28.02.2013 Views

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

! Chachiwiri, ifeyo tisa pemphere monga ngati “achikunja” - upemphera ndi mau<br />

yochulukila koma yopanda tanthauzo. Uko ndiko kupemphera kogabikana ndi<br />

kosachokela pansi pamtima. Nthawi zambiri tima zipangila pemphero yomwe<br />

timapemphera nthawi yonse ngati mwachizowerezi ndi ku iwala tanthauzo<br />

yapoyamba. Mwachisoninso, ngakhale pemphero ya chitsanzo ya Ambuye Yesu<br />

yakhali ngati imodzi ya mapemphero yamʼtunduyu. Mau yakhala ngati yalibe<br />

tanthauzo iliyonse. Akristo safunika kupemphera ndi mau yopanda tanthauzo,<br />

ubwebweta bwebweta chabe ndiku chulutsa mau kuti Mulungu atiyankhe. Iyai !<br />

Ndime 8 iti uza kuti Mulungu amatimva. Atate adziwa zonse zimene tizifuna TIKALIBE<br />

kuti tipemphere! Mulungu ndi wamʼkulu, choncho ngati tiku pemphera kulibe chimene<br />

Mulungu sanachidziwe kale.<br />

NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi tingapewe bwanji mapephero yo bwerezela ndiyopanda<br />

" pindu yomwe Ambuye Yesu anati chenjenza?<br />

! Pakuti Mulungu aziwa zonse zomwe tikufuna nichifukwa ninji tifunika<br />

upemphera? Zifukwa ndizambiri zomwe tifunikila upemphera: 1) Tinalamulilidwa -<br />

ndiku mvelela Mulungu. 2) Chosonyeza zofunikila zenizeni za moyo wathu –<br />

pachifukwa chakuti iseyo tipemphera chimvumbulutsa kuti zofunika koposa ndiziti pa<br />

umoyo wathu. 3) chitsonyeza udalila kwathu – ise ngati tikubwera kwa Ambuye ndiku<br />

peleka mapephero yathu tiku sonyeza kuti ti dalila iye kuti ndiye amatipasa zonse.<br />

Chachikulu ndi ichi, 4) chiyanjano chatu ndi Mulungu chipita patsogolo – chiyanjano<br />

ndi Mulungu chimachokela pomwe tikhala pomodzi ndi Abuye. Kuchuluka kwa nthawi<br />

yomwe ti khala ndi Mulungu mumapephero ndi kuwerenga mau tizakhala pafupi nae.<br />

Timudziwa bwino Mulungu.<br />

NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi Uopemphera kwaku nthandizani motani kuti inu mukule<br />

" mchiyanjano chanu ndi Mulunguow?<br />

PEMPHELO LA CHITSANZO:<br />

! Mu buku la Mateo 6:7-13, Ambuye Yesu anatipatsa chitsanzo mo pempherera.<br />

Tipeza zibvumbulutso zambiri momwe Yesu anali ku pempherera ndi zinthu zomwe<br />

anali kupepherera. Choyamba, apemphera ndi nzelu. Osati ngati munthu ali<br />

kupemphera kwa mulungu wakutalitali koma ngati kwa Mulungu ali pafupi ndiponso<br />

amene ali Tate wathu. Osati Tate wina chabe koma Tate wathu wa Kumwamba<br />

chichiwiri, Yesu anali upemphera pamodzi ndi ena. Yesu anali kuzi pempherera<br />

ndiponso anapemphreranso Akristu panthawi imodzi. Chachitatu, ana pemphera ???<br />

kwa Mulungu yekha.<br />

! 45

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!