FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
You also want an ePaper? Increase the reach of your titles
YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.
Anamkungwi amuonetse mtsikana kabvalidwe ka mwele bwino-bwino. Amupatse<br />
nayenso achite monga waonera mpakana akhonze ndipo anthu alulutire.<br />
Amuonetsenso kachapidwe ndi kasungidwe kache pamene nyimbo ikuimbidwabe.<br />
Potsiriza abwereze kumulongosolela kuti:<br />
While still singing, the instructresses should demonstrate and teach her well how to wear the menses<br />
linen and how to clean and take care ofthem. They should then explain the following to her:<br />
Tsopanotu iye ayenera kudzisamalira thupi lake koposa kale. Akhale waukhondo<br />
nthawi zonse ndi thupi ndi zobvala zake. Mtsikana adzisamalire kwenikweni thupi<br />
lake ndi nsaru zake panthawi imene ali mumsambo kuti asapezeke akutulutsa<br />
fungo loipa. Komanso asakhetsere paliponse mwazi wamsambo, popeza zimachititsa<br />
manyazi kuti ena aone mwazi umenewu. Kuyimba kupitirire.<br />
Now she must take care of her body more than before. She must keep her body<br />
and her clothes clean at all times, particularly when she is menstruating so that no<br />
bad smell comes out. She must make sure that no blood stains remain anywhere<br />
for is it a shameful thing for people to see the stains. The singing continues.<br />
12. Kumana, kumana mtsikana x 2<br />
Mmati undipatse<br />
Wabvundikira<br />
13. Mulungu adawauza Adamu nda aHava<br />
Muberekane, muchurukane<br />
Refuse, refuse the girl<br />
I wanted you to give me<br />
You have covered<br />
God told Adam and Eve<br />
Be fruitful, and increase in number<br />
Longosolani kuti njira imene amatipatsira ana Mulungu ndi yakugonana mwamuna<br />
ndi mkazi amene ali pabanja. Kugonana kwa mwamuna ndi mkazi amene<br />
sali pabanja ndi chimo la chigololo pamaso pa Mulungu ('Usachite chigololo'<br />
Eksodo 20:14; 1 Akorinto 6:13,19).<br />
They should explain that God gives us children through sexual activity in a marriage. Therefore<br />
sex outside marriage is adultery to God ('Do not commit adultery' Exodus 20: 14; 1 Corinthians<br />
6:13, 19).<br />
14. Kodi lamulo la Mulungu likuti chiani?<br />
Likuti Usachite chigololo<br />
15. Kodi abale simudziwa eel<br />
Simudziwaaa eel<br />
Kodi abale simudziwa eel<br />
Simudziwaa eel<br />
Thupi lanu liri kachisi, liri kachisi<br />
Wa Mzimu Woyeraaal<br />
What does God's law say?<br />
It says do not commit adultery<br />
Friends, do you not know eh!<br />
Do you not know eh!<br />
Friends, do you not know eh<br />
Do you not know eh!<br />
Your body is a temple, is a temple<br />
Ofthe Holy Spiritiii!<br />
131