Paulo awabatizidwenso.Paulo anati simungabatizidwe ndi ubatizo wa <strong>Yesu</strong> osalandira mzimuwoyera muyenera kukhala ndi ubatizo olakwika. Ngati mwabatizidwandi ubatizo wa umaphatikizanso ndi kulandira mzimu woyera. Yohaneanali kubatiza ndi madzi koma <strong>Yesu</strong> adzakubatizani ndi mzimu woyera ilindilo lonjezo la mphamvu.Kodi ana anga adzalangidwa ndi machimo anga?Mzimu wa Mulungu unati mu Ezekeli 18 kuti Mulungu amationa ifepayenkha ndiye kuti moyo umene umachimwa ndiyo payenkha ndiye kutimoyo umene umachimwa ndiyo udzafa. Mulungu adzaweluza munthu zinandi zoti tili ndi temberero lochokera kwa Adamu adzaweluza nyumbayo.Uku ndiye thandauzo la malembawa mu Ezekeli 18 Mulungu akuchtsa182 183


ulemelero wake ndiye pali mtengo waukulu wopelekedwa ku nyumbayako kumachimo ako. Ana ako sadzamvera iwe ndi kukonda iwe palikulanga pa nyumba yotere koma Ezekeli ananena kuti chilango chimenemunthu amapita nacho gehena ndi la ali yense payekha payenkha.Pali kuweluza kwa Mulungu chifukwa cha machimo anga ameneangapangitse kuti ana anga akhale osasangalatsa. Pali tembelero la dzikolonse lapansi chifukwa cha machimo la Adamu ndi Eva. Mayi ali ndi ululupakubereka kwawo tsopano, amuna ayenera kugwira ntchito yolemetsa kutiapeze chakudya ndi kugwira ntchito yolimba. Thaka imabereka minga ndiudzu, madzi a mu mtsinje amatipatsa ife matenda. Pali matemberero ambirichifukwa cha kuchimwa kw aAdamu. Ngati ndili wakumva, padzakhalakuweluza pa banja ana anga adzakhala osakondwa chifukwa cha machimoanga umene udzapangitse kuti akhale osasangalala ndiye kuti pali kulangaana anga adzapita ku chionongeko ndi machimo anga sadzapita ku jehenachifukwa cha machimo anga. <strong>Yesu</strong> ananena kuti pali mitundu ya nthakazinayi. Ngati mwana wanga akonda Mulungu ndi mau ake ndi kumumveraiye. Adzapulumuka Ezekeli amanena bwino ndithu.Ana Ndi UbatizoPali nthawi pa nthawi ya umwana pamene amakhala ndi chisankho mumtima wawo kuwulira chifukwa cha uchimo wa Adamu ndiye pamaonekakuti ana ali ndi makhalidwe amene Sali abwino koma osati kuti Machitidweotere adzapititsa ku jehena ai. <strong>Yesu</strong> anati mpaka mutakhala ngati mwanawang’ono sumungathe kulowa mu ufumu wa kumwamba.Nthawi zina pamene amaloza ana ananena kuti “ufumu wa Mulunguuli otere” ana awa sanabatizidwe. Anthu amene amabatizidwaamene amanena za machimo awo. Panalibe mbiri yonena kuti ana alikubatizidwa. Analipo ana ambiri koma palibe zonena kuti ana analikubatizidwa. Ndingathe kudziwa chifukwa chimene ana amafunakuti abatizidwe koma mau woyera amanena kuti ndi okhawo ameneakhulupirira kuti <strong>Yesu</strong> ndi mwana wa Mulungu. Amene moyo wawowapelekedwa kwa <strong>Yesu</strong> ayenera kubatizidwa. Chifukwa choti <strong>Yesu</strong> anatiufumu uli monga ana awa ndiye tiyenera kukhulupilira kuti Mulunguadzateteza ana ang’ono. Analipo ana angono nthawi ya <strong>Yesu</strong> koma palibembiri yoti anabatizidwa. Choncho <strong>Yesu</strong> amateteza moyo wa ana ang’onondipo akakula amaganiza zoukira <strong>Yesu</strong> kapena kupeleka moyo yawo kwaiye. Ndiye chisankho chiyenera kuchitika.Chikhulupiriro cha Ayuda unali mthunzi wa chikhulupiriro cha Akristu(Ahebri 10) mu chikhulupiriro cha chiyuda padzabwera tsiku limenelimatchedwa Bar Mitzuah ndi tsiku limene munthu amakhala mnyamata.Ayuda amaphunzitsa kuti anali akapolo mu nyumba ta Atate awo mpakaatafika Bar Mitzuah pakapita Bar Mitzuah pamakhala chisankho ngatiadzakhala mwa <strong>Yesu</strong> kapena mwa ine ndekha. Ana a zaka zisanu sangathekusankha. Mwana wang’ono sangathe kuti akhale mwa <strong>Yesu</strong> kapena mwaiwo wokha koma kwa ana a zaka khumi ndi khumi ndi ziwiri akhonzakusankha kukhala pa okha kapena mwa <strong>Yesu</strong> koma osati wa zisanuchifukwa saziwa kuti <strong>Yesu</strong> ndi ndani.Mu Machitidwe 2 limati kuti mubatizidwe muyenera kuti mulapemuyenera kuti mulape kuti mubatizidwe. Simungabatizidwe ngatisimungalape ndikuganiza nthawi zambiri ndi zobvuta kwa mwana wa zaka5 (ZISANU) kuti adziwe kuti chimo ndi chiani. Mukawauza kuti anaphamwana wa Mulungu kodi adzadziwa? Sitikudziwa ngati adzadziwa?Ndi munthu yekhayo amene angadziwe kuti anapha <strong>Yesu</strong> ndi machimondiye angathe kubatizidwa. <strong>Yesu</strong> anati ana ali ndi Angelo amene amaimapa kupezeka kwa Mulungu <strong>Yesu</strong> mwini ndi amene analankhura ndikuphunzitsa za izi. ndiye tiyenera kumukhulupira iye za ana athu mpakaatafika mu kukhala ndi chisankho184 185


