28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

Onse azibvina akugwira thupi lawo ndikusonyeza kumwamba kokhala Mzimu<br />

Woyera.<br />

They should be dancing while touching their bodies and pointing towards heaven where the Holy<br />

Spirit is.<br />

16. Mwendo, mwendo nkuyenda<br />

Maso, maso nkupenyera<br />

Chimodzimodzi, ziwalo zachinsinsi<br />

Ntchito yake m 'banja<br />

Leg, leg is for walking<br />

Eyes, eyes are for looking<br />

Similarly, private parts<br />

Their job is in marriage<br />

Amayiwo ayenera kusonyeza ntchito yake ya chiwalo chochulidwacho. Koma<br />

akachula ziwalo za chinsinsi, azisonyeza pongodikhula mwaubwino. Ayenera<br />

kumubvinitsanso namwaliyo.<br />

Chiphunzitso chake ndi chomwecho chakudzisunga osadzidetsa mpaka adzakwatiwe.<br />

Chiwalo chiri chonse chiyenera kugwiritsidwa ntchito molemekeza<br />

Mulungu.<br />

The women demonstrate the use of the part that is mentioned, such as leg for walking. But for the<br />

private parts, they should demonstrate by shaking their waist up and down. They should let the<br />

initiate dance also.<br />

The teaching is still on sexual purity until marriage. Each part of the body should be used to honour<br />

God.<br />

Chiphunzitso chotsatirachi chipangidwe musewero. Ndilokhuza atsikana awm<br />

kapena atatu amene akuphunzira kumachokera pakhomo pamakolo awo.<br />

The following instruction should be acted by two to three girls who are day schooling and are<br />

staying with their parents.<br />

Atsikanawo akaweruka kusukulu, mmodzi amabwerera kunyumba, koma enawo<br />

amayamba kucheza ndi anyamata nkumakafika mochedwa kunyumba. Makolo<br />

awo akawafunsa amati amagwira ntchito yasukulu. Patapita nthawi, mmodzi<br />

wapezeka ali ndi pakati nasiya sukulu. Mnyamata wake adaikana mimbayo.<br />

Mtsikanayo anabvutika nayo mimbayo popezanso makolo amtsikanayo anaipidwa<br />

nazo. Mwana atabadwa, mtsikanayo amangodwala dwala ndipo mayi wake<br />

analibe nthawi yomuthandiza, popeza anali mayi wa bizinesi. Mtsikanayo amangosilira<br />

mzake uja atatsiriza sukulu mpaka kumanga ukwati ku mpingo.<br />

Kudwala kudapitirira mpaka kumwalira. Pamaliro anthu ankangonong'onezana<br />

nkumati kodi si edzi imeneyi?<br />

132

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!