17.06.2013 Views

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

Kodi tingachite chiyani kuti titeteze moyo wa ana?

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

314<br />

MUTU<br />

21<br />

<strong>Kodi</strong> <strong>tingachite</strong> <strong>chiyani</strong> <strong>kuti</strong> <strong>titeteze</strong> <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong> <strong>ana</strong>?<br />

CHAKUDYA CHOPATSA THANZI, UKHONDO, KATEMERA<br />

NDIWO ATETEZI ATATU OFUNIKA KWAMBIRI AMENE AMAPATSA ANA<br />

MOYO WA THANZI NDI KUWATETEZA KU MATENDA OSIYANASIYANA.<br />

Mutu 11 ndi 12 ikukamba zambiri za ubwino <strong>wa</strong> chakudya chokhala ndi zofuna za<br />

thupi, ukhondo ndi katemera. Makolo ayenera kuwerenga mitu imeneyi mosamala<br />

ndikuigwiritsira ntchito posamalira ndi kuphunzitsa <strong>ana</strong> awo. Mfundo zikuluzikulu<br />

zabwerezed<strong>wa</strong>nso pano.<br />

Chakudya chopatsa thanzi<br />

MOYO NDI MATENDA<br />

A ANA<br />

Ndi kofunikira k<strong>wa</strong>mbiri <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> azidya chakudya chimene chili ndi zofunika zathupi<br />

chimene chingapezeke, kotero <strong>kuti</strong> adzikula bwino komanso asamad<strong>wa</strong>le.<br />

Zakudya zabwino k<strong>wa</strong>mbiri k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> a misinkhu yosiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> ndi izi:<br />

• Miyezi 4 yoyamba: mkaka <strong>wa</strong> m’mawere osatinso zina ayi.<br />

• Miyezi inayi kufikira chaka chimodzi: mkaka <strong>wa</strong> m’mawere komanso zakudya<br />

zokhala ndi zonse zofunika m’thupi monga chipere, mazira, nyama, zipatso<br />

zophika ndi ndiwo zamasamba, komanso nsima ndi mpunga.<br />

• Kuchokera chaka chimodzi kupita m’tsogolo, m<strong>wa</strong>na ayenera kudya zakudya<br />

zimene anthu akuluakulu amadya, koma pafupipafupi. Pa chakudya chathu<br />

chenicheni (mpunga, nsima ya chimanga, mawere, chinang<strong>wa</strong> kapena chimera)<br />

wonjezanipo ‘zakudya zothandizira’ monga zatchulid<strong>wa</strong> m’mutu <strong>wa</strong> 11.<br />

• Koposa zonse, <strong>ana</strong> ayenera kudya chakudya chok<strong>wa</strong>nira ndiponso kangapo pa<br />

tsiku.<br />

• Makolo onse ayenera kukhala tcheru ndi zizindikiro za kunyentchera k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> awo<br />

ndipo ayenera ku<strong>wa</strong>patsa zakudya zabwino koposa zimene angak<strong>wa</strong>nitse.


Ukhondo<br />

315<br />

Ana adzakhala ndi <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>thanzi ngati midzi, makomo ndi iwo eni akewo ali<br />

aukhondo. Tsatirani malangizo aukhondo amene ali m’mutu 12. Aphunzitseni <strong>ana</strong> anu<br />

kuzitsatira ndi kuzimvetsa ubwino <strong>wa</strong>ke. Pano malangizo ofunika k<strong>wa</strong>mbiri<br />

abwerezed<strong>wa</strong>.<br />

• Asambitseni <strong>ana</strong> anu ndi ku<strong>wa</strong>sintha zovala zawo nthawi zonse.<br />

• Aphunzitseni <strong>ana</strong> kusamba m’manja nthawi zonse pamene adzuka m’ma<strong>wa</strong>,<br />

akachoka ku chimbudzi, komanso as<strong>ana</strong>dye kapena kugwira chakudya.<br />

• Kumbani zimbudzi ndipo aphunzitseni <strong>ana</strong>wo kuzigwiritsira ntchito zimbudzizo.<br />

• Kumene kuli mahukuwemu, musalole <strong>ana</strong> anu kuyenda opanda nsapato; gwiritsirani<br />

ntchito nsapato.<br />

• Phunzitsani <strong>ana</strong> kutsuka mano ndipo musama<strong>wa</strong>patse mabisiketi ambiri, maswiti<br />

kapena zakum<strong>wa</strong> monga kokakola.<br />

• Dulani zikhadabo zawo <strong>kuti</strong> zikhale zazifupi.<br />

• Musalole <strong>ana</strong> amene ali od<strong>wa</strong>la kapena amene ali ndi zilonda, mphere, nsabwe,<br />

kapena chipere kugona ndi <strong>ana</strong> anzawo kapena kugwiritsira ntchito zovala zimodzi<br />

kapena nsalu yopuputira.<br />

• Apatseni chithandizo msanga <strong>ana</strong> amene ali ndi mphere, chipere, njoka<br />

zam’mimba, ndi matenda ena opatsir<strong>ana</strong> mosavuta kuchoka k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na wina<br />

kupita k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na m’nzake.<br />

• Musalole <strong>ana</strong> anu kuika zinthu zakuda m’kam<strong>wa</strong> kapena kulola galu ku<strong>wa</strong>nyambita<br />

nkhope zawo.<br />

• Musalole nkhumba, agalu, ndi nkhuku kukhala m’nyumba m<strong>wa</strong>nu.<br />

• Musaike zakudya za <strong>ana</strong> m’mabotolo, chifuk<strong>wa</strong> amavuta kutsuka k<strong>wa</strong>ke ndipo<br />

zikhoza kubweretsa matenda. Apatseni makanda mkaka <strong>wa</strong> m’mawere kuchokera<br />

mu kapu kapena ndi sipuni.<br />

• Gwiritsirani ntchito madzi otetezed<strong>wa</strong> kapena owiritsid<strong>wa</strong> monga akum<strong>wa</strong>. Izi<br />

nzofunikira k<strong>wa</strong>mbiri k<strong>wa</strong> makanda.<br />

Katemera<br />

Makatemera amateteza <strong>ana</strong> ku matenda ambiri<br />

amene ali owopsa k<strong>wa</strong>mbiri k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> monga chifu<strong>wa</strong><br />

chokoka mtima, diphtheria, kafumbata, matenda<br />

opu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo, chikuku ndi chifu<strong>wa</strong> chachikulu.<br />

Ana ayenera kupatsid<strong>wa</strong> makatemera<br />

osiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> miyezi yoyambirira ya <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>wo,<br />

monga tsamba 154 lasonyezera. Katemera <strong>wa</strong><br />

matenda opu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo a poliyo ayenera<br />

kupereked<strong>wa</strong> koyambilira pas<strong>ana</strong>the miyezi iwiri,<br />

chifuk<strong>wa</strong> matenda opu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo ndi ochuluka<br />

pakati pa <strong>ana</strong> osapitirira chaka chimodzi.<br />

Chitani izi<br />

Pofuna<br />

kuteteza<br />

izi<br />

katemera <strong>wa</strong> poliyo<br />

Zofunika kudzi<strong>wa</strong>: Kuti m<strong>wa</strong>na atetezedwe<br />

mok<strong>wa</strong>nira, makatemera a DPT (diphtheria, chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima, kafumbata) ndi<br />

poliyo ayenera kupereked<strong>wa</strong> kamodzi pa mwezi k<strong>wa</strong> miyezi itatu ndiponso kamodzi<br />

chaka chinacho.<br />

Kafumbata <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na wongobad<strong>wa</strong> kumene atha kupewed<strong>wa</strong> po<strong>wa</strong>patsa amayi<br />

katemera <strong>wa</strong> kafumbata pa nthawi imene iwo ali ndi pakati (onani tsamba 266).<br />

Onetsetsani <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> anu akulandira makatemera onse amene akufunikira.


316<br />

Kukula k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> komanso “msewu wopita<br />

ku <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong> thanzi”<br />

M<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>thanzi amakula mosabwerera m’mbuyo. Ngati iye adya<br />

zakudya zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi la munthu, komanso<br />

ngati alibe matenda ena aakulu, m<strong>wa</strong>na amalemera mowonjezera<br />

mwezi uliwonse.<br />

M<strong>wa</strong>na amene akukula bwino ndi <strong>wa</strong>thanzi.<br />

M<strong>wa</strong>na amene akukwera sikelo pang’onopang’ono kuyerekeza ndi <strong>ana</strong> ena, nasiya<br />

kukwera, kapena ngati akutsika, alibe <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>thanzi. Mwina iye sakudya mok<strong>wa</strong>nira<br />

kapena ali ndi matenda aakulu, kapena zonse ziwiri.<br />

Njira yabwino yodziwira ngati m<strong>wa</strong>na ali bwino komanso <strong>kuti</strong> akudya zakudya<br />

zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi ndiyo kukamukweza sikelo mwezi uliwonse ndi<br />

kuwona ngati iye akuwonjezera kulemera moyenera. Ngati kukwera sikelo k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na<br />

kusonyezed<strong>wa</strong> pa Matchati a Moyo <strong>wa</strong> M<strong>wa</strong>na, nk<strong>wa</strong>pafupi kuwona ngati m<strong>wa</strong>nayo<br />

akuwonjezera kulemera k<strong>wa</strong>ke moyenera.<br />

Atagwiritsid<strong>wa</strong> ntchito bwino, matchati adzadziwitsa amayi ndi ogwira ntchito<br />

zachipatala pamene m<strong>wa</strong>na sakukula moyenera, kotero <strong>kuti</strong> angachitepo kanthu.<br />

Akhoza kuyamba kuwonetsetsa <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na akudya mok<strong>wa</strong>nira, ndipo akhoza<br />

kumthandiza pa matenda ali wonse amene m<strong>wa</strong>na angakhale nawo.<br />

Tsamba lotsatira lili ndi Tchati cha Moyo <strong>wa</strong> M<strong>wa</strong>na chenicheni chosonyeza ‘Msewu<br />

Wopita ku Moyo <strong>wa</strong> thanzi’ Tchati chimenechi chitha kudulid<strong>wa</strong> ndi kusindikizid<strong>wa</strong>nso.<br />

Ndi chinthu chofunika k<strong>wa</strong>mbiri <strong>kuti</strong> amayi onse akhale ndi Matchati a Moyo <strong>wa</strong> Ana<br />

ake onse a zaka zosafika 5. Ngati pafupi pali chipatala chaching’ono kapena<br />

chipatala cha sikelo ya <strong>ana</strong>, mayi ayenera kupita ndi <strong>ana</strong> ake, ndi matchati awo, <strong>kuti</strong><br />

akakwezedwe pa sikelo ndikukawoned<strong>wa</strong> ngati akud<strong>wa</strong>la mwezi uliwonse. Ogwira<br />

ntchito zachipatala atha kuthandiza kufotokoza za patchati ndi kagwiritsidwe kake<br />

ntchito.<br />

Kuti musunge bwino Tchati cha Moyo <strong>wa</strong> M<strong>wa</strong>na, ikani mu enivelopu ya pulasitiki.<br />

Kukweza sikelo <strong>ana</strong> ang’onoang’ono<br />

SIKELO YOCHITA KUPANGA KUNYUMBA<br />

Mutha kupanga sikelo ndi mtengo wouma<br />

kapena nsungwi. Mlingo wolemera umene<br />

mungagwiritsire ntchito ndi thumba, botolo,<br />

kapena chitini chodzadza ndi mchenga.<br />

mbedza ziwiri zotalikir<strong>ana</strong> 5 cm<br />

sikelo yalendewera ku mbedza iyi<br />

mtengo (mtanda) wotalika 1 m<br />

choyangata<br />

(chonyamula)<br />

m<strong>wa</strong>na<br />

Kulemera k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na kumakhala<br />

kokhozeka pamene mtanda uli<br />

<strong>wa</strong>pingasa molunjika kapena<br />

mosapendekera mbali imodzi.<br />

chinthu<br />

chosunthikasunthika<br />

SIKELO YOMWE<br />

IMASONYEZA<br />

KULEMERA KWA<br />

MWANA MOSAPHEKA<br />

KAPENA MOKHOZA<br />

Chitchati cha m<strong>wa</strong>na<br />

chimaikid<strong>wa</strong> kumbuyo<br />

k<strong>wa</strong> sikelo pofuna <strong>kuti</strong><br />

munthu wolembera<br />

kulemera k<strong>wa</strong><br />

m<strong>wa</strong>nayo asonjeza<br />

mosalakwitsa<br />

chiwerengero<br />

chenicheni cha mmene<br />

m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>lemerera pa<br />

sikelopo.


