15.03.2015 Views

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

Pachiyambi pomwe kuitana uku kwabweletsa anthu kufuna—<br />

funa iye. Ndiye kuitanidwa kwa ifenso ndiye m’mene zilili.<br />

Sichiphunzitso ai, ndi zimene zili mkati mwa ife. Tiyanganila<br />

zimene iye ali, ndi kulankhula. “Sindingathe kukhala popanda<br />

iye kapena kukongola ndi kufunika kotani kwa iye! Sindingathe<br />

kukhala popanda izi. Sindinalole kukhala kunja kwa malingaliro<br />

a moyo wanga ndi wa cholinga chake. Ndifuna kumutsata<br />

mwana wa nkhosa popita iye. Zonse zimene afuna ndi moyo<br />

wanga, apeza iye! Ndiye mkate wa moyo umene zoyenela<br />

zonse zipezeka ndi kukwanilitsidwapo mopezeka. Iye ndiye<br />

chithunzi cha utsogoleri, ndi kukoma mtima ndi kukhululuka ndi<br />

chifundo zimene sindingathe kukhala popanda izo! Ndifuna iye<br />

wamphamvu, iye wangwilo, iye wokoma mtima, iye wokonda ndi<br />

wachifundo. Iye wanzeru zosaneneka NDIFUNA KUKHALA<br />

NDI IYE! Ndimvetsele mau onse anena. Sindifuna kutalikana<br />

naye ai nthawi ya umoyo wanga. Sindimuonetsa msana chifukwa<br />

cha kudzikonda, ulesi, kapena kupwetekedwa mtima. Sindionetsa<br />

msana wanga kwa iye. Zoyesedwa zilipo koma zoonengeka<br />

zidzakhala zazikulu.”<br />

<strong>Yesu</strong> ali ndi kupambana, ali mukuchuluka mwa zikwi—zikwi<br />

munjira, nzeru zochuluka. Ali Ambuye iye ndi <strong>Yesu</strong> sinthano<br />

ai, si nkhani chabe za timilungu olenga dziko lapansi, okhala<br />

pampando wa chifumu oyera. Ndiza munthu otchedwa <strong>Yesu</strong><br />

ndi Atate amene ali oweluza ife tonse. Ife ngati tingaone, ngati<br />

tikatenge nthawi kumudziwa iye, palibenso kumukanizanso<br />

kopitilira. Bvuto lakhala kupanda kufunitsitsa kuziletsa kumanja<br />

ake wotheka achikondi.<br />

Kukhulupirika kwake ndikopanda malile. Koma sititha nthawi<br />

zonse kukhala pafupi mokwanila kuona, chifukwa cha ntchito<br />

yathu—yathu, kuzikonda, kusasamala–osakhala ndi nthawi naye<br />

kwenikweni.<br />

Atate adziwa kuti ngati tikhala ndi nthawi ndi mwana wake,<br />

ndiye adzaonetsa khalidwe kwa ife munjira yomwe kwenikweni<br />

yotamandika. Zoyeneleza makhalidwe ake ali achipambano pali<br />

zina zomwe zili zokhala mwa iye zimene zingakutengeleni kunja<br />

kwa zonse zomwe zikugwetsa inu pansi. Kenaka muyangana za<br />

kunja kwa dziko lomwe inu muli limene kukhala muzochitika<br />

Ameneyo ndi YESU! Waitana tonse kuyenda ndi iye. Iye adzaonetsa<br />

inu, kukoma mtima, chifundo, ndi kukhululuka kosatha.<br />

Mudzaona kumwetulira mu maso ake. Mudzaona mmene<br />

mphepo iwombela pa tsisi lake. Mudzaona ndikumva<br />

zochitika kukutengelani inu kudziko lina mmene nthawi sipita.<br />

(Chivumbulutso 1:12–18) Mudzaona utsogoleri ndi mphamvu<br />

zake. Mudzaona mmene anagonjetsera uchimo. Mudzaona kuti<br />

iye ali ndi masomphenya eni—eni mmene moyo ungakhalire.<br />

Mudzamva kuzama kwa kusekelera ndi kumva kutentha kwa<br />

kulimbikisidwa kwake.<br />

Londola iye. Adzakuonetsa utsogoleri, adzakuonetsa kulimbika.<br />

Adzakuonetsa khalidwe losasuntha ndi moyo wopambana umene<br />

udzaonekera pa iwe. Umene udzakutengela kwa iye, potetezedwa<br />

kumene iye akhalako. Adzakuonetsa mtima wabwino, ndi nzeru<br />

zoyangana mtima ndi moyo yomvetsa chisoni wako—wako—<br />

ndiye iye adzasambitsa, kuyeletsa, kulonga mzimu wake mwa iwe.<br />

Adzakupatsa mwala wa mtengo wapatali ndi miala yapamwamba<br />

imene kwa iye adzakupatsa zonse. Udzakhala mfumukazi,<br />

nudzakhala mfumu.<br />

Akufuna kumanga usilikali pa otsatira ake-sinkhamwa chabe,<br />

zoganiza, zophunzitsa—“Idzakwa ine kapena mudzapita ku<br />

Gehena” chabwino, ndizoona. Koma sizilingana ndi zimene<br />

anadzaonetsa kwa ophunzira ake khumi ndi awiri, mukuganiza<br />

kuti amamutsata konse m’midzi chifukwa amaloza kwa iyo chala<br />

ndi kunena kuti tsatani ine <strong>Yesu</strong>, kapena adzapita ku chionongeko?<br />

Mukumbukira lembo liri lonse lonena chomwechi? Ndizimene<br />

anachita pamene anapita ndi kupemphera kw aAtate usiku onse?<br />

Anatelo kodi? “Atate, onetsani zimene ndinene” naima nati, “inu<br />

khumi ndi awiri, bwerani pamodzi nane, kapena, mudzapita ku<br />

chionongeko?<br />

Ai, anafuna kukhala naye chifukwa anaona kanthu, mwa iye,<br />

kamene kanadabwitsa.<br />

2 3

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!