FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
Adzichitira ulemu nyumba ya Mulungu.<br />
To respect God's house.<br />
Alangizi apitirize kulimbikitsa kuti kubvinidwa kotereku kukukhadzikitsa uChewa wake<br />
komanso chiKhristu chake. Ndipo khalidwe lake losinthika lidzakhala umboni kwa atsikana<br />
ena kuti nawonso afune kubwera kwa Yesu ndi ku mpingo wake.<br />
The instructresses need to emphasize to the initiate that going through this Christian chinamwali establishes her<br />
identity as a Chewa woman, and as a Christian. Her changed behavious should be a testimony to her friends so<br />
that they will also desire to come to Jesus, to join his church, and to go through the Christian chinamwali.<br />
Potsiriza peni peni apempherere namwali kuti Mulungu amuteteze ndi kumuthandiza<br />
adzisunge mpaka akalowe m'banja. Wopemphera amusanjike manja namwaliyo<br />
pomupempherera. Kudya ndi kumwa onse pamodzi ndi kubalalikana zitseke zonse.<br />
Alangizi ndi aphungu amuperekeze namwaliyo kwawo nthawi yakurnmawa, ndipo amwaliyo<br />
atafundira nsalu kumutu kwache. Adziyimba nyimbo iyi:<br />
At the end the initiate should be prayed for that God should protect her and help her to remain pure until<br />
marriage. The one praying should lay hands on the initiate. Eating and drinking together should end the<br />
ceremony after which people can disperse. The instructresses and the tutors should escort the girl home while<br />
singing:<br />
18. Mtetezi wanga Yesu<br />
Mtetezi wanga<br />
My protector is Jesus<br />
My protector<br />
Wotsogolera nyimbo adzisintha sintha mawu ndikuikira wena monga 'momboli wanga, ,<br />
'mchiritsi wanga,' 'ndimbuye wanga.' Akalandiridwa kunyumba alangizi apemphererenso<br />
mtsikana pamodzi ndi makolo ake, kuyamika Mulungu chifukwa cha mwambo wonse<br />
umene mtsikana walandira.<br />
The leader should be mentioning all that Jesus is, such as 'my saviour,' 'my healer,' my lord,' and so on. At<br />
home the instructress should pray with the girl and her parents thanking God for the ceremony and the<br />
instruction the girl has received.<br />
Sabata yotsatira, panthawi yamapemphero payenera kukhala kamwambo kochepa<br />
kumulandira mtsikana ku mpingo. Amfurnu aitanidwe kudzaonerera. Potsiriza mapemphero<br />
pakhale chiyanjano ndi kumwa thobwa pamodzi kusonyeza umodzi wa anthu.<br />
The following Sunday, during the worship service, there could be a small ceremony to introduce and<br />
incorporate the young woman to the wider society. The chief or his representative should be invited to the<br />
worship. A drink of sweet beer should be served at the end of the service to symbolize an act of fellowship<br />
while embracing into the corporate body offaith.<br />
212