You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
94<br />
MANKHWALA A CHILONDA CHOFIKA M’MIMBA<br />
(Komanso othandiza matenda a Apendisitisi kapena Peritonitisi)<br />
Chitani izi musanalandire chithandizo cha kuchipatala:<br />
Bayani jekeseni ya ampicillin (tsamba 367), 1 gm (machubu anayi a 250 mg)<br />
maola anayi aliwonse.<br />
Ngati palibe ampicillin:<br />
Bayani jekeseni mwamsanga ya penicillin crystalline (tsamba 367) ngati ndi<br />
kotheka mayunitsi 5 miliyoni, kenaka mayunitsi 1 miliyoni mawola anayi<br />
aliwonse.<br />
Pamodzi ndi penicillin, perekani jekeseni ya streptomycin (tsamba 368), 2 ml (1 gm)<br />
kawiri pa tsiku kapenanso chloramphenicol wam’machubu wa 250 mg. Mawola<br />
anayi aliwonse.<br />
Ngati palibe jekeseni ya maantibayotikiwa, m’mwetseni ampicillin kapena<br />
penicillin ndi chloramphenicol kapena tetracycline ndi madzi pang’ono.<br />
Kupotokola <strong>kwa</strong>mbiri <strong>kwa</strong> m’mimba<br />
Kupotokola <strong>kwa</strong> m’mimba ndi kupweteka <strong>kwa</strong>mbiri <strong>kwa</strong> m’mimba kumene<br />
kumayamba mwadzidzidzi chifu<strong>kwa</strong> cha zinthu zosiyanasiyana. Zitsanzo zake ndi<br />
atenda a nsonga yathumbo (appendicitis), peritonitisi ndi kutseka <strong>kwa</strong> m’mimba.<br />
Nthawi zambiri kupota <strong>kwa</strong> m’mimba sikudziwika kuti <strong>kwa</strong>yamba bwanji<br />
pokhapokha akatswiri a opaleshoni atang’amba pamimba ndikuwona m’katimo.<br />
Ngati munthu akumva kupweteka m’mimba ndi kumasanza koma<br />
sakutsekula m’mimba, ndi kotheka kuti ndikupota <strong>kwa</strong> m’mimba chabe.<br />
Kupotokola <strong>kwa</strong> m’mimba: Ngati m’mimba simukupotokola<br />
Mtengereni wodwala kuchipatala <strong>kwa</strong>mbiri mukhoza kulandira<br />
popeza mwina angafunike opaleshoni thandizo kunyumba<br />
• kupweteka m’mimba kosalekeza<br />
• kudzimbidwa ndiponso kusanza<br />
• kutupa ndi kuuma mimba, odwalayo<br />
nkumakaniza mukagwirapo<br />
• kudwala <strong>kwa</strong>mbiri<br />
• kutsekula m’mimba pang’ono<br />
• kupweteka kosalekeza<br />
• zizindikiro za matenda ena<br />
monga chimfine kapena zilonda<br />
zapakhosi<br />
• ngati adadwalapo kale matendawa<br />
• kudwala pang’ono<br />
• kupotokola komayamba kenaka kusiya<br />
Ngati munthu akusonyeza zizindikiro zakupota <strong>kwa</strong><br />
m’mimba, mtengereni kuchipatala msanga.