Kuyembekeza Pa AmbuyeM’moyo AthuSeptember 1996, Mlowe, Africa.(Zogawana pa nthawi yochepa pamodzi ndi abale aku Malawi)Pamodzi!Tiyeni tilindire tiyamike zina lake tonse pamodzi!Anandimva ine nandimasula ku mphamvu ya mantha!Tiyeni tiyamike zina lake tonse pamodzi kunthawi zosathaNonse yimbani zomuyamika ndi kumkwezeka iye.Mnyimbo iyi ikuchokera pa Masalimo 34. Mawu onse “pamodzi”akuyimila pakatikati ka nyimboyi. “Tiyeni tiyamike dzina lake tonsepamodzi kunthawi zonka muyaya” Tilinazo zinthu zapadera dela mnyimboyomweyi yoyamika Yehovah, kunena za Ambuye pa kumva kulira kwathummapemphelo, komanso ndi Angelo ake potisamalila ife kuchokerakuzoyipa zonse ndi mantha, komanso Ambuye pokwanilitsa zokhumbazathu ndi kutipatsa ife chakudya cha tsiku ndi tsiku kuchoka ku nthakayolengedwa ndi manja ake Yehova.Zonse tikuonazi nzapadera dala zoyikaka ndi Yehova chonse Ambuyeanapeleka kw aife kuti tipindule nazo. Mwa Ambuye wathu. Ichi ndiyechofunika pa zonse.Moyo unasanduka kuunika kwa anthuNdi ganizo loyikika kwa aliyense kuti tiyenera kuyembekezera pa Ambuyekudziwa kukhala mmsinkhano ya oyela mtima a Mulungu. Ndikufunafunankhope ya Ambuye ndi kudziwa cholinga chaka. Ichi ndiye cholinga chake.Komabe ndikukhulupirila kuti nthawi zambiri ife sitiyembekezela paAmbuye pa zimene timafuna kuchita mmisonkhano yathu; Mmalo mwake187


timamdalira Ambuye pa zokhazokha timafuna kuna kuti achite miyoyoyathu. Zinthu zambiri zimene zaphunzitsidwa kuti oyela akakhala pamodzinkubwela ku nthawi za nthawi. Ndipo oyelawo amayenda pamodzi ndikulingalila pamodzi. Pakakhala palibe kuyendeledwa ndi Yehova.Ndipo oyela pamodzi tiyenda pachimene chachitika mnthawiyo tonsepamodzi. Pamene Ambuye apanga ubale wathu tonse pamodzi mwakuya.Iye amabweretsa ziphunzitso zake kuchokera kumwamba. Nthawi zinaamaphunzitsa kupyolera mzopweteka ndi mukulephera kwa moyo uno.Nthawi zinanzo zimabwela mukupyolera mu chigonjetso, nthawi zinansomzodabwitsa zake zimene amazigwiritsa ntchito potidabwitsa ife.Komanso zinthu zonsezi zimachitika pa moyo wathu wa tsiku ndi tsiku.Pamene ife tiyembekezera pa Ambuye mmoyo wa tsiku ndi tsiku tonsepamodzi mwa Ambuye.Timalankhulana wina ndi nzake mmoyo uno wa tsiku ndi tsikuzokhuzana ndi <strong>Yesu</strong> mmoyo uno. Komanso ndikuthandizana mavutoathu pamodzi ndikuphunzira za iye nthawi zonse. Timagwilizana manjawina ndi nzake tikafooka. Chifukwa chake miyoyo yathu ngokonzekakomanso kuyembekeza pa Ambuye wathu. Zitha kuchitika kuti onseoyera akhala pamodzi, wina ayenera kuti ndiri ndi vuto, pamene winaavulala mapezanso chisangalalo cha Ambuye mkupilira kwache. Pameneoyela mtima akhala pamodzi pamenepo mlongo kapena mbale angathekulankhula ndi kugawana chimene aphunzira ndi anzao. Mungathe kuonakuti chiphunzitsochi sichikusimikizira pa kulindira pakha ayi ndi kufunsilachochita; ngakhale zotelezi zikhoza kuchitika koma zichokera kwa Ambuyepakuyembekezera pa iye. M’ubale wathu wa tsiku ndi tsiku, pakulemekezaMulungu ndi zinthu zochepa mu miyoyo yathu, ndi kukwezana wina ndinzake manja athu pothandizana wina ndi mzache. Kupyolera mmoyo watsiku ndi tsiku chiphunzitso mmawa uno pamene ndi kuyendabe mmbalimwanjira ndi m’bale kapena mlongo, pamene tikuseka or kulira pamodzikapena zinthu zotelezi zimabwera pakulingalira kwathu.Ndi Chimodzimodzi LeroM’bukhu la Yohane 1. Linena za <strong>Yesu</strong> kuti moyo unasanduka kuwala kwapa anthu ena kuona kuchokera m’moyo otisogolera. Ndi chimodzimodzilero. Pamene tikhala miyoyo yathu mwa <strong>Yesu</strong> ndi kuthandizana mnjirayoyenera kwa wina ndi nzake ndi mtima wathu onse. Koma makamakatiyembekezerabe pa Ambuye ndi moyo wathu onse. Kusonkhana kwathukumakhala chiyanjano cha wina aliyense pokondana wina ndi nzake.Kuphunzitsa kozama mmiyoyo yathu ndipo tayenera kukhala okhuzidwandi zotelozi. Mwa kukhala nacho chifundo. Pamenepo ndipamene tikhozakusawana tonse pamodzi.Zinthu izi nzofunikira kwambiri kugawana tonse. Pamodzi chifukwaambiri a ife tiri ndi maganizo oti chiyanjano ndiye potheka pa zonsemmoyo wathu onse wa chikhristu. Kodi <strong>Yesu</strong> anali ndi chiyanjano ndiophunzira ake sabata lili lonse? Osati lachiwiri lina lililonse usikuku?Ndi la Mulungu mmawa lina lilonse mmawa mawa sana chite chonchi.Mpaka na lero sachitabe. Ndi chimodzi modzi lero mpaka na kalekale.Amaphunzitsa ife pamene tidzuka natenga step oamene tiyenda komansopamene tilingalila. Kusonkhana kumakhala pamene banja lili lonsepamodzi kuimilira, kukhala pansi ndi kuyenda pa njira. PAMODZI moyounakhala kuwala kwa dziko lapansi ndi chifukwa chake pali kufunika kutitione wina ndi nzake ndi kukondana kunja kwa “misonkhano” Timatayanthawi pa moyo owonana wina ndi nzake mu 1 Akorinto 11, mtumwiPaulo anati ngati sitingakondane ndi kunyamulana mapewa wofookatsiku ndi tsiku ndiye kuti misonkhano imakhala wophana osati yabwino.Tiyeni tisankhe tokha mu miyoyo yathu osati mu msonkhano kapenachiphunzitso, ikhale kuunika kwa anthu.Tifunse Atate PamodziNdinu atate okondeka, choonde lolani kuti timve ku zinthuzimene zili zoona osati zimene Satana amabweletsa ku makutuathu ndi mitima yathu. Satana ndiye tate wa mabodza ndipoamafuna kuti adzinamabe kwa ife kutiuza zonama. Tikudziwakuti mdani wathu ndi onama ndiponso ndi wakupha amafunanjira yotiphera ife koma timadziwa kuti mumatikonda ndipomukufuna kutipatsa zinthu zabwino kuti zitimasule ife ku nsinga.Tikufunsani Inu Atate kuti mutipatse maso amene angathe kuonazonama. Tikudziwa kuti tidzakwanitsa chifukwa muli kumbaliyathu. Zikomo chifukwa cha lonjezoli zikomo chifukwa cha188 189


