FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
Anthu onse nkuseka. Ndipo anamkungwi aimirire nayambitse nyimbo (Masalimo 139:13<br />
14):<br />
Girl: Dad, look, I have hurt myself; I do not know what has cut me!<br />
Father: 0, No! How do you play? Look now you have hurt yourself, eh! Look at the<br />
blood! Let's go to the hospital!<br />
They all laugh. Then the instructresses stand and begin to sing a song from Psalm 139: 13-14.<br />
9. Ndinu mudanlenga inetu eee!<br />
Mudandiumba bwinotu eee!<br />
Ntchito zanu zonse nzodabwitsa eee!<br />
Onani lero ndakula<br />
Ndakulatu, ndakulaa.<br />
Akatha kubvina, amulongosole1e mtsikana kuti:<br />
You created me yaa!<br />
You moulded me well yaa!<br />
Your works are wonderful yaa!<br />
Look today I have matured<br />
I have matured, I have matured yee!<br />
Mulungu adatilenga kuti thupi lamunthu likamakula limasinthika mumsinkhu ndi<br />
mmaonekedwe. Akafika msinkhu wina mtsikana amayamba kusamba kwa masiku seven<br />
kapena kucheperako (kutuluka magazi kokozera). Kusambaku kumapitiria kamodzi<br />
pamwezi. Chizindikiro chimenechi chimaoneka kwa akazi onse. Chomwecho sizodetsa<br />
nkhawa kuti ndi matenda.<br />
Kusambaku kumalozera zamtsogolo. Imeneyi ndi njira yomwe anakonza Mulungu pofuna<br />
kutipatsa mphatso za ana.<br />
Apitirize kuyimba,<br />
After dancing the instructresses should give the following explanation to the girl:<br />
God created us so that as we grow our bodies change both physically and in how we look. At a certain point<br />
the girl begins to menstruate for about seven days or less (blood coming out of the private parts). This blood<br />
flow happens once a month to all women. It is not any illness to worry about. Menstruation foretells the future<br />
role. This is God's own way for us to have children.<br />
They should continue singing,<br />
10. Mwateremu dzisamaleni a Joyce x 3<br />
Bvalani mwele<br />
11. Nchenje, nchenje, taona<br />
Nchenje, yaonanji?<br />
Yaona n 'nkhole<br />
Now with this, take care ofyourself Joyce<br />
Wear menses linen<br />
Fly, fly, look<br />
Fly, what has it seen<br />
It has seen the menses<br />
Kutanthauza kwa nyimboyi ndiye kuti namwaliyo adzizisamalira maka maka akamasamba<br />
kuopa kununkha.<br />
The meaning of the song is that the girl should take care of herself whenever she is menstruating so that she<br />
does not smell.<br />
208