17.06.2013 Views

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

Ukhondo<br />

315<br />

Ana adzakhala ndi <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>thanzi ngati midzi, makomo ndi iwo eni akewo ali<br />

aukhondo. Tsatirani malangizo aukhondo amene ali m’mutu 12. Aphunzitseni <strong>ana</strong> anu<br />

kuzitsatira ndi kuzimvetsa ubwino <strong>wa</strong>ke. Pano malangizo ofunika k<strong>wa</strong>mbiri<br />

abwerezed<strong>wa</strong>.<br />

• Asambitseni <strong>ana</strong> anu ndi ku<strong>wa</strong>sintha zovala zawo nthawi zonse.<br />

• Aphunzitseni <strong>ana</strong> kusamba m’manja nthawi zonse pamene adzuka m’ma<strong>wa</strong>,<br />

akachoka ku chimbudzi, komanso as<strong>ana</strong>dye kapena kugwira chakudya.<br />

• Kumbani zimbudzi ndipo aphunzitseni <strong>ana</strong>wo kuzigwiritsira ntchito zimbudzizo.<br />

• Kumene kuli mahukuwemu, musalole <strong>ana</strong> anu kuyenda opanda nsapato; gwiritsirani<br />

ntchito nsapato.<br />

• Phunzitsani <strong>ana</strong> kutsuka mano ndipo musama<strong>wa</strong>patse mabisiketi ambiri, maswiti<br />

kapena zakum<strong>wa</strong> monga kokakola.<br />

• Dulani zikhadabo zawo <strong>kuti</strong> zikhale zazifupi.<br />

• Musalole <strong>ana</strong> amene ali od<strong>wa</strong>la kapena amene ali ndi zilonda, mphere, nsabwe,<br />

kapena chipere kugona ndi <strong>ana</strong> anzawo kapena kugwiritsira ntchito zovala zimodzi<br />

kapena nsalu yopuputira.<br />

• Apatseni chithandizo msanga <strong>ana</strong> amene ali ndi mphere, chipere, njoka<br />

zam’mimba, ndi matenda ena opatsir<strong>ana</strong> mosavuta kuchoka k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na wina<br />

kupita k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na m’nzake.<br />

• Musalole <strong>ana</strong> anu kuika zinthu zakuda m’kam<strong>wa</strong> kapena kulola galu ku<strong>wa</strong>nyambita<br />

nkhope zawo.<br />

• Musalole nkhumba, agalu, ndi nkhuku kukhala m’nyumba m<strong>wa</strong>nu.<br />

• Musaike zakudya za <strong>ana</strong> m’mabotolo, chifuk<strong>wa</strong> amavuta kutsuka k<strong>wa</strong>ke ndipo<br />

zikhoza kubweretsa matenda. Apatseni makanda mkaka <strong>wa</strong> m’mawere kuchokera<br />

mu kapu kapena ndi sipuni.<br />

• Gwiritsirani ntchito madzi otetezed<strong>wa</strong> kapena owiritsid<strong>wa</strong> monga akum<strong>wa</strong>. Izi<br />

nzofunikira k<strong>wa</strong>mbiri k<strong>wa</strong> makanda.<br />

Katemera<br />

Makatemera amateteza <strong>ana</strong> ku matenda ambiri<br />

amene ali owopsa k<strong>wa</strong>mbiri k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> monga chifu<strong>wa</strong><br />

chokoka mtima, diphtheria, kafumbata, matenda<br />

opu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo, chikuku ndi chifu<strong>wa</strong> chachikulu.<br />

Ana ayenera kupatsid<strong>wa</strong> makatemera<br />

osiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> miyezi yoyambirira ya <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>wo,<br />

monga tsamba 154 lasonyezera. Katemera <strong>wa</strong><br />

matenda opu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo a poliyo ayenera<br />

kupereked<strong>wa</strong> koyambilira pas<strong>ana</strong>the miyezi iwiri,<br />

chifuk<strong>wa</strong> matenda opu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo ndi ochuluka<br />

pakati pa <strong>ana</strong> osapitirira chaka chimodzi.<br />

Chitani izi<br />

Pofuna<br />

kuteteza<br />

izi<br />

katemera <strong>wa</strong> poliyo<br />

Zofunika kudzi<strong>wa</strong>: Kuti m<strong>wa</strong>na atetezedwe<br />

mok<strong>wa</strong>nira, makatemera a DPT (diphtheria, chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima, kafumbata) ndi<br />

poliyo ayenera kupereked<strong>wa</strong> kamodzi pa mwezi k<strong>wa</strong> miyezi itatu ndiponso kamodzi<br />

chaka chinacho.<br />

Kafumbata <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na wongobad<strong>wa</strong> kumene atha kupewed<strong>wa</strong> po<strong>wa</strong>patsa amayi<br />

katemera <strong>wa</strong> kafumbata pa nthawi imene iwo ali ndi pakati (onani tsamba 266).<br />

Onetsetsani <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> anu akulandira makatemera onse amene akufunikira.

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!