chiyembekezo sichidzakhumudwitsa ife. Timakhulupilira inundipo simudzatichititsa manyazi sitidzafa ndi mphamvu ya <strong>Yesu</strong>ndi mfumu wosatha mumafuna kuti mvula igwe ndi kuti nthakaibale zokolora. Mumafuna kuti mitambo ibweletse dangalirapamene dzuwa liwomba mumafunanso kuti mitsinje iyendebwino kutinso ilimbe ndikupangitsa ife kudwala mumakonzansokuti ana athu onse akule bwino ndi kukalamba ndi kuti za manjaahu zikhale zopambana kapena zolephera mumakonzanso ngatizolankhula zathu zibweletse chimwemwe kapena kukwiyitsa ena.Mumakonzanso kuti mukhale Mtendere kapena mphamvu mumtima wanga kapena zokwiya kapenanso zolephera. Ndinu nokhaamene mumakhululuka machimo anga ndi kutibweletsa kunjirayabwino uthenga wabwino ndi oti mumatikonda kwambiripamene muli mfumu yamuyaya ndi zonse zili pansi pa ulamulirowanu ndi uthenga wabwino kwa ife kuti ndinu odzadza ndichifundo ndi kukoma mtima. Mfumu ya muyaya. Inde komansobwenzi lokongolqa ndi lokondeka. Zikomo chifukwa chokhalabwenzi lathu. Mudzatitengera ife ku mbali ina ya chigonjetso….Dzina lanu likule.Mzimu Wotengeka TengekaSeptember 1996, Mzuzu, Africa.Malingaliro amene m’bale adagawana ndi oyera mtima mmawa wa tsiku linapamene tidali pamodzi ku Africa.Nditangotsegula maso anga mmawa walero. Ine ndidatsegula Baibulolanganso. Ndime yoyamba imene maso anga adaona idali ndi mauokhudzana ndi mnthunzi wa imfa, chimodzimodzi monga Masalimo23:1 sindikadaganiza kuti ndionetsera ichi kwa inu, kupatula poti enamwamau amenewo adali ofanana, ndipo mau oyambirira eni eniwo masoanga adaona mmawa uno adandibweretsera chikondwerero.Kukhala Pamene Mthunzi Siungatikhudze ife“Ngakhalebe, sipadzakhalanso zowona kwa iwo amene akhala alim’mavuto.”Mulungu adzachotsa zonse za zowawa ndi mavuto athu. Iye adzatsukachikayiko chathu. Ili ndilo lonjezano lake. “Anthu akuyenda mumdimaawona kuwala kwakukulu. Pa iwo akukhala mudziko la chigwa chanthunziwa infa, kuunika kwakukulu kwaoneka.” (Yesaya 9:1-2).Ndime iyi imapitirira kuyankhula za m’mene Mulungu adzakulitsiremitima yathu. Iye adzachulukitsa chimwemwe chathu. Iye adzatipangaife kuti tisangalare ngati anthu akusangalalira zokolola. Iye adzatutazothodwa zimene zili pa ife. Iye adzachotsa chitonzo zhakugonjetsedwakwathu. Ndipo apa pali m’mene iye adzapangire, “pakuti kwa ife Mwanawamwamuna wapatsidwa, ndipo ulamuliro uzakhala pa phewa pache, ndipoadzamucha dzina lace wodabwitsa, wauphungu, Mulungu wamphamvu,Atate wosatha, kalonga wa Mtendere.” (Yesaya 9:6-7)Ulamuliro wace ndi za Mtendere sizidzatha. Pa mpandowacifumu waDavide, ndi pa ufumu wace, kuukhazikitsa, ndi kuucirikiriza ndi ciweluzondi cilungzmo kuyambira tsopano ndi ka nthawi zonse. Changu chaYehova wa makamu cidzacita zimenezi.190 191


Dzina lake ndi <strong>Yesu</strong>: Immanueli, Mulungu ali nafe. <strong>Yesu</strong> adzabweretsachimwemwe chachikulu. Iye adzatsuka zowawa ndipo kuunika kudzafikam’mitima mwathu. Mtima ndi malingaliro ndi mphamvu za Mulunguwamphamvu. Zonse adzakwaniritsa ichi. Anthu akuyenda mumdima(amenewo ndi fe) adzaona kuunika kwakukulu. Mlangizi wodabwitsa iyeadzatithandiza ife mumayesero athu onse. Pamene tiyenda muchigwa chamthunzi wa imfa, ife timvetsetsa kuti mthunzi siungatipweteke ife. Ndimthunzi wa imfa chabe. Kodi mukudziwa chimene chimathamangitsamthunzi? Kuunika kwakukulu kudzathamangitsa mthunzi uliwonse.<strong>Yesu</strong>, M’busa wathu wabwino, adzathamangitsa mithunzi yonse yaimfa m’miyoyo yathu. Nthawi zina ife timayesayesa kufufuza yankhokuchoka mmitu yathu, pamene chimene tikufunika kwenikweni kuti ifetipange ndi kutembenuza nkhope zathu kwa <strong>Yesu</strong>. Iye adzatimva kulirakwa mitima yathu ndipo adzaonjeza chimwemwe chathu, kubweretsakuunika kwakukulu ku mitima yathu. Kwa ifde mwana watibadwira,mwana wapatsidwa ndi adzatithandiza ife ngati titembenuzira nkhopezathu kwa iye.