AK AT E MER A TSIKU<br />

BCG<br />

MLINGO WOYAMBA<br />

MLINGO WACHIWIRI<br />

MLINGO WACHITATU<br />

POLIO<br />

TCHATI CHOSONYEZA THANZI LA<br />

MWANA<br />

KILINIKI 1……………………………………Ay i<br />

KILINIKI 2……………………………………Ay i<br />

MLINGO WACHINAI<br />

MTSIKANA<br />

MYAMATA<br />

MLINGO WOYAMBA<br />

MLINGO WACHIWIRI<br />

MLINGO WACHITATU<br />

Diptheria<br />

DPT Chif u<strong>wa</strong> chokoka<br />

mtima<br />

Kafumbata<br />

CHIKUKU<br />

SIKELA<br />

POBADWA<br />

DZINA LA<br />

MWANA<br />

TSIKU tsiku mwezi chaka<br />

LOBADWA<br />

MLINGO WOYAMBA<br />

MLINGO WACHIWIRI<br />

MLINGO WACHITATU<br />

KATEMERA WA AMAYI<br />

TOXOID<br />

DZINA LA MAI<br />

WA MWANA<br />

DZINA NGATI<br />

SIMAI WA MWANA<br />

DZINA LA BAMBO<br />

WA MWANA<br />

MWANA<br />

AMAKHALA KUTI?<br />

MADZI OBWEZERA MCHERE MTHUPI<br />

MASIKU<br />

Adaphunzitsi<br />

d<strong>wa</strong><br />

Adagwiritsa<br />

ntchito<br />

Mai <strong>wa</strong>khala ndi <strong>ana</strong> angati?............................... .............................................<br />

A<strong>moyo</strong> angati?...........................................................Ankufa angati?...............<br />

KHATI LAPEREKEDWA NDIPO<br />

MAI WAPHUNZITSIDWA NDI:<br />

SAMALI -<br />

RANI MWA<br />

PADERA<br />

FUNSANI MAI ZIFUKWA ZOTSATIRAZI NGATI NDIZO<br />

ZAPANGITSA KUTI MWANA APAT SIDWE THANDIZA<br />

LAPAD ERA (zungulizani mzere pa yankho okhonz a)<br />

Ey a<br />

Ey a<br />

Ey a<br />

Ey a<br />

Ey a<br />

Ey a<br />

Ay i<br />

Ay i<br />

Ay i<br />

Ay i<br />

Ay i<br />

Ay i<br />

<strong>Kodi</strong> m<strong>wa</strong>na <strong>ana</strong>li <strong>wa</strong> si kelo yochepera 2.5kg pobad<strong>wa</strong><br />

<strong>Kodi</strong> m<strong>wa</strong>nayu ndi <strong>wa</strong>mapasa<br />

<strong>Kodi</strong> m<strong>wa</strong>nayu amaya mwitsi dwira m’ mbotolo<br />

<strong>Kodi</strong> mai asi<strong>wa</strong> t handizo labanja lowonj ezera<br />

<strong>Kodi</strong> abale ake a m<strong>wa</strong>nayu ndi otsi ka si kelo<br />

mosavomerezeka<br />

<strong>Kodi</strong> pali zifuk<strong>wa</strong> zina zosamalitsa pa m<strong>wa</strong>nayi<br />

M<strong>wa</strong>chits anz o - chifu<strong>wa</strong> c hikulu, khate kapena mavuto a<br />

kumudzi<br />

Kumbukirani kukambir<strong>ana</strong> zakulera<br />

317<br />

Tsiku lof ika kuchipatala ________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

_________________________________ ___________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________<br />

____________________________________________________


318<br />

.


Mmene Mungagwiritsire ntchito Tchati<br />

cha Moyo <strong>wa</strong> M<strong>wa</strong>na<br />

CHOYAMBA,<br />

lembani miyezi ya<br />

chaka cho<br />

mtimabokosi<br />

ting’onoting’ono<br />

pansi pa tchati.<br />

Lembani mwezi pamene m<strong>wa</strong>na adabad<strong>wa</strong><br />

m’kabokosi koyamba m’chaka chilichonse.<br />

Tchati ichi chikusonyeza <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na adabad<strong>wa</strong> mmwezi <strong>wa</strong> Malitchi.<br />

CHACHIWIRI, kwezani m<strong>wa</strong>na pa sikelo.<br />

Tingoyerekeza <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na adabad<strong>wa</strong> mwezi <strong>wa</strong> Epulo. Tsopano ndi<br />

Ogasiti, ndipo m<strong>wa</strong>na akulemera makilogilamu 6.<br />

CHACHITATU, yang’<strong>ana</strong>ni pa khadi.<br />

Makilogalamu amalembed<strong>wa</strong> kumbali k<strong>wa</strong> khadi.<br />

Funani pamene palembed<strong>wa</strong> makilogalamu amene<br />

m<strong>wa</strong>na akulemera (M’chitsanzo ichi ndi makilogalamu 6).<br />

Sikelo<br />

yozendewera<br />

kapena ya<br />

katungw e<br />

319<br />

Kenaka fufuzani mwezi umene tilimo pansi pa tchati<br />

(m’chitsanzo chino ndi Ogasiti <strong>wa</strong> chaka choyamba cha<br />

m<strong>wa</strong>nayo).


320<br />

CHACHINAYI,<br />

tsatirani mzere umene<br />

ukuchokera ku 6<br />

ndi<br />

mizera imene ikupita<br />

ikupita mm<strong>wa</strong>mba<br />

kuchokera ku Ogasiti.<br />

Ndi kosavuta kudzi<strong>wa</strong> pamene<br />

payenera kuikid<strong>wa</strong> kadontho ngati<br />

muika kapepala kangodya zinayi<br />

kodula bwino pam<strong>wa</strong>mba pa tchati.<br />

1.<br />

Ikani malekezero<br />

amodzi a pepala<br />

motsatira mzere <strong>wa</strong><br />

kulemera k<strong>wa</strong><br />

m<strong>wa</strong>na.<br />

Mwezi uliwonse kwezani<br />

m<strong>wa</strong>na sikelo ndikuika dontho<br />

lina pa tchati.<br />

Ngati m<strong>wa</strong>na ali <strong>wa</strong>thanzi,<br />

mwezi uliwonse kadontho<br />

kodzapita m’m<strong>wa</strong>mba m<strong>wa</strong><br />

tchati kuposa mwezi<br />

<strong>wa</strong>m’mbuyo.<br />

Kuti muwone <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na<br />

akukula bwino, lumikizani<br />

timadontho ndi kamzera.<br />

Ikani ka dontho ndi<br />

kona ya pepala.<br />

2. Ikani malekezo ena a pepala<br />

wotsatira mzere <strong>wa</strong> mwezi.


Mmene Mungawerengele Tchati cha<br />

Moyo <strong>wa</strong> M<strong>wa</strong>na<br />

Mizere iwiri yokhota yomwe ili pa tchati<br />

ikusonyeza ‘Msewu Wopita ku Moyo Wathanzi’<br />

umene m<strong>wa</strong>na ayenera kuyenda.<br />

Mzere <strong>wa</strong> madontho ukusonyeza kulemera k<strong>wa</strong><br />

m<strong>wa</strong>na kuchoka mwezi umodzi kufika wina,<br />

komanso kuchokera chaka china kufika chaka<br />

chinzake.<br />

K<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> amene akukula moyenera ndi <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>thanzi, kamzera ka madontho<br />

kamayenda pakati pa mizere yaitali yokhotayo. Ndi chifuk<strong>wa</strong> chake malo amene ali<br />

pakati pa mizere iwiriyo amatched<strong>wa</strong> Msewu Wopita ku Moyo Wathanzi.<br />

Ngati kamzere ka madontho kakwera popanda kutsika, mwezi ndi mwezi, kulowera<br />

mbali imodzi monga mizere yaitali yokhotayo, ichinso ndi chizindikiro choti m<strong>wa</strong>na ali<br />

ndi thanzi.<br />

M<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>thanzi, amene amalandira chakudya chok<strong>wa</strong>nira chokhala ndi zonse<br />

zofunikira m’thupi, nthawi zambiri amayamba kukhala, kuyenda, ndi kuyankhula<br />

pafupifupi nthawi zimene zatchulid<strong>wa</strong> pansipa.<br />

Chithunzi chenicheni cha<br />

MWANA WATHANZI,<br />

WODYETSEDWA BWINO<br />

K<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong><br />

<strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>thanzi,<br />

wodyetsed<strong>wa</strong><br />

bwino, sikelo<br />

imakwera<br />

mosalekeza.<br />

Madontho nthawi<br />

zambiri amakhala<br />

m’kati m<strong>wa</strong> mizere<br />

yosonyeza Msewu<br />

Wopita ku Moyo<br />

Wathanzi.<br />

m<strong>wa</strong>na akukhala<br />

osagwiririd<strong>wa</strong><br />

m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong><br />

miyezi 6<br />

mpaka 8<br />

<strong>wa</strong>yamba kuyenda<br />

timasitepe tingapo<br />

m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong><br />

miyezi 12<br />

mpaka 16<br />

.<br />

<strong>wa</strong>yamba<br />

kulankhala<br />

nau amodzi<br />

m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong> miyezi<br />

11 mpaka 18<br />

321<br />

<strong>wa</strong>yamba kunena<br />

maganizo omweka<br />

m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong><br />

zaka zitatu


322<br />

M<strong>wa</strong>na amene sadya mok<strong>wa</strong>nira, ndi wod<strong>wa</strong>lad<strong>wa</strong>la akhoza kukhala ndi tchati<br />

monga chimene tikuchiona pansipa. Onani <strong>kuti</strong> kamzera ka madontho (kulemera<br />

k<strong>wa</strong>ke) kali pansi pa Msewu Wopita ku Moyo Wathanzi. Mzera <strong>wa</strong>kenso <strong>wa</strong> madontho<br />

ndi osokonekerasokonekera ndipo siukwera k<strong>wa</strong>mbiri. Izi zikusonyeza <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na<br />

akupita koipa.<br />

Mmene tchati cha MWANA WOSALEMERA<br />

PASIKELO NDINSO WOSOWA ZAKUDYA<br />

MTHUPI LIMAONEKERA<br />

M<strong>wa</strong>na amene ali ndi tchati ngati chili pam<strong>wa</strong>mbachi ali ndi vuto lalikulu la<br />

kusalemera. Chikhoza kukhala chifuk<strong>wa</strong> choti sakudya zok<strong>wa</strong>nira zokhala ndi zonse<br />

zofunikira m’thupi. Kapena chifuk<strong>wa</strong> choti ali ndi matenda monga chifu<strong>wa</strong> chachikulu<br />

kapena malungo. Kapenanso zonse ziwiri. Ayenera kupatsid<strong>wa</strong> chakudya chokhala ndi<br />

zonse zofunikira m’thupi chimene chilipo, ndiponso ngati kuli kotheka, ayenera<br />

kumutengera k<strong>wa</strong> munthu wogwira ntchito zachipatala pafupipafupi kufikira tchati chake<br />

chitayamba kusonyeza <strong>kuti</strong> <strong>wa</strong>yamba kulemera ndi kubwerera ku Msewu Wopita ku<br />

Moyo Wathanzi.<br />

Chofunikira: Khalani tcheru komwe kamzere ka madontho kakulowera.<br />

ZOOPSA: M<strong>wa</strong>nayu sakuwonjezera sikelo yake.<br />

Ngakhale madontho a<br />

m<strong>wa</strong>nayu adakali m’kati<br />

m<strong>wa</strong> mizera yaitali<br />

yokhota, m<strong>wa</strong>nayu<br />

sakukwera bwino k<strong>wa</strong><br />

miyezi yochuluka.<br />

ALI BWINO! M<strong>wa</strong>nayu akukwera bwino sikelo.<br />

Ngakhale <strong>kuti</strong> madontho a<br />

m<strong>wa</strong>nayu ali kunsi k<strong>wa</strong>mizere<br />

ikuluikulu yokhota iwiriyo, kupita<br />

k<strong>wa</strong>wo m’m<strong>wa</strong>mba kukusonyeza<br />

<strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na akukula bwino.<br />

M<strong>wa</strong>chilengedwe, <strong>ana</strong> ena<br />

amakhala aang’ono matupi kuposa<br />

ena. Mwinanso makolo a m<strong>wa</strong>nayu<br />

ndi aang’ono kathupi kuposa<br />

mmene zimayenera kukhalira.<br />

Kumene madontho akulowelera kumatiuza zambiri za <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na kuposa ngati<br />

madontho ali m’kati kapena kunsi k<strong>wa</strong> mizere yokhotayo. Monga chitsanzo, onani<br />

tsamba lotsatirali.<br />

.<br />

Madontho akusonyeza <strong>kuti</strong><br />

kulemera kapena sikelo ya<br />

m<strong>wa</strong>nayu yakhala<br />

isakukwera <strong>moyo</strong>nera ndipo<br />

pa miyezi yapitayi m<strong>wa</strong>nayu<br />

<strong>wa</strong>taya kulemera k<strong>wa</strong>ke.


TCHATI CHA MOYO WA MWANA CHOSONYEZA MOYO WENIWENI WA MWANA<br />

M<strong>wa</strong>nayu <strong>ana</strong>li <strong>wa</strong>thanzi Ali ndi miyezi 6, mayi Ali ndi miyezi 10 <strong>ana</strong>yamba Ali ndi miyezi 13<br />

ndipo amakwera bwino sikelo adapezekanso ali od<strong>wa</strong>la ndipo kutsekula m’mimba ndipo mayi ake adaphunzira<br />

miyezi yoyambirira 6 ya <strong>moyo</strong> adasiya kumuyamwitsa. Adayambanso kutsika sikelo. Ubwino wompatsa<br />

<strong>wa</strong>ke, chifuk<strong>wa</strong> choti mayi M<strong>wa</strong>na adayamba kudya tinthu adawonda ndi kud<strong>wa</strong>la chakudya choyenera.<br />

ake ankamuyamwitsa. tosak<strong>wa</strong>nira monga chimanga k<strong>wa</strong>mbiri. Sikelo yake inayamba<br />

ndi mpunga. Adasiya kuwonjezera kukwera msanga. Ali<br />

kulemera. ndi zaka ziwiri <strong>ana</strong>li<br />

akuyam<strong>wa</strong><br />

akunenepa<br />

bwino<br />

kusiy<strong>ana</strong> kuyamba<br />

pa miyezi 6<br />

sakudya<br />

bwino<br />

sikelo ikukwera<br />

pang’ono<br />

kutsekula m’mimba<br />

kuyambika pa<br />

miyezi 10<br />

akuwonda<br />

akutsekula<br />

m’mimba<br />

kudya zakudya zathanzi<br />

kuyambika pa miyezi 13<br />

ali pa msewu Wopita<br />

ku Moyo <strong>wa</strong> Thanzi.<br />

akunenepa<br />

bwino<br />

Matchati osonyeza <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na ndi ofunika. Atagwiritsid<strong>wa</strong> ntchito bwino,<br />

amathandiza amayi kudzi<strong>wa</strong> pamene <strong>ana</strong> awo akufunikira k<strong>wa</strong>mbiri zakudya<br />

za kasinthasintha ndi chisamaliro chapadera. Amathandiza ogwira ntchito za<br />

chipatala kumvetsa bwino zoso<strong>wa</strong> za m<strong>wa</strong>na ndi banja lake. Zimathandizanso mayi<br />

kudzi<strong>wa</strong> pamene <strong>wa</strong>chita ntchito yotamandika.<br />

