28.02.2013 Views

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

Tsiku 1 - strategic impact

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

! Pemphero, tsono, ndi chida cha mpamvu kwambiri. Pemphero isonyeza uzi<br />

chepetsa ndi kudalila mpamvu za Mulungu. Pemphero isonyezanso kuti tidalila u<br />

lemelelo wa Mulungu ndi mpamvu yache kuti lingo lache lichitidwe. Pamene ti<br />

pemphera, tisonyeza chiyamiko pa nchito yomwe Ambuye yesu anachita pamtanda.<br />

Pemphero isonyedza kui MULUNGU ndiye amene amatipasa zonse za umoyo<br />

ndiposo tipeza njila momwe tingamulimekezele po limbisa Ophunzila azathu ndi ku<br />

panga ophunzila ena.<br />

! Mbali zonse za utumiki wathu zifunika udzadzidwa ndi pemphelo. Ifeyo tili<br />

ozipereka ku pemphero , koma siti tanthauza kuti timapemphera chabe. Tisa chite<br />

kanthu kalikonse popanda ku pemphera kwa Ambuye. Tika ika zonse mʼmanja ya<br />

Mulungu, ndipo pomwe tinga pite patsogolo mwa chitsimikizo kuti Iye azati tsogolela.<br />

NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi ndizinthu zotani zomwe mukuchite zomwe mukuganizila<br />

" kuti mwenamwache mufunikila kuti mu pempherereponso mwa ka nthawi?<br />

! Modzi ya mapemphero yomwe tiyenera kupemphera ndi kupempherera Anchitor<br />

workers. Mubuku la Luka10:2-3, Yesu anauza ophunzila bake kuti, “The harvest is<br />

plentiful, but the laborers are few. Therefore pray earnestly to the Lord of the harvest to<br />

send out laborers into his harvest. Go your way; behold, I am sending you out as<br />

lambs in the midst of wolves.” Anauza ophunzila bake kuti apempherere Anchito, ndiku<br />

watumanso iwowo PAMENEPO! Tipempherera anchito koma sitikhala tikudikhila<br />

anchito kuti abwere tisane yambe nchito ifeyo. Kuti nchito ya ulaliki ikwanilitsidwe<br />

ambili anchito azachokela mzokololazo! Ganizilani mau aya pampindi imodzi yokha.<br />

Ambila mwa iwo omwe azatengako mbali ku nchito yopereka uthenga kwa amitundu<br />

akalibe kuti amʼzindikile Yesu ngati Mʼpulumutsi wao! Choncho , pomwe tikupempha<br />

Mulungu kuti atume anchito, tikupempha kuti anthu osowa amʼdziwe Yesu – kuti<br />

tipanga ophunzila! TIFUNIKA UPEMPHA! Tifunika ulandila malamulo ku chokela kwa<br />

Ambuye! Tifunika kusewenza ndi mphamvu Zache, osati zathu ai. TIFUNIKA KUZI<br />

PEREKA KU MAPEMPHERO, ndiku sonkanitsa Anthu athu kuti achite chimodzi<br />

modzi! Ambili mwa ise tina ika nkholoko zathu za Alamu panthawi ya 10:02 mʼʼmawi<br />

kuti tipempherere otuta za mʼmunda kulingana ndi Luka 10:2.<br />

NDEMANGA/MAFUNSO: Ta imani pompa ndiku lola anthu onse amʼgulu lanu kuti aike<br />

" Nkoloko zao kapena ma selo foni yali ndi ma Alamu pa nthawi ya 10:02 mʼmawa.<br />

" Pemphererani panthawi iyi kuti Mulungu atume okolola zamʼmunda!<br />

! Yesu ali ndi ulamulilo onse wa padziko lakumwamba ndi dziko la pansi.<br />

Talamulilidwa ndi iyi kuti tipelike uthenga kwa amitundu onse. Pemphani Mbuye wa zo<br />

kolola kuti atume otuta zamʼmunda! Indetu Zinthu zonse ndizotheka ndi Mulungu<br />

(Matteo 19:26)<br />

! 31

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!