Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
STRATEGIC IMPACT - SUKULU YOCHULUTSA AZITSOGOLELI<br />
PHUNZILO 9 - UBYALA MIPINGO<br />
“MFUNDO 3 & 4: SONKHANITSANI NDI KUPHUNZITSA OPANGA OPHUNZILA”<br />
Pamene muyamba ukumana, gawanikani mʼmagulu ya anthu ANAI pagulu limodzi<br />
pampindi zokwanila ngati makumi yatatu mwina mwache mochepekela.<br />
Muphephererani wina ndi mzache ndipo mufunsane mafunso ya ungwilo. Pambuyo<br />
pache nkhalaninso mʼmagulu anu ndiku werenga phunzilo ili ndiku ponyapo<br />
ndemanga.<br />
Mphunzitsani GULU, osati chabe “Mtsogoleli”<br />
! Mtsogoleli wachi kristu aliyese ali kuchita zazikhulu padziko lapansi, sachita<br />
zimenezi payekha ai. Yesu Kristu anali ndi ʻguluʼ la atumwi khumi ndi awiri amene iye<br />
ana phunzitsa ndi ku wutuma padziko lapansi. Mtumwi Paulo anali ndi gulu lakenso.<br />
Sanachite utumiki payekha. Ngati mukufuna ukwanilisa ku itanidwa kwa Mulungu pa<br />
umoyo wanu ndi bwino kuti mumange gulu lo chulukitsa Ophunzila amene ali<br />
ozipereka ku utumiki wa mau pa dziko lapansi. Lingalilani izi po sonkhanitsa ndi<br />
kuphunzitsa gulu lanu;<br />
1. Zindikilani maso mpenya ya Mulungu pa umoyo wanu.<br />
! Malemba yakuti pa nkhani ya Davide, “pamene Davide ana tumikila lingo la<br />
! Mulungu kwa mʼbadwe wake kulingani ndi chifunila cha Mulungu, ana<br />
! mwalila.” [Acts 13:36]<br />
! Kulibe mau yabwino yopambana aya kuti yakalankhulidwe pa imoyo wathu - kuti<br />
! tina kwanilitsa chifunilo cha Mulungu mu ʻbadwo wathu! Inu simunalengedwe ai.<br />
! Sichangozi kuti inu ndinu mwana wa Mulungu pa nthawi ino ndi pamalo pomwe<br />
! mukukhala. Mulungu ali ndi lingo lalikhula pa umoyo wanu. Ana ku itanani kuti<br />
! muchite chifunilo chache!<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Nichifukwa ninji Mulungu ana ku ikani padziko lapansi pa<br />
" nthawi ino?<br />
" Kodi ku itana kwa Mulungu pa umoyo wanu mukukudziwa?<br />
" Kodi chomwe mukufunisisa pa umoyo wanu chopambana zonse ndi chiani?<br />
2. Mupepheni Mulungu kuti abweletse Anthu okuthandizani kuti mukwanilitse<br />
Maso Mpenya yanu.<br />
! Mako 3:14 itisonyeza momwe Yesu anasankhila gulu yake kuti akwanilitse lingo<br />
! lache padziko lapansi.“ndipo anasakha khumi ndi awiri kuti akhale nao , andi<br />
! kuwa tuma kuti akalalike uthenga wa Mulungu.”<br />
! 40