FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
Gwiritsani ntchito ndime zalembedwa kotsirilizira kwa kabukhu aka pokambirana ndi<br />
atsikana za chipulumutso chao. Alangizi ayenera kuwatsogolera atsikanawo kukula ndi<br />
makhalidwe a chiKhristu, mpaka akalowe mbanja.<br />
Teaching the girls the Christian way oflife. The instructresses should lead the girls who do not know Christ to<br />
receive Jesus as their Lord and Saviour. They can use the verses which are at the back of this booklet. It is the<br />
instructresses' responsibility to mature the girls in their faith until they are married.<br />
2. Kulangiza. Alangizi ayenera kulangiza mtsikana pamene watha msinkhu; ayenera<br />
kumulangiza mmene angakhalire ndi bwezi lake; amulangize paukwati wake, pamimba<br />
yoyamba, ndi pamene mwana wabadwa. Alangizi ayeneranso kupitiriza kulangiza azimayi<br />
. .<br />
magawo oSlyanaslyana.<br />
Counsel. The instructresses should give appropriate counsel when a girl has matured, when she is dating<br />
someone, on her wedding, at her fIrst pregnancy, and when the fIrst baby is born. The instructresses should<br />
also give continuous counsel to the women in their congregation.<br />
MAPHUNZIRO A ALANGIZI<br />
TRAINING FOR THE INSTRUCTRESSES<br />
Alangizi, monga anamkungwi, ayenera kukhala odziwa bwino ntchito yao. Chomwecho ndi<br />
udindo wampingo kukonza maphunziro a alangizi pamene angosankhidwwa, komanso<br />
nthawi ndi nthawi. Kawiri kawiri m'busa ndi mai busa ndi atsogoleri ena ayenera<br />
kuphunztisa alangizi awo.<br />
Atsogoleri a Association naonso ayenera kukonza maphunziro a alangizi kamodzi ngakhale<br />
kawiri pachaka.<br />
Like the anamkungwi, alangizi should know their work well. Therefore, it is the responsibility of every<br />
congregation to arrange training sessions for her instructresses as soon as they are chosen, and from time to<br />
time. Normally it is the pastor, or his wife, or other church elders who should conduct the training.<br />
MAU KWA ALANGIZI ONSE<br />
WORD <strong>TO</strong> ALL THE INSTRUCTRESSES<br />
Ambuye akutsogolereni pamene mwabvomera kutumikira Ambuye mugawo la ulangizi iri!<br />
Zinthu zina zimene muyenera kuzindikira ndi izi:<br />
May God guide you in this ministry which you have accepted to do. Some ofthe things you need to know are:<br />
• Musaziderere, Mulungu ndi amene wakusankhani, ndipo akuthandizani.<br />
You should not undermine yourself. God is the one who has chosen you and he will help you.<br />
• Onenetsetsani kuti mwalandira maphunziro a ulangizi pampingo panu, komanso<br />
pitani kumaphunziro a Association a zaulangizi. Musayambe ntchito pamene<br />
simunaphunzitsidwe.<br />
Make sure that you have received the necessary training for your job. You must also attend the<br />
Association's leadership training. Do not start to work when you have not been trained.<br />
• Muyenera kudzipereka ndi kukhala wokhulupirika pantchito imene Mulungu<br />
wakudalirani nayo. Dziwitsani mpingo ngati pali zifukwa zimene zikulepheretseni<br />
kutumikira.<br />
202