Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
! Chachitatu - ndipo chopambana - ndi Akugwilitsa nchito ndime yamalemba<br />
yomwe tawelenga mu Baibulo. Njila imodzi yogwilitsila nchito ndiku sewendzetsa njila<br />
zinai zomwe Paulo ana nena kuti ndiyo lingo lomwe Mulungu anati pasila malemba- -<br />
“Uphunzitsa, kudzudzula, kukonza cholakwa ndi kulangiza za chilungamo,” (2<br />
Timoteyo 3:16). Zomwe mwa phunzila, gwilitsani nchito malemba awa pa zocita mu<br />
umoyo wanu paku sewenzetsa njila izi:<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Nchifukwa chiani muganiza kuti njila iyi ya chitatu,<br />
" “KUGWILITSA NCHITO”, ndi yo yenela kopotsa pa ku phunzila Baibulo?<br />
ZOCHITA<br />
Uphunzitsa: WKodi Ndizoonadi zotani Kudzudzula: kodi chomwe ndi khulipirera<br />
zomwe Mulungu amagwilitsa nchito kuti ndi cholakwika ndi chiti? Chifukwa<br />
zomwe inenso nifunikila kugwilitsa nchito. ninji? Kodi maziko yachiganizo kapena<br />
chikhalidwe ichi ndichiti?<br />
Kuphunzitsa mchilungamo: kodi ndinga<br />
tukule bwanji mbali iyi yamoyo wanga?<br />
Kodi ndinga yambe bwanji maganizo<br />
kapena machitidwe achikhalidwe<br />
chatsopano?<br />
Lankhulani ndi Mulungu pabou pazomwe<br />
Iye afuna kuti muchite ndi kulemba<br />
ndmundandanda wa zomwe muzachita?<br />
Kulungamitsa cholakwa: kodi ndizatani?<br />
Kodi ndiza lungamitsa bwanji chikhalidwe<br />
kapena chichitidwe ichi choipa?<br />
Ndime yaikulu yakuti mukumbuke:<br />
ZOCHITA SABATA LINO:<br />
Phunzilo (Yanganilani, Matsulilani, Chitani) 2 Timotoye 2:1-7 kusewnzetsa dongotsolo<br />
ya pamwamba.<br />
! 37