323<br />

wodyetsed<strong>wa</strong><br />

bwino


324<br />

Kubwereza: Mavuto pa<strong>moyo</strong> <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na amene<br />

afotokozed<strong>wa</strong> m’mitu ina<br />

Ambiri m<strong>wa</strong> matenda takambir<strong>ana</strong> m’mitu ina ya buku lino amapezeka ndi <strong>ana</strong>. Pano<br />

ena m<strong>wa</strong> mavuto obwera kawirikawiri abwerezed<strong>wa</strong>nso m<strong>wa</strong>chidule. Kuti mudziwe<br />

zambiri pa vuto lililonse, onani masamba osonyezed<strong>wa</strong>.<br />

Kuti mudziwe kasamalidwe kapadera ndiponso zovuta za <strong>ana</strong> ongobad<strong>wa</strong> kumene,<br />

onani tsamba 286 kufikira 292.<br />

Kumbukirani: K<strong>wa</strong> <strong>ana</strong>, matenda amakula mofulumira. Matenda amene amatenga<br />

masiku kapena milungu yambiri <strong>kuti</strong> avulaze kapena kupha munthu <strong>wa</strong>mkulu atha<br />

kupha m<strong>wa</strong>na mawola owerengeka. Choncho, ndi bwino kudzi<strong>wa</strong> zizindikiro<br />

zoyambirira za matenda ndi kuchitapo kanthu nthawi yomweyo.<br />

Ana oso<strong>wa</strong> zakudya m’thupi<br />

Ana ambiri ndi wonyentchera chifuk<strong>wa</strong> choti sadya chakudya chok<strong>wa</strong>nira. Koma ena<br />

amanyentchera chifuk<strong>wa</strong> choti amadya zakudya zopatsa mphamvu zokha basi monga<br />

chimanga, mpunga, chinang<strong>wa</strong>, kapena nthochi, m’malo m<strong>wa</strong>kudya zakudya zomanga<br />

thupi ndi zoteteza kumatenda monga mkaka, mazira, nyama, nyemba, zipatso, ndi<br />

ndiwo zamasamba. M’maiko amene ali otentha ndi achinyontho, zakudya zosungid<strong>wa</strong><br />

zikhoza kuwonongeka, ndipo kenaka zikhoza kuwononga thanzi la <strong>ana</strong>. Kuti mumve<br />

tsatanetsatane <strong>wa</strong> zakudya zimene <strong>ana</strong> akufunikira, werengani Mutu 11, makamaka<br />

masamba 115 ndi 127. Za makanda, onani masamba 125 ndi 126.<br />

ANA AWIRIWA AKUSOWA ZAKUDYA ZOFUNIKIRA M’THUPI<br />

Vuto laling’onopo Vuto lalikulu<br />

amaoneka:<br />

wochepa<br />

wosalemera<br />

mimba<br />

yotukumuka<br />

manja owonda<br />

ndi miyendo<br />

yowonda<br />

amaoneka:<br />

wosalemera (akhoza<br />

kukhala wolemerapo<br />

chifuk<strong>wa</strong> chotupa)<br />

khungu<br />

lamadonthomadontho,<br />

lamfundu kapena<br />

tizilonda<br />

mapazi otupa


325<br />

Kuperewera k<strong>wa</strong> zakudya m’thupi kungabweretse mavuto osiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong>,<br />

kuphatikizapo a<strong>wa</strong>:<br />

Kuperewera zakudya k<strong>wa</strong>pang’ono: Kuperewera zakudya kodetsa nkha<strong>wa</strong>:<br />

• kupinimbira<br />

• kutupa mimba<br />

• kathupi kowonda<br />

• kusafuna kudya<br />

• kufowoka<br />

• kuso<strong>wa</strong> magazi<br />

• kufuna kudya zoipa<br />

• tizilonda m’mbali m<strong>wa</strong> kam<strong>wa</strong><br />

• chimfine pafupi pafupi ndi<br />

matenda ena<br />

• kuchita khungu usiku<br />

• sikelo kukwera pang’ono kapena osakwera<br />

kumene<br />

• kutupa miyendo (nthawi zinanso nkhope)<br />

• kuwonda kapena kuthothoka k<strong>wa</strong> tsitsi<br />

• kusafuna kusekerera kapena kusewera<br />

• tizilonda tam’kam<strong>wa</strong><br />

• kulephera kukula ndi nzeru moyenerela<br />

• m’maso mopanda madzi (xerosis)<br />

• khungu (tsamba 237)<br />

• madontho oderapo, tizilonda<br />

Kusiyanitsa ndi kuf<strong>ana</strong>niza k<strong>wa</strong> kunyentchera ‘kokhala ndi madzi’ (wet malnutrition)<br />

ndi ‘kosakhala ndi madzi’ (dry malnutrition), zochititsa zake, ndi kapewedwe kake<br />

zalembed<strong>wa</strong> m’matsamba a 117 ndi 118.<br />

Zizindikiro za kuperewera k<strong>wa</strong> zakudya m’thupi zimadziwika koyamba m<strong>wa</strong>na<br />

atad<strong>wa</strong>la k<strong>wa</strong>mbiri matenda monga kutsekula m’mimba kapena chikuku. M<strong>wa</strong>na<br />

amene akud<strong>wa</strong>la, kapena amene achira atad<strong>wa</strong>la, amafunikiranso zakudya zowonjera<br />

zokhala ndi zofunika zonse za thupi kuposa m<strong>wa</strong>na amene ali bwino.<br />

Pe<strong>wa</strong>ni ndi kuchiritsa matenda obwera chifuk<strong>wa</strong> choso<strong>wa</strong> zakudya m’thupi<br />

po<strong>wa</strong>patsa <strong>ana</strong> anu zakudya zabwino zopatsa thanzi ndi zakudya zomanga thupi<br />

zok<strong>wa</strong>nira ndi zoteteza ku matenda, monga mkaka, mazira, nyama, nsomba,<br />

nyemba, zipatso, ndi masamba,<br />

NDIPO ADYETSENI ZIMENEZI KAWIRIKAWIRI.<br />

Kutsekula m’mimba ndi m’mimba m<strong>wa</strong> kam<strong>wa</strong>zi<br />

(Tsatanetsatane <strong>wa</strong> zonse akupezeka kuyambira tsamba 162<br />

mpaka 169.)<br />

Ngozi yaikulu k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> amene akutsekula m’mimba makamaka<br />

ngatinso akusanza ndi kutha k<strong>wa</strong> madzi m’thupi. Apatseni<br />

zakum<strong>wa</strong> zobwezeretsa madzi m’thupi (onani tsamba 161).<br />

Ngati m<strong>wa</strong>na ali oyam<strong>wa</strong>, pitirizani kumuyamwitsa, koma<br />

mupatseninso zakum<strong>wa</strong> zobwezeretsa madzi m’thupi.<br />

Ngozi yaikulu yachiwiri k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> amene akutsekula m’mimba ndi<br />

kunyentchera. Mupatseni m<strong>wa</strong>na chakudya chokhala ndi zonse<br />

zofunikira m’thupi akangoyamba kudya.<br />

Kutentha k<strong>wa</strong> thupi (onani tsamba 77)<br />

K<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> aang’ono kutentha thupi (koposa madigiri 39) kukhoza<br />

kuyambitsa khunyu kapena kuwononga bongo. Ngati kutentha<br />

thupi kuli kocheperapo, mvuleni zovala m<strong>wa</strong>na. Ngati akulira ndi<br />

kusonyeza kusakond<strong>wa</strong>, mupatseni mankh<strong>wa</strong>la ochepetsa ululu a<br />

acetaminophen (paracetamol) kapena aspirin pa mlingo woyenera<br />

(onani tsamba 393), ndipo mupatseninso zakum<strong>wa</strong> zochuluka.<br />

Ngati <strong>wa</strong>tentha k<strong>wa</strong>mbiri ndipo akunjenjemera, mziziritseni ndi<br />

madzi (osati ozizira kapena otentha) ndipo mkupizeni.


326<br />

Kuphiriphitha ngati wog<strong>wa</strong> khunyu (onani tsamba 188)<br />

Kawirikawiri zochititsa kuphiriphitha ngati wog<strong>wa</strong> khunyu<br />

ndiponso kutentha thupi k<strong>wa</strong>kukulu ndi malungo, kufa zi<strong>wa</strong>lo<br />

ndi matenda oumitsa khosi. Ngati thupi litentha k<strong>wa</strong>mbiri,<br />

chepetsani kutenthako m<strong>wa</strong>changu (tsamba 77). Khalani<br />

tcheru ndi zizindikiro za kutha madzi k<strong>wa</strong> m’thupi<br />

(tsamba 160) ndi matenda oumitsa khosi (a kakhosi,<br />

tsamba 195). Kuphiriphitha kumene kumadza m<strong>wa</strong>dzidzidzi<br />

popanda kutentha thupi kapena zizindikiro zina zili zonse ndi khunyu limenelo<br />

(tsamba 188), makamaka ngati m<strong>wa</strong>na akhala ali bwinobwino akadzidzimuka<br />

pamenepo. Zizindikiro za khunyu kapena kuuma k<strong>wa</strong> mafupa a m’zib<strong>wa</strong>no kenaka<br />

thupi lonse kungathe kukhala matenda a kafumbata (tsamba 192).<br />

Matenda oumitsa khosi (Meningitis, tsamba 195)<br />

Nthenda yowopsa imeneyi ingathe kubwera chifuk<strong>wa</strong> cha<br />

chikuku kapene matenda ena aakulu. Ana a mayi amene ali<br />

ndi chifu<strong>wa</strong> chachikulu akhoza kud<strong>wa</strong>la matenda oumitsa<br />

khosi ogwiriz<strong>ana</strong> ndi matendawo. M<strong>wa</strong>na amene <strong>wa</strong>d<strong>wa</strong>la<br />

k<strong>wa</strong>mbiri ndipo akungolira ndi kumaku<strong>wa</strong>, ndi mutu <strong>wa</strong>ke<br />

wogadamitsa, amene khosi lake lili louma g<strong>wa</strong> kulephera<br />

kulipindira kutsogolo, komanso amene thupi lake likusuntha<br />

mozizwitsa (zizindikiro za khunyu) atha kukhala ndi matenda oumitsa khosi a meningitis.<br />

Matenda a kuchepa k<strong>wa</strong> magazi m’thupi (tsamba 129)<br />

Zizindikiro zodziwika msanga m<strong>wa</strong> <strong>ana</strong>:<br />

• thupi la mbee lowonetsa <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na alibe magazi, makamaka<br />

m’kati m<strong>wa</strong> zikope za maso, nkam<strong>wa</strong>, ndi zikhadabo<br />

• ndi ofowoka, amatopa msanga<br />

• amakonda kudya zinthu zoipa<br />

Zomwe zimayambitsa kawirikawiri:<br />

• malungo (tsamba 181)<br />

• matenda aja obad<strong>wa</strong> nawo a kuchepa k<strong>wa</strong> magazi (tsamba 336)<br />

• zakudya zosakhala ndi chakudya chimene chimabweretsa<br />

magazi m’thupi monga chiwindi (tsamba129)<br />

• matenda osatha a zilonda zam’mimba ndi m’matumbo (zitsanzo<br />

zili pa tsamba 151)<br />

Kupe<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong>ke ndi chithandizo:<br />

• Sinthani madyedwe pochulukitsa zakudya zobweretsa magazi<br />

m’thupi monga nyemba, mtedza ndi ndiwo zamasamba obiriwira; wonjezeranipo<br />

nyama, chiwindi ndi mazira ngati kuli kotheka.<br />

• Mupatseni mankh<strong>wa</strong>la a malungo <strong>kuti</strong> apewe, kapena kuchiritsa, malungo.<br />

• Pitani naye k<strong>wa</strong> ogwira ntchito zachipatala <strong>kuti</strong> akawone ngati akud<strong>wa</strong>la matenda<br />

aakulu ochokera k<strong>wa</strong> makolo a kuchepa magazi m’thupi, ndi matenda ena aliwonse<br />

omwe angakhale nawo, m<strong>wa</strong>chitsanzo matenda a mchikhodzodzo.<br />

• Ngati kuli koyenera mupatseni mankh<strong>wa</strong>la ochita kum<strong>wa</strong> a mchere obweretsa<br />

magazi m’thupi (tsamba 406), koma osati k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na yemwe akud<strong>wa</strong>la akud<strong>wa</strong>la<br />

matenda aakulu ochokera k<strong>wa</strong> makolo a kuchepa magazi m’thupi. Afunikira<br />

mankh<strong>wa</strong>la okhala ndi mbali ya vitamini B amene amathandiza kuchulukitsa magazi<br />

ofiira (folic acid) ndi mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> kapena kuletsa malungo (tsamba 336).<br />

• Zitavutitsitsa kukalandira magazi kuchipatala kungafunikire.<br />

Chenjezo: Osapereka mibulu ya ayironi k<strong>wa</strong> khanda kapena k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>mng’ono. Akhoza<br />

kumud<strong>wa</strong>litsa k<strong>wa</strong>mbiri kapena kumupha. Mupatseni iron <strong>wa</strong> madzimadzi;<br />

kapena sinjani mbulu ukhale ngati ufa ndipo sakanizani ndi chakudya.


