FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
tion and gift-giving time. While all are seated, the mother should begin commending and rebuking<br />
the initiate while throwing her gifts to the girl. Other relatives should follow. The instructresses<br />
should repeat for emphasis where necessary. The rest do likewise while throwing their gifts. The<br />
instructresses should repeat instruction on the following points:<br />
Lero mwakula chifukwa cha chikondi cha Mulungu. Yesu adanena kuti lamulo<br />
lalikulu ndi kukonda Mulungu ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi<br />
nzeru zako zonse, ndi mphamvu yako yonse, ndi kukonda mzanko monga<br />
udzikonda mwini (Marko 12:30-31). Chikondi choterechi chidzakupangitsa iwe<br />
kumvera izi:<br />
Today you are now an adult because of God's love. Jesus said that the greatest command is 'to<br />
love God with all your heart, with all your soul, with all your mind, and with all your strength,'<br />
followed by loving your friend as you love yourself (Mark 12:30-31). This kind of love should be<br />
the driving force for you to obey these things:<br />
Asamasewere ndi ana ochepa msinkhu popeza iye wateremu wakula tsopano.<br />
Not to play with children since she has now matured.<br />
Adzilemekeza makolo, mafumu ndi akulu.<br />
To respect parents, chiefs and elders.<br />
Adzikhala womvera.<br />
To be obedient.<br />
Adzipewa mabodza, kuba, ndi ndeu.<br />
To avoid lying, stealing, and fighting.<br />
Adzikhala wolimbikira pa kugwira ntchito pakhomo, mmudzi, ndi kumpingo.<br />
To be industrious in the home, in the village, and in the church.<br />
Adzilimbika kupita kuchalichi kukapemphera.<br />
To be committed in attending church services.<br />
Asamalumbira ndi kutchula dzina la Mulungu pachabe.<br />
Not to swear and mention God's name in vain.<br />
Adzichitira ulemu nyumba ya Mulungu.<br />
To respect God's house.<br />
Alangizi aptirize kulimbikitsa kuti kubvinidwa kotereku kukukhadzikitsa uChewa<br />
wake komanso chiKhristu chache. Ndipo khalidwe lake losinthika lidzakhala<br />
134