28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

Ndi udindo wa alangizi kukonza maphunziro a atsikana onsewa kamodzi pamwezi.<br />

It is the responsibility ofthe instructresses to arrange meeting with the girls once every month.<br />

CHINAMWALl (KUTHA MSINKHU)<br />

PUBERTY RITE CEREMONY<br />

Malangizo kwa Alangizi<br />

For the Instructresses<br />

Pamene alangizi mwadziwitsidwa kuti mtsikana watha msinkhu, muyenera mukumane ndi<br />

mtsikanayo mwansanga. Mumuuze mwachidule tanthauzo la zimene zamuchitikirazo.<br />

Mumuphunzitsenso kabvalidwe ndi kasamalidwe ka mwele. Mtsikanayo asagwire ntchito<br />

yolemetsa, komanso asayende yende mpaka atabvinidwa potsirizira pa msambowo.<br />

When you have been informed that a girl has matured, you must meet with the girl as soon as possible. Briefly,<br />

instruct her on the meaning of the menses, how to wear and take care ofthe linen. She must do light work and<br />

should remain in seclusion until the chinamwali ceremony at the end ofher menses.<br />

Muyenera kudziwitsa amayi busa anu amene adziwitsanso abusa. Dziwitsaninso<br />

anamkungwi popeza ndiwo amene ayenera kukanena kwa mfumu. Mayi wa mtsikana<br />

apereka nkhuku yokanenera kwa mfumu.<br />

You must inform the pastor's wife who should inform the pastor. Inform also the traditional anamkungwi who<br />

will inform the chief. The girl's mother must pay the chiefs dues.<br />

Alangizi ndi mpingo, mogwirizana ndi makolo mukonzekere kumubvinira namwaliyo usiku<br />

wonse potha pa msambo wakewo. Simba labwino ndi kunyumba kwa mlangizi, komabe<br />

mukhoza kusankha malo ena opangira chinamwalicho. Alangizi, machembere a mumpingo,<br />

makolo a mtsikana (osati mai ake), ndi atsikana olangizidwa kale a mumpingo (koma awiri<br />

akhale aphungu), ayenera kudza kuchinamwalicho.<br />

The instructresses and the church, together with the parents, should prepare for the night's vigil chinamwali at<br />

the end of the girl's menses at the instructress' house, or any other house. The instructresses, the elderly<br />

women ofthe church, the girl's aunt or grandmother, and the younger women ofthe church should be invited to<br />

attend the chinamwali. Let two ofthem be tutors.<br />

Anthu onse oitanidwawo atatha kudya chakudya chamadzulo pamodzi, abusa kapena akulu a<br />

mpingo ayenera kutsegula mwarnbo ndi pemphero ndi mawu apang'ono achilimbikitso.<br />

Chonde onenetsetsani kuti kuimba, kubvina, ndakatulo, ngakhale masewero, ziyenera<br />

kutenga gawo lalikulu pachinamwali, kuti namwaliyo amvetse mwambo. Baibulo mukhoza<br />

kuwerenga koma osati Bukhu la alangizi ayi.<br />

When all the invited people have taken their evening meal, let the pastor or an elder begin with prayer and a<br />

word ofexhortation from the vernacular Bible.<br />

Please note that singing, dancing, and acting should be used in instructing the girl. You can use the Bible but<br />

not the instructresses' booklet.<br />

Mwambo wa usiku ukhoza kukhala motere. (Ichi ndi chitsanzo chimodzi, koma alangizi<br />

muyenera kukonza nyimbo zambiri ngakhalenso maseweero ndi mau ochokera m'Bukhu<br />

Loyera kuti chinamwali chikhale chopambana kwa namwali.)<br />

204

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!