28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

Anamkungwi amuonetse mtsikana kabvalidwe ka mwele bwino-bwino. Amupatse<br />

nayenso achite monga waonera mpakana akhonze ndipo anthu alulutire.<br />

Amuonetsenso kachapidwe ndi kasungidwe kache pamene nyimbo ikuimbidwabe.<br />

Potsiriza abwereze kumulongosolela kuti:<br />

While still singing, the instructresses should demonstrate and teach her well how to wear the menses<br />

linen and how to clean and take care ofthem. They should then explain the following to her:<br />

Tsopanotu iye ayenera kudzisamalira thupi lake koposa kale. Akhale waukhondo<br />

nthawi zonse ndi thupi ndi zobvala zake. Mtsikana adzisamalire kwenikweni thupi<br />

lake ndi nsaru zake panthawi imene ali mumsambo kuti asapezeke akutulutsa<br />

fungo loipa. Komanso asakhetsere paliponse mwazi wamsambo, popeza zimachititsa<br />

manyazi kuti ena aone mwazi umenewu. Kuyimba kupitirire.<br />

Now she must take care of her body more than before. She must keep her body<br />

and her clothes clean at all times, particularly when she is menstruating so that no<br />

bad smell comes out. She must make sure that no blood stains remain anywhere<br />

for is it a shameful thing for people to see the stains. The singing continues.<br />

12. Kumana, kumana mtsikana x 2<br />

Mmati undipatse<br />

Wabvundikira<br />

13. Mulungu adawauza Adamu nda aHava<br />

Muberekane, muchurukane<br />

Refuse, refuse the girl<br />

I wanted you to give me<br />

You have covered<br />

God told Adam and Eve<br />

Be fruitful, and increase in number<br />

Longosolani kuti njira imene amatipatsira ana Mulungu ndi yakugonana mwamuna<br />

ndi mkazi amene ali pabanja. Kugonana kwa mwamuna ndi mkazi amene<br />

sali pabanja ndi chimo la chigololo pamaso pa Mulungu ('Usachite chigololo'<br />

Eksodo 20:14; 1 Akorinto 6:13,19).<br />

They should explain that God gives us children through sexual activity in a marriage. Therefore<br />

sex outside marriage is adultery to God ('Do not commit adultery' Exodus 20: 14; 1 Corinthians<br />

6:13, 19).<br />

14. Kodi lamulo la Mulungu likuti chiani?<br />

Likuti Usachite chigololo<br />

15. Kodi abale simudziwa eel<br />

Simudziwaaa eel<br />

Kodi abale simudziwa eel<br />

Simudziwaa eel<br />

Thupi lanu liri kachisi, liri kachisi<br />

Wa Mzimu Woyeraaal<br />

What does God's law say?<br />

It says do not commit adultery<br />

Friends, do you not know eh!<br />

Do you not know eh!<br />

Friends, do you not know eh<br />

Do you not know eh!<br />

Your body is a temple, is a temple<br />

Ofthe Holy Spiritiii!<br />

131

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!