Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
kanthu ndipo ena onse amakhala ndi kumvetsela. Izi ndi zinthu<br />
zimene maphunzitso ake, <strong>Yesu</strong> anati, amadana nazo, ndimene<br />
zimalamulila anthu mokakamiza, koma Mulungu akuti zonsezi<br />
zisinthe, pa ubwino wa iye ndi ife.<br />
Mwachoncho, ine ndikuganiza motele kwa inu kuti ngati tifuna<br />
kulemekeza mphatso imene ili mwa ife, ndikubweletsa mphatso<br />
zonse zili mwa anthu a Mulungu ndiye pafunika kusintha<br />
zinthu zambiri. Zopusa mmamvekedwe, mwa zina ndi mmene<br />
timakhalila mu msonkhano pamene takumana pamodzi. Pamene<br />
<strong>Yesu</strong> anali pano, iye, anthu amazungulila—Awa ndiwo anali<br />
abale, alongo Mariko 3. kukhala mozungulila iye! Zizoyenela<br />
kukhala motelo, pamene tili pamodzi ndi kumvetsera kwa<br />
iye osati munthu wamba okhala ndi mphatso zochepa ai?<br />
Zimenezi zosabvuta kwa inu zingaonekeso ngati zosafunikila,<br />
koma ndinenetsa kwa inu kuti mau oti “Pupeti” ndi “thupi”<br />
amanenedwanso choncho mu chi french.<br />
Pamene tikhala tonse kuona ku tsogolo, zimaonetsela munthu<br />
m’modzi yekha. Sitikhalanso ofanana ai ndimakhala kapolo wa<br />
iye amene wakhala kutsogolo kwanga monga Ambuye, kapena<br />
undidziwitsa za pamseu, msilikali kapena mu kalasi kapenanso<br />
mumapemphelo. Pamene timaika mipando mmizire mmalo<br />
mwa chokala mozungulila <strong>Yesu</strong>, zimakhala ngati kuonekela kwa<br />
munthu mmodzi yekha ali owonekera izi ndi zoipa chifukwa pali<br />
mphatso zambiri mwa ife ndipo zili mbali ya <strong>Yesu</strong>. Ngati tiika<br />
anthu onse kuona patsogolo, ndiye tikukweza mphatso imodzi<br />
yokha. Kungatheke bwanji munthu modzi wonyada kulora yekha<br />
nthawi zonse kukhala patsogolo kapenanso poonekela.<br />
Mu chithunzi chili pansichi, kweni kweni chipembetso<br />
mmachitidwe owonetsela mu anthu, ndi “mipingo ya nyumba”<br />
alipo munthu wamba amene amakhala otsogolera, mwa iye onse<br />
amatsalira. Iye amayamba amamaliza amaphunzitsa kapena<br />
kugawa ntchito zina, kuphunzitsa “kupembedza” amalamulira<br />
zonse, kuyankha mafunso. Ndi kutsogolera onse Awa simau<br />
abaibulo ai 1 Akorinto 14:26 kuchepela monga mofunikila<br />
chotupitsa mu mtanda, umadzimitsa mphatso, ndi <strong>Yesu</strong> amataya<br />
umbuye mmaonetseledwe amenewa. Komanso njira zimenezo<br />
mulibe mbaibulo siziyenela kuhala choncho.<br />
Munthu oimba kapena<br />
Olankhula nthawi zonse<br />
Kwa dziko lonse (kudziko lonse) chipembetso, kuphatikiza<br />
chikhalidwe cha chikristu) kupondeleza anthu mmachitidwe<br />
ndi zokozelathu zochitika sizili mu Baibulo, kapena pamtima<br />
wa Mulungu ndi maganizo ake. <strong>Yesu</strong> adalankhula mwachindunji<br />
ndi momveka, nazipatsa maina kotsutsana machitidwe odzadza<br />
ndi miambo ndi kuitanidza odzalalikila ndi ozikweza okha pa<br />
anthu a Mulungu. Ngakhale atumwi khumi ndi awili aja a mwana<br />
wa nkhosa adali abale pakati pa abale pakati pa oyela mtima<br />
osati oposa ena, monga mw a<strong>Yesu</strong> mwini. Mulungu amakonda<br />
utsogoleri wa Samueli pakati pakati pa moyo wa abale osati<br />
udindo kapena kutchuka, koma chikondi ndi mphatso monga<br />
zifunikila. “Timakana Mulungu” pamene tifuna mtundu wa<br />
mtsogoleri wa Sauli, monga mwa chitsimikizo cha Samueli<br />
ndi anthu ake mwa choncho uku ndi kuitanidwa kopambana<br />
koposa miambo ya anthu zomwe zili zochokera mukuganiza za<br />
mmutu mu nthawi zino, koma mpaka titabwelelanso mu njira ya<br />
malemba, ndidzapitilabe kukhala ofunda, zotsalira za zotupitsa,<br />
monga mmene chikhalidwe cha chipembedzo chimachita.<br />
28 29