MAPHUNZIRO A MATENDA A EDZI
MAPHUNZIRO A MATENDA A EDZI MAPHUNZIRO A MATENDA A EDZI
PHUNZIRO 2: KODI EDZI IMAFALA BWANJ? Werengani zokambirana za ana anzanu ndipo muyankhe funso pansipo polemba mukope lanu. P EDZI! EDZI! H Masiku ano nkhani koma EDZI. P EDZI, EDZI, akuti ingathe kufala mofulumira. H Komanso akuti ngati tisamala, EDZI ridiyosavuta kuti ithe. P Indedi, akuti tonse tizimvera malangizo basi. H Akuti jakisoni wosaphitsa, kulandira magazi wosapimidwa, chiwerewere - zidzetsa EDZI. 11. Mukuona chiani apa? 4
12. Mal woyembekezera naye angathe kumpatsira EDZI mwaa pobadwa. Imbani nyimbo zirmene zimamveka pa M.B.C. zothandiza kulewa EDZI. 5
- Page 1 and 2: MAPHUNZIRO A MATENDA A EDZI A BOOK
- Page 3 and 4: BOOK FOUR PHUNZIRO 1: EDZI NDI CHIA
- Page 5: Munthu wa EDZI amaonda ndi kufooka
- Page 9 and 10: PHUNZIRO 3: EDZI SAPATSANA MU NJIRA
- Page 11 and 12: NTCHITO 1. Sewero la ndipo ena banj
- Page 13 and 14: posamala anthu odwala EDZI tiyenera
- Page 15 and 16: PHUNZIRO 5: ZOMWE EDZI INGACHITE PA
- Page 17 and 18: . . r-- 24. Kuweta ng'ombe. 25. K
- Page 19: ACKNOWLEDGEMENT Acknowledgement and
PHUNZIRO 2: KODI <strong>EDZI</strong> IMAFALA BWANJ?<br />
Werengani zokambirana za ana anzanu ndipo muyankhe<br />
funso pansipo polemba mukope lanu.<br />
P <strong>EDZI</strong>! <strong>EDZI</strong>!<br />
H Masiku ano nkhani koma <strong>EDZI</strong>.<br />
P <strong>EDZI</strong>, <strong>EDZI</strong>, akuti ingathe kufala mofulumira.<br />
H Komanso akuti ngati tisamala, <strong>EDZI</strong> ridiyosavuta kuti ithe.<br />
P Indedi, akuti tonse tizimvera malangizo basi.<br />
H Akuti jakisoni wosaphitsa, kulandira magazi wosapimidwa,<br />
chiwerewere - zidzetsa <strong>EDZI</strong>.<br />
11. Mukuona chiani apa?<br />
4