“Nchachikulu bwanji chikondi cha Atate chimene chidagwera pa ife, kuti ifetitchedwe ana a Mulungu, pakuti ichi ndicho chimene tili! Ife tikhonza opandanthumazi ndipo opanda manyazi pamaso pake pa kubwera kwake.” (1 Yohane3:1,2:28) mu chiyankhulo cha chi Greek, chimanena kuti “Taonani ichindipo dabwani zachikondi chodabwitsa chimene Mulungu ali nacho paife. ichi ndi chionetsero cha “kutsegula maso athu ndi kuona mmene ukuluwa chikondi chake ulili.Pali nyimbo yina imene nthawi zina timayimba. Imayankhula za mmenetiliri oposa agonjetsi.Ife tili anthu a Mulungu, otchedwa ndi dzina lake.Oyitanidwa kuchokera kumdima ndiomasulidwa kuchoka kumnyozoFuko limodzi loyera – oyera mtima aliyense.Chifukwa cha Mwazi wa Khristu, <strong>Yesu</strong> MwanaNdi milomo yathu tiyeni tiyimbe kuvomereza kumodzi.Ndi mitima yathu tigwire choonadi chimodzi chokha.Pakuti iye wafafaniza machimo athuWatilanda ife ndipo watitcha ife ake.Ake omwe enieni.Timveni ife, mizimu ya kumidimaTsono inu mudzadzidwa pamene tiyimaIfe tili anthu ake, ogulidwa ndi zipyeraOgulira ndi mwazi wa mwana wa Nkosa.Mwaza wa Mwana wa NkhosaIchi ndi chifukwa chake pali chiyembekezo chachikulu pa tonse a ife. Ichindi chifukwa satana adzalephera, ndipo ichi ndichifukwa chake tili oposaagonjetsi: ife tidagulidwa ndi mwazi wa Mwana wa Nkhosa! Tsono ndimitima yathu tiyimbe chivomerezo chimodzi. Ife tigwiritse ku choonadichimodzi chokha. Chifukwa <strong>Yesu</strong> wathu wagonjetsa tchimo ndipowagonjetsa imfa, satana ali ngati galu opanda mano. <strong>Yesu</strong> watikonda ifendipo watipanga ife Ake, Ake enieni.Ntahwi zina tiyenera kudzikumbutsa tokha za choonadi ichi. Ndi chovutakukhala ndi tsiku pamene ife tikumbuka zinthu izi. ife tili opsa agonjetsikudzera mwa mwana wa chikondi cha Atate.Kutengeka ndi ZochitikaPali njira yomutsatira <strong>Yesu</strong> imene ili yokhazikika pa momvedwe a matupiathu. Pamene mamvekedwe a matupi athu ali bwino, ife timamkonda<strong>Yesu</strong>, ife timasangalala, ndipo ife timayimba. Koma pamene ife sitimvabwino, ife sitiyimba nyimbo ndipo sitimpembedza iye. Ine ndikuganizakuti anthu ambiri apamanga mu ubwino. Iwo amakhala ali ndi cholingachabwino. Koma pali njira yomtsatira <strong>Yesu</strong> imene ili yamphamvukwambiri ndipo imene siyiyelekezera kukhala yauzimu. Palinso njira inaimene ili yosakhudzikika. Ine sindikuthandauza chilichonse choipa. Inendingoganiza kuti nthawi zina ife sitimvetsetsa njira yeniyeni yomtsatira<strong>Yesu</strong>. Njira yeniyeni siyiyendera mmene ife tikumvera matupi mwathu.192 193


Pamene ife tikuyankhula za uzimu oyendera mamvekedwe amthupi, ifesitikutanthauza kuti wina ali ndi malingaliro oyipa kapena zolinga zoyipa.Mwina iwo sadaone nkhope ya <strong>Yesu</strong> munjira yamphamvu imene iwo tsikulina adzayiona.Moyo Wa YobuIfe tawerenga kuti Yobu adali munthu olungama kwambiri pa dziko lonselapansi. Kuchokera mwa anthu mazikwi ndi ngakhale miyanda, Yobuadakonda Mulungu koposa wina aliyense wa anthuwa. Yobu adamveraMulungu koposaonse mwa anthu apadziko lapansi, ndipo komabe padalinjira yokuya imene iye sadamudziwire Mulungube.Padali zinthu zambiri zoipa zimene zidamuchitikira Yobu. Iye adali ndikuwawa mtima kwambiri ndi kuwawa kwambiri. Thanzi lake lidapitiratu.Ana ake apamwamba adafa, Chuma chake chidatengedwa.Mkazi wake adamuuza kuti atukwane Mulungu ndipo afe. Iye adasiyaosapitiriza kumkakamiza kutero. Ndipo tsono mtima wa Yobu udaswekakudzamuyendera iye, ndipo ndikhulupirira iye anthu amenewoamamkondadi Yobu. Iwo adasiya mabanja awo ndipo adakhala ndiYobu kwamasiku asanu ndi awiri mu chete watunthu. Ndikhulupirirakuti iwo amamkonda Yobu ndipo iwo amatanthauza ubwino. Komaiwo sadamudziwe Mulungu bwino lomwe. Iwo adanena zodabwitsazambiri, zinthu za uzimu kwa Yobu zokhudza mmene munthu wabwinoamapezera zinthu zabwino nthawi zonse. Yobu adadziwa izi sizidalizoona. Iye adaonapo zoyipa zikuchitika kwa anthu abwino ndipo zabwinozikuchitiks kwa anthu oyipa. Tsono iye sadadzilandire zinthu zimeneanzake amanena kwa iye.Munjira imodzi Yobu adali ndi uzimu oyendera mamvekedwe a thupichifukwa iye sadalore Mulungu kupanga ntchito yakuya mu mtima mwake.Iye adali okondwa kwambiri ndi mmene amamudziwira Mulungu. Iyeadadziyesa yekha munthu wabwino kwambiri. Chifukwa iye adali chifupindi Mulungu kuposa munthu wina aliyense, iye amaganiza kuti ali chifupikwambiri ndi Mulungu. Iye sadazindikire kuti tsamba la udzu liri pafupi ndidzuwa kuposa nyerere. Mtengo uli pafupi ndi dzuwa kuposa tsamba la udzu.Komabe mtengo ulibe kutali kwambiri ndi dzuwa. Mtengo ndi wautalikuposa tsamba la udzu, komabe ukadalibe waung’ono kwambiri. Yobusadamvetsetse phunziro ili. Iye adadziwa kuti iye adali chifupi ndi Mulungumaganizo a mmene iye adaliri kutali ndi Mulungube. Mtima wake sudaliosweka za m’mene iye adaliri kutali ndi Mulungu. Chidatengera kuwawakwakukulu kumeneku ndi kuonongeka kwa zinthu zonse za Yobu, munthuolungama kwambiri pa onse apadziko lapansi, kuti amvetsetse zinthuizi………….. atatha kudutsa mzowawa zimenezi, iye adati. “makutu angaamva za inu, koma tsopano ine ndikhonza kuona chimene inu muli chenicheni.”