Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
! Chachiwiri, ifeyo tisa pemphere monga ngati “achikunja” - upemphera ndi mau<br />
yochulukila koma yopanda tanthauzo. Uko ndiko kupemphera kogabikana ndi<br />
kosachokela pansi pamtima. Nthawi zambiri tima zipangila pemphero yomwe<br />
timapemphera nthawi yonse ngati mwachizowerezi ndi ku iwala tanthauzo<br />
yapoyamba. Mwachisoninso, ngakhale pemphero ya chitsanzo ya Ambuye Yesu<br />
yakhali ngati imodzi ya mapemphero yamʼtunduyu. Mau yakhala ngati yalibe<br />
tanthauzo iliyonse. Akristo safunika kupemphera ndi mau yopanda tanthauzo,<br />
ubwebweta bwebweta chabe ndiku chulutsa mau kuti Mulungu atiyankhe. Iyai !<br />
Ndime 8 iti uza kuti Mulungu amatimva. Atate adziwa zonse zimene tizifuna TIKALIBE<br />
kuti tipemphere! Mulungu ndi wamʼkulu, choncho ngati tiku pemphera kulibe chimene<br />
Mulungu sanachidziwe kale.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi tingapewe bwanji mapephero yo bwerezela ndiyopanda<br />
" pindu yomwe Ambuye Yesu anati chenjenza?<br />
! Pakuti Mulungu aziwa zonse zomwe tikufuna nichifukwa ninji tifunika<br />
upemphera? Zifukwa ndizambiri zomwe tifunikila upemphera: 1) Tinalamulilidwa -<br />
ndiku mvelela Mulungu. 2) Chosonyeza zofunikila zenizeni za moyo wathu –<br />
pachifukwa chakuti iseyo tipemphera chimvumbulutsa kuti zofunika koposa ndiziti pa<br />
umoyo wathu. 3) chitsonyeza udalila kwathu – ise ngati tikubwera kwa Ambuye ndiku<br />
peleka mapephero yathu tiku sonyeza kuti ti dalila iye kuti ndiye amatipasa zonse.<br />
Chachikulu ndi ichi, 4) chiyanjano chatu ndi Mulungu chipita patsogolo – chiyanjano<br />
ndi Mulungu chimachokela pomwe tikhala pomodzi ndi Abuye. Kuchuluka kwa nthawi<br />
yomwe ti khala ndi Mulungu mumapephero ndi kuwerenga mau tizakhala pafupi nae.<br />
Timudziwa bwino Mulungu.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi Uopemphera kwaku nthandizani motani kuti inu mukule<br />
" mchiyanjano chanu ndi Mulunguow?<br />
PEMPHELO LA CHITSANZO:<br />
! Mu buku la Mateo 6:7-13, Ambuye Yesu anatipatsa chitsanzo mo pempherera.<br />
Tipeza zibvumbulutso zambiri momwe Yesu anali ku pempherera ndi zinthu zomwe<br />
anali kupepherera. Choyamba, apemphera ndi nzelu. Osati ngati munthu ali<br />
kupemphera kwa mulungu wakutalitali koma ngati kwa Mulungu ali pafupi ndiponso<br />
amene ali Tate wathu. Osati Tate wina chabe koma Tate wathu wa Kumwamba<br />
chichiwiri, Yesu anali upemphera pamodzi ndi ena. Yesu anali kuzi pempherera<br />
ndiponso anapemphreranso Akristu panthawi imodzi. Chachitatu, ana pemphera ???<br />
kwa Mulungu yekha.<br />
! 45