28.07.2013 Views

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

FROM CHINAMWALI TO CHILANGIZO:

SHOW MORE
SHOW LESS

You also want an ePaper? Increase the reach of your titles

YUMPU automatically turns print PDFs into web optimized ePapers that Google loves.

Please note that singing, dancing, and acting should be used in instructing the girl. You can use the<br />

Bible but not the instructresses' booklet.<br />

Mwambo wa usiku ukhoza kukhala motere. Ichi ndi chitsanzo chimodzi, koma<br />

alangizi muyenera kukonza nyimbo zambiri ngakhalenso masewero ndi mau<br />

ochokera mBukhu Loyera kuti chinamwali chikhale chopambana kwa namwali<br />

(anamwali).<br />

The night's programme may be as follows. This is just one example of chinamwali. The instructresses<br />

should come up with many songs and drama with words from the Scripture to make the rite<br />

more meaningful and interesting to the girls.<br />

Machembere ayimbe nyimbo (ziwiri ngakhale zitatu) kuti namwali adziwe<br />

chimene anthu abwerera, monga,<br />

The women should sing two or three songs concerning the purpose for the vigil, such as,<br />

1. M'Baibulo, m 'Baibulo<br />

Muli mwambooo<br />

M'Baibulo, m 'Baibulo<br />

Muli mwalankhula<br />

In the Bible, in the Bible<br />

There is counsel<br />

In the Bible, in the Bible<br />

There is speaking<br />

Machembere aziimba akumuzungulira mtsikana atakhala. Ena a amayiwo atanyamula<br />

maBaibulo kumanja kwawo. Tanthauzo lake ndikuti ulangizi umene<br />

apatsidwe tsikanayo ndiochokera m'Baibulo. Popeza baibulo ndi Mau a Mulungu,<br />

ndipo Mulungu ndi amene adatilenga. Mwambo wa Mulungu ndiye wotiyenera<br />

ife.<br />

The women should be singing while going round in a circle with the initiate seated. Some of the<br />

women can hold a Chichewa Bible in their hands. They show it to the initiate. The meaning is that<br />

their counsel is from the Word of God, who is our Creator. It is God's counsel which we must<br />

follow.<br />

2. Sinkadabweratu ine<br />

Sinkadabweratu pano<br />

Yandiendetsa mnkhole yakoyi<br />

I would not have come here<br />

I would not have come here<br />

It is your menses that have made me walk<br />

Mtsikana ali chikhalire ndi phungu wake pambali, onse adziimba atachita bwalo.<br />

Azizungulira, koma ena atayerekeza kubvala mwele, koma osabvula zobvala<br />

zawo.<br />

Atanthauza kuti onse abwera chifukwa cha mtsikana amene wakula. 'Tsopanotu<br />

walowa mbungwe la anthu akulu.'<br />

126

Hooray! Your file is uploaded and ready to be published.

Saved successfully!

Ooh no, something went wrong!