FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
Onse azibvina akugwira thupi lawo ndikusonyeza kumwamba kokhala Mzimu<br />
Woyera.<br />
They should be dancing while touching their bodies and pointing towards heaven where the Holy<br />
Spirit is.<br />
16. Mwendo, mwendo nkuyenda<br />
Maso, maso nkupenyera<br />
Chimodzimodzi, ziwalo zachinsinsi<br />
Ntchito yake m 'banja<br />
Leg, leg is for walking<br />
Eyes, eyes are for looking<br />
Similarly, private parts<br />
Their job is in marriage<br />
Amayiwo ayenera kusonyeza ntchito yake ya chiwalo chochulidwacho. Koma<br />
akachula ziwalo za chinsinsi, azisonyeza pongodikhula mwaubwino. Ayenera<br />
kumubvinitsanso namwaliyo.<br />
Chiphunzitso chake ndi chomwecho chakudzisunga osadzidetsa mpaka adzakwatiwe.<br />
Chiwalo chiri chonse chiyenera kugwiritsidwa ntchito molemekeza<br />
Mulungu.<br />
The women demonstrate the use of the part that is mentioned, such as leg for walking. But for the<br />
private parts, they should demonstrate by shaking their waist up and down. They should let the<br />
initiate dance also.<br />
The teaching is still on sexual purity until marriage. Each part of the body should be used to honour<br />
God.<br />
Chiphunzitso chotsatirachi chipangidwe musewero. Ndilokhuza atsikana awm<br />
kapena atatu amene akuphunzira kumachokera pakhomo pamakolo awo.<br />
The following instruction should be acted by two to three girls who are day schooling and are<br />
staying with their parents.<br />
Atsikanawo akaweruka kusukulu, mmodzi amabwerera kunyumba, koma enawo<br />
amayamba kucheza ndi anyamata nkumakafika mochedwa kunyumba. Makolo<br />
awo akawafunsa amati amagwira ntchito yasukulu. Patapita nthawi, mmodzi<br />
wapezeka ali ndi pakati nasiya sukulu. Mnyamata wake adaikana mimbayo.<br />
Mtsikanayo anabvutika nayo mimbayo popezanso makolo amtsikanayo anaipidwa<br />
nazo. Mwana atabadwa, mtsikanayo amangodwala dwala ndipo mayi wake<br />
analibe nthawi yomuthandiza, popeza anali mayi wa bizinesi. Mtsikanayo amangosilira<br />
mzake uja atatsiriza sukulu mpaka kumanga ukwati ku mpingo.<br />
Kudwala kudapitirira mpaka kumwalira. Pamaliro anthu ankangonong'onezana<br />
nkumati kodi si edzi imeneyi?<br />
132