17.06.2013 Views

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

333<br />

Ngati muli ndi maganizo oti m<strong>wa</strong>na ali ndi diphtheria:<br />

• Mgonekeni mchipinda chayekha.<br />

• Kalandireni chithandizo cha kuchipatala m<strong>wa</strong>msanga. Pali mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi<br />

tizilombo toyambitsa matenda a diphtheria.<br />

• Perekani penicillin, mbulu umodzi <strong>wa</strong> mayunitsi 400,000, katatu pa tsiku k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong><br />

akuluakulu.<br />

• Amwe madzi ofunda othira mchere pang’ono.<br />

• Mkonzereni <strong>kuti</strong> apume mpweya <strong>wa</strong> madzi otentha kawirikawiri ndi mosalekeza<br />

(tsamba 177).<br />

• Ngati m<strong>wa</strong>na ayamba kutsam<strong>wa</strong> ndi kusandulika buluwu (blue), chotsani kangaude<br />

kummero k<strong>wa</strong>ke pogwiritsa ntchito kansalu kamene m<strong>wa</strong>veka chala chanu.<br />

Diphtheria ndi nthenda yowopsa imene ingapewedwe m<strong>wa</strong>changu ndi katemera <strong>wa</strong><br />

DPT. Onetsetsani <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> anu alandira katemerayu.<br />

Poliyo (Polio, Poliomyelitis)<br />

Poliyo akupezeka k<strong>wa</strong>mbiri pakati pa <strong>ana</strong> osak<strong>wa</strong>na zaka<br />

ziwiri zakubad<strong>wa</strong>. Imabwera ndi kachilombo ka vairasi ngati<br />

kamene kamachititsa chimfine, kawirikawiri ndi kutentha<br />

k<strong>wa</strong> thupi, kusanza, kutsekula m’mimba, ndi zilonda<br />

m’minofu. Nthawi zambiri m<strong>wa</strong>na amachira kotheratu<br />

m’masiku owerengeka. Koma nthawi zina chi<strong>wa</strong>lo china<br />

chathupi chimafowoka kapena kupu<strong>wa</strong>la. Nthawi zambiri izi<br />

zimachitika ku mwendo umodzi kapena yonse iwiri.<br />

Pakapita nthawi mwendo kapena mkono wofowoka uja<br />

umawonda ndipo siukula mofulumira ngati unzake uja.<br />

Chithandizo:<br />

Matenda<strong>wa</strong> akangoyamba, palibe mankh<strong>wa</strong>la amene<br />

adzaletse kupu<strong>wa</strong>lako. (Komabe, nthawi zina mbali kapena<br />

mphamvu ina yonse imene yataika imabwerera<br />

pang’onopang’ono.) Mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha<br />

tizilombo toyambitsa matenda m’thupi sathandiza. Monga<br />

chithandizo choyambirira, chepetsani ululu ndi p<strong>ana</strong>dolo<br />

(paracetamol) kapena aspirin ndipo ikani nsalu<br />

zonyowetsed<strong>wa</strong> ndi madzi otentha paminofu yo<strong>wa</strong><strong>wa</strong>yo.<br />

Mkhazikeni m<strong>wa</strong>nayo m<strong>wa</strong> njira yoti amve bwino ndi kuletsa<br />

kupinda kapena kuunjik<strong>ana</strong> k<strong>wa</strong> minofu ya zi<strong>wa</strong>lo.<br />

Pang’onopang’ono wongolani manja ake ndi miyendo kotero<br />

<strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>nayo akhale mowongoka mmene angathere. Ikani<br />

zinsalu pansi pa mawondo ake, ngati kuli kofunika <strong>kuti</strong> ululu uchepe, koma onetsetsani<br />

<strong>kuti</strong> mawondo ake ndi owongoka.<br />

Kapewedwe kake:<br />

• Katemera <strong>wa</strong> poliyo ndiye chitetezo chabwino k<strong>wa</strong>mbiri.<br />

• Musapereke jekeseni <strong>wa</strong> mankh<strong>wa</strong>la a mtundu wina uliwonse k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na amene ali<br />

ndi zizindikiro za chimfine, kutentha thupi, kapene zizindikiro zina zili zonse zimene<br />

zitha kuchititsid<strong>wa</strong> ndi vairasi ya poliyo. Ululu wochititsid<strong>wa</strong> ndi jekeseni utha<br />

kusintha poliyo yapang’ono yosapu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo kukhala yodetsa nkha<strong>wa</strong>,<br />

yotsag<strong>ana</strong> ndi kupu<strong>wa</strong>la zi<strong>wa</strong>lo. Musabaye jekeseni <strong>wa</strong> mankh<strong>wa</strong>la ena<br />

aliwonse pokhapokha ngati kuli koyenera.<br />

Onetsetsani <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> alandira katemera <strong>wa</strong> poliyo, <strong>wa</strong> ‘madontho a poliyo’<br />

pamene ali ndi miyezi iwiri, itatu kapena inayi yakubad<strong>wa</strong>.

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!