(Yobu 42:5) Yobu, munjira zina adali wa uzimu oyendera mamvedwe athupi.Yobu amapanga izi muubwino ndipo iye adali munthu wabwino. Iye sadalikunamizira kapena kuyesezera koma iye adali kutali ndi chimene Mulunguali chenicheni.Ngati Yobu adali wa uzimu oyendera mamvekedwe a thupi, ine ndikhonzakunena kuti tonse aife tilinso chincho. Ndi zoona ndi anthu ena ameneamangomizira ukhristu. Iwo amangoyesezera chabe. Iwo amapangankhope zawo zioneke za uzimu. Iwo amafuna kusangalatsa anthuawaone iwo akukonda Mulungu. Koma ife kodi, mukupusa kwithu ndikusatetezedwa kwithu ndi kunyada ndiponso kusakhwima kwithu, nthawizina sitigweramo mu zinthu zonga zimenezi? Ichi ndicho uzimu uyenderamamvekedwe athupi. Koma pali njira yeniyeni yamukondera <strong>Yesu</strong>imene imabwera kuchokera mkudzichepesa kwakukulu, ndipo ilibe nazontchito kapena kusamala ngati wina akuyang’ana kapena ayi. Imachokeramu mtima. Uzimu weniweni umachokera kukusweka mtima pamasopa Mulungu. Imachokera mu kugwa m’chikondi ndi Mulungu ameneamakhululukira machimo athu. Mwina chinthu chenicheni chikhala ndimaonetsera a pankhope nachonso! Koma chimachokera mukuswekamtima osati kuchokera mmkudzionetsera. Njira yabwino yothaniranandi uzimu oyendera mamvekedwe a thupi kuchokera mmitima yathundi kudzichepetsa ife tokha pamaso pa Mulungu ndi kumufunsa iye kutiatiphunzitse ife. Kumufunsa iye kuti sule ife ndi moto, kuti ife tikhonzakulira ngati Yobu, “ngakhale inu mwandilasa ine, ine ndidzakhulupirita inu!”Vuto la uzimu oyendera mamvekedwe a thupi sioti kuti tikungoyesezerakwenikweni, koma kuti ife sitidadziwebe ntchito yakuya imeneMulungu agwira mmitima yathu, monga iye afunira. Ndi chifunika kutiife tisaweruzane wina ndi mnzake, koma koposa kuti ife tithandizane194 195


wina ndi mnzake, koma koposa kuti ife tithandizane wina ndi mnzakekudziwa Mulungu oona. Ife tidziyike tokha pamaso pa Mulungu oonandi kusiya iye atiotche ndi moto wake monga njira yomwe adachitirandi Yobu. Padzakhala tsiku lakukondwa ngati ife tidziyika tokha pamasopa Mulungu ndi kusiya iye awotche ife. Padzabwera tsiku la kukondwandi mphamvu. Ili lidzakhala tsiku lenileni kuchokera mkati mwakuya –osati kuti tisangalatse wina aliyense kapena kuti tidzipanga tokha kumvabwino, koma chifukwa ife taona nkhope ya Mulungu ndi mzimu wathu.Mpingo ndi gulu la anthu amene amayenda dzanja ndi dzanja wina ndimnzake mu chigonjetso ndi muzawawa kuti athandizane wina ndi mnzakekukhala enieni. Ndizoona mtengo uli chifupi ndi dzuwa kuposa tsambala udzu, koma tilibe ndi ntunda waukulu ati tiyende. Mulungu adati kwaYobu, “Kodi udali kuti pamene ine ndinkayika madziko a dziko lapansi?Kodi udali kuti pamene ndinkalamula nyanja m’mene zingapitile muukuluwake? Kodi udali kuti pamene ine ndinkalamulira kutuluka ndi kulowakwa dzuwa? Kodi udali kuti pamene ndinkapereka kwa nyenyezi iliyonseya mlengalenga dzina? Ndipo kodi ukuganiza kuti iwe umadziwa mmeneungandipembezere ine? Ndipo iwe uganiza kuti dzuwa kundimvera ine?Khala chete: ine ndikuphunzitsa iwe.” Ngati ife tili ndi mtima umeneudzazipereka kumoto wa Mulungu, iye adzatiphunzitsa ife kudziwa,iye mu mtima wake. Ichi chimabwera ndi zowawa koma ndi chabwinokwambiri. Kodi aliyense akhonza kuyenda ulendo ndi ife?FunsoTsono, kodi mmapanga chiyani pamene pali nyengo patsogolo pa inu imene inumumaona china chake chimene mumadziwa chiyenera kukhala munjira inayake, koma chilichonse mkati mwanu chikukuwa, “ichi sichili choncho!” kodi inumumasintha mtima wanu ndi malingaliro anu bwanji kuti mukhale munzereumodzi ndi chimene mudziwacho? Mtima wanu ndi mamvekedwe athupi lanuali njira imodzi, koma inu mukudziwa kuti ichi sinjira imene chiyenera kukhalira.Kodi inu mumalimbana nacho bwanji ndi chikhulupiriro kuti chisinthe?Kodi alipo wina aliyense amene adaonapo nkhondo iyi mkati mwake?Paulo adati kwa Agalatiya kuti mzimu ndi thupi zimenyana nkhondowina ndi mnzake. Ife tiyenera kuyembekezera kuti pazakhala nkhondomu mitima ndi malingaliro athu. Tsiku limeneli silidzabwera pamenepali nkhondo mu mitima ndi malingaliro athu. Koma Mulungu waperekakwa ife zida za uzimu kuti togwetse zimphamvu izi. Mulungu siamapangaadani kuti athawe. Adani Mulungu amatulutsa anthu aku Iguputo kudzeramchipululu kupita ku dziko la malonjezano, padali zimphona ndi zidam’dzikolo. Kodi ichi chikumveka ngati malo a malonjezano? Kodi ichichikumveka ngati malo osangalatsa kukhalamo---------- ndi zimphonazazikulu zamkwiyo? Koma ichi chinthu cha padera chimene Mulunguanachita. Iye amalibweretsa mu dziko lamkaka ndi uchi limene liri ndizimphona zambiri. Kudabwitsa kw amalo amene Mulungu afuna atipatseife, chimodzimodzi ukulu ndi