28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

The night's ceremony may be as follows. (This is just oneexample of chinamwali. The instructresses should<br />

come up with many songs and drama with words from the Scriptures to make the rite more meaningful and<br />

interesting to the young women.)<br />

Machemebere ayimbe nyimbo (ziwiri ngakhale zitatu) kuti namwali adziwe chimene anthu<br />

abwerera, monga,<br />

The women should sing two or three songs concerning the purpose for the vigil, such as,<br />

1. M'Baibulo, m 'Baibulo<br />

Muli mwambooo<br />

M'Baibulo, m 'Baibulo<br />

Muli mwalankhula<br />

In the Bible, in the Bible<br />

There is counsel<br />

In the Bible, in the Bible<br />

There is speaking<br />

Machembere aziimba akumuzungulira mtsikana atakhala. Ena a amayiwo atanyamula<br />

maBaibulo kumanja kwawo ndikumamusonyeza namwaliyo. Tanthauzo lake ndikuti<br />

ulangizi umene apatsidwe tsikanayo ndiochokera m'Baibulo. Popeza baibulo ndi Mau a<br />

Mulungu, ndipo Mulungu ndi amene adatilenga. Mwambo wa Mulungu ndiye wotiyenera<br />

ife.<br />

The women should be singing while going round in a circle with the initiate seated. Some of the women can<br />

hold a Bible in their hands and show it to the initiate. The meaning is that their counsel is from the Word of<br />

God, who is our Creator. It is God's counsel which we must follow.<br />

2. Sinkadabweratu ine<br />

Sinkadabweratu pano<br />

Yandiendetsa mnkhole yakoyi<br />

I would not have come me<br />

I would not have come here<br />

It is your menses that have made me walk<br />

Mtsikana ali chikhalire ndi phungu wake pambali, onse adziimba atachita bwalo.<br />

Azizungulira, koma ena atayerekeza kubvala mwele, koma osabvula zobvala zawo.<br />

Atanthauza kuti onse abwera chifukwa cha mtsikana amene wakula. 'Tsopanotu walowa<br />

mbungwe la anthu akulu. '<br />

While the girl is seated with her tutors, the others should be dancing in a circle while wearing something like<br />

the menses linen, but not actually taking offtheir clothes.<br />

They should explain the meaning that 'now you are mature, you are no more a child!'<br />

3. Mukatere, mukatere<br />

Ndiko kukula kumeneku<br />

What you have done, you have done<br />

This is what maturity is<br />

Zimene zikuchitika panOZl ndichifukwa chakuti mwakula ndipo mulandire mwambo<br />

woyenera.<br />

What is happening here is because you have now come ofage and you need to be instructed.<br />

Tsopano ndi nthawi yakuti atsikana akale aperekere maumboni a khalidwe lawo kupyolera<br />

mu nyimbo ndi kubvina. Popezatu iwo tsopano ndi anthu akhalidwe labwino kunyumba<br />

kwawo, mmudzi, komanso kumpingo kwawo.<br />

After singing and dancing, the older girls should take the floor. The aim is to give their testimonies through<br />

songs and dancing that it is because they received the same teaching they are now good girls in their<br />

community, in their homes, even at church.<br />

205

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!