327<br />

Njoka za m’mimba ndi mmatumbo ndi zilombo zina (onani tsamba 146)<br />

Ngati m<strong>wa</strong>na mmodzi m’banja ali ndi njoka zam’mimba, banja lonse liyenera kulandira<br />

mankh<strong>wa</strong>la. Kupe<strong>wa</strong> kukhala ndi njoka zam’mimba, <strong>ana</strong> ayenera:<br />

• Kutsata malangizo aukhondo (tsamba 138).<br />

• Kugwiritsira ntchito zimbudzi.<br />

• Kusayenda opanda nsapato.<br />

• Kusadya nyama yaiwisi kapena yosapsa.<br />

• Kum<strong>wa</strong> madzi okha owiritsa kapena otetezed<strong>wa</strong>.<br />

Mavuto a pakhungu (onani Mutu 15)<br />

Odziwika k<strong>wa</strong>mbiri pakati pa <strong>ana</strong> akuphatikizapo a<strong>wa</strong>:<br />

• Mphere (tsamba 211).<br />

• Matenda a zilonda ndi impetigo (tsamba 213 ndi 214).<br />

• Chipere ndi matenda ena obwera ndi tizilombo totched<strong>wa</strong><br />

fungus (tsamba 217).<br />

Kuti mupewe matenda apakhungu, tsatirani malangizo a za<br />

ukhondo (tsamba 138).<br />

• Sambitsani ndi ku<strong>wa</strong>chotsa nsabwe <strong>ana</strong> anu nthawi zonse.<br />

• Chotsani utitiri, nsabwe ndi mphere.<br />

• Musalole <strong>ana</strong> amene ali ndi mphere, nsabwe, chipere, kapena matenda opatsir<strong>ana</strong> a<br />

zilonda kusewera kapena kugona limodzi ndi <strong>ana</strong> ena. Apatseni chithandizo<br />

m<strong>wa</strong>msanga.<br />

Matenda a maso (Conjunctivitis) (onani tsamba 230)<br />

Thirani m’kati m<strong>wa</strong> zikope za diso mankh<strong>wa</strong>la a madzi<br />

olimb<strong>ana</strong> ndi kuwononga tizilombo toyambitsa matenda k<strong>ana</strong>yi<br />

pa tsiku. Musalole m<strong>wa</strong>na amene <strong>wa</strong>d<strong>wa</strong>la maso kusewera<br />

kapena kugona limodzi ndi anzake. Ngati sakupezabe bwino<br />

k<strong>wa</strong> masiku angapo, kawonaneni ndi adotolo.<br />

Chimfine ndi flu (onani tsamba 172)<br />

Chimfine, chotsag<strong>ana</strong> ndi mamina, kutentha thupi<br />

pang’ono, kutsokomola, nthawi zambiri ndi zilonda<br />

zapakhosi, nthawi zinanso ndi kutsekula m’mimba ndi<br />

matenda obwera kawirikawiri k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> koma si <strong>kuti</strong> ndi<br />

owopsa k<strong>wa</strong>mbiri.<br />

Athandizeni po<strong>wa</strong>patsa aspirin kapena paracetamol (tsamba 393) ndi zakum<strong>wa</strong><br />

zochuluka. Aloleni <strong>ana</strong> amene akugonabe kutero. Chakudya chabwino ndi zipatso<br />

zochuluka zimathandiza <strong>ana</strong> kupe<strong>wa</strong> chimfine ndi kukhalanso bwino msanga.<br />

Penicillin, tetracycline, ndi mankh<strong>wa</strong>la ena olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo toyambitsa<br />

matenda sathandiza konse ku matenda a chimfine kapena ‘flu’. Majekeseni safunikira<br />

pa matenda a mtundu <strong>wa</strong> chimfine.<br />

Ngati m<strong>wa</strong>na amene ali ndi chimfine ad<strong>wa</strong>la k<strong>wa</strong>mbiri, kutentha thupi k<strong>wa</strong>mbiri ndi<br />

kupuma cham’katikati, komanso pafupipafupi, atha kukhala <strong>kuti</strong> chibayo<br />

chikulowererapo (onani tsamba 180), ndipo mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo<br />

ayenera kupereked<strong>wa</strong>. Khalaninso tcheru ndi matenda a m’khutu (onani tsamba<br />

lotsatira) kapena mtundu wina <strong>wa</strong> zilonda zapakhosi (tsamba 329). Pitani kuchipatala.


328<br />

Matenda ena a <strong>ana</strong> amene s<strong>ana</strong>fotokozedwe m’mitu ina<br />

Kupweteka k<strong>wa</strong> khutu ndi matenda a khutu<br />

Matenda a m’khutu ndi ochuluka pakati pa <strong>ana</strong> aang’ono.<br />

Matenda<strong>wa</strong> amayamba patatha masiku pang’ono m<strong>wa</strong>na<br />

akud<strong>wa</strong>la chimfine. Kutentha k<strong>wa</strong> thupi kutha kukula, ndipo<br />

m<strong>wa</strong>na nthawi zambiri amangolira kapena amangosisita mbali<br />

ina ya mutu <strong>wa</strong>ke. Nthawi zina mafinya akhoza kuwonekera<br />

mkhutu. K<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> aang’ono, matenda a mkhutu atha<br />

kuyambitsa matenda otsekula m’mimba. Choncho ngati<br />

m<strong>wa</strong>na ad<strong>wa</strong>la matenda otsekula m’mimba ndi kutentha<br />

thupi, onetsetsani <strong>kuti</strong> muli tcheru ndi makutu ake.<br />

Chithandizo:<br />

• Ndi kofunikira kuchiritsa matenda a m’khutu mofulumira.<br />

Perekani mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo toyambitsa matenda monga<br />

penicillin (tsamba 365) kapena co-trimoxazole (tsamba 372). K<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> osak<strong>wa</strong>nira<br />

zaka zitatu (3), ampicillin (tsamba 367) nthawi zambiri amathandiza koposa.<br />

Komanso perekani aspirin kapena p<strong>ana</strong>dolo (paracetamol) woletsa ululu.<br />

• Puputani mosamala mafinya pogwiritsira ntchito thonje, koma osatseka ndi thonje,<br />

masamba, kapena chinthu china chilichonse m’khutu.<br />

• Ana amene ali ndi mafinya amene akutuluka mkhutu ayenera kusamba kawirikawiri<br />

koma sayenera kusambira kapena kuchita masewera osambira k<strong>wa</strong> milungu iwiri<br />

kuchokera nthawi imene achirira.<br />

Kapewedwe kake:<br />

• Aphunzitseni <strong>ana</strong> anu kupuputa koma osati kumina pamene ali ndi chimfine.<br />

• Osadyetsera <strong>ana</strong> anu m’botolo – kapena ngati mutero, musalole m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>nu<br />

kum<strong>wa</strong> atagona chagada, chifuk<strong>wa</strong> mkaka utha kutaikila mmphuno ndi kuchititsa<br />

matenda a m’khutu.<br />

• Ngati mphuno za <strong>ana</strong> zitseked<strong>wa</strong>, gwiritsirani ntchito madontho a madzi a mchere<br />

ndipo kenaka yam<strong>wa</strong>ni mamina monga k<strong>wa</strong>fotokozedwera pa tsamba 173.<br />

Matenda a m’kati m<strong>wa</strong> njira ya m’khutu:<br />

Kuti tidziwe ngati njira kapena chubu chopita m’kati m<strong>wa</strong> khutu ili ndi matenda,<br />

kokani khutulo pang’ono. Ngati kutero kukuchititsa kumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong>, ndiye <strong>kuti</strong> njirayo<br />

ndi yod<strong>wa</strong>la. Donthezeranimo mkhutu madzi a viniga katatu kapena k<strong>ana</strong>yi pa tsiku.<br />

(Sakanizani supuni imodzi ya viniga ndi sipuni imodzi ya madzi owiritsid<strong>wa</strong>.) Ngati pali<br />

kutentha thupi kapena mafinya, gwiritsiraninso ntchito mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi<br />

tizilombo toyambitsa matenda.<br />

Matenda a mtundu <strong>wa</strong> zilonda zapakhosi (tonsils ndi sore throat)<br />

Mavuto amene<strong>wa</strong> amayambika chifuk<strong>wa</strong> cha chimfine.<br />

Kummero kukhoza kufiira ndi kumapweteka pamene m<strong>wa</strong>na<br />

ameza. Nsungu ziwiri (zikuwoneka ngati mawuma mbali<br />

zonse ziwiri kumbuyo k<strong>wa</strong> mmero) zikhoza kukula ndi<br />

kupweteka kapenanso kutulutsa mafinya. Thupi litha kutentha<br />

kufika madigiri 40 o .<br />

Chithandizo:<br />

• Tsukani ndi madzi ofunda k<strong>wa</strong>mbiri a mchere (supuni<br />

imodzi ya mchere mu kapu ya galasi ya madzi).<br />

• Amwetseni aspirin kapena paracetamol wothetsa ululu.<br />

• Ngati kumva ululu ndi kutentha thupi kubwera m<strong>wa</strong>dzidzidzi<br />

kapena kupitilira kuposa masiku atatu, onani masamba<br />

otsatira.


329<br />

Zilonda zapakhosi ndi zotsatira za kumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> m’nkhongono ndi minye<strong>wa</strong><br />

kapena <strong>kuti</strong> minofu (rheumatic fever):<br />

K<strong>wa</strong> zilonda zimene zimabwera limodzi ndi chimfine kapena (ving<strong>wa</strong>ng<strong>wa</strong>) fuluwenza,<br />

mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo toyambitsa matenda sayenera kugwiritsid<strong>wa</strong><br />

ntchito chifuk<strong>wa</strong> palibe chabwino chimene angabweretse. M’mwetseni wod<strong>wa</strong>la madzi<br />

ofunda k<strong>wa</strong>mbiri a mchere ndi p<strong>ana</strong>dolo (paracetamol) kapena aspirin.<br />

Komabe, mtundu umodzi <strong>wa</strong> zilonda zapakhosi wotched<strong>wa</strong> strep throat uyenera<br />

kuchiritsid<strong>wa</strong> ndi penicillin. Umapezeka k<strong>wa</strong>mbiri pakati pa <strong>ana</strong> ndi anyamata<br />

ang’onoang’ono. Umayamba m<strong>wa</strong>dzidzidzi ndi vuto lalikulu la zilonda zapakhosi ndi<br />

kutentha thupi, nthawi zambiri popanda zizindikiro za chimfine kapena chifu<strong>wa</strong>.<br />

Kumbuyo k<strong>wa</strong> mkam<strong>wa</strong> ndi mmero zikhoza kufiira k<strong>wa</strong>mbiri ndipo nsungu zimene ili<br />

kunsi k<strong>wa</strong> mafupa a zib<strong>wa</strong>no zikhoza kutupa ndi kufe<strong>wa</strong>.<br />

Perekani penicillin (tsamba 365) kufikira masiku khumi (10). Mankh<strong>wa</strong>la a penicillin<br />

atapereked<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>msanga ndi kupitiriza kufikira masiku 10, mpata woti nkud<strong>wa</strong>la<br />

matenda a kumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> mnkhongono ndi minye<strong>wa</strong> ya minofu (rheumatic fever)<br />

n’ngochepa. M<strong>wa</strong>na amene akud<strong>wa</strong>la strep throat ayenera kudyera ndi kugona patali<br />

ndi anzake, kupe<strong>wa</strong> <strong>kuti</strong> enawo angatengeko matendawo.<br />

Matenda akumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> ndi kuwotcha malo okum<strong>ana</strong> mafupa ndi<br />

m’minofu (Rheumatic fever)<br />

Matenda<strong>wa</strong> ndi a <strong>ana</strong> ndi anyamata ang’onang’ono. Amayamba mlungu umodzi<br />

kufikira itatu chiyambireni kud<strong>wa</strong>la strep throat (onani m’m<strong>wa</strong>mbamu).<br />

Zizindikiro zikuluzikulu (nthawi zambiri zitatu kapena zinayi za zizindikiro<br />

zimenezi zingawonedwe):<br />

• Kutentha k<strong>wa</strong> thupi.<br />

• Kumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> m’malo okum<strong>ana</strong> mafupa,<br />

makamaka manja, mawondo ndi m’nkhongono.<br />

Malo<strong>wa</strong> amatupa ndipo nthawi zambiri amawotcha.<br />

• Zotupa pansi pa khungu.<br />

• Pamene vutoli lafika poipa, kufowoka, kusapuma<br />

mok<strong>wa</strong>nira, kapenanso kumamva ululu mumtima.<br />

Chithandizo:<br />

• Ngati mukuganiza <strong>kuti</strong> ndi matenda akumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> ndi kuwotcha malo okum<strong>ana</strong><br />

mafupa ndi minye<strong>wa</strong> ya minofu (rheumatic fever), kawonaneni ndi adotolo. Pali<br />

ngozi yoti mtima utha kuwononged<strong>wa</strong>.<br />

• Im<strong>wa</strong>ni aspirin <strong>wa</strong>mbiri (tsamba 392). M<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong> zaka 12 atha kum<strong>wa</strong> mapiritsi<br />

awiri kapena tatu a ma miligalamu 300. Nthawi zok<strong>wa</strong>na 6 pa tsiku. Apatseni<br />

limodzi ndi mkaka kapena chakudya kupe<strong>wa</strong> kumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> m’mimba. Ngati<br />

makutu ayamba kumva kulira ngati beru, im<strong>wa</strong>ni pang’ono.<br />

• Perekani penicillin, mapiritsi a mayunitsi 400,000, piritsi limodzi k<strong>ana</strong>yi pa tsiku<br />

k<strong>wa</strong> masiku ok<strong>wa</strong>na khumi (10) (onani tsamba 365).<br />

Mapewedwe ake:<br />

• Kuti mupewe matenda<strong>wa</strong>, chiritsani ‘strep throat’ m<strong>wa</strong>msanga ndi penicillin k<strong>wa</strong><br />

masiku khumi.<br />

• Kupe<strong>wa</strong> matenda akumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> ndi kuwotcha m’malo okum<strong>ana</strong> mafupa ndi<br />

minye<strong>wa</strong> ya minofu kubwereranso, komanso kupe<strong>wa</strong> kuwonjezera kuwonongeka<br />

k<strong>wa</strong> mtima, ayenera kum<strong>wa</strong> penicillin k<strong>wa</strong> masiku khumi pamene awona zizindikiro<br />

za zilonda zapakhosi. Ngati asonyeza ndikale zizindikiro za kuwonongeka k<strong>wa</strong><br />

mtima, ayenera kum<strong>wa</strong> penicillin mosadukiza kapena kulandira majekeseni okhala<br />

ndi benzathine penicillin (tsamba 367) kapena <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>ke wonse. Tsatirani<br />

malangizo opereked<strong>wa</strong> ndi ogwira ntchito zachipatala kapena dotolo.