ukali wa zimphona za mkatimo. Mulunguamapanga ichi ndi cholinga. Iye amapanga ichi kuti atipanga ichi ndicholinga. Iye amapanga ichi kuti atipange ife tikhale olimba. Chifukwa iyeali ndi zinthu zapadera zotipatsa ife, iyenso amalipa ife zimphona zazikulukuti zilimbane nafe.Mu Yakobo 1, mmanena kuti Mulungu iye yekha amapereka mayeserokuti ife tikhonze kukula mu kupirira ndi mphamvu. Ngati ife tikula mumphamvu kenaka tikula mu kukhwima ndi ntunthu.Yakobo 1:2–8: “muchiyese cimwemwe cokha abale anga m’mene mukugwamumayesero a mitundu mitundu; pozindikira kuti ciyesedwe ca cikhulupirirocanu cicita cipiriro. Koma cipiriro cikhale nayo ntchito yao ndi opanda cirema.Osasowa kanthu konse.Koma wina wa inu ikamsowa nzeru apemphe kwa Mulungu amene apatsa kwaonse modzala manja, niwosatonza. Ndipo adzamupatsa iye. Koma apemphendi chikhulupiriro wosakayika konse. Pakuti wokayikakayo afanana ndipfunde la nyanja lotengeka ndi mphepo ndi kuwinduka nayo. Pakuti asayesemunthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye; munthu wa mitima iwiriakhala wosinkhasinkha pa njira zace zonse.Mu vesi yachiwiri ikunena kuti, “chiyeseni chachikondwerero kutimukuyesedwa.” Ichi ndi chinsisi cha mphamvu zazikulu za Mzimu Oyera.Ngati mufuna kuona mphamvu za Mulungu mmoyo wanu, muyenerakusankha muchikondwerero pamene zovuta zibwera. Muli ndi chisankhopamene chimphona chidza kwa inu ndi lupanga lalikulu. Inu mukhonza,196 197


monga okazonda khumi aja, kunena, “ine ndimadana ndi zimphona ndipondili ndi mantha.” Kapena,ngati Yoswa ndi Kalebi mukhonza kunena“Zikomo chifukwa cha zimphona.”Mulungu wathu adzatipulumutsa ku ziphona. Pamene izo zidzabwera kumoyo wanu ndi kutsutsana ndi inu, inu mukhonza kukhala ndi maganizooyipa ndi mantha kapena mkwiyo, kapena, inu mukhonza kutenga lupangala Mzimu, kuthokoza Mulungu chifukwa cha chimphona chimenechitsutsana nanu, ndipo ndikudula mutu wake. Pamene mayesero abwera,ndipo adzabweradi, chiyeseni chachikondwerero. Ndipo ngati inumudzachiyesa chachikondwerero, mudzakula mu kupilira ndi pamenezimphona zitsutsana nanu, ngati muli ndi chimwemwe, chikhulupirirondi kulimbika mtima pakukumana nazo, zipangeni nokha kukhulupiriraMulungu mu mtima wanu kuti mupambane mchigonjetso mudzina la<strong>Yesu</strong>. Kenako mudzakula mu kupilira ndi chikhulupiriro. Ili ndi lamulokuti tichiyesa chachimwemwe pamene chimphona chibwera. Ngati inumukula mu chipiliro mudzakula mu kukhwima. Mudzakula mu ubwenzindi Mulungu ndi mu mphamvu ya Mzimu. Ngati mufuna kukulamu chikondi ndi mphamvu ya Mzimu ndiye muyenera kuvomerezankhondo izi.Kuthamangira ku NkhondoMulungu amabweretsa, nkhondo izi kuti ife tikhonza kukhala ndi ubalendi iye. Muli zimphona nthawi zonse mudziko la malonjezano. Mongadzikolo liriri la padera, chimodzi modzi ukulu wa ziphona. Abale,tengani malupanga anu. Alongo tengani malupanga anu ndi kuchiyesachachimwemwe. Sankhani monga Davide, kuti ngati muzaona dzenjemunthaka muli mkango, mudzadumphira mdzenjemo ndikuphamkangowo. Uwu ndiwo mtima wa munthu wamphamvu wa Mulungu.Kuona adani ndi kuthamangira kunkhondo. Davide adathamangira kwaGoliati. Yoswa ndi Kalebi, Mose, Davide, <strong>Yesu</strong> ndi aliyense wa munthuwa mphamvu wa Mulungu adathamangira ku nkhondo. Iwo adadumphiramdzenje ndi kupha mkango. Ufumu ulowedwa mokakamiza. <strong>Yesu</strong> adanenakuti kutenga motsophola kw aufumu kudzera mukukakamiza. Mulunguamayika zimphona mu dziko lonjezano chifukwa cha ife. Ndi chabwinobwino ngati izo zili kutitsutsa ife. Khalani akondwa kukhala ndi zimphonazomwe zikufuna kuzipha ife, chifukwa ife tidzawina. Zimphona zitipangaife kukhala amphamvu ndi okhwima, izo zitipanga ife monga <strong>Yesu</strong>.Davide adayenera kutsutsana nao mkango ndi chimbalangondo kutiapulumutse mwana wa nkhosa. Keneko, pamene adakumana ndi Goliyati,iye adali olimba mtima. Chifukwa Davide adali ndi nkhondo yaying’onondi mkango ndi chimbalangondo, iye sadali owopa chimphonachotchedwa Goliati ndipo adali ndi kuthekera kuchipha icho. Davideadali nako kuthekera kupulumutsa anthu a Mulungu, chifukwa tsopanoadali ndi kulimbika mtima. Ichi ndi chifukwa chake Yakobo akhonzakunena kuti chiyeseni chachimwemwe pamene mukumana ndi nkhondomu mtima ndi malingaliro anu. Pamene ubale uli ovuta kwambiri nthawizina, pamene mayesero ali ovuta, pamene m’mimba mwathu mulimwanjala, pamene anthu adana nafe kapena atinyoza ife, pamene ifeatichotsa ntchito, kapena pamene mwana afa, zonse mwa izi ndi nkhondomonga mkango ndi chimbalangondo.Pamene nkhondo izi zibwera mumtima mwathu ndi malingaliro mwathu(ndipo izo zidzabwera) pamene Mulungu ayika chimphona mudzikola malonjezano pa ife, tichiyese chachimwemwe. Khalani okondwa ndizazimphona. Zimphona izi zidzakuthandizani