28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

9. Ndinu mudanlenga inetu eee!<br />

Mudandiumba bwinotu eee!<br />

Ntchito zanu zonse nzodabwitsa eee!<br />

Onani lero ndakula<br />

Ndakulatu, ndakulaa.<br />

Akatha kubvina, amulongosolele mtsikana kuti:<br />

You created me yaa!<br />

You moulded me well yaa!<br />

Your works are wonderful yaa!<br />

Look today I have matured<br />

I have matured, I have matured ye!<br />

Mulungu adatilenga kuti thupi lamunthu likamakula limasinthika mumsinkhu ndi<br />

mmaonekedwe. AkafIka msinkhu wina mtsikana amayamba kusamba kwa masiku<br />

seven kapena kucheperako (kutuluka magazi kokozera). Kusambaku kumapitiria<br />

kamodzi pamwezi. Chizindikiro chimenechi chimaoneka kwa akazi onse. Chomwecho<br />

sizodetsa nkhawa kuti ndi matenda.<br />

Kusambaku kumalozera zamtsogolo. Imeneyi ndi nJlra yomwe anakonza<br />

Mulungu pofuna kutipatsa mphatso za ana.<br />

Apitirize kuyimba,<br />

After dancing the instructresses should give the following explanation to the girl:<br />

God created us so that as we grow our bodies change both physically and in how we look. At a<br />

certain point the girl begins to menstruate for about seven days or less (blood coming out of the<br />

private parts). This blood flow happens once a month to all women. It is not any illness to worry<br />

about. Menstruation foretells the future role. This is God's own way in order for us to have children.<br />

They should continue singing,<br />

1O.Mwateremu dzisamaleni a Joyce x 3<br />

Bvalani mwele<br />

11. Nchenje, nchenje, taona<br />

Nchenje, yaonanji?<br />

Yaona n 'nkhole<br />

Now with this, take care ofyourself Joyce<br />

Wear menses linen<br />

Fly, fly, look<br />

Fly, what has it seen<br />

It has seen the menses<br />

Kutanthauza kwa nyimboyi ndiye kuti namwaliyo adzidzisamalira maka akamasamba<br />

kuopa kununkha.<br />

The meaning of the song is that the girl should take care of herself whenever she is menstruating<br />

so that she does not smell.<br />

130

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!