FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:
Create successful ePaper yourself
Turn your PDF publications into a flip-book with our unique Google optimized e-Paper software.
7. Papanda Mulungu kundikonda ine<br />
Nkadakhala yanii lera<br />
Papanda Yesu kundisintha ine<br />
Nkadakhala ndiri kuti lera<br />
Without God loving me<br />
Who would I be today<br />
Without Jesus changing me<br />
Where would I be today<br />
Onse atakhala pansi, mlangizi abwereze kufotokoza za chikondi cha Mulungu<br />
kwa ife mwa Yesu Kristu, ifetu tiyenera kumumvera iye. Tiyenera kumvera<br />
malamulo ake chifukwa timamukonda. Onse ayimbe nyimbo iyi kulimbikitsa kuti<br />
pamene timvera Yesu, iye adzatimangira mabanja athu, mpingo wathu, ngakhale<br />
mudzi wathu, ndi china chili chonse.<br />
While all are seated, one instructress should stress the fact that since God loved us through his<br />
Son, Jesus Christ, we return this love by obeying his commands. They should all sing the following<br />
song to emphasize when we obey Jesus he will build our families, our church, our community,<br />
and so on.<br />
8. Limanga banja a dzina la Yesu<br />
Limanga banjaa dzina la Yesu<br />
Limanga mpinga a dzina la Yesu<br />
Limanga mpingaa dzina la Yesu<br />
Limanga mudzi a dzina la Yesu<br />
Limanga mudzii dzina la Yesu<br />
It builds marriage oh the name ofJesus<br />
It builds marriagee the name ofJesus<br />
It builds the church 0 the name ofJesus<br />
It builds the church the name ofJesus<br />
It builds society 0 the name ofJesus<br />
It builds society the name ofJesus<br />
Onse atakhala pansi, amayi awm asonyeze sewero lamtsikana amene wakula<br />
koma akuganiza kuti waphweteka.<br />
While all are seated two women act showing a girl who has matured but knows<br />
nothing and thinks she is hurt. She therefore tells her dad who takes her to the<br />
hospital.<br />
Mtsikana: Adadi, taonani ine ndaphweteka, kaya ndi chiyani chandicheka!<br />
Abambo: Aaa! Kodi mumasewera bwanji? Taonani tsopano waphweteka eeh!<br />
Onani magazi! Tiyeni kuchipatala!<br />
Anthu onse nkuseka. Ndipo anamkungwi aimirire nayambitse nyimbo (Masalimo<br />
139:13-14):<br />
Girl: Dad, look, I have hurt myself; I do not know what has cut me!<br />
Father: 0, No! How do you play? Look now you have hurt yourself, eh! Look at the blood! Let's<br />
go to the hospital!<br />
They all laugh. Then the instructresses stand and begin to sing a song from Psalm 139: 13-14.<br />
129