inu kukhala ndi chipiliro.Zimphona izi zidzakubweretserani watunthu mwa <strong>Yesu</strong>. Ngati ifetidzatenga malo athu ankhondo ndi kulimbana ndi mdani ameneyu ndiosathawa ndi kukabisala, Mulungu adzagwiritsa ntchito izi kutipanga ifekukhala a ufulu ndi mphamvu. Ife sitili a ufulu ndi mphamvu chifukwaMulungu amachotsapo mavutowa. Ife tili aufulu ndi mphamvu chifukwaMulungu amatipanga ife a akulu kuposa mavutowa. Inu muyenerakudziwa izi. iyi ndi nkhani ya <strong>Yesu</strong> mkati mwa inu. Ife sitifuna ziphonakuti zithawire kutali. Ife tifuna kudumphira mdzenje ndi kudula mutu wachiphona. Ife sitifuna Goliati kuti adzipita, tifuna iye athamangire kwaife kuti ife timuphe iye. Ife sitikuyesa kupewa nkhondo. Ife tigonjetsa pankhondoyi chifukwa ife tikufuna kukhala monga <strong>Yesu</strong> ndi ufulu mkati,ndi mitima yamphamvu ndi chikondi chakuya.Inu mukhonza kupanga chibwana ndi pemphero la mgwirizano. Komangati mitima yanu ili yachidwi pa <strong>Yesu</strong> pa nkhondo, inu mudzakhalabwino bwino.198 199


Kuonetsa pa Moyo Wa PauloIfe timayankhula poyamba m’mawa uno zokhudza moyo wa Paulo. Pauloadali ndi kukumana ndi Mulungu kwa padera, ndipo Mulungu adatsegulamaso ake kuti aone mavumbulutso aakulu ambiri. <strong>Yesu</strong> adaoneka kwaiye ndipo adamuonetsa iye paradiso. <strong>Yesu</strong> adamuuza Paulo ziphunzitsozimene munthu sadamvepo kuyambira kale. Tsono ichi chitanthauza kutiPaulo akadakhala ndi moyo wodabwitsa sichoncho? Kodi mukuzindikira,Paulo adakhala mtumwi zaka makumi awiri asanamvetsetse ziphunzitsoza mu Akorinto achiwiri 12:8. iye adapempha Mulungu katatu kutiamuchotsere zowawa zake. Mulungu adanena china chake kwa iyechimene chovuta kuchikhulupirira. Monga anzake a Yobu atatu aja, ifetifuna kukhulupirira kuti zoipa sizichitika kwa munthu wabwino. KomaMulungu ndi wabwino. Ndipo Paulo anati “Chotsani kuwawa kwa inendili oputidwa ndi mtenga wa satana.” koma Mulungu anati kwa mtumikiwake Paulo, “chifukwa ndakupatsa zinthu zodabwitsa zambiri ndiyendiyenera kuti mkati mwa mtima wako umveululu kuti usakhale onyadandi kunyengedwa ndi zinthu zimene zapatsidwa kwa iwe.Paulo anali odabwa ndi zimenezi Mulung ananena kuti chifukwa alikuganiza kuti apemphera ndi kuti ululu wuchoka kwa iye. Mulungu Atateanati kwa Paulo kodi sukumbuka? Kuti mwana wanga anapachikidwamu kufooka. <strong>Yesu</strong> anali ndi kuthekera kokhulukira uchimo mu dziko. Izindi choncho chifukwa anapachikidwa mu kufooka, osati kuti anali ndimphamvu, koma chifukwa anali mu kufooka. Osati kuti sanali kumvakuwawa koma kuti ululu unali waukulu. Mmene Mulungu akufunira kutiulemerero wake uwonekere ndi kuwonetsedwa. Chomwechonso akufunakuti ife tinyamule imfa mu matupi athu kuti tibweletse moyo kwa anthuena otizungulira. Pamene Mulungu amatipatsanso mphatso zodabwitsakuti timutumikire iye. Ayeneranso kupeleka ululu mu mtima mwathu kutitisakhale ndi kunyada kapena kunamizidwa kuti tidziwe kuti zabwino zonsezimachokera kwa iye .Sindife eni ake amphatso zimenezi nzeru ndi bvumbulutso sizibwera kwaife chifukwa ndife abwino. Monga Mulungu anachita ndi Yobu ndi Paulondi momwemo anachitira ndi mwana wake <strong>Yesu</strong> mu Yesaya 53. Anadulamiyendo yathu kuchokera pansi pathu. Atate amaononga miyendo yathundi kuti tikwanitse kuwelama ndi lkumupembedza iye. Amachita zimenezikuti atigwilitse ntchito kuti tisakhale wonyada. Pali mbali ya mtengo wakemu 2 Akorinto 12. “Paulo anati chifukwa choti zonse izi ndi za <strong>Yesu</strong> ndipozimachititsa iye kukondwa ndiye ndidzakondwera ndi ululu wanga ndipondipo tidzakondwera mu kufooka.”Sindidzakondwanso ndi uchimo koma ululu ndi wabwino chifukwatikufuna cholinga cha Mulungu kuchokera mu mtima tiyenera kuti timvekupwetekeka mphamvu ya Mulungu imakhala ya ngwiro mu kufookakwathu. Ngati tidzabvomeleze ululu ndi kulambira iyeyo. Mphamvu yake yaUmulungu idzagwira ntchito mw aife munjira zambiri mbiri modabwitsa.Ndiye timakweza manja athu kwa Mulungu ndi kunena monga Pauloananena tigawana chiyanjano cha zowawa chake kuti tigawanenso mumphamvu yakuuka kwa moyo wake. Uwu ndi uthenga wopambanasiwaanthu ozikonda koma ndi wa anthu amene ali ozichepetsa pa masoa Mulungu. Ichi ndi chi kristu choona osati chongokhuzidwa chabe ndimaganizo athu.