28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

While the girl is seated with her tutors, the others should be dancing in a circle while wearing<br />

something like the menses linen, but not actually taking offtheir clothes.<br />

They should explain the meaning that 'now you are mature, you are no more a child!'<br />

3. Mukatere, mukatere<br />

Ndiko kukula kumeneku<br />

What you have done, you have done<br />

This is what maturity is<br />

Zimene zikuchitika panozl ndichifukwa chakuti mwakula ndipo mulandire<br />

mwambo woyenera.<br />

What is happening here is because you have now come ofage and you need to be instructed.<br />

Tsopano ndi nthawi yakuti atsikana akale aperekere maumboni a khalidwe lawo<br />

kupyolera mu nyimbo ndi kubvina. Popezatu iwo tsopano ndi anthu akhalidwe<br />

labwino kunyumba kwawo, m'mudzi, komanso kumpingo kwawo.<br />

After singing and dancing, the older girls should take the floor. The aim is to give their testimonies<br />

through songs and dancing that it is because they received the same teaching they are now good<br />

girls in their community, in their homes, even at church.<br />

Machembere ayenera kumawafupa atsikanawa pamene akuimba ndi kubvina.<br />

The women should give money gifts to the girls as they dance.<br />

4. Yeti yelele, tandiona mzako lero<br />

Yeti, nkakumana ndi amfumu, yelele!<br />

Mpo mmagwada lero yelele!<br />

Mwambo wake ngomwewu, Yeti yelele!<br />

Joy yaaa, look at me today<br />

Joy, when I meet with the chief, yaaa!<br />

I kneel down today yaaa!<br />

It is the same counsel, Joy yaaa!<br />

Mizere yachiwiri ndi chitatu ya nyimboyi kumasintha nkumachula zimene adasintha<br />

monga, anzanga akandiputa, mpo simbwezera; nkaona agogo asinja, mpo<br />

mmawalandira; nkapita kutchalichi, mpo mmasesa lero, ndi zina. Akatha apitilire<br />

kuyimba nyimbo iyi:<br />

Tanthauzo ndi lakuti, mwambo wake ndiomwewu umene tonse tinasinthira<br />

khalidwe lathu loipa kutsata labwino. Ndi Yesu yekha angasinthe munthu kukhala<br />

wakhalidwe labwino.<br />

In the second and third lines, one girl at a time goes inside and mentions the thing she has changed<br />

from, such as 'I do not pay back evil for evil,' 'I now help the elderly;' 'I now clean the church<br />

building;' and so on. They should continue to sing the following song:<br />

127

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!