15.03.2015 Views

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

kanthu ndipo ena onse amakhala ndi kumvetsela. Izi ndi zinthu<br />

zimene maphunzitso ake, <strong>Yesu</strong> anati, amadana nazo, ndimene<br />

zimalamulila anthu mokakamiza, koma Mulungu akuti zonsezi<br />

zisinthe, pa ubwino wa iye ndi ife.<br />

Mwachoncho, ine ndikuganiza motele kwa inu kuti ngati tifuna<br />

kulemekeza mphatso imene ili mwa ife, ndikubweletsa mphatso<br />

zonse zili mwa anthu a Mulungu ndiye pafunika kusintha<br />

zinthu zambiri. Zopusa mmamvekedwe, mwa zina ndi mmene<br />

timakhalila mu msonkhano pamene takumana pamodzi. Pamene<br />

<strong>Yesu</strong> anali pano, iye, anthu amazungulila—Awa ndiwo anali<br />

abale, alongo Mariko 3. kukhala mozungulila iye! Zizoyenela<br />

kukhala motelo, pamene tili pamodzi ndi kumvetsera kwa<br />

iye osati munthu wamba okhala ndi mphatso zochepa ai?<br />

Zimenezi zosabvuta kwa inu zingaonekeso ngati zosafunikila,<br />

koma ndinenetsa kwa inu kuti mau oti “Pupeti” ndi “thupi”<br />

amanenedwanso choncho mu chi french.<br />

Pamene tikhala tonse kuona ku tsogolo, zimaonetsela munthu<br />

m’modzi yekha. Sitikhalanso ofanana ai ndimakhala kapolo wa<br />

iye amene wakhala kutsogolo kwanga monga Ambuye, kapena<br />

undidziwitsa za pamseu, msilikali kapena mu kalasi kapenanso<br />

mumapemphelo. Pamene timaika mipando mmizire mmalo<br />

mwa chokala mozungulila <strong>Yesu</strong>, zimakhala ngati kuonekela kwa<br />

munthu mmodzi yekha ali owonekera izi ndi zoipa chifukwa pali<br />

mphatso zambiri mwa ife ndipo zili mbali ya <strong>Yesu</strong>. Ngati tiika<br />

anthu onse kuona patsogolo, ndiye tikukweza mphatso imodzi<br />

yokha. Kungatheke bwanji munthu modzi wonyada kulora yekha<br />

nthawi zonse kukhala patsogolo kapenanso poonekela.<br />

Mu chithunzi chili pansichi, kweni kweni chipembetso<br />

mmachitidwe owonetsela mu anthu, ndi “mipingo ya nyumba”<br />

alipo munthu wamba amene amakhala otsogolera, mwa iye onse<br />

amatsalira. Iye amayamba amamaliza amaphunzitsa kapena<br />

kugawa ntchito zina, kuphunzitsa “kupembedza” amalamulira<br />

zonse, kuyankha mafunso. Ndi kutsogolera onse Awa simau<br />

abaibulo ai 1 Akorinto 14:26 kuchepela monga mofunikila<br />

chotupitsa mu mtanda, umadzimitsa mphatso, ndi <strong>Yesu</strong> amataya<br />

umbuye mmaonetseledwe amenewa. Komanso njira zimenezo<br />

mulibe mbaibulo siziyenela kuhala choncho.<br />

Munthu oimba kapena<br />

Olankhula nthawi zonse<br />

Kwa dziko lonse (kudziko lonse) chipembetso, kuphatikiza<br />

chikhalidwe cha chikristu) kupondeleza anthu mmachitidwe<br />

ndi zokozelathu zochitika sizili mu Baibulo, kapena pamtima<br />

wa Mulungu ndi maganizo ake. <strong>Yesu</strong> adalankhula mwachindunji<br />

ndi momveka, nazipatsa maina kotsutsana machitidwe odzadza<br />

ndi miambo ndi kuitanidza odzalalikila ndi ozikweza okha pa<br />

anthu a Mulungu. Ngakhale atumwi khumi ndi awili aja a mwana<br />

wa nkhosa adali abale pakati pa abale pakati pa oyela mtima<br />

osati oposa ena, monga mw a<strong>Yesu</strong> mwini. Mulungu amakonda<br />

utsogoleri wa Samueli pakati pakati pa moyo wa abale osati<br />

udindo kapena kutchuka, koma chikondi ndi mphatso monga<br />

zifunikila. “Timakana Mulungu” pamene tifuna mtundu wa<br />

mtsogoleri wa Sauli, monga mwa chitsimikizo cha Samueli<br />

ndi anthu ake mwa choncho uku ndi kuitanidwa kopambana<br />

koposa miambo ya anthu zomwe zili zochokera mukuganiza za<br />

mmutu mu nthawi zino, koma mpaka titabwelelanso mu njira ya<br />

malemba, ndidzapitilabe kukhala ofunda, zotsalira za zotupitsa,<br />

monga mmene chikhalidwe cha chipembedzo chimachita.<br />

28 29

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!