You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
STRATEGIC IMPACT - SUKULU YOCHULUTSA AZITSOGOLELI<br />
PHUNZILO 8 - UTUKULA UTSOGOLELI<br />
“CHIKHALIDWE: ZOFUNIKILA PA UMOYO WA MTOGOLELI”<br />
Pamene muyamba ukumana, gawanikani mʼmagulu ya anthu ANAI pagulu limodzi<br />
pampindi zokwanila ngati makumi yatatu mwina mwache mochepekela.<br />
Muphephererani wina ndi mzache ndipo mufunsane mafunso ya ungwilo. Pambuyo<br />
pache nkhalaninso mʼmagulu anu ndiku werenga phunzilo ili ndiku ponyapo<br />
ndemanga.<br />
! Mtsogoleli anga khale ndi maso mpenya yayakhulu ndi mchango koma kuli<br />
chikhalidwe chichikulu chomwe afunika ukhala nacho, afunika ukhala okhulupilika.<br />
Chilibe kanthu ngakhali kuti mstogoleli ali ndi mchangu ndi maso mpenya yampamvu<br />
koma ngati sakhulupirika zonsezi zili mwachabe, anthu sadzalondola mtsogoleli otele!<br />
Ngati mstogoleli mataya chikhulupililo cha anthu, anthu saza mulondola. Choncho<br />
ngati mtsogoleli wa umulungu akufuna utakasa ina ndiku kwanilisa maso mpenya yaya<br />
kulu ndibwino kuti akhale ndi CHIKHALIDWE chabwino.<br />
! Kodi chikhalidwe ndi chiani? Chikhalidwe ndi ku khulupirika komwe kumabwera<br />
kamba ka kusonyeza.<br />
! Modzi wa atsogoleli ampamvu mu Baibulo ndi Mfumu Davide. Nichifukwa ninji<br />
anali woposa? Masalimo 78:72 itipasa yankho. “And ndipo Davide ana tsogolela ndi<br />
mtima wa mtima wa Ungwilo ndi manja ya luso.” Davide sana tsogolele chabe ndi luso<br />
komabe anasonyeza ukhulupirika. Ukhulupirika ndiku nkhala okwana ndipo<br />
osagawikana.ʼ Ndiku khali ukhulupirika ndipo opanda chinyengo kapena<br />
kunyalanyaza. Munthu okhulupilika ndi munthu amene ali oyela mtima. Sasintha<br />
pomwe ali okha ndi pmwe ali pakati ka anthu. Ndi okhulupirika ndiponso odalilika.<br />
Achita zomwe alankhula ndipo asonga mau yao. Munthu wa ungwilo kapena<br />
okhulupilika siuja munthu wamene alibe chilema kapena banga kapena wamene<br />
sachimwa ai. Ichi sichotheka ai. Komabe ndi munthu wamene avomeleza ngati alakwa<br />
ndi ku ululila machimo yake. Chifukwa chakuti asonyeza ukhulupilika nthawi zonse,<br />
ena aphunzila ndi ku dalila iwo.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO:<br />
1. Nichifukwa ninji chikhalidwe kapena ungwilo chili chofunika kwa atsogoleli a<br />
umulungu?<br />
2. Nichifukwa ninji chikhalidwe chosa yeluzika ndi cho optsa osogoleli wa chikristu?<br />
3. Ndi njila zotani zomwe mtsogoleli wa chi kristu kusonyeza kuti ndi okhulupilikay?<br />
! 38