17.06.2013 Views

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

338<br />

Nkhope ya m<strong>wa</strong>nayo imawoneka yefufuma, ndipo imawoneka ya tondovi, lirime lake<br />

limayenda kunja, ndipo chipumi chonse chitha kukhala ndi tsitsi. Ngofowoka, sadya<br />

moyenera, amalira pang’ono, ndipo amagona k<strong>wa</strong>mbiri. Amaganiza moched<strong>wa</strong> ndipo<br />

atha kukhala ogontha. Adzayamba kuyenda ndi kuyankhula moched<strong>wa</strong> kuyerekeza ndi<br />

<strong>ana</strong> oti ali bwinobwino.<br />

Pofuna kuthandiza kupe<strong>wa</strong> vuto lobwera k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na chifuk<strong>wa</strong> choso<strong>wa</strong><br />

mchere <strong>wa</strong> ayodini (iodine) m’thupi m<strong>wa</strong> mayi (cretinism), amayi apakati<br />

ayenera kugwiritsira ntchito mchere wokhala ndi iodine m’malo m<strong>wa</strong> mchere<br />

<strong>wa</strong>mba (onani tsamba 135).<br />

Ngati mukuganiza <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>nu atha kukhala ndi vuto la cretinism pitani naye<br />

kuchipatala kapena k<strong>wa</strong> dotolo nthawi yomweyo. Kulandira mankh<strong>wa</strong>la m<strong>wa</strong>changu<br />

(a thyroid) kumatanthauza kukhalanso bwino m<strong>wa</strong>changu.<br />

3. Kusuta kapena kum<strong>wa</strong> zakum<strong>wa</strong> zaukali pamene mayi ali ndi mimba kumachititsa<br />

<strong>ana</strong> kubad<strong>wa</strong> aang’ono thupi kapena kukhala ndi mavuto ena (onani tsamba 156).<br />

Osamam<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong>mbiri kapena kusuta makamaka pamene muli ndi pakati.<br />

4. Zikadutsa zaka 35, mpata ndi <strong>wa</strong>ukulu woti mayi adzakhala ndi m<strong>wa</strong>na wokhala<br />

ndi vuto lina lake la pathupi. Matenda a mongolism kapena Down’s disease, amene<br />

amawoneka ngati cretinism ndi ochuluka pakati pa <strong>ana</strong> amene mayi ali <strong>wa</strong>chikulire<br />

k<strong>wa</strong>mbiri.<br />

Ndi bwino kukonzeratu za ukulu <strong>wa</strong> banja lanu kotero <strong>kuti</strong> simukukhalanso<br />

ndi <strong>ana</strong> ena pamene mupyola zaka 35 (onani mutu 20).<br />

5. Mitundu yosiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> ya mankh<strong>wa</strong>la itha kuvulaza m<strong>wa</strong>na amene akukula<br />

m’mimba m<strong>wa</strong> mayi.<br />

Gwiritsirani ntchito mankh<strong>wa</strong>la ochepa monga mmene mungathere pa<br />

mthawi imene muli ndi pakati ndipo akhale okhawo amene mukudzi<strong>wa</strong> <strong>kuti</strong><br />

saika <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na pa chiswe.<br />

6. Ngati makolo ali pachibale (pachisuweni, m<strong>wa</strong>chitsanzo), pali mpata <strong>wa</strong>ukulu<br />

<strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> awo adzakhala ndi vuto lapathupi kapena adzakhala oganiza moched<strong>wa</strong>. Maso<br />

a ntchefu, zala zowonjezereka, mapazi okhota, mlomo <strong>wa</strong>m’m<strong>wa</strong>mba<br />

woga<strong>wa</strong>nika ndi mavuto a pathupi odziwika bwino.<br />

Pofuna kuchepetsa mpata <strong>wa</strong> mavuto amene<strong>wa</strong> ndi ena, musak<strong>wa</strong>tire <strong>wa</strong>chibale<br />

<strong>wa</strong>pafupi. Komanso ngati muli ndi vuto lobad<strong>wa</strong> nalo lachilendolendo pa <strong>ana</strong> omwe muli<br />

nawo, ganizirani zosiya kukhalanso ndi <strong>ana</strong> ena (onani Ndondomeko za Kulera, mutu 20).<br />

Ngati m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>nu abad<strong>wa</strong> ndi vuto lapathupi, pitani naye<br />

kuchipatala. Nthawi zambiri kena kake kakhoza kuchitid<strong>wa</strong>.<br />

• Ngati lili vuto lokhala ndi maso antchefu (cross-eyes), onani<br />

tsamba 234.<br />

• Ngati m<strong>wa</strong>na abad<strong>wa</strong> ndi chala chowonjezereka chaching’ono<br />

k<strong>wa</strong>mbiri ndipo ndi chopanda fupa m’kati m<strong>wa</strong>ke, chimangeni<br />

ndi kachingwe mothinitsa k<strong>wa</strong>mbiri. Chotsatira chake ndi<br />

cha<strong>kuti</strong> chalacho chidzauma ndipo kenaka chidzaduka. Ngati<br />

chili chachikulu ndipo chokhala ndi fupa, muchisiye<br />

choncho kapena mupite kuchipatala <strong>kuti</strong> akachichotse.<br />

• Ngati mapazi a m<strong>wa</strong>na wobad<strong>wa</strong> kumene ali okhotera m’kati<br />

kapena apanga chibonga, yesetsani kuma<strong>wa</strong>wongolera<br />

monga mmene ayenera kukhalira. Ngati mungachite<br />

zimenezi msanga, chitani zimenezi kambirimbiri tsiku<br />

lililonse. Mapazi (kapena phazi) ayenera kukula<br />

pang’onopang’ono <strong>kuti</strong> akhale monga mmene ayenera<br />

kukhalira. Ngati simungathe kuwongola mapazi a<br />

m<strong>wa</strong>nayo <strong>kuti</strong> akhale m’malo m<strong>wa</strong>ke, pitani naye<br />

nthawi yomweyo kuchipatala kumene mapazi ake atha<br />

kumangid<strong>wa</strong> <strong>kuti</strong> akhale mchimake, m<strong>wa</strong>kuika mu<br />

chikhakha. Kuti pakhale zotsatira zabwino ndi pofunika<br />

kutero m’kati m<strong>wa</strong> masiku awiri akabad<strong>wa</strong>.<br />

Phazi<br />

lokhotera<br />

m’kati<br />

Phazi lokhala<br />

ngati<br />

chibonga

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!