330<br />

Matenda a <strong>ana</strong> ofalitsid<strong>wa</strong> ndi tizilombo<br />

Katsabola (Chickenpox)<br />

Matenda<strong>wa</strong> amayamba milungu iwiri kapena itatu kuchokera<br />

nthawi imene m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>khudz<strong>ana</strong> ndi mnzake amene ali ndi<br />

matenda<strong>wa</strong>.<br />

timadontho,<br />

matuza ndi<br />

Zizindikiro:<br />

ipsera<br />

Poyambirira, timadontho ting’onoting’ono tofiira ndi toyab<strong>wa</strong><br />

timawonekera. Iti timasintha ndikuwoneka ngati ziphuphu,<br />

kenaka matuza, kalikonse ngati dontho la madzi pa khungu. Izi<br />

zimakula ndipo kenako zimapanga tizipsera. Timayambira<br />

kums<strong>ana</strong> kapena kutsogolo k<strong>wa</strong> thupi, kenako pa nkhope,<br />

manja ndi miyendo. Pakhoza kukhala madontho, matuza ndi<br />

tizipsera, zonse nthawi imodzi. Kutentha k<strong>wa</strong> thupi<br />

kumakhalapo pang’ono chabe.<br />

Chithandizo:<br />

Matenda<strong>wa</strong> amatha mlungu umodzi. Msambitseni m<strong>wa</strong>na tsiku lirilonse ndi sopo ndi<br />

madzi ofunda. Dulani zikhadabo zawo <strong>kuti</strong> zikhale zazifupi k<strong>wa</strong>mbiri. Ngati zipsera<br />

zigwid<strong>wa</strong> ndi matenda, pakani mankh<strong>wa</strong>la otched<strong>wa</strong> gentian violet kapena mankh<strong>wa</strong>la<br />

olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo.<br />

Chikuku<br />

Matenda obwera ndi mavairasi oipitsitsa<strong>wa</strong> ndi owopsa k<strong>wa</strong>mbiri<br />

k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> amene ndi osadyetsed<strong>wa</strong> bwino kapena ali ndi chifu<strong>wa</strong><br />

chachikulu. Patapita masiku khumu chikhalire pafupi ndi munthu<br />

yemwe akud<strong>wa</strong>la chikuku, zizindikiro za chimfine, kutentha thupi,<br />

kuchita mamina, zilonda za mmaso, ndi kukosomola zimawoneka<br />

monga chiyambi cha chikuku.<br />

Matenda a m<strong>wa</strong>na amakulirakulira. Mlomo <strong>wa</strong>ke ukhoza kukhala<br />

ndi zilonda zambirimbiri ndipo atha kuyamba kutsekula m’mimba.<br />

Patatha masiku atatu a kutentha thupi, pamatuluka totupatupa tating’onoting’ono<br />

k<strong>wa</strong>mbiri kapena ziwengo, poyambirira pachipumi ndi m’khosi, kenako nkhope yonse,<br />

thupi ndi manja ndi miyendo. Poyambirira totupati ndi tovuta <strong>kuti</strong>ona pa khungu lakuda.<br />

Khalani tcheru ndi kukhakhala k<strong>wa</strong> khungu pamene ku<strong>wa</strong>la kug<strong>wa</strong> pa m<strong>wa</strong>nayo<br />

kuchokera mbali imodzi. Totupato tikatuluka m<strong>wa</strong>na amayamba kumva bwino. Kunyala<br />

kumayambika, tizipsera toyera timawonekera, koma khungu lake limabweleranso<br />

akachira. Nthawi zina, kuwonjezera pa tizotupatupa toyembekezereka ngati madontho<br />

akuda patalipatali obwera chifuk<strong>wa</strong> cha magazi oyendelera pa khungu angawoneke<br />

(‘chikuku chakuda’). Izi zimasonyeza <strong>kuti</strong> matendawo ndi aakulu, ndipo mavuto ena<br />

angabukepo, komanso zitenga nthawi yaitali <strong>kuti</strong> achire kotheratu. Kafuneni<br />

chithandizo cha mankh<strong>wa</strong>la ku chipatala.<br />

Mavuto amene angabukepo:<br />

K<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na aliyense amene ali ndi chikuku amakhala ndi mphamvu yochepa<br />

yoziteteza ku matenda ena, monga chibayo, kam<strong>wa</strong>zi, matenda a m’khutu, zithupsa<br />

(makamaka minofu yozungulira mafupa a m’mutu), ndi zilonda zam’mutu, komanso<br />

m’kati m<strong>wa</strong> diso. Zilonda zamkam<strong>wa</strong> zimachititsanso <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na asafune kudya.<br />

Zimene zili m’diso, kupanda kulandira chithandizo, zingayambitse khungu. Kuso<strong>wa</strong><br />

k<strong>wa</strong> zakudya m’thupi nthawi zambiri kumatsatira chikuku, ndipo chifu<strong>wa</strong> chachikulu<br />

chinga dziwike, kudzera mu kutsika k<strong>wa</strong> sikelo, komanso kutu<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> khungu.<br />

Chithandizo:<br />

• M<strong>wa</strong>na ayenera kugoneked<strong>wa</strong>, kum<strong>wa</strong> zakum<strong>wa</strong> zambirimbiri, ndipo apatsidwe<br />

chakudya chokhala ndi zonse zofunikira m’thupi. Ngati m<strong>wa</strong>na sangathe kuyam<strong>wa</strong>,<br />

mpatseni mkaka <strong>wa</strong> m’mawere pa supuni (tsamba 125).


331<br />

• Ngati iye akutentha thupi komanso kumva kukhala wosatakasuka, mupatseni<br />

p<strong>ana</strong>dolo (paracetamol) kapena aspirin.<br />

• Ngati ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> khutu kuyamba, mupatseni mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha<br />

tizilombo toyambitsa matenda (tsamba 365).<br />

• Ngati zizindikiro za chibayo, matenda oumitsa khosi, kapena ululu <strong>wa</strong>mphamvu<br />

m’khutu kapena m’mimba uyamba, kalandireni chithandizo kuchipatala.<br />

• Chithupsa chiyenera kutumbulid<strong>wa</strong> (tsamba 214).<br />

Kapewedwe kake ka chikuku:<br />

Ana od<strong>wa</strong>la chikuku asasakanikirane ndi <strong>ana</strong> ena, chifuk<strong>wa</strong> matenda<strong>wa</strong> amafalikira<br />

msanga. Ngakhale <strong>ana</strong> ena a m’banja lomwelo ayenera kukhala pafupi ndi od<strong>wa</strong>lawo<br />

mphindi pang’ono k<strong>wa</strong>mbiri. Komabe nawo adzad<strong>wa</strong>la chikuku masiku 10 kapena 14<br />

obwerawo, ndipo kuchuluka k<strong>wa</strong> nthawi imene <strong>ana</strong>li pafupi ndi od<strong>wa</strong>la chikuku<br />

kudzatanthauza kud<strong>wa</strong>la kodetsa nkha<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> iwo. Choncho yesetsani ku<strong>wa</strong>lekanitsa.<br />

Ana enawo agone k<strong>wa</strong>wokha kufikira wod<strong>wa</strong>la chikukuyo alibe totupatupa tija.<br />

K<strong>wa</strong>kukulu, tetezani <strong>ana</strong> amene ali oso<strong>wa</strong> zakudya zofunikira m’thupi, kapena amene<br />

ali ndi matenda ena. Chikuku chimatha kupha.<br />

Kuti chikuku chisaphe <strong>ana</strong>, onetsetsani <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> onse akudya zakudya<br />

zoyenerera ndi zok<strong>wa</strong>nira. Ana anu alandire katemera <strong>wa</strong> chikuku pamene<br />

ali ndi miyezi ya pakati pa 8 ndi 14 yakubad<strong>wa</strong>.<br />

Chikuku cha German (German measles)<br />

Chikuku cha German si chowopsa ngati chikuku <strong>wa</strong>mba. Chimatha pakati pa masiku<br />

atatu kapena <strong>ana</strong>yi. Zotupatupa zakenso ndi zapang’ono. Nthawi zambiri sungu zake<br />

kumbuyo k<strong>wa</strong> mutu ndi khosi zimatupa komanso zimafe<strong>wa</strong>. M<strong>wa</strong>na ayenera<br />

kugoneked<strong>wa</strong> ndi kum<strong>wa</strong> paracetamol kapena aspirin ngati kuli kofunika.<br />

Amayi amene ad<strong>wa</strong>la chikuku cha German miyezi itatu yoyambirira ya mimba yawo<br />

atha kubereka m<strong>wa</strong>na wosakhala bwino ndi wopu<strong>wa</strong>la. Chifuk<strong>wa</strong> cha chimenechi,<br />

amayi a pakati amene alibe chikuku cha German kapena sakudzi<strong>wa</strong> asamayandikire<br />

<strong>ana</strong> amene ali ndi matenda a mtundu umenewu.<br />

Masagwidi/Kadukutu<br />

Zizindikiro zoyamba za matenda<strong>wa</strong> zimayamba kuwoneka pakati pa milungu iwiri<br />

kapena itatu kuchokera nthawi imene m<strong>wa</strong>na <strong>ana</strong>yandik<strong>ana</strong> ndi od<strong>wa</strong>la masagwidi.<br />

Amayamba ndi kutentha k<strong>wa</strong> thupi ndi kumva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> poyasamula kapena kudya.<br />

M’masiku awiri, chotupa chofe<strong>wa</strong> chimawonekera m’munsi m<strong>wa</strong> khutu pa ngondya ya<br />

fupa la m’chib<strong>wa</strong>no. Nthawi zambiri chimayamba mbali imodzi, kenaka mbali inayo.<br />

Pomeza samva ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong>.<br />

Chithandizo:<br />

Chotupa chimatha chokha pakatha masiku pafupifupi 10, popanda<br />

mankh<strong>wa</strong>la. P<strong>ana</strong>dolo (paracetamol) kapena aspirin atha kumwetsed<strong>wa</strong><br />

kuchepetsa kutentha k<strong>wa</strong> thupi ndi ululu. Mdyetseni m<strong>wa</strong>na zakudya<br />

zofe<strong>wa</strong> ndi zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi ndipo onetsetsani <strong>kuti</strong><br />

m,kam<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>ke ndi motsuka bwino. Mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha<br />

tizilombo toyambitsa matenda si ofunika.<br />

Mavuto otsatira:<br />

K<strong>wa</strong> akuluakulu ndi <strong>ana</strong> a zaka zoposa 11, patatha mulungu umodzi<br />

akhoza kuyamba kumva ululu m’mimba, kapena atha kukhala ndi<br />

kutupa ndi kupweteka k<strong>wa</strong> machende (amuna). Anthu amene ali ndi<br />

chotupa chotere ayenera kukhala osasunthasuntha ndi kuika madzi a<br />

matalala kapena nsalu yonyowetsed<strong>wa</strong> ndi madzi ozizira m’malo<br />

otupawo kuthandiza kuchepetsa ululu ndi kutupa. Ngati zizindikiro za<br />

matenda oumitsa khosi ziwoneka, kalandireni chithandizo kuchipatala<br />

(tsamba 195).


