FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
Ndi udindo wa alangizi kukonza maphunziro a atsikana onsewa kamodzi pamwezi.<br />
It is the responsibility ofthe instructresses to arrange meeting with the girls once every month.<br />
CHINAMWALl (KUTHA MSINKHU)<br />
PUBERTY RITE CEREMONY<br />
Malangizo kwa Alangizi<br />
For the Instructresses<br />
Pamene alangizi mwadziwitsidwa kuti mtsikana watha msinkhu, muyenera mukumane ndi<br />
mtsikanayo mwansanga. Mumuuze mwachidule tanthauzo la zimene zamuchitikirazo.<br />
Mumuphunzitsenso kabvalidwe ndi kasamalidwe ka mwele. Mtsikanayo asagwire ntchito<br />
yolemetsa, komanso asayende yende mpaka atabvinidwa potsirizira pa msambowo.<br />
When you have been informed that a girl has matured, you must meet with the girl as soon as possible. Briefly,<br />
instruct her on the meaning of the menses, how to wear and take care ofthe linen. She must do light work and<br />
should remain in seclusion until the chinamwali ceremony at the end ofher menses.<br />
Muyenera kudziwitsa amayi busa anu amene adziwitsanso abusa. Dziwitsaninso<br />
anamkungwi popeza ndiwo amene ayenera kukanena kwa mfumu. Mayi wa mtsikana<br />
apereka nkhuku yokanenera kwa mfumu.<br />
You must inform the pastor's wife who should inform the pastor. Inform also the traditional anamkungwi who<br />
will inform the chief. The girl's mother must pay the chiefs dues.<br />
Alangizi ndi mpingo, mogwirizana ndi makolo mukonzekere kumubvinira namwaliyo usiku<br />
wonse potha pa msambo wakewo. Simba labwino ndi kunyumba kwa mlangizi, komabe<br />
mukhoza kusankha malo ena opangira chinamwalicho. Alangizi, machembere a mumpingo,<br />
makolo a mtsikana (osati mai ake), ndi atsikana olangizidwa kale a mumpingo (koma awiri<br />
akhale aphungu), ayenera kudza kuchinamwalicho.<br />
The instructresses and the church, together with the parents, should prepare for the night's vigil chinamwali at<br />
the end of the girl's menses at the instructress' house, or any other house. The instructresses, the elderly<br />
women ofthe church, the girl's aunt or grandmother, and the younger women ofthe church should be invited to<br />
attend the chinamwali. Let two ofthem be tutors.<br />
Anthu onse oitanidwawo atatha kudya chakudya chamadzulo pamodzi, abusa kapena akulu a<br />
mpingo ayenera kutsegula mwarnbo ndi pemphero ndi mawu apang'ono achilimbikitso.<br />
Chonde onenetsetsani kuti kuimba, kubvina, ndakatulo, ngakhale masewero, ziyenera<br />
kutenga gawo lalikulu pachinamwali, kuti namwaliyo amvetse mwambo. Baibulo mukhoza<br />
kuwerenga koma osati Bukhu la alangizi ayi.<br />
When all the invited people have taken their evening meal, let the pastor or an elder begin with prayer and a<br />
word ofexhortation from the vernacular Bible.<br />
Please note that singing, dancing, and acting should be used in instructing the girl. You can use the Bible but<br />
not the instructresses' booklet.<br />
Mwambo wa usiku ukhoza kukhala motere. (Ichi ndi chitsanzo chimodzi, koma alangizi<br />
muyenera kukonza nyimbo zambiri ngakhalenso maseweero ndi mau ochokera m'Bukhu<br />
Loyera kuti chinamwali chikhale chopambana kwa namwali.)<br />
204