28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

Anthu onse nkuseka. Ndipo anamkungwi aimirire nayambitse nyimbo (Masalimo 139:13­<br />

14):<br />

Girl: Dad, look, I have hurt myself; I do not know what has cut me!<br />

Father: 0, No! How do you play? Look now you have hurt yourself, eh! Look at the<br />

blood! Let's go to the hospital!<br />

They all laugh. Then the instructresses stand and begin to sing a song from Psalm 139: 13-14.<br />

9. Ndinu mudanlenga inetu eee!<br />

Mudandiumba bwinotu eee!<br />

Ntchito zanu zonse nzodabwitsa eee!<br />

Onani lero ndakula<br />

Ndakulatu, ndakulaa.<br />

Akatha kubvina, amulongosole1e mtsikana kuti:<br />

You created me yaa!<br />

You moulded me well yaa!<br />

Your works are wonderful yaa!<br />

Look today I have matured<br />

I have matured, I have matured yee!<br />

Mulungu adatilenga kuti thupi lamunthu likamakula limasinthika mumsinkhu ndi<br />

mmaonekedwe. Akafika msinkhu wina mtsikana amayamba kusamba kwa masiku seven<br />

kapena kucheperako (kutuluka magazi kokozera). Kusambaku kumapitiria kamodzi<br />

pamwezi. Chizindikiro chimenechi chimaoneka kwa akazi onse. Chomwecho sizodetsa<br />

nkhawa kuti ndi matenda.<br />

Kusambaku kumalozera zamtsogolo. Imeneyi ndi njira yomwe anakonza Mulungu pofuna<br />

kutipatsa mphatso za ana.<br />

Apitirize kuyimba,<br />

After dancing the instructresses should give the following explanation to the girl:<br />

God created us so that as we grow our bodies change both physically and in how we look. At a certain point<br />

the girl begins to menstruate for about seven days or less (blood coming out of the private parts). This blood<br />

flow happens once a month to all women. It is not any illness to worry about. Menstruation foretells the future<br />

role. This is God's own way for us to have children.<br />

They should continue singing,<br />

10. Mwateremu dzisamaleni a Joyce x 3<br />

Bvalani mwele<br />

11. Nchenje, nchenje, taona<br />

Nchenje, yaonanji?<br />

Yaona n 'nkhole<br />

Now with this, take care ofyourself Joyce<br />

Wear menses linen<br />

Fly, fly, look<br />

Fly, what has it seen<br />

It has seen the menses<br />

Kutanthauza kwa nyimboyi ndiye kuti namwaliyo adzizisamalira maka maka akamasamba<br />

kuopa kununkha.<br />

The meaning of the song is that the girl should take care of herself whenever she is menstruating so that she<br />

does not smell.<br />

208

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!