15.03.2015 Views

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

Konzekera Wekha<br />

Namwali Iwe!<br />

Kuitana kwa Mulungu ku dziko lapansi ndiyo<br />

malo pamodzi ndi Atate, Mwana ndi Mzimu<br />

Woyera—kukhala mkwatibwi wokonzeka kubwera kwa<br />

mkwatibwi wokongolayo, <strong>Yesu</strong>. (Yohane 13:15, Aefeso 2–5,<br />

Chibvumbulutso 19–7) ngati mukuganiza za chithunzi cha<br />

malembo mmene moyo, wa, kristu umakomanilana—uli<br />

bwanji? Yofunsilana—ndi madyelero a ukwati Mulungu<br />

atifunsa ife, ati, “ Ndili nacho chiyembekezo ine. Ngati<br />

ukhala ndi ine, yanganila kuti ndine yani, palibenso wina<br />

ofanana nane. Palibe padziko lapansi amene adzakwanilitse<br />

moyo wako monga: ine—chifukwa ndinakulenga wa ine.<br />

Zina ndi zonse ndi zochotsera iwe, koma ngati ungathe<br />

kulowera mbali yanga, udzaona mmene moyo umayenela,<br />

ndipo tidzakhala pa ukwati.”<br />

“ Konzeka Mkwatibwi”<br />

1

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!