17.06.2013 Views

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

339<br />

• Ngati mlomo <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na kapena m’m<strong>wa</strong>mba m<strong>wa</strong><br />

mlomo <strong>wa</strong>ke uga<strong>wa</strong>nika pawiri, atha kukhala ndi mavuto a<br />

kuyam<strong>wa</strong> ndipo ayenera kumadzamudyetsera sipuni.<br />

M<strong>wa</strong>kuchita opaleshoni <strong>wa</strong> mlomo <strong>wa</strong> m’m<strong>wa</strong>mba zikhoza<br />

kubwezeretsa mlomowo m’malo m<strong>wa</strong>ke. Nthawi yabwino<br />

yochitira opaleshoni ya mlomo ndi pamene ali ndi miyezi 4<br />

mpaka 6, ndipo miyezi 18 ngati ili opaleshoni ya<br />

m’m<strong>wa</strong>mba m<strong>wa</strong> mlomo.<br />

Mlomo woga<strong>wa</strong>nika pawiri<br />

7. Zovuta pa nthawi yobereka nthawi zina zingachititse kuwonongeka k<strong>wa</strong><br />

bongo. Zimene zingachititse m<strong>wa</strong>na kukhala ndi zi<strong>wa</strong>lo zouma ndi zizindikiro za<br />

kug<strong>wa</strong> khunyu. Mpata <strong>wa</strong> kuwonongekaku ndi <strong>wa</strong>ukulu ngati pa nthawi yobad<strong>wa</strong><br />

m<strong>wa</strong>nayo sapuma mofulumira, kapena ngati mzamba adapereka jekeseni yofulumizitsa<br />

kubad<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na m<strong>wa</strong>nayo as<strong>ana</strong>badwe (tsamba 282).<br />

Khalani osamala ndi mmene mumasankhira mzamba <strong>wa</strong>nu ndipo musalole<br />

mzamba <strong>wa</strong>nu kugwiritsira ntchito mankh<strong>wa</strong>la ofulumizitsa kubereka m<strong>wa</strong>na<br />

<strong>wa</strong>nu as<strong>ana</strong>badwe.<br />

M<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong> minofu yomangika (Celebral Palsy)<br />

Miyendo yopiringidz<strong>ana</strong><br />

kapena yopitama ngati<br />

sizesi.<br />

M<strong>wa</strong>na wod<strong>wa</strong>la matenda<strong>wa</strong> amakhala ndi minofu<br />

yomangika ndi youuma kotero <strong>kuti</strong> satha kusuntha zi<strong>wa</strong>lo<br />

bwinobwino. Nkhope yake, khosi lake, kapena thupi lake litha<br />

kupotoka, ndipo mayendedwe ake amadzandira. Nthawi<br />

zambiri minofu yomangika m’kati m<strong>wa</strong> miyendo yake<br />

imachititsa <strong>kuti</strong> miyendo yake ikhale yopachik<strong>ana</strong> ngati<br />

sizesi.<br />

Pa nthawi yobad<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>nayo akhoza kuwoneka ngati ali<br />

bwinobwino kapena womasuka bwinobwino. Kumangika<br />

kumabwera iye akamakula. M<strong>wa</strong>nayo atha kudzakhala<br />

woganiza msanga kapenanso moched<strong>wa</strong>.<br />

Palibe mankh<strong>wa</strong>la amene amachiritsa kuwonongeka k<strong>wa</strong><br />

bongo kumene kumachititsa kumangika k<strong>wa</strong> minofu. Koma<br />

m<strong>wa</strong>na afunikira chisamaliro chapadera. Pofuna kule<strong>wa</strong><br />

kumangika k<strong>wa</strong> minofu m’miyendo kapena mapazi, perekani<br />

chithandizo monga cha mafupa olek<strong>ana</strong> m’chiuno (tsamba 335)<br />

ndiponso mwendo wokhota (tsamba 338), ngati kuli kofunika.<br />

Mthandizeni m<strong>wa</strong>nayo kusuntha, kukhala komanso kuima<br />

kenaka kuyenda monga lasonyezera tsamba 334.<br />

Mlimbikitseni kugwiritsira ntchito kuganiza ndi thupi<br />

mulimonse mmene angathere. Mthandizeni kuphunzira (onani<br />

tsamba lotsatirali). Ngakhale <strong>kuti</strong> iye ali ndi vuto la<br />

kuyankhula atha kukhala ndi mphamvu yabwino ya kuganiza<br />

ndi kutha kuphunzira zinthu zochuluka atapatsid<strong>wa</strong> mpata.<br />

Mthandizeni <strong>kuti</strong> adzithandize yekha.<br />

Kuched<strong>wa</strong> kukula m’miyezi yoyambirira ya <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>ke<br />

(Retardation)<br />

Ana ena amene ali ndi thanzi labwino pa nthawi yobad<strong>wa</strong> sakula bwino. Amayamba<br />

kuganiza moched<strong>wa</strong> chifuk<strong>wa</strong> sadya chakudya chokhala ndi zonse zofunikira m’thupi<br />

la munthu. M’kati m<strong>wa</strong> miyezi yochepa yoyambirira ya <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>wo, bongo umakula<br />

mofulumira kuposa pa nthawi ina iliyonse. Chifuk<strong>wa</strong> cha chimenechi chakudya<br />

choyenera k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na ndi chofunika k<strong>wa</strong>mbiri. Mkaka <strong>wa</strong> m’mawere ndicho chakudya<br />

chabwino koposa k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na (onani chakudya chabwino cha m<strong>wa</strong>na, tsamba 125).

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!