You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
NDEMANGA/MAFUNSO: Ndi lingo yotani yomwe Mulungu aku itanani kuti muchite<br />
" panthawi ino kapena pamalo yano? Kodi lingo imeneyi ivomelezana ndi lingo<br />
" yolalika uthenga kwa osowa? Mateo28:18-20<br />
Motsiliza:<br />
Ngati ulibe mchangu, ulibe UTSOGOLELI.<br />
! Ngati ulibe Anthu, ulibe UTSOGOLELI.<br />
! Ngati SIUKWANILISA zofunika PANCHITO, ulibe UTSOGOLELI.<br />
ZOCHITA SABATA LINO:<br />
<strong>Tsiku</strong> 1: talingalilani zinthu zimene azitsogoleli amachita kuti minu mutakasidwe ndiku<br />
! tengako mbali. Talembani zinthu zambiri zimene zisonyeza chikhalidwe cha<br />
! munthu odziwa utakasa ena:<br />
Kudi mzatani inu kuti mukhale ndi chikhalidwe chodziwa utakasa ena?<br />
<strong>Tsiku</strong> 2: Ndi anthu oti amene MULUNGU alikuku itanani kuti inu mupereke utsogoleli?<br />
Nichifukwa ninji inu muli mtsogoleli wao?<br />
Tapimani ngati anthu ali afunisisa utsogoleli wanu kapena yayi. Mungawa takase<br />
bwinji anthu kuti akutsatileni inu?<br />
<strong>Tsiku</strong> 3 and 4: Tengani masiku awiri yakuti mupephere ndiku fufuza nkope ya<br />
! Mulungu kuti akupatseni zimene mufunikila kuchita panthawi inu ndi pamalo<br />
! yanu. Lembani zimenezi mwachidule: __________________________________<br />
!<br />
! ________________________________________________________________<br />
! ________________________________________________________________<br />
Tapimani chomwe mufunukila kuchita. Kodi chigwilizana ndi nchito yopereka ulaliku<br />
kwa anthu osowa?<br />
! 19