332<br />

Chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima<br />

Chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima chimayamba pakati pa sabata imodzi kapena<br />

masabata awiri kuchokera nthawi imene m<strong>wa</strong>na <strong>ana</strong>yandik<strong>ana</strong> ndi<br />

m<strong>wa</strong>na amene ali ndi matenda<strong>wa</strong>. Amayamba ngati chimfine ndi<br />

kutentha k<strong>wa</strong> thupi, kuchita mamina, ndi kutsokomola.<br />

Masabata awiri otsatirawo kutsokomola kwenikweni kokoka mtima ndi<br />

minofu yonse (‘cough spasm’) kumayamba. M<strong>wa</strong>na amatsokomola<br />

pafupipafupi ndi nthawi zambiri popanda kupuma, kufikira atatulutsa makhololo onanda<br />

amene <strong>ana</strong>tseka kukhosi. Kutsokomolaku kumathera mu kusanza, ndipo nthawi zina<br />

ndi phokoso la kukoka k<strong>wa</strong> mtima, nthawi imene mpweya ukubwerera m’chifu<strong>wa</strong>.<br />

Nthawi imene iye sakutsokomola m<strong>wa</strong>nayo amawoneka ngati ali bwinobwino, ndipo<br />

chochititsa kutsokomola sichidziwika kufikira nthawi imene kutsokomola kokoka<br />

mtimako kuyambiranso.<br />

Chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima n’chowopsa k<strong>wa</strong>mbiri k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong> osapitirira chaka chimodzi.<br />

Sangathe kutsokomola kapena kusanza pamene agwid<strong>wa</strong> ndi matenda<strong>wa</strong>, koma<br />

amangosiya kupuma mphindi imodzi kapena ziwiri. Khungu lawo limasanduka lobiliwira<br />

(blue), ndipo atha kufa. Choncho apatseni katemera m<strong>wa</strong>changu. Ngati m<strong>wa</strong>na<br />

<strong>wa</strong>gwid<strong>wa</strong> ndi matenda otsokomola ndi maso awo atupa kapena kuwoneka ngati muli<br />

utsi pamene m’dera lanu muli mliri <strong>wa</strong> matenda a chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima, mupatseni<br />

mankh<strong>wa</strong>la a chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima nthawi yomweyo.<br />

Chithandizo:<br />

• M’masiku oyambirira a chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima, kutsokomola kus<strong>ana</strong>yambe,<br />

mankh<strong>wa</strong>la a erythromycin (tsamba 369), tetracycline (tsamba 370), kapena<br />

ampicillin (tsamba 367) atha kupereked<strong>wa</strong>. Mankh<strong>wa</strong>la a chloramphenicol<br />

amathandizanso koma ndi ochititsa ngozi. Kaperekedwe ka mankh<strong>wa</strong>la<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong>,<br />

onani tsamba 372. Ndi bwino koposa kupereka chithandizo cha mankh<strong>wa</strong>la k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong><br />

osapitirira miyezi 6 pamene zizindikiro zoyamba zikawoneka.<br />

• Zikafika povutitsitsa, mankh<strong>wa</strong>la a phenobarbital (tsamba 402) atha kuthandiza,<br />

makamaka ngati kutsokomola sikuchititsa m<strong>wa</strong>na kugona kapena ngati<br />

kukuchititsa kug<strong>wa</strong> ngati <strong>wa</strong> khunyu.<br />

• Ngati m<strong>wa</strong>na asiya kupuma atamaliza kutsokomola, mutembenuzeni ndi kuchotsa<br />

mankhololo a m’kam<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>ke ndi chala chanu. Kenaka mumenyeni mbama<br />

pams<strong>ana</strong>.<br />

• Pofuna kupe<strong>wa</strong> kutsika k<strong>wa</strong> sikelo ndi kunyentchera, m<strong>wa</strong>na ayenera kudyetsed<strong>wa</strong><br />

chakudya chokhala ndi zonse zofunikira m’thupi ndipo ayenera kudya akangomaliza<br />

kusanza.<br />

• Mankh<strong>wa</strong>la othetsa kutsokomola sathandiza. Mankh<strong>wa</strong>la a chifu<strong>wa</strong> cha asima,<br />

monga ephedrine akhoza kuchepetsa kutsokomola kokoka mtima. Kafuneni<br />

chithandizo kuchipatala ngati zili zodetsa nkha<strong>wa</strong>.<br />

• Kutsokomola k<strong>wa</strong> chifu<strong>wa</strong> chokoka mtimachi kutha kupitirira mpaka miyezi itatu<br />

kapena kupitirira, koma chithandizo cha mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo<br />

toyambitsa matenda m’thupi si chodalirika pamene sabata imodzi yadutsa, ndipo si<br />

chiyenera kubwerezed<strong>wa</strong>.<br />

Mavuto otsatira:<br />

Magazi ofiira monyezimira m’mbali zoyera za diso atha kuchititsid<strong>wa</strong> ndi<br />

kutsokomola. Chithandizo cha mankh<strong>wa</strong>la ndi chosafunikira (onani tsamba 236).<br />

Ngati kukomoka kapena zizindikiro za chibayo (tsamba 180) kapena matenda<br />

oumitsa zi<strong>wa</strong>lo (tsamba 195) zioneka, kalandireni chithandizo kuchipatala.<br />

Tetezani <strong>ana</strong> anu ku matenda a chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima. Onetsetsani<br />

<strong>kuti</strong> alandira katemera koyamba ali ndi miyezi iwiri ya kubad<strong>wa</strong>.<br />

Diphtheria<br />

Matenda<strong>wa</strong> amayamba ngati chimfine ndi kutentha thupi, ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong><br />

mutu, ndi zilonda zapakhosi. Kanthu kopyapyala komwe kamayala<br />

kapena kuteteza kummero ndi ka mtundu <strong>wa</strong>chikasu konkira ku mtundu<br />

wokhala ngati phulusa (gireyi) katha kupangid<strong>wa</strong> kunsi k<strong>wa</strong> mmero,<br />

ndipo nthawi zina m’mphuno ndi pamilomo. Khosi la m<strong>wa</strong>na litha kutupa.<br />

Mpweya umene amapuma umakhala wonunkha.


333<br />

Ngati muli ndi maganizo oti m<strong>wa</strong>na ali ndi diphtheria:<br />

• Mgonekeni mchipinda chayekha.<br />

• Kalandireni chithandizo cha kuchipatala m<strong>wa</strong>msanga. Pali mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi<br />

tizilombo toyambitsa matenda a diphtheria.<br />

• Perekani penicillin, mbulu umodzi <strong>wa</strong> mayunitsi 400,000, katatu pa tsiku k<strong>wa</strong> <strong>ana</strong><br />

akuluakulu.<br />

• Amwe madzi ofunda othira mchere pang’ono.<br />

• Mkonzereni <strong>kuti</strong> apume mpweya <strong>wa</strong> madzi otentha kawirikawiri ndi mosalekeza<br />

(tsamba 177).<br />

• Ngati m<strong>wa</strong>na ayamba kutsam<strong>wa</strong> ndi kusandulika buluwu (blue), chotsani kangaude<br />

kummero k<strong>wa</strong>ke pogwiritsa ntchito kansalu kamene m<strong>wa</strong>veka chala chanu.<br />

Diphtheria ndi nthenda yowopsa imene ingapewedwe m<strong>wa</strong>changu ndi katemera <strong>wa</strong><br />

DPT. Onetsetsani <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> anu alandira katemerayu.<br />

Poliyo (Polio, Poliomyelitis)<br />

Poliyo akupezeka k<strong>wa</strong>mbiri pakati pa <strong>ana</strong> osak<strong>wa</strong>na zaka<br />

ziwiri zakubad<strong>wa</strong>. Imabwera ndi kachilombo ka vairasi ngati<br />

kamene kamachititsa chimfine, kawirikawiri ndi kutentha<br />

k<strong>wa</strong> thupi, kusanza, kutsekula m’mimba, ndi zilonda<br />

m’minofu. Nthawi zambiri m<strong>wa</strong>na amachira kotheratu<br />

m’masiku owerengeka. Koma nthawi zina chi<strong>wa</strong>lo china<br />

chathupi chimafowoka kapena kupu<strong>wa</strong>la. Nthawi zambiri izi<br />

zimachitika ku mwendo umodzi kapena yonse iwiri.<br />

Pakapita nthawi mwendo kapena mkono wofowoka uja<br />

umawonda ndipo siukula mofulumira ngati unzake uja.<br />

Chithandizo:<br />

Matenda<strong>wa</strong> akangoyamba, palibe mankh<strong>wa</strong>la amene<br />

adzaletse kupu<strong>wa</strong>lako. (Komabe, nthawi zina mbali kapena<br />

mphamvu ina yonse imene yataika imabwerera<br />

pang’onopang’ono.) Mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi kupha<br />

tizilombo toyambitsa matenda m’thupi sathandiza. Monga<br />

chithandizo choyambirira, chepetsani ululu ndi p<strong>ana</strong>dolo<br />

(paracetamol) kapena aspirin ndipo ikani nsalu<br />

zonyowetsed<strong>wa</strong> ndi madzi otentha paminofu yo<strong>wa</strong><strong>wa</strong>yo.<br />

Mkhazikeni m<strong>wa</strong>nayo m<strong>wa</strong> njira yoti amve bwino ndi kuletsa<br />

kupinda kapena kuunjik<strong>ana</strong> k<strong>wa</strong> minofu ya zi<strong>wa</strong>lo.<br />

Pang’onopang’ono wongolani manja ake ndi miyendo kotero<br />

<strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>nayo akhale mowongoka mmene angathere. Ikani<br />

zinsalu pansi pa mawondo ake, ngati kuli kofunika <strong>kuti</strong> ululu uchepe, koma onetsetsani<br />

<strong>kuti</strong> mawondo ake ndi owongoka.<br />

Kapewedwe kake:<br />

• Katemera <strong>wa</strong> poliyo ndiye chitetezo chabwino k<strong>wa</strong>mbiri.<br />

• Musapereke jekeseni <strong>wa</strong> mankh<strong>wa</strong>la a mtundu wina uliwonse k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na amene ali<br />

ndi zizindikiro za chimfine, kutentha thupi, kapene zizindikiro zina zili zonse zimene<br />

zitha kuchititsid<strong>wa</strong> ndi vairasi ya poliyo. Ululu wochititsid<strong>wa</strong> ndi jekeseni utha<br />

kusintha poliyo yapang’ono yosapu<strong>wa</strong>litsa zi<strong>wa</strong>lo kukhala yodetsa nkha<strong>wa</strong>,<br />

yotsag<strong>ana</strong> ndi kupu<strong>wa</strong>la zi<strong>wa</strong>lo. Musabaye jekeseni <strong>wa</strong> mankh<strong>wa</strong>la ena<br />

aliwonse pokhapokha ngati kuli koyenera.<br />

Onetsetsani <strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> alandira katemera <strong>wa</strong> poliyo, <strong>wa</strong> ‘madontho a poliyo’<br />

pamene ali ndi miyezi iwiri, itatu kapena inayi yakubad<strong>wa</strong>.


334<br />

M<strong>wa</strong>na amene <strong>wa</strong>lumala chifuk<strong>wa</strong> cha poliyo ayenera<br />

kudya zakudya zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi ndi<br />

kuchita masewero olimbitsa thupi <strong>kuti</strong> minofu yotsalayo<br />

ikhale ya mphamvu.<br />

Thandizani m<strong>wa</strong>nayo kuyenda mulimonse mmene<br />

angathere. Pangani mitengo iwiri yoti adzigwira<br />

akamayenda, monga tikuwonera pano, ndipo kenako<br />

mpangireni ndodo zoyendera. Zogwirira mwendo, ndodo,<br />

ndi zipangizo zina zothandizira kuyenda zitha kuthandiza<br />

m<strong>wa</strong>na kuyenda bwino ndipo zitha kuletsa kulumala.<br />

MMENE MUNGAPANGIRE NDODO ZOYENDERA OLUMALA


Mavuto amene <strong>ana</strong> amabad<strong>wa</strong> nawo<br />

Mwendo kuchoka malo amene umakum<strong>ana</strong> ndi fupa la m’chiuno<br />

Ana ena amabad<strong>wa</strong> ndi mwendo wochoka malo ake pamene umakum<strong>ana</strong> ndi fupa la<br />

mchiuno. Izi zimachitika kawirikawiri ndi <strong>ana</strong> aakazi. Chisamaliro cha m<strong>wa</strong>msanga<br />

chitha kuthetsa vutoli ndi kutsimphina kumene kungabukepo. Choncho <strong>ana</strong> onse<br />

ayenera kuunikid<strong>wa</strong> bwino kuwona ngati ali ndi vuto la kulek<strong>ana</strong> k<strong>wa</strong> mafupa m’chiuno<br />

pamene ak<strong>wa</strong>nitsa masiku 10 chibadwireni.<br />

2. Gwirani miyendo ndipo<br />

yonse iwiri mawondo<br />

akhale pamodzi motere,<br />

1. F<strong>ana</strong>nizani miyendo iwiriyo. Ngati ntchafu imodzi siili<br />

m’malo m<strong>wa</strong>ke, mbali inayo idzasonyeza <strong>kuti</strong>:<br />

Mwendo <strong>wa</strong>m’m<strong>wa</strong>mba ukutseka mbali iyi ya thupi ku mbali<br />

imene mafupa alek<strong>ana</strong>.<br />

Minofu yapanga makwinya (tsinya) ochepa apa.<br />

Mwendo ukuwoneka <strong>wa</strong>ufupi kapena ukamasuntha pa mlingo<br />

wodabwitsa.<br />

ikhanyuleni motere<br />

(itayanitseni).<br />

Ngati mwendo umodzi<br />

umaliza usiya msanga<br />

kapena udukiza kapena<br />

umveka kulira pamene<br />

mukukhanyula<br />

(mukuitayanitsa), ndiye<br />

<strong>kuti</strong> mafupa mchiuno<br />

ngolek<strong>ana</strong>.<br />

Chithandizo:<br />

Mawondo a m<strong>wa</strong>na akhale m’m<strong>wa</strong>mba komanso okanulid<strong>wa</strong>:<br />

Pogwiritsira ntchito kapena pomangirira miyendo kapena pochita izi:<br />

motere m<strong>wa</strong>na akamagona<br />

Kugwiritsa ntchito matewera<br />

okhuthala ngati apa:<br />

Kumadera kumene amayi amatenga <strong>ana</strong> awo kotero <strong>kuti</strong> miyendo yawo imatsamira<br />

chiuno chawo, chithandizo chapadera si chofunikiranso.<br />

335


336<br />

Nthenda yobad<strong>wa</strong> nayo ya kuchepa k<strong>wa</strong> magazi m’thupi<br />

Ana ena amabad<strong>wa</strong> ‘ofowoka pa magazi’, matenda amene amatched<strong>wa</strong> sickle cell pa<br />

Chingerezi. Nthendayi imachokera k<strong>wa</strong> makolo, ngakhale <strong>kuti</strong> makolowo sadzi<strong>wa</strong> zoti<br />

ali nawo. Amakhala <strong>kuti</strong> nthendayi ali nayo m’magazi m<strong>wa</strong>wo. M<strong>wa</strong>na atha kuwoneka<br />

