You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
NDEMANGA/MAFUNSO: Kulingana ndi mau aya Mako 3:14, kodi lingo loyamba lomwe<br />
" Mulungu ana itanila inu ndi a Kristu ena? Kodi chimenechi chitanthauza chiani<br />
" kwa inu ndi Agulu lanu pakhani ya zofunikila?<br />
" Yesu akalibe usankha Atumwi ake khumi ndi awiri, ana pemphera usiku onse<br />
" kwa Mulungu (werengani Luka 6:12). Kodi mwakhala mukupephera kuti Mulungu<br />
" “Atume okolola zamʼmundaʼ? (Luka 10:2)<br />
3. Sonyezani maso mphenya:<br />
! Lembani mundandanda wa anthu omwe mukhulupirira kuti Mulungu akuku<br />
! tumani kuti musewenze nao, ndikuwa takasa kuti asewenze pamodzi ndi inu kuti<br />
! akwanilitse nchito yopeleka uthenga kwa amitundu.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi mungakope bwanji mitima za ena kuti asate maso mpenya<br />
" yanu?<br />
4. Pangani njila kapena mapulano ndi ku gawa zinchito kuti inu mu kwanilise<br />
nchito yopeleka uthenga ku mzinda wanu/ndziko lanu/dela lanu/ ndi dziko<br />
lonse lapanse:<br />
! Sankhani zithu zitatu zofunikila zomwe muzachita tchaka chino t<br />
! Gawilani anthu zi nchito zomwe aliyense membala yamu gulu afunika kuchita<br />
! kuti mu kwanilise maso mpenya.<br />
5. Pimani za phindu:<br />
! Pamene enu ndi agulu lanu aku sewenza nchito ya ulaliki ndi chofunika kuti<br />
! mupime za mpindu zomwe zikuchitika. (werengani Luka 10:1, 17). Ichi chi<br />
! tanthauza kuti mufunika ku zi ikila chipimo cha zochita zomwe Mulungu<br />
! azakutsogolelani.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi muzaziwa bwanji ngati mukupita patsogolo kuti mu kwanilitse<br />
! maso mpenya yanu?<br />
! 41