<strong>Yesu</strong> ali kubwera kudzatitenga ife. Ndipo tsiku limeneli chimwemwechidzadzaza miyoyo yathu koma pano tili ndi ntchito pokozekeramkwatibwi amenewu ndi ntchito yathu kukondana wina ndi mzake ndikuthandizana kuti tonse monga mpingo tikonzekere kubwera kwache <strong>Yesu</strong>.Ndiye maonekedwe athu adzakhala monga <strong>Yesu</strong> pamene adzabwererekwa mpingo wake tidzafanana naye. Tidzakhala mkwatibwi monga <strong>Yesu</strong>,Mkwatibwi amene ali wa mphamvu monga <strong>Yesu</strong> amene ali ndi chifundondi chikondi monga iye sizophweka ai. Koma kuyanganira maso pa Atate,monga <strong>Yesu</strong> anachitira. Ngati tiika maso athu pa iye <strong>Yesu</strong> tidzakhala mbaliya chikondwelero cha mfusulo wa mwana wa nkhosa ndipo chimwemwechake chidzadza mitima yathu.Miyoyo Yolumikizizana Ndi KulukanaTiyenera kutchura kuti kuli abale oyera mtima mu mizinda amene alikupemphera chifukwa cha ufumu wa Mulungu kuti uwonenetsedwe padziko lino lapansi. Ndipo ali ozipeleka koposa mu moyo wa <strong>Yesu</strong> ndimtima wawo yonse kufuna kaye ufumu. Monganso mutipemphelerensoife komanso kwa iwo amene sanalambire mabondo awo kwa Balaa.Pemphelaninso iwowo chifukwa alinso mbali ya ife.200 201


Ndizofunikanso kudziwa kuti ngati palinso china chimene tingatumikire,ndi zopezeka ndi kulukana kwa miyoyo wathu pamodzi ndi moyo wathutsiku ndi tsiku. Zinthu zimene <strong>Yesu</strong> wawonetsera kwa ife kuno ndi kwinakonse ndi zopezeka mu kugwirana mapewa ndi kuthandizana wina ndimzake. Nthawi zimene uchimo umatchutsidwa mu miyoyo yathu nthawiimene manja athu ofooka amakwezedwa mu khosi lathu ndi nthawiimene imasonyeza mmene ife tili. Ngati pali china chimene tingapeleke,chimabwera chifukwa ena ayesetsa kuthandiza ife. Choncho, pamenemukuwelenga bukhu ili la moyo wanu. Dziwani kuti simuli kuona anthuochepa chabe kapena zana chabe koma ochuluka amene ali kuthandizamu msinkhu wa wina ndi mzake, ndi miyoyo yathunso. Tiyeni ife tonsepamodzi tipitilire kusintha miyoyo yathu pokweza ndi kulambira ulemererowa Mulungu. <strong>Yesu</strong> alandire ulemerero ndi matamando!Unsembe wa OkhulupiliraMu thupi la kristu pali ziwalo zambiri ndipo zina ndi zowonekera kuposazina. Koma tisachite molakwa pa mphamvu ya mphatso imene ndiyosawonekera. Mu mpingo wa mu mzinda umene inu muli mudzakhalandi anthu amene amalankhula – lankhula koposa anzawo komamusanyoze kapena kudelera mphatso imene ili mkati mwanu angakhalekuti simulankhura – lankhula. Inu ndi ena amene amalankhula lankhulamuli ndi mulingo umodzi umene umathandiza iwo kuti akhale mongaali. Mwina nonse a inu simungakhale wowonekera monga ena ali. Komamphatso yanu ndi yofunika ndipo gwilitsani ntchito zimenezi.Mbale kapena mlongo amene ali pano mwina sangalankhule kwambirimu msonkhano koma ine ndekha koma alipo amene mphatso yawondiyopambana kundipanga ine ndekha. Koma alipo amene mphatsoyawo ndi yopambana kundipanga ine kukhala chimene ine ndili komansokulimbikitsa zinthu mu moyo kuti zichitike, koposa kulankhula mauoposa 10,000. ngati sindingathe kuthandiza aliyense kuti akhale monga<strong>Yesu</strong> mu moyo wanga, ndipo ndidzanena kuti tili kuthokonza koposakwa <strong>Yesu</strong> kuti ali kunditumizira anthu. Amene akuthandiza kuti ndikhalemonga m’mene ine ndili. Ndikunena choncho chifukwa posakhala kutindinu ndani mungathe kuchita posintha dziko kwa <strong>Yesu</strong>. Musaganize kutindinu opambana pamene muli kulankhula kwambiri pa msonkhano enasangalankhule kwambiri koma mu njira zina ndi opambana chifukwa chazimene ali pa miyoyo yathu zimene zili zowelengedwa kwa Mulungu.Ndifuna kuti mudziwe m’mene wina inu anga thandizire dziko mmenemungakhalire mwa Mulungu wina ndi mzake kuthandizana kutimukhale monga <strong>Yesu</strong>. Mulungu safuna wozipambanitsa kapena otchuka.Ali kufuna anthu amene angazichepetse kwa wina ndi mzake. Mulunguakufuna anthu amene ali ndi kuthekera kugwilitsidwa ndi iye.Funso limafunsidwa posachedwapa“Kukhudzana ndi zinthu zimene talankhulazi unsembe wa okhulupilira,mmene tingakhalire pafupi ndi <strong>Yesu</strong> mmene mpingo uli - kodi ndife utsalirandi madera ena? Kodi alipo ena mu maiko amene akuzidziwa zinthu izi ndikuyenda mu zimenezi?”Ndifuna inu kuti mudziwe udindo wanu chifukwa ndinu oyambilira kwaanthu mu dziko ndi kuti muyende mu izi. alipo ochepa onse choonadiichi cha Mulungu. Alipo ochepa amene amazimvetsa izi m’maiko onsechoonadi ichi cha Mulungu. Mulungu wakulamulilani kuti mupite kumaiko onse ndi mau ake kumalo amene ali pafupi ndi inu. Pitani ndikulalikira uthenga wabwino wa ufumu woyera wa Mulungu. (1 Akorinto12, Machitidwe 2:42-47) Mulungu wakusankhani ngati apadera dera ndiuthenga wapadera uwu pang’ono ku India kapena Polande ndi kwinakonse amene amadziwa zinthu izi zimene zili pamtima wa Mulungu.(Aefeso 3:10) Mulungu ali kunong’oneza zinthu izi mu makutu anu zampingo kuti mukhale mu moyo uwu ndi peleka uthenga wotere. Kodimudzapititsa uthengawu kwa onse? Uthenga wabwino wa ufumu uyenerakupita ku maiko onse. Pamene chionongeko chidzabwera! Ndili ndichiyembekezo choti mudzalimbika ndi chikhulupiriro pochita izi.202 203

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!