<strong>wa</strong>thanzi miyezi isanu ndi umodzi yoyambirira, koma zizindikiro zina zimayambano<br />

kuwoneka.<br />

Zizindikiro zake:<br />

• Kutentha k<strong>wa</strong> thupi ndi kulira. M<strong>wa</strong>na amawoneka opanda<br />

magazi, ndipo akhoza kuwonetsa mtundu <strong>wa</strong>chikasu m’maso<br />

m<strong>wa</strong>ke.<br />

• Mapazi ndi zala zake zitha kuwonetsa zotupa zimene<br />

zimabisala pakatha mulungu umodzi kapena milungu iwiri,<br />

ndipo kenaka amakhala bwino.<br />

• Mimba itha kutupa ndi kulimba chifuk<strong>wa</strong> cha kukula k<strong>wa</strong> zi<strong>wa</strong>lo<br />

za khoma la mimba kapamba (sathamagazi) ndi chiwindi.<br />

• Pamene ak<strong>wa</strong>nitsa zaka ziwiri zakubad<strong>wa</strong> mutu ukhoza<br />

kuyamba kuwonetsa mabampu mu ngondya za mafupa. Uku<br />

kumatched<strong>wa</strong> ‘bossing’ m’chingerezi.<br />

• M<strong>wa</strong>na amakhala wopanda mphamvu yodzitchinjiriza nayo ku<br />

matenda ndipo kawirikawiri amad<strong>wa</strong>la malungo, chifu<strong>wa</strong>, kutsekula m’mimba ndi<br />

matenda ena.<br />

• Amakula moched<strong>wa</strong> poyerekeza ndi <strong>ana</strong> ena.<br />

• Nthawi ndi nthawi m<strong>wa</strong>na amakhala ndi chimake cha vuto la ‘kufowoka k<strong>wa</strong><br />

magazi’, nthawi zambiri chifuk<strong>wa</strong> cha malungo , kapena matenda ena obwera<br />

chifuk<strong>wa</strong> cha tizilombo m’magazi. M<strong>wa</strong>na amatentha thupi k<strong>wa</strong>mbiri ndi kupweteka<br />

k<strong>wa</strong>mbiri m’mafupa am’manja kapena miyendo, kapenanso m’mimba. Vuto la<br />

kuso<strong>wa</strong> magazi limafika poipa mosataya nthawi. Zotupa pamafupa zitha kuyamba<br />

kutulutsa mafinya. Vutoli litha kubweretsa imfa.<br />

Chithandizo:<br />

Palibe njira imene ingachitike <strong>kuti</strong> kufowoka k<strong>wa</strong> kapangidwe ka magazi kungasinthe,<br />

koma m<strong>wa</strong>na atha kutetezed<strong>wa</strong> ku zinthu zimene zimabweretsa mavuto, ndipo<br />

payenera kukhala makonzedwe oti azikawon<strong>ana</strong> ndi anthu ogwira ntchito zachipatala<br />

mwezi ndi mwezi mosadukiza <strong>kuti</strong> azikamuunika ndikumampatsa chithandizo cha<br />

mankh<strong>wa</strong>la.<br />

1. Malungo. M<strong>wa</strong>nayo ayenera kulandira mankh<strong>wa</strong>la olimb<strong>ana</strong> ndi malungo <strong>kuti</strong><br />

nthendayi isawonekere, nthawi zambiri pogwiritsira ntchito mankh<strong>wa</strong>la a pyrimethamine<br />

kapena chloroquine (tsamba 379 ndi 381). Pa amene mankh<strong>wa</strong>la<strong>wa</strong> muyenera<br />

kuwonjezeranso mankh<strong>wa</strong>la okhala ndi gulu la mavitamini B osiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> amene<br />

amachulukitsa magazi (folic acid, tsamba 406). Mankh<strong>wa</strong>la a magazi a iron a ferrous<br />

sulfate si ofunika kwenikweni.<br />

2. Matenda obwera chifuk<strong>wa</strong> cha tizilombo tam’magazi. Tetezani m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>nu<br />

ku matenda a chikuku, chifu<strong>wa</strong> chokoka mtima, ndi chifu<strong>wa</strong> chachikulu po<strong>wa</strong>patsa<br />

katemera m<strong>wa</strong>msanga nthawi imene ili yovomerezeka. Chiritsani zizindikiro monga<br />

kutentha thupi, kutsokomola, kutsekula m’mimba, kukodza pafupipafupi, kapena<br />

ku<strong>wa</strong><strong>wa</strong> paliponse k<strong>wa</strong> m’mimba, miyendo kapena mikono, popita ndi m<strong>wa</strong>na k<strong>wa</strong><br />

ogwira ntchito zachipatala mofulumira monga mmene mungathere. Mankh<strong>wa</strong>la<br />

olimb<strong>ana</strong> ndi kupha tizilombo toyambitsa matenda atha kukhala ofunikira. Mupatseni<br />

madzi ochuluka akum<strong>wa</strong>, ndi p<strong>ana</strong>dolo (tsamba 393) pochepetsa ululu <strong>wa</strong> m’mafupa.<br />

3. Asayandikire malo ozizira. Ayenera <strong>kuti</strong> akhale malo ofunda ndipo afunde<br />

bulangeti usiku ngati kuli kofunika. Gwiritsirani ntchito matiresi ofe<strong>wa</strong> bwino ngati kuli<br />

kotheka.<br />

4. Mimba. Mayi <strong>wa</strong>chichepere ayenera kupe<strong>wa</strong> zimenezi, pokhapokha ngati kuli<br />

kotheka kukachirira kuchipatala, chifuk<strong>wa</strong> cha kukulitsa kufowoka k<strong>wa</strong> magazi<br />

k<strong>wa</strong>kukulu. Njira yakulera ya jekeseni (tsamba 312) ndiyo yovomerezeka k<strong>wa</strong> amayi<br />

amene ali ndi matenda a vuto la kapangidwe ka magazi m’thupi monga njira<br />

yotetezed<strong>wa</strong> koposa yoletsera mimba, ndipo ithanso kuchepetsa mavuto omwe<br />

angabwerepo chifuk<strong>wa</strong> cha zochititsa zina.


Kutalika mchombo<br />

Mchombo umene umatalika<br />

chotere si vuto ayi. Mankh<strong>wa</strong>la<br />

kapena chithandizo china<br />

chilichonse nzosafunikira<br />

kufupikitsira mchombo.<br />

Kumanga mimba ndi kansalu<br />

kapena lamba <strong>wa</strong> pamimba<br />

sizingathandize.<br />

Tchende lotupa (Hydrocele kapena Hernia)<br />

Ngati tchende la m<strong>wa</strong>na litupa mbali imodzi, ichi ndi chifuk<strong>wa</strong><br />

choti ladzadza madzi kapena chifuk<strong>wa</strong> choti kanthu kena kake<br />

ka mbali ya thupi kathawira kumeneko (hernia). Kuti mudziwe<br />

chochititsa chenicheni, unikani ndi nyali <strong>kuti</strong> muwone ngati<br />

ku<strong>wa</strong>la kudutsa chotupacho.<br />

Ngati ku<strong>wa</strong>la kudutsa<br />

chotupacho msangamsanga<br />

ndiye <strong>kuti</strong> m’tchendemo muli<br />

madzi (hydrocele).<br />

Madzi nthawi zambiri amachoka<br />

okha pakapita nthawi popanda<br />

chithandizo chapadera. Koma<br />

pakatha chaka chathunthu,<br />

kafuneni chithandizo ku<br />

chipatala.<br />

Ngati ku<strong>wa</strong>la sikudutsa m’katimo,<br />

komanso ngati chotupa chikula<br />

m<strong>wa</strong>na akamatsokomola kapena<br />

kulira, ndiye <strong>kuti</strong> kachi<strong>wa</strong>lo kena<br />

kake kam’thupi kathawira<br />

kumeneko (hernia).<br />

Hernia imafunika opaleshoni (onani<br />

tsamba 97).<br />

Ana oganiza moched<strong>wa</strong> (operewera), ogontha kapena<br />

opu<strong>wa</strong>la<br />

Nthawi zina makolo adzakhala ndi m<strong>wa</strong>na amene adzabad<strong>wa</strong> osamva, woganiza<br />

moched<strong>wa</strong>, kapena <strong>wa</strong> mavuto obad<strong>wa</strong> nawo (chomwe chikusonyeza china chake<br />

cholakwika pa thupi pake). Nthawi zambiri palibe chifuk<strong>wa</strong> chimene chingaperekedwe.<br />

Palibe aliyense amene ayenera kudzudzulid<strong>wa</strong>. Nthawi zambiri<br />

zimangochitika m<strong>wa</strong>ngozi.<br />

Komabe, zinthu zina zimakulitsa mpata woti m<strong>wa</strong>na abadwe ndi<br />

mavuto ena. Ndi povuta <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na abadwe ndi vuto lina lake la<br />

pathupi ngati makolo atsatira machenjezo ena ake.<br />

1. Kuso<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> zakudya zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi<br />

nthawi imene mayi ali ndi pakati kukhoza kuchititsa kuganiza<br />

moched<strong>wa</strong> kapena vuto lina lobad<strong>wa</strong> nalo lapathupi pa m<strong>wa</strong>na.<br />

Kuti mukhale ndi <strong>ana</strong> athanzi, amayi apakati ayenera kudya<br />

zakudya zokhala ndi zonse zofunikira m’thupi (tsamba 115).<br />

2. Kusoweka k<strong>wa</strong> mchere <strong>wa</strong> ayodini mu zakudya za mayi<br />

<strong>wa</strong>pakati kungabweretse vuto lina lobad<strong>wa</strong> nalo lotched<strong>wa</strong> cretinism<br />

m’chingerezi.<br />

337<br />

Ngakhale mchombo<br />

<strong>wa</strong>ukulu chotere ngati uwu<br />

si owopsa ndipo udzatha<br />

wokha. Ngati udakalipobe<br />

kufikira ali ndi zaka 5,<br />

opaleshoni itha kuchitika.<br />

Kalandireni malangizo<br />

kuchipatala.<br />

Nthawi zina hernia imachititsa<br />

chotupa pam<strong>wa</strong>mba komanso<br />

mbali imodzi ya tchende, osati<br />

m’kati.<br />

Mukhoza kudzi<strong>wa</strong> izi powona<br />

chotupacho (tsamba 89)<br />

chifuk<strong>wa</strong> hernia imatupa ngati<br />

m<strong>wa</strong>na akulira kapena <strong>wa</strong>imirira<br />

mowongoka, ndipo imaso<strong>wa</strong> ngati<br />

iye akhala chete.


338<br />

Nkhope ya m<strong>wa</strong>nayo imawoneka yefufuma, ndipo imawoneka ya tondovi, lirime lake<br />

limayenda kunja, ndipo chipumi chonse chitha kukhala ndi tsitsi. Ngofowoka, sadya<br />

moyenera, amalira pang’ono, ndipo amagona k<strong>wa</strong>mbiri. Amaganiza moched<strong>wa</strong> ndipo<br />

atha kukhala ogontha. Adzayamba kuyenda ndi kuyankhula moched<strong>wa</strong> kuyerekeza ndi<br />

<strong>ana</strong> oti ali bwinobwino.<br />

Pofuna kuthandiza kupe<strong>wa</strong> vuto lobwera k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na chifuk<strong>wa</strong> choso<strong>wa</strong><br />

mchere <strong>wa</strong> ayodini (iodine) m’thupi m<strong>wa</strong> mayi (cretinism), amayi apakati<br />

ayenera kugwiritsira ntchito mchere wokhala ndi iodine m’malo m<strong>wa</strong> mchere<br />

<strong>wa</strong>mba (onani tsamba 135).<br />

Ngati mukuganiza <strong>kuti</strong> m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>nu atha kukhala ndi vuto la cretinism pitani naye<br />

kuchipatala kapena k<strong>wa</strong> dotolo nthawi yomweyo. Kulandira mankh<strong>wa</strong>la m<strong>wa</strong>changu<br />

(a thyroid) kumatanthauza kukhalanso bwino m<strong>wa</strong>changu.<br />

3. Kusuta kapena kum<strong>wa</strong> zakum<strong>wa</strong> zaukali pamene mayi ali ndi mimba kumachititsa<br />

<strong>ana</strong> kubad<strong>wa</strong> aang’ono thupi kapena kukhala ndi mavuto ena (onani tsamba 156).<br />

Osamam<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong>mbiri kapena kusuta makamaka pamene muli ndi pakati.<br />

4. Zikadutsa zaka 35, mpata ndi <strong>wa</strong>ukulu woti mayi adzakhala ndi m<strong>wa</strong>na wokhala<br />

ndi vuto lina lake la pathupi. Matenda a mongolism kapena Down’s disease, amene<br />

amawoneka ngati cretinism ndi ochuluka pakati pa <strong>ana</strong> amene mayi ali <strong>wa</strong>chikulire<br />

k<strong>wa</strong>mbiri.<br />

Ndi bwino kukonzeratu za ukulu <strong>wa</strong> banja lanu kotero <strong>kuti</strong> simukukhalanso<br />

ndi <strong>ana</strong> ena pamene mupyola zaka 35 (onani mutu 20).<br />

5. Mitundu yosiy<strong>ana</strong>siy<strong>ana</strong> ya mankh<strong>wa</strong>la itha kuvulaza m<strong>wa</strong>na amene akukula<br />

m’mimba m<strong>wa</strong> mayi.<br />

Gwiritsirani ntchito mankh<strong>wa</strong>la ochepa monga mmene mungathere pa<br />

mthawi imene muli ndi pakati ndipo akhale okhawo amene mukudzi<strong>wa</strong> <strong>kuti</strong><br />

saika <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na pa chiswe.<br />

6. Ngati makolo ali pachibale (pachisuweni, m<strong>wa</strong>chitsanzo), pali mpata <strong>wa</strong>ukulu<br />

<strong>kuti</strong> <strong>ana</strong> awo adzakhala ndi vuto lapathupi kapena adzakhala oganiza moched<strong>wa</strong>. Maso<br />

a ntchefu, zala zowonjezereka, mapazi okhota, mlomo <strong>wa</strong>m’m<strong>wa</strong>mba<br />

woga<strong>wa</strong>nika ndi mavuto a pathupi odziwika bwino.<br />

Pofuna kuchepetsa mpata <strong>wa</strong> mavuto amene<strong>wa</strong> ndi ena, musak<strong>wa</strong>tire <strong>wa</strong>chibale<br />

