15.03.2015 Views

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

PDF - Yesu Kristo

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

malonda amalamula kuti amene ali ndi maganizo ndi mtsutso ndi<br />

odzitcha okha “akatswiri” ali ndi china choti awonetse, zipatso<br />

mumiyoyo yawo, awonekera kuti ali dni ufulu wolamulira,<br />

kuphunzitsa kapena kutsutsa ena. Mudziko lachipembedzo,<br />

modabwitsa, ali ndi ungiro ochepa kuposa ngakhale zimene<br />

amafano amaonetsera. Muchipembedzo, ngakhale, anthu ali<br />

akhungu ndi wozunguzidwa kwambiri.<br />

Mtsutso, ukatswiri, zigamulo, ndi ngakhale ubale ndi zonyoza<br />

zimayenda mophweka kuchokera kwa iwo azipatso zoyipa<br />

miyoyo yawo, m’mabanja ndi m’mabwalo awo. Zodabwitsa, koma<br />

zoona ngati inu muona chipembedzo chamunthu mosamalitsa<br />

ndi moona. Munthu amene amapanga zinthu zotere ngati bodza<br />

kapena m’nyozo kapena kukhala ngati katswiri pa njiniaring’I,<br />

zamakhwala kapena malonda akhonza kusonkhanitsa pamodzi<br />

gulu lomvera mpphweka anthu akuopa, m’mene akhonza<br />

kunderedwa pansi, kapena kuyamikiridwa mpusitsa ku—<br />

kuzipereka ku makina osabereka zipatso ndi “akatswiri” zonga<br />

zamisala koma ndi zoona. Zimachitika kunthawi zonse, chifukwa<br />

umu ndi m’mene maufumu a vuto amasungira nambala yao.<br />

Mantha ndi kuyimikira kopusitsa, mjedo, m’nyozo kapena<br />

kuyenderedwa pansi. Nchifukwa chake ziri zosadabwitsa kuti<br />

<strong>Yesu</strong> sanapange bwino mu chipembedzo chovomerezedwa<br />

kudziko lapansi cha munthawi yake. Koma, likhonza kuphunzira<br />

kwa iye ndi kusunga malembo, ndi kuyang’ana zipatso, osati<br />

kumvera—kunena kwa mfundo ndi mabanjeti, ndiponso kunena<br />

kufuna kwa yenkha kwa munthu kuti ateteze.<br />

(Pamenepo mwatengapo mfundo. :)<br />

Utsogoleli Wa <strong>Yesu</strong><br />

Mu Msonkhano<br />

China chimene tiyenela kulimba mtima kusintha ndikukhala<br />

ndi msonkhano monga baibulo limanane mu 1 Akorinto 14:<br />

“Pamene mubwela pamodzi, abale mpingo onse uli pamodzi,<br />

zilizonse zichitike mukumanga tonse pamodzi aliyense ali ndi<br />

chimangililo, nyimbo, bvumbulutso” ngati tidzakhala motero,<br />

potero osakhulupilira adzagwetsa nkhope nanena kuti, “Mulungu<br />

ali nanu”.<br />

Palibe bwana wina pambali pa <strong>Yesu</strong> “Musamutche wina<br />

mtsogoleri, Ambuye mphunzitsi, kapena mbusa. Ndinu nonse<br />

abale” muli ndi <strong>Yesu</strong> ndipo ndiofanana mwa inu nonse. Inde pali<br />

kusiyana kwa makulidwe, ndipo mphatso zina ndi “zoonekera”<br />

ndipo zina ai kapena zochepa kuonekera pa malongosodwe.<br />

Koma zonse zilipo ndipo zili ndi mwai. Nthawi zina timafuna<br />

chifundo cha <strong>Yesu</strong> ndipo nthawi zina timafuna kuphunzira<br />

kwa <strong>Yesu</strong>. Nthawi zina nyimbo kwa <strong>Yesu</strong>. Ndipo nthawi zina<br />

timafuna kuthandizidwa kwa <strong>Yesu</strong> pothana ndi zobvuta. Koma<br />

zonse ndi zofanana mwa <strong>Yesu</strong> chonde werengani 1 Akorinto<br />

14:26–40. Palibe amene ali olamula, koma <strong>Yesu</strong> yekha.<br />

Timasonkhana pozindikila kukhalira pamodzi, mchikondi<br />

ndi ntchito zabwino” (Aheberi 10:24–26) Tiyenela kuganiza<br />

za pemphelo mmene tingathandizilane wina ndi mnzake<br />

pamene tili pamodzi, ndipo yense wa ife ali ndi udindo pa<br />

mau a Mulungu ndi chikondi chake. Popanda wina opambana”<br />

oikidwa kuchita kalikonse kupatula kumvela ndi kubvomereza<br />

kwa Mulungu monga wina aliyense ngati wina abweletsa<br />

chiphunzitso kuchokera kwa <strong>Yesu</strong> ndipo ena chimangiliro<br />

kapena nyimbo, kapena bvumbulutso, ngati mbale, mlongo<br />

agawa kanthu kamene <strong>Yesu</strong> waunetsela ndipo bvumbulutso<br />

lidza kwa wina okhalapo ndipo olankhulawo akhale pansi—<br />

ngati timvela malangizo a Mulungu, osati mwambo ya anthu<br />

chabe. Baibulo limanena nthawi zonse, ngati bvumbulutso<br />

lidza kwa wina okhalapo. “OYAMBA AYENELA KUKHALA<br />

PANSI” ndi zimene amanena mu 1 Akorinto 14.<br />

Izi sizabwino kwa iwo amene amafuna kukhala otchuka ndi<br />

okonda kukhala akulu utsogolera ndipo owoneka ngati auzimu<br />

ndikumatenga ndalama za abale woyera mtima ife tatengela<br />

katundu olemela mu miambo kuchokera kwa Akatolika ndiponso<br />

kwa ma potesistant, ndi mpingo ya chipembedzo ndi ya makolo<br />

athu, akale. Mbusa kapena otsogolera zochitika amakhala<br />

patsogolo pathu kulankhula ndi ang’ono, anthu osadziwa<br />

26 27

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!