FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
for a while from norrnallife and put into seclusion to receive instruction or mwambo in order to live according<br />
to the accepted standards of the society. These ancestral customs are passed on from generation to generation<br />
through the chinamwali rite.<br />
Kuyambira kale Chikhristu chakhala chikufika kwa anthu amene akhazikika mumiyambo<br />
yamakolo awo. Ndipo pakuona kuti chinamwali ndichofunika kumitundu ya anthu ambiri,<br />
Akhristu adaona kuti ndikofunika kukonza zinamwali zachikhristu kuti zilowe m'malo mwa<br />
zamakolo. Kuno ku Malawi aKhristu adaika chilangizo mmalo mwa chinamwali. Ndiye<br />
kuti chilangizo ndi chiphunzitso cha chiKhristu chimene namwali amalandira pamene watha<br />
msinkhu, pakukwatiwa, mimba yoyamba ndi kubadwa kwa mwana. Koma mwambo weniweni<br />
womubvinira mtsikiana uchedwebe ndi dzina loti chinamwali. Alangizi (mlangizi,<br />
mmodzi) ndiwo adalowa mmalo mwa anamkungwi.<br />
Christianity has always come to a people who believe in the ancestral customs. Initiation is very important to<br />
many societies. It is therefore important for Christianity to take initiation very seriously. Here in Malawi<br />
chilangizo was introduced to take the place of chinamwali. Chilangizo is therefore a general term referring to<br />
the Christian instruction or teaching that is given to a girl upon her first menstruation, on marriage, during the<br />
first pregnancy, and the birth of the fust baby. Alangizi took the place of anamkungwi. However, the actual<br />
ceremony retains the term chinamwali. The instructresses are called alangizi (mlangizi, singular).<br />
Popeza anthu onse adalengedwa ndi Mulungu, muchifaniziro chake ndi mchikhalidwe chake<br />
(Genesis 1:26), ndiye kuti mwambo wa Mulungu ndi umene upatsa munthu khalidwe<br />
loyenera, osati makolo adafa kale. Uwu tiupeza rnBukhu lake Lopatulika.. Ndi chifukwa<br />
chake Chikhristu chiyenera kuphunzitsa anthu ache chikonzero cha Mulungu pa kutha<br />
msinkhu, ukwati, mimba, komanso kubereka ndi kulera mwana, kuti aliyense akhale monga<br />
Mulungu afunira. Mau a Mulungu akhale otisonyeza zoyenera, kuti anthu azimvera ndi<br />
kuchita zomwe Bible likubvomereza.<br />
Since all people were created by God, in his own image and in his likeness (Genesis 1:26), it is God's mwambo<br />
(instruction/teaching) that gives us true chikhalidwe (character). We fmd God's mwambo in his Holy Bible.<br />
That is why it is important for the Chritian tradition to teach its people God's purpose for puberty, marriage,<br />
pregnancy, child-birth, and upbringing. The Bible must therefore be the people's life map. They must obey<br />
only what the Bible affirms from their cultures.<br />
Ndi udindo wa mpingo uliwonse kuphunzitsa anthu ake mwambo wa Chikhristu kupyolera<br />
muzinamwali, popeza ndi njira imene mitundu yambiri imaphunzirira miyambo.<br />
It is the responsibility of every congregation to teach her members the Christian customs through chinamwali<br />
for that is the method through which many societies learn well.<br />
WOYENERA KULANGIZIDWA NDANI?<br />
WHO SHOULD BE COUNSELLED?<br />
Potsatira chinamwali chamakolo, ndikofuna kuti ulangizi wachiKhristu utsatirenso magawo<br />
onse a paumoyo wa munthu. Ndiye amene ayenera kulangizidwa ndi mwana, msungwana,<br />
komanso mayi. Ndiye ulangizi umene uli m'kabukhumu ndi wa msungwana asanathe<br />
msinkhu, pamene watha msinkhu, pamene wapeza bwenzi lokwatirana naye, ukwati wake,<br />
mimba yoyamba, kubadwa mwana woyamba, komanso wa amayi onse. Popeza imfa irinso<br />
ndi mwambo wake, Mpingo uyenera kukonza malangizo ndi ziphunzitso zosiyana-siyana<br />
zokhuzana ndi imfa.<br />
Following the traditional way, the Christian initiation should follow the person's life from birth to death. So a<br />
child, a girl, and a woman or mother should receive counsel. The instruction in this booklet therefore is for a<br />
girl before her puberty, upon her puberty, in courtship, at her marriage, at her first pregnancy, after the birth of<br />
200