<strong>wa</strong>pafupi. Komanso ngati muli ndi vuto lobad<strong>wa</strong> nalo lachilendolendo pa <strong>ana</strong> omwe muli<br />

nawo, ganizirani zosiya kukhalanso ndi <strong>ana</strong> ena (onani Ndondomeko za Kulera, mutu 20).<br />

Ngati m<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong>nu abad<strong>wa</strong> ndi vuto lapathupi, pitani naye<br />

kuchipatala. Nthawi zambiri kena kake kakhoza kuchitid<strong>wa</strong>.<br />

• Ngati lili vuto lokhala ndi maso antchefu (cross-eyes), onani<br />

tsamba 234.<br />

• Ngati m<strong>wa</strong>na abad<strong>wa</strong> ndi chala chowonjezereka chaching’ono<br />

k<strong>wa</strong>mbiri ndipo ndi chopanda fupa m’kati m<strong>wa</strong>ke, chimangeni<br />

ndi kachingwe mothinitsa k<strong>wa</strong>mbiri. Chotsatira chake ndi<br />

cha<strong>kuti</strong> chalacho chidzauma ndipo kenaka chidzaduka. Ngati<br />

chili chachikulu ndipo chokhala ndi fupa, muchisiye<br />

choncho kapena mupite kuchipatala <strong>kuti</strong> akachichotse.<br />

• Ngati mapazi a m<strong>wa</strong>na wobad<strong>wa</strong> kumene ali okhotera m’kati<br />

kapena apanga chibonga, yesetsani kuma<strong>wa</strong>wongolera<br />

monga mmene ayenera kukhalira. Ngati mungachite<br />

zimenezi msanga, chitani zimenezi kambirimbiri tsiku<br />

lililonse. Mapazi (kapena phazi) ayenera kukula<br />

pang’onopang’ono <strong>kuti</strong> akhale monga mmene ayenera<br />

kukhalira. Ngati simungathe kuwongola mapazi a<br />

m<strong>wa</strong>nayo <strong>kuti</strong> akhale m’malo m<strong>wa</strong>ke, pitani naye<br />

nthawi yomweyo kuchipatala kumene mapazi ake atha<br />

kumangid<strong>wa</strong> <strong>kuti</strong> akhale mchimake, m<strong>wa</strong>kuika mu<br />

chikhakha. Kuti pakhale zotsatira zabwino ndi pofunika<br />

kutero m’kati m<strong>wa</strong> masiku awiri akabad<strong>wa</strong>.<br />

Phazi<br />

lokhotera<br />

m’kati<br />

Phazi lokhala<br />

ngati<br />

chibonga


339<br />

• Ngati mlomo <strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na kapena m’m<strong>wa</strong>mba m<strong>wa</strong><br />

mlomo <strong>wa</strong>ke uga<strong>wa</strong>nika pawiri, atha kukhala ndi mavuto a<br />

kuyam<strong>wa</strong> ndipo ayenera kumadzamudyetsera sipuni.<br />

M<strong>wa</strong>kuchita opaleshoni <strong>wa</strong> mlomo <strong>wa</strong> m’m<strong>wa</strong>mba zikhoza<br />

kubwezeretsa mlomowo m’malo m<strong>wa</strong>ke. Nthawi yabwino<br />

yochitira opaleshoni ya mlomo ndi pamene ali ndi miyezi 4<br />

mpaka 6, ndipo miyezi 18 ngati ili opaleshoni ya<br />

m’m<strong>wa</strong>mba m<strong>wa</strong> mlomo.<br />

Mlomo woga<strong>wa</strong>nika pawiri<br />

7. Zovuta pa nthawi yobereka nthawi zina zingachititse kuwonongeka k<strong>wa</strong><br />

bongo. Zimene zingachititse m<strong>wa</strong>na kukhala ndi zi<strong>wa</strong>lo zouma ndi zizindikiro za<br />

kug<strong>wa</strong> khunyu. Mpata <strong>wa</strong> kuwonongekaku ndi <strong>wa</strong>ukulu ngati pa nthawi yobad<strong>wa</strong><br />

m<strong>wa</strong>nayo sapuma mofulumira, kapena ngati mzamba adapereka jekeseni yofulumizitsa<br />

kubad<strong>wa</strong> k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na m<strong>wa</strong>nayo as<strong>ana</strong>badwe (tsamba 282).<br />

Khalani osamala ndi mmene mumasankhira mzamba <strong>wa</strong>nu ndipo musalole<br />

mzamba <strong>wa</strong>nu kugwiritsira ntchito mankh<strong>wa</strong>la ofulumizitsa kubereka m<strong>wa</strong>na<br />

<strong>wa</strong>nu as<strong>ana</strong>badwe.<br />

M<strong>wa</strong>na <strong>wa</strong> minofu yomangika (Celebral Palsy)<br />

Miyendo yopiringidz<strong>ana</strong><br />

kapena yopitama ngati<br />

sizesi.<br />

M<strong>wa</strong>na wod<strong>wa</strong>la matenda<strong>wa</strong> amakhala ndi minofu<br />

yomangika ndi youuma kotero <strong>kuti</strong> satha kusuntha zi<strong>wa</strong>lo<br />

bwinobwino. Nkhope yake, khosi lake, kapena thupi lake litha<br />

kupotoka, ndipo mayendedwe ake amadzandira. Nthawi<br />

zambiri minofu yomangika m’kati m<strong>wa</strong> miyendo yake<br />

imachititsa <strong>kuti</strong> miyendo yake ikhale yopachik<strong>ana</strong> ngati<br />

sizesi.<br />

Pa nthawi yobad<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>nayo akhoza kuwoneka ngati ali<br />

bwinobwino kapena womasuka bwinobwino. Kumangika<br />

kumabwera iye akamakula. M<strong>wa</strong>nayo atha kudzakhala<br />

woganiza msanga kapenanso moched<strong>wa</strong>.<br />

Palibe mankh<strong>wa</strong>la amene amachiritsa kuwonongeka k<strong>wa</strong><br />

bongo kumene kumachititsa kumangika k<strong>wa</strong> minofu. Koma<br />

m<strong>wa</strong>na afunikira chisamaliro chapadera. Pofuna kule<strong>wa</strong><br />

kumangika k<strong>wa</strong> minofu m’miyendo kapena mapazi, perekani<br />

chithandizo monga cha mafupa olek<strong>ana</strong> m’chiuno (tsamba 335)<br />

ndiponso mwendo wokhota (tsamba 338), ngati kuli kofunika.<br />

Mthandizeni m<strong>wa</strong>nayo kusuntha, kukhala komanso kuima<br />

kenaka kuyenda monga lasonyezera tsamba 334.<br />

Mlimbikitseni kugwiritsira ntchito kuganiza ndi thupi<br />

mulimonse mmene angathere. Mthandizeni kuphunzira (onani<br />

tsamba lotsatirali). Ngakhale <strong>kuti</strong> iye ali ndi vuto la<br />

kuyankhula atha kukhala ndi mphamvu yabwino ya kuganiza<br />

ndi kutha kuphunzira zinthu zochuluka atapatsid<strong>wa</strong> mpata.<br />

Mthandizeni <strong>kuti</strong> adzithandize yekha.<br />

Kuched<strong>wa</strong> kukula m’miyezi yoyambirira ya <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>ke<br />

(Retardation)<br />

Ana ena amene ali ndi thanzi labwino pa nthawi yobad<strong>wa</strong> sakula bwino. Amayamba<br />

kuganiza moched<strong>wa</strong> chifuk<strong>wa</strong> sadya chakudya chokhala ndi zonse zofunikira m’thupi<br />

la munthu. M’kati m<strong>wa</strong> miyezi yochepa yoyambirira ya <strong>moyo</strong> <strong>wa</strong>wo, bongo umakula<br />

mofulumira kuposa pa nthawi ina iliyonse. Chifuk<strong>wa</strong> cha chimenechi chakudya<br />

choyenera k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na ndi chofunika k<strong>wa</strong>mbiri. Mkaka <strong>wa</strong> m’mawere ndicho chakudya<br />

chabwino koposa k<strong>wa</strong> m<strong>wa</strong>na (onani chakudya chabwino cha m<strong>wa</strong>na, tsamba 125).


340<br />

Pothandiza kuthetsa vuto la kuganiza moched<strong>wa</strong> kapena mavuto a pathupi<br />

amene <strong>ana</strong> amabad<strong>wa</strong> nawo, mayi ayenera kuchita zinthu zotsatirazi:<br />

1. Osak<strong>wa</strong>ti<strong>wa</strong> ndi msuweni kapena <strong>wa</strong>chibale wina aliyense.<br />

2. Adye zakudya zabwino ndi zok<strong>wa</strong>nira mmene angathere nthawi imene ali wod<strong>wa</strong>la:<br />

nyama yochuluka, mazira, zipatso, ndi ndiwo zamasamba zochuluka mmene<br />

angathere.<br />

3. Mugwiritsire ntchito mchere wokhala ndi iodine m’malo m<strong>wa</strong> mchere <strong>wa</strong>mba,<br />

makamaka nthawi imene ali ndi mimba.<br />

4. Musasute fodya kapena kum<strong>wa</strong> zoledzeretsa m<strong>wa</strong>uchidak<strong>wa</strong> pa nthawi imene muli<br />

ndi mimba (onani tsamba 156).<br />

5. Pamene muli ndi mimba, pe<strong>wa</strong>ni mankh<strong>wa</strong>la ngati kuli kotheka ndipo gwiritsirani<br />

ntchito mankh<strong>wa</strong>lawo okhawo amene akudziwika <strong>kuti</strong> ndi otetezed<strong>wa</strong>.<br />

6. Pamene ali ndi mimba, asayandikire anthu amene ali ndi chikuku cha German.<br />

7. Samalani kasankhidwe ka azamba ndipo musalole mzamba kugwiritsira ntchito<br />

mankh<strong>wa</strong>la ofulumizitsa mimba <strong>kuti</strong> mudzachire msanga m<strong>wa</strong>na as<strong>ana</strong>badwe<br />

(onani tsamba 282).<br />

8. Musakhalenso ndi pakati ngati muli ndi <strong>ana</strong> oposa mmodzi amene ali<br />

ndi chilema chof<strong>ana</strong>na (onani Ndondomeko zakulera, tsamba 302).<br />

9. Ganizirani zosiya kubereka mukak<strong>wa</strong>nitsa zaka 35.<br />

KUTHANDIZA ANA KUPHUNZIRA<br />

Pamene m<strong>wa</strong>na akula, mbali ina ya zinthu zimene amaphunzira ndi<br />

zimene <strong>wa</strong>phunzitsid<strong>wa</strong>. Nzeru ndi maluso amene amaphunzira ku sukulu<br />

zitha kumuthandiza kumvetsa ndi kuchita zambiri m’tsogolo. Kotero sukulu ndi<br />

yofunikira.<br />

Koma k<strong>wa</strong>kukulu m<strong>wa</strong>na amaphunzira kunyumba kapena m’tchire kapena<br />

m’munda. Amaphunzira kudzera mu zimene akuwona, kumva, ndi kuyesa payekha<br />

kuchita zimene ena akuchita. Saphunzira zambiri kudzera m’zimene ena akumuuza,<br />

koma m’zimene akuwona mmene ena akuchitira. Zina m<strong>wa</strong> zinthu zofunika<br />

k<strong>wa</strong>mbiri zimene m<strong>wa</strong>na angaphunzire ndi monga chifundo, udindo, ndi<br />

kuwolo<strong>wa</strong> manja kapena kuga<strong>wa</strong>na. Zonsezi zitha kuphunzitsid<strong>wa</strong><br />

powonera chitsanzo chabwino.<br />

M<strong>wa</strong>na amaphunzira kudzera mu kuyenda ndi kudziwonera yekha ndi maso.<br />

Ayenera kuphunzira kachitidwe ka zinthu payekha, ngakhale athe kumachita<br />

molakwitsa. Pamene iye ali <strong>wa</strong>mng’ono, mtetezeni ku ngozi. Koma pamene iye<br />

akukula, mphunzitseni kudzidalira yekha. Mupatseni udindo wina <strong>wa</strong>ke. Lemekezani<br />

maganizo ake, ngakhale akusiy<strong>ana</strong> ndi maganizo anu.<br />

Pa nthawi imene m<strong>wa</strong>na ali <strong>wa</strong>mng’ono, amafuna <strong>kuti</strong> zofuna zake zimveke basi.<br />

Kenaka amazindikira kusangalatsa kochita zinthu zothandiza ndi kuchitira anthu<br />

ena. Landirani chithandizo chawo ndipo asonyezeni <strong>kuti</strong> muku<strong>wa</strong>yamikira.<br />

Ana amene alibe mantha amafunsa mafunso ambirimbiri. Ngati makolo, aphunzitsi,<br />

ndi anthu ena alephera kuyankha msanga mafunso awo ndi mowona mtima – ndi<br />

kunena <strong>kuti</strong> sadzi<strong>wa</strong> pamene akudzi<strong>wa</strong> – m<strong>wa</strong>na adzapitiriza kufunsa mafunso.<br />

Ndipo pamene akukula atha kufunafuna njira <strong>kuti</strong> malo ake ozungulira kapena mudzi<br />

<strong>wa</strong>ke ukhale malo abwino wokhalamo.<br />

Maganizo ena othandizira <strong>ana</strong> kuphunzira ndi kulowetsed<strong>wa</strong>mo mu njira za <strong>moyo</strong><br />

zokhudza dera limene akukhala opangid<strong>wa</strong> ndi dongosolo lotched<strong>wa</strong> CHILD-to-child<br />

Program imene tsopano ikugwira ntchito m’maiko ambiri amene akukwera kumene.<br />

Kuti mudziwe zambiri alembereni kalata pa keyala iyi:<br />

CHILD-to-child Program<br />

Institute of Education<br />

20 Bedford Way<br />

London WC1 OAL, UK

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!