17.06.2013 Views

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

Kutalika mchombo<br />

Mchombo umene umatalika<br />

chotere si vuto ayi. Mankh<strong>wa</strong>la<br />

kapena chithandizo china<br />

chilichonse nzosafunikira<br />

kufupikitsira mchombo.<br />

Kumanga mimba ndi kansalu<br />

kapena lamba <strong>wa</strong> pamimba<br />

sizingathandize.<br />

Tchende lotupa (Hydrocele kapena Hernia)<br />

Ngati tchende la m<strong>wa</strong>na litupa mbali imodzi, ichi ndi chifuk<strong>wa</strong><br />

choti ladzadza madzi kapena chifuk<strong>wa</strong> choti kanthu kena kake<br />

ka mbali ya thupi kathawira kumeneko (hernia). Kuti mudziwe<br />

chochititsa chenicheni, unikani ndi nyali <strong>kuti</strong> muwone ngati<br />

ku<strong>wa</strong>la kudutsa chotupacho.<br />

Ngati ku<strong>wa</strong>la kudutsa<br />

chotupacho msangamsanga<br />

ndiye <strong>kuti</strong> m’tchendemo muli<br />

madzi (hydrocele).<br />

Madzi nthawi zambiri amachoka<br />

okha pakapita nthawi popanda<br />

chithandizo chapadera. Koma<br />

pakatha chaka chathunthu,<br />

kafuneni chithandizo ku<br />

chipatala.<br />

Ngati ku<strong>wa</strong>la sikudutsa m’katimo,<br />

komanso ngati chotupa chikula<br />

m<strong>wa</strong>na akamatsokomola kapena<br />

kulira, ndiye <strong>kuti</strong> kachi<strong>wa</strong>lo kena<br />

kake kam’thupi kathawira<br />

kumeneko (hernia).<br />

Hernia imafunika opaleshoni (onani<br />

tsamba 97).<br />

Ana oganiza moched<strong>wa</strong> (operewera), ogontha kapena<br />

opu<strong>wa</strong>la<br />

Nthawi zina makolo adzakhala ndi m<strong>wa</strong>na amene adzabad<strong>wa</strong> osamva, woganiza<br />

moched<strong>wa</strong>, kapena <strong>wa</strong> mavuto obad<strong>wa</strong> nawo (chomwe chikusonyeza china chake<br />

cholakwika pa thupi pake). Nthawi zambiri palibe chifuk<strong>wa</strong> chimene chingaperekedwe.<br />

Palibe aliyense amene ayenera kudzudzulid<strong>wa</strong>. Nthawi zambiri<br />

zimangochitika m<strong>wa</strong>ngozi.<br />

Komabe, zinthu zina zimakulitsa mpata woti m<strong>wa</strong>na abadwe ndi<br />

mavuto ena. Ndi povuta <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na abadwe ndi vuto lina lake la<br />

pathupi ngati makolo atsatira machenjezo ena ake.<br />

1. Kuso<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> zakudya zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi<br />

nthawi imene mayi ali ndi pakati kukhoza kuchititsa kuganiza<br />

moched<strong>wa</strong> kapena vuto lina lobad<strong>wa</strong> nalo lapathupi pa m<strong>wa</strong>na.<br />

Kuti mukhale ndi <strong>ana</strong> athanzi, amayi apakati ayenera kudya<br />

zakudya zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi (tsamba 115).<br />

2. Kusoweka k<strong>wa</strong> mchere <strong>wa</strong> ayodini mu zakudya za mayi<br />

<strong>wa</strong>pakati kungabweretse vuto lina lobad<strong>wa</strong> nalo lotched<strong>wa</strong> cretinism<br />

m’chingerezi.<br />

337<br />

Ngakhale mchombo<br />

<strong>wa</strong>ukulu chotere ngati uwu<br />

si owopsa ndipo udzatha<br />

wokha. Ngati udakalipobe<br />

kufikira ali ndi zaka 5,<br />

opaleshoni itha kuchitika.<br />

Kalandireni malangizo<br />

kuchipatala.<br />

Nthawi zina hernia imachititsa<br />

chotupa pam<strong>wa</strong>mba komanso<br />

mbali imodzi ya tchende, osati<br />

m’kati.<br />

Mukhoza kudzi<strong>wa</strong> izi powona<br />

chotupacho (tsamba 89)<br />

chifuk<strong>wa</strong> hernia imatupa ngati<br />

m<strong>wa</strong>na akulira kapena <strong>wa</strong>imirira<br />

mowongoka, ndipo imaso<strong>wa</strong> ngati<br />

iye akhala chete.

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!