28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

tion and gift-giving time. While all are seated, the mother should begin commending and rebuking<br />

the initiate while throwing her gifts to the girl. Other relatives should follow. The instructresses<br />

should repeat for emphasis where necessary. The rest do likewise while throwing their gifts. The<br />

instructresses should repeat instruction on the following points:<br />

Lero mwakula chifukwa cha chikondi cha Mulungu. Yesu adanena kuti lamulo<br />

lalikulu ndi kukonda Mulungu ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi<br />

nzeru zako zonse, ndi mphamvu yako yonse, ndi kukonda mzanko monga<br />

udzikonda mwini (Marko 12:30-31). Chikondi choterechi chidzakupangitsa iwe<br />

kumvera izi:<br />

Today you are now an adult because of God's love. Jesus said that the greatest command is 'to<br />

love God with all your heart, with all your soul, with all your mind, and with all your strength,'<br />

followed by loving your friend as you love yourself (Mark 12:30-31). This kind of love should be<br />

the driving force for you to obey these things:<br />

Asamasewere ndi ana ochepa msinkhu popeza iye wateremu wakula tsopano.<br />

Not to play with children since she has now matured.<br />

Adzilemekeza makolo, mafumu ndi akulu.<br />

To respect parents, chiefs and elders.<br />

Adzikhala womvera.<br />

To be obedient.<br />

Adzipewa mabodza, kuba, ndi ndeu.<br />

To avoid lying, stealing, and fighting.<br />

Adzikhala wolimbikira pa kugwira ntchito pakhomo, mmudzi, ndi kumpingo.<br />

To be industrious in the home, in the village, and in the church.<br />

Adzilimbika kupita kuchalichi kukapemphera.<br />

To be committed in attending church services.<br />

Asamalumbira ndi kutchula dzina la Mulungu pachabe.<br />

Not to swear and mention God's name in vain.<br />

Adzichitira ulemu nyumba ya Mulungu.<br />

To respect God's house.<br />

Alangizi aptirize kulimbikitsa kuti kubvinidwa kotereku kukukhadzikitsa uChewa<br />

wake komanso chiKhristu chache. Ndipo khalidwe lake losinthika lidzakhala<br />

134

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!