28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

Create successful ePaper yourself

Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.

7. Papanda Mulungu kundikonda ine<br />

Nkadakhala yanii lera<br />

Papanda Yesu kundisintha ine<br />

Nkadakhala ndiri kuti lera<br />

Without God loving me<br />

Who would I be today<br />

Without Jesus changing me<br />

Where would I be today<br />

Onse atakhala pansi, mlangizi abwereze kufotokoza za chikondi cha Mulungu<br />

kwa ife mwa Yesu Kristu, ifetu tiyenera kumumvera iye. Tiyenera kumvera<br />

malamulo ake chifukwa timamukonda. Onse ayimbe nyimbo iyi kulimbikitsa kuti<br />

pamene timvera Yesu, iye adzatimangira mabanja athu, mpingo wathu, ngakhale<br />

mudzi wathu, ndi china chili chonse.<br />

While all are seated, one instructress should stress the fact that since God loved us through his<br />

Son, Jesus Christ, we return this love by obeying his commands. They should all sing the following<br />

song to emphasize when we obey Jesus he will build our families, our church, our community,<br />

and so on.<br />

8. Limanga banja a dzina la Yesu<br />

Limanga banjaa dzina la Yesu<br />

Limanga mpinga a dzina la Yesu<br />

Limanga mpingaa dzina la Yesu<br />

Limanga mudzi a dzina la Yesu<br />

Limanga mudzii dzina la Yesu<br />

It builds marriage oh the name ofJesus<br />

It builds marriagee the name ofJesus<br />

It builds the church 0 the name ofJesus<br />

It builds the church the name ofJesus<br />

It builds society 0 the name ofJesus<br />

It builds society the name ofJesus<br />

Onse atakhala pansi, amayi awm asonyeze sewero lamtsikana amene wakula<br />

koma akuganiza kuti waphweteka.<br />

While all are seated two women act showing a girl who has matured but knows<br />

nothing and thinks she is hurt. She therefore tells her dad who takes her to the<br />

hospital.<br />

Mtsikana: Adadi, taonani ine ndaphweteka, kaya ndi chiyani chandicheka!<br />

Abambo: Aaa! Kodi mumasewera bwanji? Taonani tsopano waphweteka eeh!<br />

Onani magazi! Tiyeni kuchipatala!<br />

Anthu onse nkuseka. Ndipo anamkungwi aimirire nayambitse nyimbo (Masalimo<br />

139:13-14):<br />

Girl: Dad, look, I have hurt myself; I do not know what has cut me!<br />

Father: 0, No! How do you play? Look now you have hurt yourself, eh! Look at the blood! Let's<br />

go to the hospital!<br />

They all laugh. Then the instructresses stand and begin to sing a song from Psalm 139: 13-14.<br />

129

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!