17.06.2013 Views

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

336<br />

Nthenda yobad<strong>wa</strong> nayo ya kuchepa k<strong>wa</strong> magazi m’thupi<br />

Ana ena amabad<strong>wa</strong> ‘ofowoka pa magazi’, matenda amene amatched<strong>wa</strong> sickle cell pa<br />

Chingerezi. Nthendayi imachokera k<strong>wa</strong> makolo, ngakhale <strong>kuti</strong> makolowo sadzi<strong>wa</strong> zoti<br />

ali nawo. Amakhala <strong>kuti</strong> nthendayi ali nayo m’magazi m<strong>wa</strong>wo. M<strong>wa</strong>na atha kuwoneka<br />

<strong>wa</strong>thanzi miyezi isanu ndi umodzi yoyambirira, koma zizindikiro zina zimayambano<br />

kuwoneka.<br />

Zizindikiro zake:<br />

• Kutentha k<strong>wa</strong> thupi ndi kulira. M<strong>wa</strong>na amawoneka opanda<br />

magazi, ndipo akhoza kuwonetsa mtundu <strong>wa</strong>chikasu m’maso<br />

m<strong>wa</strong>ke.<br />

• Mapazi ndi zala zake zitha kuwonetsa zotupa zimene<br />

zimabisala pakatha mulungu umodzi kapena milungu iwiri,<br />

ndipo kenaka amakhala bwino.<br />

• Mimba itha kutupa ndi kulimba chifuk<strong>wa</strong> cha kukula k<strong>wa</strong> zi<strong>wa</strong>lo<br />

za khoma la mimba kapamba (sathamagazi) ndi chiwindi.<br />

• Pamene ak<strong>wa</strong>nitsa zaka ziwiri zakubad<strong>wa</strong> mutu ukhoza<br />

kuyamba kuwonetsa mabampu mu ngondya za mafupa. Uku<br />

kumatched<strong>wa</strong> ‘bossing’ m’chingerezi.<br />

• M<strong>wa</strong>na amakhala wopanda mphamvu yodzitchinjiriza nayo ku<br />

matenda ndipo kawirikawiri amad<strong>wa</strong>la malungo, chifu<strong>wa</strong>, kutsekula m’mimba ndi<br />

matenda ena.<br />

• Amakula moched<strong>wa</strong> poyerekeza ndi <strong>ana</strong> ena.<br />

• Nthawi ndi nthawi m<strong>wa</strong>na amakhala ndi chimake cha vuto la ‘kufowoka k<strong>wa</strong><br />

magazi’, nthawi zambiri chifuk<strong>wa</strong> cha malungo , kapena matenda ena obwera<br />

chifuk<strong>wa</strong> cha tizilombo m’magazi. M<strong>wa</strong>na amatentha thupi k<strong>wa</strong>mbiri ndi kupweteka<br />

k<strong>wa</strong>mbiri m’mafupa am’manja kapena miyendo, kapenanso m’mimba. Vuto la<br />

kuso<strong>wa</strong> magazi limafika poipa mosataya nthawi. Zotupa pamafupa zitha kuyamba<br />

kutulutsa mafinya. Vutoli litha kubweretsa imfa.<br />

Chithandizo:<br />

Palibe njira imene ingachitike <strong>kuti</strong> kufowoka k<strong>wa</strong> kapangidwe ka magazi kungasinthe,<br />

koma m<strong>wa</strong>na atha kutetezed<strong>wa</strong> ku zinthu zimene zimabweretsa mavuto, ndipo<br />

payenera kukhala makonzedwe oti azikawon<strong>ana</strong> ndi anthu ogwira ntchito zachipatala<br />

mwezi ndi mwezi mosadukiza <strong>kuti</strong> azikamuunika ndikumampatsa chithandizo cha<br />

mankh<strong>wa</strong>la.<br />

1. Malungo. M<strong>wa</strong>nayo ayenera kulandira mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi malungo <strong>kuti</strong><br />

nthendayi isawonekere, nthawi zambiri pogwiritsira ntchito mankh<strong>wa</strong>la a pyrimethamine<br />

kapena chloroquine (tsamba 379 ndi 381). Pa amene mankh<strong>wa</strong>la<strong>wa</strong> muyenera<br />

kuwonjezeranso mankh<strong>wa</strong>la okhala ndi gulu la mavitamini B osiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> amene<br />

amachulukitsa magazi (folic acid, tsamba 406). Mankh<strong>wa</strong>la a magazi a iron a ferrous<br />

sulfate si ofunika kwenikweni.<br />

2. Matenda obwera chifuk<strong>wa</strong> cha tizilombo tam’magazi. Tetezani m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>nu<br />

ku matenda a chikuku, chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima, ndi chifu<strong>wa</strong> chachikulu po<strong>wa</strong>patsa<br />

katemera m<strong>wa</strong>msanga nthawi imene ili yovomerezeka. Chiritsani zizindikiro monga<br />

kutentha thupi, kutsokomola, kutsekula m’mimba, kukodza pafupipafupi, kapena<br />

ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> paliponse k<strong>wa</strong> m’mimba, miyendo kapena mikono, popita ndi m<strong>wa</strong>na k<strong>wa</strong><br />

ogwira ntchito zachipatala mofulumira monga mmene mungathere. Mankh<strong>wa</strong>la<br />

olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo toyambitsa matenda atha kukhala ofunikira. Mupatseni<br />

madzi ochuluka akum<strong>wa</strong>, ndi p<strong>ana</strong>dolo (tsamba 393) pochepetsa ululu <strong>wa</strong> m’mafupa.<br />

3. Asayandikire malo ozizira. Ayenera <strong>kuti</strong> akhale malo ofunda ndipo afunde<br />

bulangeti usiku ngati kuli kofunika. Gwiritsirani ntchito matiresi ofe<strong>wa</strong> bwino ngati kuli<br />

kotheka.<br />

4. Mimba. Mayi <strong>wa</strong>chichepere ayenera kupe<strong>wa</strong> zimenezi, pokhapokha ngati kuli<br />

kotheka kukachirira kuchipatala, chifuk<strong>wa</strong> cha kukulitsa kufowoka k<strong>wa</strong> magazi<br />

k<strong>wa</strong>kukulu. Njira yakulera ya jekeseni (tsamba 312) ndiyo yovomerezeka k<strong>wa</strong> amayi<br />

amene ali ndi matenda a vuto la kapangidwe ka magazi m’thupi monga njira<br />

yotetezed<strong>wa</strong> koposa yoletsera mimba, ndipo ithanso kuchepetsa mavuto omwe<br />

angabwerepo chifuk<strong>wa</strong> cha zochititsa zina.

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!