Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
Konzekera Wekha<br />
Namwali Iwe!<br />
Kuitana kwa Mulungu ku dziko lapansi ndiyo<br />
malo pamodzi ndi Atate, Mwana ndi Mzimu<br />
Woyera—kukhala mkwatibwi wokonzeka kubwera kwa<br />
mkwatibwi wokongolayo, <strong>Yesu</strong>. (Yohane 13:15, Aefeso 2–5,<br />
Chibvumbulutso 19–7) ngati mukuganiza za chithunzi cha<br />
malembo mmene moyo, wa, kristu umakomanilana—uli<br />
bwanji? Yofunsilana—ndi madyelero a ukwati Mulungu<br />
atifunsa ife, ati, “ Ndili nacho chiyembekezo ine. Ngati<br />
ukhala ndi ine, yanganila kuti ndine yani, palibenso wina<br />
ofanana nane. Palibe padziko lapansi amene adzakwanilitse<br />
moyo wako monga: ine—chifukwa ndinakulenga wa ine.<br />
Zina ndi zonse ndi zochotsera iwe, koma ngati ungathe<br />
kulowera mbali yanga, udzaona mmene moyo umayenela,<br />
ndipo tidzakhala pa ukwati.”<br />
“ Konzeka Mkwatibwi”<br />
1