You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
! Pemphero, tsono, ndi chida cha mpamvu kwambiri. Pemphero isonyeza uzi<br />
chepetsa ndi kudalila mpamvu za Mulungu. Pemphero isonyezanso kuti tidalila u<br />
lemelelo wa Mulungu ndi mpamvu yache kuti lingo lache lichitidwe. Pamene ti<br />
pemphera, tisonyeza chiyamiko pa nchito yomwe Ambuye yesu anachita pamtanda.<br />
Pemphero isonyedza kui MULUNGU ndiye amene amatipasa zonse za umoyo<br />
ndiposo tipeza njila momwe tingamulimekezele po limbisa Ophunzila azathu ndi ku<br />
panga ophunzila ena.<br />
! Mbali zonse za utumiki wathu zifunika udzadzidwa ndi pemphelo. Ifeyo tili<br />
ozipereka ku pemphero , koma siti tanthauza kuti timapemphera chabe. Tisa chite<br />
kanthu kalikonse popanda ku pemphera kwa Ambuye. Tika ika zonse mʼmanja ya<br />
Mulungu, ndipo pomwe tinga pite patsogolo mwa chitsimikizo kuti Iye azati tsogolela.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Kodi ndizinthu zotani zomwe mukuchite zomwe mukuganizila<br />
" kuti mwenamwache mufunikila kuti mu pempherereponso mwa ka nthawi?<br />
! Modzi ya mapemphero yomwe tiyenera kupemphera ndi kupempherera Anchitor<br />
workers. Mubuku la Luka10:2-3, Yesu anauza ophunzila bake kuti, “The harvest is<br />
plentiful, but the laborers are few. Therefore pray earnestly to the Lord of the harvest to<br />
send out laborers into his harvest. Go your way; behold, I am sending you out as<br />
lambs in the midst of wolves.” Anauza ophunzila bake kuti apempherere Anchito, ndiku<br />
watumanso iwowo PAMENEPO! Tipempherera anchito koma sitikhala tikudikhila<br />
anchito kuti abwere tisane yambe nchito ifeyo. Kuti nchito ya ulaliki ikwanilitsidwe<br />
ambili anchito azachokela mzokololazo! Ganizilani mau aya pampindi imodzi yokha.<br />
Ambila mwa iwo omwe azatengako mbali ku nchito yopereka uthenga kwa amitundu<br />
akalibe kuti amʼzindikile Yesu ngati Mʼpulumutsi wao! Choncho , pomwe tikupempha<br />
Mulungu kuti atume anchito, tikupempha kuti anthu osowa amʼdziwe Yesu – kuti<br />
tipanga ophunzila! TIFUNIKA UPEMPHA! Tifunika ulandila malamulo ku chokela kwa<br />
Ambuye! Tifunika kusewenza ndi mphamvu Zache, osati zathu ai. TIFUNIKA KUZI<br />
PEREKA KU MAPEMPHERO, ndiku sonkanitsa Anthu athu kuti achite chimodzi<br />
modzi! Ambili mwa ise tina ika nkholoko zathu za Alamu panthawi ya 10:02 mʼʼmawi<br />
kuti tipempherere otuta za mʼmunda kulingana ndi Luka 10:2.<br />
NDEMANGA/MAFUNSO: Ta imani pompa ndiku lola anthu onse amʼgulu lanu kuti aike<br />
" Nkoloko zao kapena ma selo foni yali ndi ma Alamu pa nthawi ya 10:02 mʼmawa.<br />
" Pemphererani panthawi iyi kuti Mulungu atume okolola zamʼmunda!<br />
! Yesu ali ndi ulamulilo onse wa padziko lakumwamba ndi dziko la pansi.<br />
Talamulilidwa ndi iyi kuti tipelike uthenga kwa amitundu onse. Pemphani Mbuye wa zo<br />
kolola kuti atume otuta zamʼmunda! Indetu Zinthu zonse ndizotheka ndi Mulungu<br />
(Matteo 19:26)<br />
! 31