28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

the first baby, as well as to all women. Since death is also a type of initiation, the church must prepare<br />

appropriate instructions and teachings concerning death.<br />

TISANKHE BWANJI ALANGIZI?<br />

HOW <strong>TO</strong> CHOOSE ALANGIZI<br />

Posankha alangizi, makolo amumpingomo ayenera kusankha amayi awiri, atatu, kapena<br />

anayi amene akhala mumpingo zaka zisanu kapena kupitililapo ngati kuli kotheka. Ayenera<br />

kukhala amayi okhulupirika ndiokula muuzimu, ndikuwonetsa zitsanzo zabwino<br />

pamakhalidwe awo (Tito 2:3-5). Amayiwa akhoza kukhala pamabanja kapena ai, koma<br />

ambiri yabwino. Alangizi asankhidwe chaka ndi chaka, kapena zaka ziwiri ziri zonse, ndipo<br />

akale awiri kapena mmodzi ayenera kupitiriza pamodzi ndi alangizi osankhidwa atsopano.<br />

When choosing alangizi, all parents in the congregation should choose two, three or four women who have<br />

been members for five or more years if possible. Alangizi should be faithful and mature Christian women of<br />

exemplary lifestyle (Titus 2:3-5). They can be married or not as long as they are of good repute. The alangizi<br />

should be chosen every year or every two years, making sure there is an old one with the new ones.<br />

UDINDO WA ALANGIZI<br />

THE ROLE OF THE INSTRUCTRESSES<br />

Ulangizi ndiwofunika kwambiri pakati pa anthu onse. Mwana ngakhale munthu wamkulu<br />

kuti akhale wa makhalidwe abwino, ayenera kulangizidwa nthawi ndi nthawi. Tikayang'ana<br />

muBukhu Lopatulika tiona kuti mwazaza ndi ulangizi wosiyana-siyana wokhudza munthu<br />

mmene angakhalire ndi khalidwe labwino lokondweretsa Mulungu amene anamulenga. Mau<br />

a Mulungu amati:<br />

Malemba Oyera onse ndi Mulungu amene adawalembetsa mochita ngati<br />

kuwauzira, ndipo amathandiza pakuphunzitsa choona, pakutsutsa zolakwa,<br />

pakuwongola zokhota, ndi pakuphunzitsa anthu za kukhala olungama.<br />

2 Timoteo 3:16<br />

Counsel or advice is important for all people. For a young person or an adult to live well he or she must be<br />

counselled all the time. Scripture is full of God's counsel on how people can live lives pleasing to God.<br />

Scripture says:<br />

All Scripture is God-breathed and is useful for teaching, rebuking, correcting and training in<br />

righteousness.<br />

2 Timothy 3:16<br />

Alangizi ayenera kudziwa kuti iwo anasankhidwa ndi mpingo kugwira ntchito ya Mulungu.<br />

Chomwecho ayenera kukhala ophunzira Mau a Mulungu nthawi zonse kuti akakhoze<br />

kulangiza bwino. Ntchito ya alangizi iri pawiri motere:<br />

The instructresses should realize that the congregation has chosen them to serve God. Therefore they must<br />

study the Word of God all the time so that they are able to counsel properly. The role of the instructresses is<br />

two-fold:<br />

1. Kuphunzitsa atsikana njira ndi makhalidwe a Chikhristu. Alangizi ayenera kutsogolera<br />

atsikana amene sadziwa Khristu kubvomereza lye monga Mbuye ndi Mpulumutsi wawo.<br />

201

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!