28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

Gwiritsani ntchito ndime zalembedwa kotsirilizira kwa kabukhu aka pokambirana ndi<br />

atsikana za chipulumutso chao. Alangizi ayenera kuwatsogolera atsikanawo kukula ndi<br />

makhalidwe a chiKhristu, mpaka akalowe mbanja.<br />

Teaching the girls the Christian way oflife. The instructresses should lead the girls who do not know Christ to<br />

receive Jesus as their Lord and Saviour. They can use the verses which are at the back of this booklet. It is the<br />

instructresses' responsibility to mature the girls in their faith until they are married.<br />

2. Kulangiza. Alangizi ayenera kulangiza mtsikana pamene watha msinkhu; ayenera<br />

kumulangiza mmene angakhalire ndi bwezi lake; amulangize paukwati wake, pamimba<br />

yoyamba, ndi pamene mwana wabadwa. Alangizi ayeneranso kupitiriza kulangiza azimayi<br />

. .<br />

magawo oSlyanaslyana.<br />

Counsel. The instructresses should give appropriate counsel when a girl has matured, when she is dating<br />

someone, on her wedding, at her fIrst pregnancy, and when the fIrst baby is born. The instructresses should<br />

also give continuous counsel to the women in their congregation.<br />

MAPHUNZIRO A ALANGIZI<br />

TRAINING FOR THE INSTRUCTRESSES<br />

Alangizi, monga anamkungwi, ayenera kukhala odziwa bwino ntchito yao. Chomwecho ndi<br />

udindo wampingo kukonza maphunziro a alangizi pamene angosankhidwwa, komanso<br />

nthawi ndi nthawi. Kawiri kawiri m'busa ndi mai busa ndi atsogoleri ena ayenera<br />

kuphunztisa alangizi awo.<br />

Atsogoleri a Association naonso ayenera kukonza maphunziro a alangizi kamodzi ngakhale<br />

kawiri pachaka.<br />

Like the anamkungwi, alangizi should know their work well. Therefore, it is the responsibility of every<br />

congregation to arrange training sessions for her instructresses as soon as they are chosen, and from time to<br />

time. Normally it is the pastor, or his wife, or other church elders who should conduct the training.<br />

MAU KWA ALANGIZI ONSE<br />

WORD <strong>TO</strong> ALL THE INSTRUCTRESSES<br />

Ambuye akutsogolereni pamene mwabvomera kutumikira Ambuye mugawo la ulangizi iri!<br />

Zinthu zina zimene muyenera kuzindikira ndi izi:<br />

May God guide you in this ministry which you have accepted to do. Some ofthe things you need to know are:<br />

• Musaziderere, Mulungu ndi amene wakusankhani, ndipo akuthandizani.<br />

You should not undermine yourself. God is the one who has chosen you and he will help you.<br />

• Onenetsetsani kuti mwalandira maphunziro a ulangizi pampingo panu, komanso<br />

pitani kumaphunziro a Association a zaulangizi. Musayambe ntchito pamene<br />

simunaphunzitsidwe.<br />

Make sure that you have received the necessary training for your job. You must also attend the<br />

Association's leadership training. Do not start to work when you have not been trained.<br />

• Muyenera kudzipereka ndi kukhala wokhulupirika pantchito imene Mulungu<br />

wakudalirani nayo. Dziwitsani mpingo ngati pali zifukwa zimene zikulepheretseni<br />

kutumikira.<br />

202

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!